02a-smcp stage 1 v2.0 chichewa ltr kutembenuke mtima pamene paulo adali m’asia).! 4 ntchito...

76
IF FOUND, PLEASE RETURN TO: ______________________________PHONE: _______________ SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO © “LEARN & LIVE THE GREAT COMMISSIONGAWO 1 v2.0 (2014) Chichewa STRATEGIC IMPACT P.O. BOX 830337, RICHARDSON, TX 75083 WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM © Zowonera, Strategic Impact. Pasakhale kusintha kulikonse kwa bukhuli, koma mukhoza kukopera mwaulere ndi kugawa osasintha kanthu. © Copyright, Strategic Impact. No changes may be made to this manual, but you may freely copy and distribute without making changes to content.

Upload: dominh

Post on 10-Mar-2018

292 views

Category:

Documents


12 download

TRANSCRIPT

IF FOUND, PLEASE RETURN TO: !!

______________________________PHONE: _______________!!

� !

SUKULU YOCHULUKITSA!OBZALA MIPINGO ©!

“LEARN & LIVE THE GREAT COMMISSION”!!

GAWO 1!!v2.0 (2014) Chichewa!!

STRATEGIC IMPACT!P.O. BOX 830337, RICHARDSON, TX 75083!

WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM!© Zowonera, Strategic Impact.  Pasakhale kusintha kulikonse kwa bukhuli, !

koma mukhoza kukopera mwaulere ndi kugawa osasintha kanthu.!!© Copyright, Strategic Impact.  No changes may be made to this manual, but you!

may freely copy and distribute without making changes to content.!

!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!�2

!STRATEGIC IMPACT !

SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO©!!GAWO 1!

!ZAMKATIMU!

!! Chiyambi! 4!! Strategic Impact - Maonekedwe Ake Pa Tsamba! 6!! Njira 10 Zofikira Dziko Lanu! 7!! Dongosolo La Strategic Impact! 8!! Mapu a Strategic Impact! 9!! Mafunso Ositha Moyo! 11!!!! GAWO 1 - “Phunzirani cholinga chachikulu cha Mulungu”! 13!! ! Ntchito 1 - “Kukhudzika ndi Khristu”! 14! ! ! Ntchito 2 - “Sinthani Maganizo ndi Kukumbatira”! 17! ! ! Ntchito 3 - “Nthawi Yokumana ngdi Ambuye”! 20! ! ! Ntchito 4 - “Kufunika kwa Unthenga Wabwino”! 23! ! ! Chida Cholalikira cha SI! 25-27! ! ! Ntchito 5 - “Umbuye wa Khristu”! 29! ! ! Ntchito 6 - “Kupemphera Pamodzi”! 32! ! ! Ntchito 7 - “Munthu wa Mawu a Mulungu”! 35! ! ! Ntchito 8 - “Kupanga Ophunzira Ochuluka Ena”! 38! ! ! Ntchito 9 - “Kumvetsera kwa Mulungu”! 42! ! ! Ntchito 10 - “Tingaphunzitse Bwanji mwa Ntchito”! 45! ! ! Ntchito 11 - “Pempherani!”! 51! ! ! Ntchito 12 - “Sankhani Malo Omwe Mutsegule Selo Yatsopano”! 55! ! ! Ntchito 13 - “Kuvomereza Machimo ndi Kuyanjana ndi Mulungu ndi Ena”! 60! ! ! Ntchito 14 - “Kodi Mpingo ndi Chiyani Nanga Mpingo Umatani?”! 63! ! ! Poolokera Gawo 2 - “KHAZIKITSANI SELO YATSOPANO YA MPINGO”! 68! !!! “Mapu A Utumiki”! 70-71!! Zolwmba! 72-73!! Mawu A Chikhulupiriro! 74-75!! Version Release Notes! 76!!!

�3

CHIYAMBI!!Masomphenya a strategic impact ndi kuphunzitsa atsogoleli omw adzachulukitssa pa mlingo uliwonse monga: ophunzira, obzala mipingo, mipingo, atsogoleri ndi zochitikachitika za kubvala mipingo. Ngati mipingo yadzala ndi ophunzira ochulutsa anzawo ikuchuluka, uthenga wabwino wa ufumu wa Khristu udzalalikidwa paliponse ndi kufunika komanso mfundo za ufumu wa Khristu zidzaonetsedwa mmadera mwathu.!!!Kuphunzitsa atsogoleri ndi ophunzira omwe adzachulukitsa anzawo sidzimangochitika wamba kuti mukhale mtsogoleri woopa Mulungu ndi wochulukitsa ena ndi dongosolo la moyo onse.Zimafunika chikhulupiliro, kuwerenga mau, kupemphera ndi kumvera Ambuye.Zimafunanso kuzochepetsa ndi kudalira Mzimu woyera.Zimachitika bwino monthandizana ndi chilimbikitso komanso kukhulupirira ndi anthu ena.!!!M’buku la machitidwe a tumwi chipangano chatsopano tomaona momwe ufumu wa Mulungu umafalikira. Limaonetsa machitidwe a Mzimu woyera kudzera mwa anthu a Malungu m’mipingo pokwaniritsa ntchito yake yokhala mboni mu Yerusalemu, Yudeya ndi Samaria ndi kumalekezero a dziko lapansi (Machitidwe 1:8) pamene akhristu adapereka uthenga wabwino kwa anthu apadziko, tiona chiyambi cha chimango cha mpingo. Poyamba tikuona mpingo wa ku Yerusalemu, (Machitidwe 1-7), kenako tinanso mpingo wa ku Antiokeya (Machitidwe 11-13) ndiponso pomaliza mipingo ya amitundu yomwe mtumwi Paulo anabwela (machitidwe 14-20).!!!Umodzi mwa mipingo yochititsa chidwi ndi mpingo wa ku Aefeso. Pamene Mtumwi Paulo ifenso, machitidwe 19:9-10 tanaona kuti anatenga ophunzira ndikumawaphunzitsa mau a Mulungu tsiku ndi tsiku m’sukulu yotchedwa Turano. Izi zidachitika kwa zaka ziwiri kotero Ayuda ndi Ahelene omwe amakhala m’ Asia adamva mawu a Ambuye. Kupyolera m’sukulu ya Turano, Mtumwi Paulo anachurutsa ophunzira omwe adabzala mipingo m’malo achiloma a ku Asia, ichi chidapangitsa anthu a mdera lonse kumva uthenga wabwino. Zosagalatsa kwambiri.!!!Mmodzi mwa ophunzira ochulukitsa ena adali Epafra, zikuoneka kuti iye adakhala Khristu ndipo adaphunzitsidwa ndi Paulo ku Efenso panthawi imeneyo. Kenaka Apafre adapita ku mzinda wa ku KOlose mdera la ku Asia (zikuoneka kuti uku kudali kumudzi kwawo kwa Epafra). Adalalikira uthenga wabwino wa Yesu Khristu ndi kuyambitsa mpingo kumeneko ndi ku malo oyandikana nawo ku Herapoli ndi ku Laodikapa (werengani Akolose 1:6-7, 2:1, 4 :12-13). Tikudziwa kuchokera mndime zimenezi kuti Paulo sadakhaleko m’midzinda imeneyi (akolose 2:1), komabe mipingo idabzalidwa kumeneko chifukwa cha utumiki ea Paulo ku Efenso.!!!Mawu a Mulungu akusonyeza kuti ena mwa iwo amene adaphunzitsidwa ndi kutumidwa ndi Paulo pa nthawi imeneyi ku Efenso, adapita ku Roma kukathandidza kuyambitsa mipingo kumeneko (onani Aroma 16:5, imatchula Epeneto, yomwe adali woyamba kutembenuke mtima pamene Paulo adali m’Asia).!

�4

Ntchito yolalikira idapatsidwa kwa ife ndi Ambuye Sesu ndipo chitsanzo ndi “sukulu ya Turano” ku Efenso ndiyenso chitsanzo chathu cha sukulu yochukikitsa atsogoleli ochulukitsa mipingo, imenenso ili mmanja mwanu ndi sukulu yochulukitsa atsogoleri imene idzayambenso mtsogolomu. Ngati muli ndi buku ili ndiye kuti mudatenga mbali kapena kuti mwangomalidza kumene mamphunziro atsogoleri (a leadership thrust). Ndi pemphero lanthu kuti Mulungu agwiritse ntchito maphunziro amanewo pokulimbikitsani kukula moyo wanu ndi kuphunsira maluso osiyanasiyana ofunika pa utsogoleri.Mudamvaponso za magawo khumi zokafikila dziko lanu. Tikukhulipirira kuti mudaonapo Mulungu akukugwiritsani ntchito pamodzi ndi abale ena, polalikira ndi kuphunzitsa anthuotayika pokhazikitsa mipingo yatsopano mdera lanu.!!!Kukula ndi kutukula kwanu muntchito iyi sikunathe ayi. Tikuyenera kuzipereka ndi kupitiliza ntchitoyi kuti tipambane. Kuchita nawo maphunziro atsogoleri (leadership thrust) chinali chiyambi chabe. Ndi chofunika kupitiliza dongosolo la kukula ngati mtsogoleri wochulukitsa ena. Maphunziro otsatirawa apangidwa kuti alimbikitse zomwe mudaphunzira ku maphunziro a atsogoleri (leadership thrust) ndi kutambasula mitu yake. Maphunzirowa apangidwa m’magawo awiri akuluakulu awa: !!

1. Kukula kwa umoyo wathu!2. Kubzala mipingo!!

Phunziro lililonse lapangidwa kutha pa sabata imodzi. Maphunziro onse khumi ndi anayi a GAWO 1 la sukulu ya atsogoleri ochulukitsa abzala mipingo (pamodzi ndi zochita zawo zomwe) akuyenera kumalidziwa kwa miyezi inayi , komabe chifunika kwambiri ndi kukwaniritsa ntchito ndi zochita kuposa kungothamangira kumaliza bukuli.!!Kuti muoloke moyenera kuchokera GAWO 1 kupita GAWO 2 ndi kupitiriza maphunziro anu mukuyenera kukwaniritsa zinthu zinayi izi:!!

1. Kumanani sabats lililonse ndi anzanu a mgulu lanu ndi kukambirana mafiunso khumi a angwiro.!!

2. Kwaniritsani zochitika ponokha za m’sabata pamne muzikona pagulu lanu.!!3. Falitsani uthenga wabwino sabata lililonse kwa omwe sakumudziwa

Khristu. !!4. Yambitsani selo ya mpingo yatsopano ndi anthu awiri mpaka khumi kapena

kuposera apo ndi gulu lanu. !!!Mulungu akudalitseni pamene mukutsatira ndi kumtumikira Ambuye pokwaniritsa ntchito yolalikira uthenga wabwino.!!!Gulu la atsogoleri a Strategic Impact. !!!!

�5

� !�6

� !�7

� !

�8

� !

�9

!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!�10

STRATEGIC IMPACT!MAFUNSO OSITHA MOYO*!!

MAFUNZO AIKIDWA KUTI AKUTHANDIZENI MMAKHALIDWE NDI KUULULA MACHIMO. AKUYENERA KUFUNSIDWA NDI KUYANKHIDWA MOKHULUPIRIKA, MWACHISOMO POCHOKERA MMADZIKO A CHIKONDI. CHOKAMBIRANA MGULULI SICHIKUYENERA KULANKHULUDWA KUNJA KWA GULULI.!!1. Kodi mwakula mchikondi ndi mmoyo wopembeza Khristu m’sabatayi? Motani?!

2. Kodi mwamaliza ndime yanu yoewrenga m’sabatayi? Kodi Mulungu adalankhula chiyani kwa inu? (Gwirizanani za ndime yomwe mukhale mukuwerenga sabata ikudzayi; musapite kundime yatsopano mpaka mutamaliza ndime yakale.)!

3. Kodi mudamvetsera, kumvera ndi kudalira mzimu woyera pokhala ndi kuchita chomwe Mulungu akufuna? M’njira yanji?!

4. Kodi mudawerengapo, kuonera ndi zinthu zolauta. Poganiza kapena pochita; kapena kukhala m’chizolowezi cha chikhalidwe choipa m’sabatayi?!

5. Kodi mudasowa ugwiro pa chuma m’sabatayi kapena kusirira chithu chomwe si chanu?!

6. Kodi mwayenda mchikondi ndi abale wanu pa banja, anzanu, oyandikana nawo kapena mpingo m’sabatayi?!

7. Kodi mwapitiriza kukhala wa mkwiyo ndi kusakhululuka wina, kapena kukhumudwitsidwa wina ndi mawu, poyankhula nawo kapena mwa miseche ndi kudandaula kwa ena m’sabatayi?!

8. Kodi mwakhala mboni yabwino pa ukulu wa Yesu Khristu m’mawu kapena ntchito zanu? Ndani amene samadziwa Khristu yemwe inu mwamuuza za iye?!

9. Kodi mudamaliza zoyenera kuchita msabatayi ?ndi chiyani chomwe mwaphunzira? Kodi nchiyani chomwe chadakupingani pokwaniritsa zimenezo? Nchifukwa chiyani? (Musapite m’phunziro lotsatira pokhapokha aliyense atakwanira zomwe anayenera kuchita).!

10.Kodi mwandiyankha mokhulipirika?!!!!!*ADAPTED FROM NEIL COLE'S LIFE TRANSFORMATION GROUPS CARDS © 1999. WWW.CMARESOURCES.ORG!

�11

!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! !!!!

�12

!!

GAWO 1!“Phunzirani Ntchito Yaikulu”!

Ntchito 1-14!!Takulandirani pa ulendo wophunzirira momwe mungakhalire wobzala mipingo wochulukitsa. Mgawo ili, inu ndi gulu lanu mudazkula m’moyo wanu wa uaimu pogwira ntchito limodzi ndi kulalikira Khristu ndi kuyambitsa mpingo watsopano. Pamene inu ndi gulu lanu mwamaliza ntchito ndi kukhazikitsa selo yatsopano, mudzakhala oyenera kuoloka mlato ndi kupita gawo 2 la Sukulu Yochulukitsa Obzala Mipingo.!!!

� !!�13

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!NTCHITO 1 - “KUKHUDZIKA NDI KHRISTU”!!

Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi

kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi mukuganiza kuti Mulungu amafuna chiyani kwa inu chachikulu kuposa !! chilichonse?!!!!Anthu ambiri amaganiza kuti Mulungu amafuna zambiri kwa ife monga: kumvera atumiki (ntchito), kupembeza maluso. Zinthu zonsezi zili ndi malo ma ubale anthu and Mulungu, koma Yesu adayankhula momveka bwino kwa ife chopatsa chilichonse.!!Choyamba chachikulu chomwe Mulungu amafuna kwa ife timachipeza mu lamulo lalikulu m’baku la Mateyu 22:37-39, “ndipo Yesu adati kwa ife, uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mzeru zako zones, ili ndilo lamulo lalikulu ndi loyamba. Ndipo lachiwiri lolingana nalo ndi ili, uzikonda mzako monga idzikonda iwe mwini. Pa malamulo awiri awa mpokolowekapo chilamulo chonse ndi aneneri.’”!!Mulungu amafuna kuchokera kwa inu koposa chilichonse kuti mumkonde ndi moyo wanu wonse. Amafuna chiyanjano cha chikondi cha poyamba ndi inu, Mulungu amafuna kuyanjana naye mchikondi koposa ntchito zomwe mamamgwirira iye.Ichi nchithu chodabwitsa, cha mphamvu, cha muyaya. Mulungu wamphamvu amafuma ubale wa chikondi ndi inu.!!Dandaulo la Mulungu pa anthu ake a Israel silidali lokhudzana ndi chikhalidwe chawo kapena nsembe zawo, kome chifukwa anasithanitsa zinthu izi ndi kuyanjana naje kapena kokomana naye mchikondi. Werengani Masalimo 40:6-8; 50:7-17. Mkwiyo wa Mulungu udayaka chifukwa cha kupemphera mafano kwao, mmalo mopempherera iye adaikapo zina, (werengani Ezekieli 6:9). Yohane adatichenjezanso kuti tipewe kupembeza mafano. (1 Yohane 5:21).!!!Werengani Chimvumbulutrso 2:1-7. Yesu adayamikila mpingo wa ku Efenso chifukwa cha kulimba kwawo, chipiliro, chiphunzitso chabwino ndi kumva zowawa chifukwa cha iye. Uwu udali mpingo wabwino ndithu! Komabe iye anadandaula mowatsutsa chifukwa choti adataya chikondi chawo cha poyamba (ndime 4)! Yesu adawaudza kuti alape ndi kuyamba kukhunzika naye, ndi kuyanjana naye ndi chikondi cha poyamba, kapena iye adzabwera ndi kuchotsa choikapo ngati chawo, chimene chidali mpingo wawo (ndime 5. Onaninso Chivumbulutso 1:20). Yesu akuyankhula kwa iwo ndi ife, kuti kapena sadzakhale ndi mpingo koposa kukhala ndi mpingo wabwino wopanda chikondi.! !!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi sikhalidwe ziti za chipembezo zomwe zingasinthe kukhudzika pa !! kupembeza Mulungu? Kode kuopsa kotaya kukhuzika ndi chikondi chapoyamba ndi Yesu !! ndi kotani?!!!

�14

Choopsa kwa ife ndi choti tasinthanitsa ntchito ya Mulungu m’malo mwa chikondi cha pa Mulungu. Anthu nthawi zonse amakhutitsidwa ndi maudindo, maina, chuma ndi mphamvu, komanso mpingo! Komabe Mulungu amakhutitsidwa ndi mtima wozipereka kwa thunthu kwa iye (Sal 40:6-8).!!Zimatengera kukhala chifupi, kukhala mu ubale wachikondi ndi Khristu kuti chilichonse chiyende mwa Chikhristu.Zotikopa zonse zizapita, chikondi cha pa yesu ndi chomw chingatipyoletsa ife kuzovuta ndi muzonkhumudwitsa. Chikondi cha pa Yesu ndi chomwe chingathandize kukonda anthu ena. Chikondi cha pa Yesu ndi chomwe chingatipangitse kupitiliza kugawa uthenga wabwino kwa otayika. C hikondi cha pa Yesu ndi chomwe chingatipangitse kukopeka pa kukwaniritsa ntchito yaikulu yolalikira chikondi cha pa Yesu ndi chomwe chongatithandize kupambana mayesero ndi chisunzo. Chikondi cha pa Yesundi chokhacho chingatipangitse kupitiliza kukhala wamphamvu poyenda ndi kumvera khristu. Yesu anati “ngati mukonda ine, mudzasunga malamulo anga” (Yohane 14:15) m’chikondi muli kumvera.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi chiyani chidzakuthandizeni kusungabe chikondi cha poyamba?!!!!PHUNZIRO LALIKULU: MULUNGU SAFUNA ANTHU OPHUNZIRA BWINO ABUSA NDI !! ATSOGOLERI AMENE ADZAMTUMIKIRE NDI ZIKHALIDWE ZOPANDA PAKE, KOME !! ANTHU OMWE NDI OZIPEREKA KWANTHUNTHU AMENE AMAKHUZIKA M’CHIKONDI !! NDI KHRISTU.!!!!ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Werenganinso Chimvumbulutso 2:1-7, kodi chikondi cha ubale wanu ndi Yesu !! chilibwanji lero? Ngati mwataya chikondi chanu choyamba pa iye, pezani nthawi lapani !! ndi kupempha kuti akukhululukireni (1 Yohane 1:9).!!!!!� Tsiku 2: Kodi !ndi zochita ziti tapeza zikhalidwe ziti pa moyo wanu wa chikhristu zomwe !! zachotsa kukhazika mozipereka kwa Yesu?!!!!!!!!! Kodi mungazipewe motani kuti zisakhale mofano amene achotsa ubale wanu ndi Yesu?!!!!!!!!

�15

� Tsiku 3: Tchulani njira zitatu zomwe zingakuthandizeni kukhalabe pa ubale wa chikondi cha !! poyamba ndi Yesu. Fotokozani momwe mudzachitire zinthu izi kwa mwezi otsatira kapena !! chaka.!!!

1. ____________________________________________________________!! Motani?!!!!!!!!

2. ____________________________________________________________!! Motani?!!!!!!!!

3. ____________________________________________________________!! Motani?!!!!!!!!� Tsiku 4: lembani kalata yanu yachikondi kwa Yesu/sungani ndi ndikumaona kamodzi pa !! sabata kwa chaka. Mudzaonjezera pamene mukukula mchikondi cha pa Yesu.!!!!!!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!!

�16

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 2 - “SINTHANI MAGANIZO ANU NDI KUKUMBATIRA”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Mutha kuwerenga mosamalitsa ndi kuphunzira chipangano cha tsopano di kutsapeza lamulo lochita zimene abusa ambiri ndi atsogoleri a mpingo akuchita lero. Pamene abusa ambiri ndi atsogoleri ali ndi chikhumbokhumbo chofuna kulemekezedwa pa ntchito yabwino yomw akugwira, si chimene Ambuye akufuna kuti ife tikhale ayi. Kodi chikhumbo chosocheretsa chimene atsogoleri ambiri alinacho ndi chiyani? Ndi ndikumanga mpingo waukulu koma, Yesu sadatikane ife kunangira Mulungu mpingo waukulu! Sadatilamule ife kumanga mpingo waukulu, kungoti simudzapeza lamulo lakuti tibzale mpingo. Kodi sizoona kuti ambiri a ife tikutumikira |Mulungu tikufuna zinthu zomwezi? Mwatsoka tatengera zolinga zolakwika.!!Nthawi zonse timatanthauzira kuti mpingo waukulu ndi womwe uli ndi anthu ambiri, zochitika zazikulu, ndondomeko yailiku ya kangwirindwe ntchito ka nmdalama ndi wa mbiri yabwino. Kumeneku pamaso pa Mulungu kapena ayi. Chimodzimodzi mpingo waung’ono wa zochitika zochepa kapena wopanda nyumba yopehphereramo utha kusakhalanso waukulu. Ndipo timapangazovuta zachikunja posiyanitsa mpingo wathu ndi mipingo ina potengera zimenezi. Izi sizomwe Mulungu amadzifuna. Abale ndi alongo tikuyenera kusitha maganizo anthu pa chenicheni chomwe Mulungu adatiitanira.!!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi Mudapanikizikapo pakumangira Mulungu mpingo waukulu molingana !! ndi muyeso uwu?!!!!Ngati Yesu sadatitane ife kumanga mpingo waukulu kapena ngakhale kubzala mipingo, chiyani, tsopano chomwe tikuchita? Yesu adayakhula momveka bwino pa lamulo lake lotsiriza “pitani ndi kupanga ophunzira a mitundu yonse…” Mateyu 28:19. Iyi ndiye ntchito yathu yaikkulu kuchokera kwa Yesu Khristu. Cholinga chathu choyambirira ndi kutengera uthenga kwa otiyandikira mmidzi, m’mizinda, dziko lathu ndi dziko lonse lapansi; kukapindula miyoyo yochuluka ngati kotheka ku chikhulupiriro cha mwa Khristu , kuphunzitsa ndi kupanga ophunzira kenaka ndi kuwatuma kukachulikitsa ufumu wa Mulungu. Iyi ndi ndondomeko yomw tikuyiona m’buku la Machitidwe. Atumwi ndi ophunzira kenaka ndi uthenga wabwino pa dziko lonse. Chifukwa cha ichi, mipingo inayambitsidwa, inakula ndi kuchulukitsidwa (onani Machitidwe 6:1, 7; 9:31; 19:10). Koma choyambirira sichidali kubvala mipingo koma kupanga ophunzira monga adachitira, kuchulukitsidwa kwa mipingo kudali chifukwa chomveka ntchito yaikulu yolalikira. Ichi ndi chipambano chofunika. Cholinga chathu sikumanga mipingo yaikuli koma kuchulukitsa ophunzira. Pamene tisunga xholinga ichi m;mitima yathu, zotsatira zake ndi kukhala ndi mipingo yabwiono.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi kusitha kwa mtundu wanji komwe mungapange pamene mulimbikira !! kuchulukitsa ophunzira (mmalo momanga mpingo waukulu)?!!!!

�17

Pamene mukuwerenga chipangano chatsopano mupeza mpingo wosavuta uli ndi dongosolo losavuta, omw unachulukitsidwanso mosavuta. Umatsogoleredwa ndi atsogoleri (1 Timoteo 3, Tito 1) ndipo adachita zinthu zosavuta monga kupembeza, kutumikira wina ndi mzake, kupanga ophunzira mofanana dni kuchita umboni kwa ena (onani 1 Akorinto 14; Akolose 3:15-17; 4:2-6). Mtsogoleri wina wampingo akuti mipingo yosavuta ya m’chipangano chatsopano idali ndi chodwi pa zinthu zitatu zofunika izi:!!! ! 1) Kudzipereka ku chonadi cha mulungu,!!! ! 2) Kukonda ndi kutumikira ena mumpingo, !!! ! 3) Kuchitira umboni ku dziko lapansi.1 !!!Mosiyana, mipingo yambiri lero yacuta, dongosolo lathu ndi zochita nthawi zambirizimatichotsa pa kupanga okhulupirira kukhala ochulutsa ophunzira, chimene ndi chilinga cha mpingo. Tikuyenera kuika chidwi chathu pa zimene ena angathe kutulutsa. Funso lomwe tingamadzifunse mosasunthika ndi loti “kodi ena amayha kutulutsa mosavuta zomwe ine ndikuchita?”!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi zinthu ziti zomwe gulu lathu lingachite kuti mipingo yathu ikhale !! yosavuta molingana ndi zinthu zili muntundamu? !!!!!Choncho, chidwi chathu ndi cholinga chathu choyambirira chichoke pa kumanga mpingo waukulu ndi kukhala wochulutsa ophunzira. Tisachite chibwana pa kupanga ophunzira amene adzabeleke ndi kusakhutitsidwa ndi anthu omwe amangosonkhana mumpingo. Pa nthawi yomweyonso tikuyenera kuphweketsa dongosolo la mipingo yathu ndi zochita kuti enanso athe kuzichita ndi kuzichulukita. Lamulo pa chochita cha mpingo uliwonse ndi ichi:!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi zinthu ziti mu utumuki wa mpingo wanu zomwe ndi zovuta kwa !! mkhristu wamba kuzichita? N’chifukwa chiyani mukuganiza kuti zitha kusokoneza !! kuchulukitsa kwa ophunzira?!!!!!!PHUNZIRO LALIKULU: MAITANIDWE ATHU SIKUMANGA MPINGO WAUKULU KOMA !! KUCHULUKITSA OPHUNZIRA.!!!!!!Pamene mukuganizira ndi kuonanso phunziroli, onaniso utumiki wa mpingo wanu pamene mukuchita zochita m’sabatayi:!!!!

�18

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Onaninso zochita za utumuki wanu m’mwezi wathawu ndipo mokhulupilika ! yankhani mafunso awa: Munganene kuti cholinga chanu choyambirira ngati ! m’busa / mtsogoleri ndi:!!! � Kumanga mpingo waukulu?! � Kupanga ophunzira omwe adzachulukitsa ena?!!! N’chifukwa chiyani mwayankha chotero?!!!!!!!� Tsiku 2: Kodi ndi chochita kapena dongosolo lanji limene inu mukukhuzidwa nalo pa mpingo !! zomwe zakuchotsani pa cholinga choyambirira chochulukitsa ophunzira?!!!!!!!!!!� Tsiku 3: Kodi ndi zochita kapena dongosolo lanji lomwe Ambuye akukutsogolerani kulithetsa !! kapena kulisintha kuti mulimbikitse dongosolo la mpingo losavuta pokwaniritsa ntchito !! yaikulu yolalikira?!!!!!!!!!� Tsiku 4: Werengani chipangizo “panga ophunzira chulukitsa.” Kodi ndi ndani amene mwakhala !! mukulankulana naye za Yesu amene mukufuna kumthadiza kuti akule ndi kukhwima ndi !! kukhala wochulukitsa ophunzira? Kodi mudzakomana naye liti koyamba? Nanga ndi kuti?!! !!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!1Neil Cole, Organic Church, Chapter 8.!!

�19

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 3 - “NTHAWI YOKOMANA NDI AMBUYE”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!

Ngati tikufuna kukhalabe okhudzika ndi Khristu, ngati tikufuna kusintha magawo athu, ngati tikufuna kukula m’chikondi chathu ndi kumvera Kristu, ngati tikufuna kukhala oona ku maitanidwe athu ndi kuzipereka, ndiye tikuyenera kumakhala ndi nthawi patokha yokomana ndi Mulungu. Nthawiyi kawirikawiri imatchedwa “nthawi yopembezera” kapena “nthawi yachete.”!!Umboni ndi ntchito ya anthu a Mulungu m’baibulo ndi mbiri yao yomwe ndizoti amazipereka tsiku ndi tsiku mosinthasintha kwa Mulungu pa kuwerenga mawu ndikuphunzira mawu ndikupemhpera, Khalidwe lauzimu ili ndilofunika kwamwana wa Mulungu aliyense. Popanda ichi sitingamve bwino ubale wathu ndi Mulungu womwe amaufuna pa ife. Kodi timadziwa bwanji izi? Chifukwa timadzipeza mm’oyo wa Yesu khristu mwana wa Mulungu wamoyo. Ngati nthawi yosasinthasintha yokomana ndi Mulungu yekha idali yofunika kwa Yesu- Wosachimwa, kotani ife ofooka, auchimo ndi ana osowa a Mulungu.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi mukuvomereza kuti Simungakule kukhala munthu amene Mulungu !! akufuna kapena kukwanitsa zonse zomwe Mulungu akufuna pa inu popanda kukhala ndi !! khalidwe lokhala ndi nthawi yokomana ndi Mulungu tsiku ndi tsiku? Chifukwa chiyani ! !! simukugwirizana nazo?!!!!Tiyeni tione moyo ndi ntchito ya Yesu kuti tipeze momwe amachitira chikhalidwe ichi pa moyo wake. Tiwerenge pamodzi Marko 1:35-39. Izi zidachitika mmawa zitatha zomwe zimanenedwa kuti tsiku lachitatu mu utumiki wa Yesu. Dzulo lake nkuti Yesu adayamba kumphuzitsa m’sunagoge mm’awa kwambiri, kenaka adapita kunyumba ya Petulo pamene adachiritsa mpongozi wake wa petulo, Madzulo amenewo anthu onse a mu mzindawo adapita kunyumba ya Petulo kumene Yesu adachiritsa iwo onse kufikira usiku (onani ndime 21-34) Chikhalirecho Yesu sadachipange kukhala Choyambira Kudzaka ndikukhala ndi nthawi yokomana ndi Mulungu mmawa wotsatirawo.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Werengani limodzindime 35 kawiri. Kodi ndi zinthu izi zomwe Yesu adakhala !! chitsanzo kuti ifenso tingachite!kupatula nthawi yokoma na ndi Mulungu?!!!!Ziwani kuti Yesu adadzuka mm’awa kwambiri iye adachipanga pa nthawiyi. Adachoka pakati pa anthu,adapita pa malo pena ake a yekha.!!TIWERENGE LIMODZI (LUKA 5:15-16). Kodi ndi ziti zomwe anthu amafuna kuchokera kwa Yesu pa nthawiyi? Kodi ntchito ya Yesu ya nthawi ndi nthawi idali yotani?(ndime 16)!!Kachiwiri, tikaona mmoyo wa Yesu kuti adachipanga kukhala choyambirira kuchoka ndikukhala yekha ndi Mulungu amadzichotsa pa gulu la anthu amapita pa malo ena ake!Amakhala ndi nthawi kupempherera ndi kumvetsera kwa Mulungu.!!

�20

FUNSO LOKAMBIRANA: Gawanani ndi ena mgulu lanu zomwe mwakhala mukuchita ndi zomwe !! zidakuthandizani pa nthawi yanu yokomana ndi Mulungu. Kodi chovuta chachikulu chomwe !! mwakhala mukukomana nacho pokhala nd inthawi yachete ndi chani ?!!!!!Powunikira chitsanzo cha Yesu, timapeza zofunikira zomwe zimapanga nthawi yokomana ndi Mulungu motere:!!

1. Nthawi idali yoyambirira pa Yesu.!!2. Udali m’chitidwe wake nthawi ndi nthawi. !!3. Amkazichotsa pakati pa anthu ndikukhala yekha ndi Mulungu.!!4. Amapita pa ena pa nthawi yake yokomana ndi Mulungu.!!5. Amapemphera ndi kuyankhula ndi Atate wake.!!6. Amawerenga kulingalira ndikukweza mawu a Mulungu (onani Mateyu 4:1-10 pamene

adasala kudya kwa masiku 40 ndipo adayesedwa ndi satana. Chitetezo chake chidali pa kugwiritsa ntchito mawu a Mulungu kuchokera m’buku la Deuteronomo amene adawaloweza. Moyembekezera amkawerenga ndi kulingalira pa ndimezi pa nthawi imeneyi).!!!

Ndiye, ngati titsatira chitsanzo cha Yesu pa nthawi yathu yokomana ndi Mulungu tikuyenera:!1. Kuyitiratu nthawi yokhala ndi Mulungu. Ena apeza kuti m’bandakucha ndi nthawi yabwino,

pamene ena amakonda nthawi ya usiku. Sikufinika kuti tione kuti nthawi yabwino, pamene ena amakonda nthawi ya usiku. Sikafunika kuti tione kuti nthawi yabwino ndi iti, koma mwayenera kapanga nthawiyo kukhala choyambirira.!!

2. Khalani nokha pa inu nokha potalikirana ndi anthu kapena zosokoneza.!!3. Pezani malo ena ake pamene mungachite izi.!!4. Pempherani ndi kuwerenga mawu ake.!!!

Zinthu zina zomwe anthu apeze kukhala zothandiza pa ichi ndi izi: khalani napo polemba kuti kuti muzilembepo maganizo anu ndi mapemphero ndi chimene Mulungu akukuphunzitsani. Nthawi zina buku lofotokoza momwe mungakomanire ndi Mulungulimatha kuthandizanso mwapadera nthawi yoonjezera ya kusala kudya, kupemphera ndi kulingalira mawu a Mulungu. Kumbukirani, nthawi yokomana ndi Mulunguyi si ya utumiki kapena kokonzekera kotumira, koma kuonjezera abale wanu ndi Mulungu.!!PHUNZIRO LALIKULU: NTHAWI YOKOMANA NDI MULUNGU TSIKU NDI TSIKU NDI YOFUNIKAA !! NGATI TITAFUNA KUKULA MU UBALE WATHU NDI MULUNGU!!!!

�21

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Ganizani momwe mungapangire nthawi yokomana ndi Mulunguyi kukhala !! choyambirira pa moyo wanu. Kodi ndi zinthu ziti zomwe ziyenera kusintha kuti nthawiyi !! ikhale choyambirira pa moyo wanu?!!!!!!!!!� Tsiku 2: Kodi ndi kuti komanso liti limene mudzakhala ndi nthawi yoyanjana ndi Mulungu tsiku !! ndi tsiku. Kodi ndi kuti kapena nthawi yanji imene inu mungakhale nokha ndi kulumilazana !! ndi Mulungu?!!!!!!!!!!� Tsiku 3: Kodi dongosolo lanu lowerenga Baibulo, mawu, kuwalingalira ndi kuloweza mawu !! lidzakhala lotani panthawi yokomana ndi Mulungu?!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Lembani mwapadera zomwe mungakhale mukuchita pa nthawi yoyanjana ndi !! Mulunguyi. Chitani izi mongoyeserera kwa sabata imodzi keneka fufuzani momwe !! mungamapangire nthawi kukhala yaphindu kwa inu.!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�22

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 4 - “KUFUNIKA KWA UTHENGA WABWINO”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Chilichonse chomwe chimachitika ku strategic impact chayenera kuthera pa kulalikira, kutengera uthenga wabwino wa Yesu Khristu ku dziko lotayika. Awa ndi maitanidwe athu aakulu mwa Yesu Khristu. Iye amafunitsitsa aliyense atamva uthenga wabwino ndi kukhala mchiziwitso cha kupulumutsa kwa Yesu Khristu. Tikuyenera kugwira motsatira mathero amenwa mpaka dziko lapansi litamva za Yesu ndi momwe angamdziwire iye.!!Ngati mbali imodzi ya Suklulu Yochulukitsa Obzala Mipingo, mukuyenera kupitiliza kugawa uthenga wabwino kwa anthu a mdera lanu. Ndipofunika kwambiri kudziwa kuti uthenga wabwino ndiwofunika bwanji ndi momwe tingagawire kwa ena momveka bwino komanso mosabvuta kuti enanso abwere ku chikhulupiriro cha kupulumutsa mwa khristu. Nthawi zambiri timakhala okhudzawa kuti Akhristu – ngakhalenso abusa ndi atsogoleri akusokonezeka pa chinthu chofunika kwambirichi.!!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi mauthenga a mtundu wanji omwe takhala tikumva kuchokera kwa !! Akhristu, mipingo kapena abusa poyankha funso loti, “Kodi nditani kuti ndipulumutsidwe?”!!!!!Ndipofunika kwambiri kuti tisasokoneze anthu pa chinthu chofunika kwambiri pa chinthu chofunika kwambiri pa munthu aliyense; ngakhale bwanji ndi moyo wosatha ndi Mulungu. Mfundo zofunika kwambiri za uthenga wabwino zimapezeka pa 1 Akorinto 15:1-8 (Tiwerenge limodzi). Timapeza m’nzimenezi mtima weniweni wa uthenga wabwino.!!

1. Yesu Khristu adafa chifukwa cha machismo athu, ndime 3.!!2. Thupi lake lidaikidwa m’manda, ndime 4.!!3. Adanka kwa akufa mwamphavu pa tsiku lachitatu, ndime 5-8!!4. Iwo amene aika chikhulupiriro chawo pa Yesu Khristu ngati Mpulumutsi wa moyo wao

machino awo adzakhululukidwa ndi kukhala ndi moyo wosatha. (1 Akorinto 15:1-2, 51-53)!!!Pamene tigawa uthenga wabwino wa Yesu Khristu kwa ena, tikuyenera kufotokoza momveka bwino MFUNDO ZOFUNIKAZI za uthenga wabwino ndi kuwapatsa mwayi woyankha ndi chikhulupiriro mwa Yesu ngati njira yokhayo ya kumoyo wosatha. Tiyenera kutsatira chitsanzo cha Paulo, amene adapempha pemphero kuti akhale ndi mwayi wogawa uthenga wa bwino ndi kuti alalikire nawo. (Werengani Aefenso 6:19-20); Akolose 4:3-4)!!!

�23

Ndiye, kodi wina angamvetse ndi kuchita chiyani kuti akhale mkhristu ndi kukhala ndi moyo wosatha? Izi ndi mfundo zosavuta ndi zomveka bwino za uthenga wathu:!!

1. Mulungu amakonda anthu ndipo amafuna aliyense kuti apulumutsidwe ku machismo ake ndi kukhala ndi moyo wosatha. (Yohane 3:16; 1 Timoteyo 2:4)!!

2. Munthu aliyense adachimwa pamaso pa Mulungu. (Aroma 3:23)!!3. Machismo athu amatisiyanitsa ndi Mulungu komanso amaapangitsa imfa yauzimu, yaythupi

ndi imfa yosatha. (Aroma 6:23)!!4. Yesu Khristu ndi yekhayo mwana wa Mulungu wosachimwa amene adalipira chilango cha

machismo athu. (Aroma 5:8; 2 Akorinto 5:21)!!5. Yesu Khristu ndiye njira yokhayo yakukhakhala ndi ubale watsopano ndi Mulungu –

palibenso njira ina. (Yohane 14:6) Sitinapulumutsidwe ndi ntchito zothu zabwino kapena za chipembezo kapena zomwe timadziwa monga ubatizo kulowa mumpingo, kulandira mphatso za uzimu ndi zina.!!

6. Anthu akuyenera kulandira mphatso yachisomo yaulere yachipulumutso mwa chikhulupiriro kukhulupirira mwa Yesu Khristu yekha kuti akhululukire machismo awo ndi kuwapatsa mopyo wosatha. (Yohane 1:12, 3:16; Aroma 10:9-10; Aefeso 2:8-9)!!!!

FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi m’chikhalidwe chanu ndi chiyani chomwe anthu amaganiza kuti !! angachite kuti akhale ndi ubale wabwino ndi Mulungu? Kodi uthenga wabwino umasiyana !! bwanji ndi zomwe anthu amaganiza?!!!!Strategic Impact yapanga chipangizo cholalikira kuti chikuthandizeni pogawa uthenga wabwino mosavuta ndikupatsa ena mwayi woika chikhulupiriro chawo mwa Yesu Khristu. Pamodzi, werenganimalangizo pa masamba otsatirawa pa momwe mungagwiritsire ntchito chipangizochi.!!!!!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi ndani amene mukufuna kugawana naye chipangizo cha SI !! m’sabatayi?!!!!!!PHUNZIRO LALIKULU: TIKUYENERA KUPANGA UTHENGA WABWINO WOMVEKA BWINO KWA !! ANTHU AMBIRI NGATI N’KOTHEKA NDI KUWAPATSA MWAYI WOIKA CHIKHULUPIRIRO !! CHAWO MWA YESU KHRISTU YESU KUTI APEZE MOYO WOSATHA.!!!

�24

TINGAGWIRITSE BWANJI CHIDA CHOLALIKIRA CHA STRATEGIC IMPACT!!

� !!

� !1. Gawani umboni wanu wa: !

• Kodi moyo wanu udali bwanji musanakhulupirire Yesu, !

• Kodi mudatani poika chikhulupiriro chanu mwa Yesu ngati mpulumutsi wanu,!

• Kodi moyo wanu udasiyana bwanji mdi wakale pamene/mutatha mudakhulupirira mea Yesu pa chipulumutso. ! !

Awonetseni mbali ya patsogolo ya chipangizocho. !

Nenani: “Ndingakufunseni mafunso ochepa pa za chomwe mumakhulupirira ndi kukuonetsani kuchokera m’baibulo momwe mungazitsimikizir kuti muli ndi moyo wosatha?”!

2. Aonetseni chithunzi cha ngodya zitatu kuti, chikuimirira Mulungu. Afunseni , “Kodi mukukhulupirira kuti iye amakukondani?” Dikirani kuti munthuyo akuyankheni. Mafunso awa achititsa kuti muzikambirana osati kumangoyankhula nokha pa iwo.!!

3. Ndi kofunika kuwerenga ndimeyo kuchokera m’baibulo motsatana ndi chithunzi chirichonse. Yamabani ndi Yohane 3:16. (1)!

• Funsani ngati munthuyo ali ndi Baibulo. Ngati alinalo, awuzeni alitenge ndi kuwathandiza kuyang’ana ndimezi m’baiibulomo.!

• Zingakhale bwino ngati munthuyu awerenge ndimezo. Komabe, muwazindikire ngati sangathe kuwerenga. Ngati azengereze kapena kunena kenakake monga: “ndilibe magalasi,” pamenepo awerengereni.!!

4. Awonetseni chithunzi cha munthu chomwe chilli m’munsi pa gawo loyambalo. Afunse, “Kodi chinthunzichi mukugaaniza kuti chikuimira chiyani?” Atha kunena kuti ‘‘anthu’’ kapena ‘‘satana’’ kapena munthu wina wake. Auzeni kuti chithunzichi chikuimirira wina aliyense pa dziko lapansi; inu, ine ndi aliyense. Lozani chipata chaduda chimene chikuonetsa kuti anthu alekanitsidwa ndi Mulungu. Werengani Aroma 3:23 (2) ndi kufunsa, “Baibulo limati ife tidalekanitsidwa ndi Mulungu chifukwa aliyense wa ife adachimwa. Kodi mukhulupira kuti mudachimwira Mulungu?”!!

5. Werengani Aroma 6:23 (3) Werengani Aroma 6:23 (3) mkati mwa chimpata chakuda chomwe chikuonetsa anthu olekanitsidwa ndi Mulungu. Afunseni kuti, “kodi mumakhulupirira kuti machisomo anu amabweretsa imfa kulekana ndi Mulungu kwa muyaya?”!

�25

� !!!!!

� !!

6. Pitani pagawo lotsatira lomwe likuonetsa mtanda. Werengani Aroma 5:8 (4) ndi kunena kuti, “Mulungu amatikonda ndipo adapereka njira kwa ife kuti timziwe iye potumiza mwana wake, Yesu Khristu kuti afe pamtanda polipira machismo athu. Kodi mukhulupirira kuti Yesu adafera pa mtanda chifukwa cha inu?”!!

7. Werengani Yohane 14:6 (5) ndi kunfunsa kuti, “kodi mukukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi njira yokhayo yopezera moyo wosatha mwa Mulungu?”!!

8. Werengani 1 Akorinto 15:3-8 (6) ndi kunfunsa kuti, “kodi mukukhulupirira kuti Mulungu adamuukitsa Yesu kwa akufa?”!!!

9. Pitani pa gawo lotsatira lomwe likuonetsa chithunzi cha mphatso ndi kunenea kuti, “Mulungu akufuna inu kuti mukhale ndi moyo wosatha komanso iye amapereka moyo wosatha ngati mphatso yaulere.” Kenaka werengani Aefeso 2:8-9 (7) nenani, “Ngati mukukhulupirira pa dzina la Yesu, Mulungu akupangani kukhala mwana wa Mulungu” Kenaka werengani Yohane 1:12 (8). !!!

10.“Mulungu akanena izi kwa iwo amene akukana mphatso yake:” werengani (2 Atesalonika 1:8-10) (9). Koma ngati muvomereza kuti mudakhala ndi moyo wosatha ndi iye (1 Yohane 5:11-12) (10). !!

11. FUNSANI: “Kodi mukufun akulandira mphatso ya moyo wosatha mwa chikhulupiliro mwa Yesu Kristu lero?” !!

12.Ngati ayankhe kuti “Inde,” werengani Aroma10:9-10 (11). mutha kulandira Khristu mwa kukhulupirira mumtima mwanu ndi kuvomereza ndi pakamwa panu. Pemphero silingakupulumutseni. Ndi chikhulupiriro chanu mwa Yesu Khristu chomwe chingakupulumutseni.Mawu a pemphero atha kukuthandizani kufotokoza chikhulupiriro chanu. Apa pa pemphero losavuta: “Ambuye Yesu, ndikusowani, ndikumvomereza kuti ndakuchimwirani, chonde khululukirani machimo anga, ndikulandira mphatso yanu ya chikhululukiro cha machimo ndi moyo wosatha lero mwa Chikhulupiriro . M’dzina la Yesu, Amen.”!!

�26

!!!!

� !

!!!!!13.Atatha wina kulandira mphatso yaulere ya

Mulungu ya moyo wosatha mwa chikhulupiriro, mfunseni, “Kodi mudakhulupirira mwa Khristu kuti atikhululukireni ndi kukupatsani moyo wosatha?” Kenaka alimbikitseni m’chikhulupiriro ndi kuwapempherera.!!!!

14.Ng’ambani gawo lotsiriza la chipangizocho. Lembani dzina keyala ndi foni zawo m’malo oyenenera. !!!!

15.Ngati nkotheka khazikitsani nthawi yokomana nawo mawa kuti mnyambe kuwaphunzitsa pogwiritsa ntchito chipangizo cha Strategic Impact.!!!!

16.Perekani dzina, keyala kapenanso foni nambala za munthu yemwe walandira kumene Yesu Khristu kwa Mtsogoleri wa Seko ya mpingo imene idabzalidwa.!!!!

!!!!!!!!!!!!!!!!!!�27

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Yambani kubweza ndime (Mavesi) a chipangizo cholalikira cha Strategic Impact kuti !! mudzathe kugawana ndi aliyense nthawi iliyonse.!!!!!!!!!� Tsiku 2: Yambani kupemphera tsiku ndi tsiku komanso ngati gulu kuti Mulungu akupatseni !! mwayi wogawana uthenga wabwino ndi ena.!!!!!!!!!!!� Tsiku 3: Ziperekeni pakugawa uthenga wabwino. Pangani nthawi ndi iwo kuwaonetsa momwe !! angagwiritsire ntchito ntchito chipangizo cha strategic Impact cholalikira.!!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Kodi ndi Mkhristu uti amene mungamphunzitse kugawa uthenga wabwino. Pangani !! nthawi ndi iwo kuwaonetsa momwe angagwiritsire ntchito chipangizo cha Strategic Impact.!!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�28

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 5 - “UMBUYE WA KHRISTU”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Yesu adayambapo wafunsa ophunzira ake - ndi aliyense wa ife. Mafunso awiri ofunika kwambiri kuti aliyense wa ife aliyankhe m’moyo uno mafunsowa akupezeka pa Marko 8:27-38 (Chonde werengani limodzi). !!!Funso loyamba ndiloti kodi kwenikweni Yesu ndi ndani. Pamene Yesu ankatumikira pa dziko lapansi pamene Yesu adali wotchuka, magulu a anthu adali angati ndi maganizo osiyanasiyana okhudza iye. Amayerekeza kuti iye adali mwina Yohane m’batizi, kapena Eliya kapena m’modzi wa aneneri ena. Koma Yesu akufunsa ophunzira ake (ndi inu ndi ine) “koma inu muti ndine yani?” !(ndine 29). Tsogolo lanu lamuyaya ndi moyo wanu padziko udalira momwe muyakhira funsoli. Aliyense kuti pali china chake chapaderadera mwa Yesu. Anthu ena amaganiza kuti mwina iye ndi mpunzitsi wamkulu wa chipembezo kapena munthu wa chitsanzo chabwino. Koma yankho lokhalo lovomerezeka pa funsoli ndi lomwe Petro adayankha. “Ndinu Khristu mwana wa Mulungu wa moyo!” Kuvomereza kwa kwa Petro kukutsimikizira kuti Yesu waposa pogokhala munthu chabe. Iye ndi wapaderadera ndi yekhayo Messiya, mwana wa Mulungu wosatha yemwe adakhala munthu ndi kufa chifukwa cha machismo athu. Iye ndi Ambuye wouka kwa akufa amene tsiku lina adzabweratso ku dziko lapansi kuzaweruza munthu aliyense ndi kulamulira kuti ife timakhulupirire kuti Yesu ndi ndani. !!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi mudazindikira liti kuti Yesu waposa mphunzitsi wabwino wa !! chipembezo? Kodi ndi yankho lanji lomwe anthu a m’mudzi wanu kapena adera lanu !! angapereke ku funsoli, “Kodi mukuganiza kuti Yesu Khristu ndi ndani?”  !!!!!Funso lachiwiri lofunika kwambiri m’moyo likuperekedwa m’chiphunzitso chimene Yesu adapereka atangitha Petro kuvomereza. Yesu adalosera masautso ake, kukanidwa , imfa ndi kuuuka kwake. Atatha kumdzudzula Petro pokana choonadi, adapereka malangizo awa kwa aliyense yemwe amamvetsera iye:!!

“Ngati munthu afuna kudza pambuyo panga, adzikaniza yekha nanyamula mtanda wache, nanditsata ine. Pakuti yense wakufuna kupulumutsa moyo wake adzautaya, ndipo yense wakuwutaya moyo wake chifukwa cha ine adzaupulumutsa. Pakuti munthu apindulanji akadzilemezera dziko lonse natayapo moyo wake? Pakuti munthu adzapereka chiyani chosinthana nancho moyo wake? Pakuti yense wakutaya moyo wake chifukwa cha ine ndi cha mawu anga mu mbadwa uno wachigololo ndi wochimwa. Mwana wa munthu adzachitanso manyazi chifukwa cha iyeyu, pamene iye adzifika nawo angelo ache oyera mu ulemerero wa Atate wake.” (Marko 8:34-38, ESV).!!

�29

Funso la chiwiri lopambana yomwe tifunika kuyankha ndi yakuti “Kodi ndani, kapena ndi chiani chomwe ine ndiza khalila pano padziko lapansi?” Ifeyo tili ndi masankho  awiri chabe. Sankho loyamba niyakuti ifeyo tingasankhe umoyo odzikonda ndi ku pata zinthu zonse za padziko lapansi., kenaka tinga pereke umoyo wathu kwa Ambuye Yesu ndi ku utumiki wa mau ache.Munthu aliyense mwa ise akhoza usankha umoyo wo tumikila Mulungu kapena zinthu za padziko lapansi ndiponso za umoyo udzikonda..  !!Momwe mumayankhira funso lachiwiri lofunikali zili ndi zotsatire zazikulu. Ngakhale ndi chikhalidwe kuganiza kuti chinthu chabwino chomwe tingachite m’moyo ndi kukhalira pa zokhumba zathundi kupindula momwe tingathere, Yesu akuti mathero a chisankho cjhimenecho ndi kutaya moyo wathu. Tiyenera ndithu kupindula zambiri za ife eni m’moyo wosakhalitsa uno, koma tidzataya chomwe chilli chofunika kwambiri – chenicheni chauzimu. Ife taposa kungokhale nthupi losakhalitsa. Ndife uyamba komanso koposa zonse, amuyaya, miyoyo yauzimu yapangidwa mlengi wathu ndi cholinga chake.!!Ndiye, yankho labwino ku funso ili: “Kodi ndi ndani kapena chiyani chomwe mudzachikhalire moyo?” Ndi kukhalira moyo Yesu Khristu ndi uthenga wabwino wake. Pamene tikulimbikira kumtsatira iye ndi kukhala chifukwa cha uthenga wabwino wake, pamenepo tikuzikaniza tokha ndi kusenza mtanda tsiku ndi tsiku, pamenepo tidzapeza moyo uno, ndiponso tili ndi lonjezo lalikuru la mphoto pamene Yesu adzabwera. Mkulu wa mishoni uno, Jimu Elioti, yemwe adataya moyo wake wakufuna kutengera uthenga wabwino ku mtundu wa ma India m’nkhalango ya Ekuado adati, “Si wopusa yemwe amapereka chimene sangathe kuchisunga pa chomwe sangathe kuchitaya.” !!FUNSO LOKAMBIRANA: Chifukwa chiyani mukuganiza kuti ndi kuvuta kuzikana nokha chifukwa!! cha khristu ndi uthenga wabwino wake? Fotokozani momwe zingamaonekere kwa inu !! kunyamula mtanda weniweni ndi kutsata Yesu.!!!!Mafunso ofunika kwambiri pa moyo ndi awa: !!

1. Kodi Yesu Khristu ndi ndani?!!2. Kodi ndi ndani kapena chiyani chomwe ine ndidzachikhalire moyo?  !!!

Mayankho okhawo olondola kumafunsowa ndi awa:!!1. Yesu Khristu mwana wa Mulungu wosatha!!2. Iye ndi Ambuye yekhayo ndi mphulumutsi wa moyo wanga!!!!!!

PHUNZIRO LALIKULU: YESU KHRISTU NDI MWANA WA MULUNGU WOSATHA NDIPO !! KUKANIZA ZOKHUMBA ZANGA NDI KUMTSATA IYE NGATI AMBUYE ZOTSATIRA ZAKE !! NDI MOYO WABWINO.!!!!

�30

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Lowezani ndi kubwerezanso Marko 8:34-35 tsiku ndi tsiku m’sabatayi,!! Chongani m’bokosi pamene mwamaliza kupemphera tsiku lililonse!!� Lamulungu � Lolemba � Lachiwiri � Lachitatu � Lachinayi � Lachisanu � Loweruka!!!

� Tsiku 2: Funsani kwa anthu osachepera mmodzi (yemwe si wa m’banja lanu kapena mpingo !! wanu) m’sabatayi funso ili, “Kodi mumati Yesu Khristu ndi ndani?”!!!!!!!!!!� Tsiku 3: Lembani momwe mungafotokozere wina kuti Yesu Khristu wopaosa kungokhala !! mphunzitsi wabwino wa chipembezo:!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Fotokozani kodizikutanthauza chiyani kwa inu kuzikana nokha ndi kusenza mtanda !! wanu tsiku ndi tsiku ndi kunsata:!!!!!!!!!!� Tsiku 5: Werengani Marko 8:34-38 mosamala. Kodi mungawalimbikitse bwanji omwe asankha !! kukumsata iye ngati Ambuye wa miyoyo yawo ndi kufuna kugawa uthenga wake?!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�31

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 6 - “KUPEMPHERA PAMODZI”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

WERENGANI: Machitidwe 2:42, Akolose 4:2-4, Aroma 12:12, 1 Yohane 5:14-15, ndi Luka 10:2-3!!Pamene mudayamba kusintha kuganiza kuchoka pa kumanga ufumu wanu (nyumba zopemphereramo/ madongosolao / ndodndomeko ya momwe mungagwiritsire ndalama ndi zina ndi kuyamba kumanga ufumu wa Mulungu, mudzayambatso kuona kukula kwa ntchito yomwe tidayitanidwira ndi ntchito yaikulu: “Pitani ndi kupanga ophunzira a mitundu yonse,” (Mateyu 28:18-20, Machitidwe 1:8). Koma kupanga ophunzira ochuluka ndi ntchito Ya Mzimu Woyera (Yohane 6:65, 3:27). Ndipo Lamulo La ntchito yaikulu likukhudza dziko lonse lapansi. palibe njira ina yomwe ife patokha mwa umunthu wathu tingafikire gulu lililonse la anthu pa dziko lapansi.!!Yesu adati, Mphamvu “Mphamvu zones kumwamba ndi dziko lapansi dzapatsidwa kwa ine.” Adatinso, ‘‘koma mudzalandira mphamvu pamene Mzimu woyera atadza pa inu.’’ Komanso “Ndidzakhala nanu nthawi zonse, mpaka chimaliziro.” Ngati Mulungu watipatsa zonse zomwe tizifuna kuti tikwanitse lamulo lake – ngati tipempha mwachikhulupiriro! 1 Yohane 5:14-15, malemba akutiuza ife, “Ndipo ichi ndi chilimbiko chimene tili nacho mwa iye, kuti ngati tidzapempha chilli chonse monga tidziwa kuti atimvera chilli chonse monga mwa chifuniro chake, atimvera. Ndipo ngati tidziwa kuti atimvera chilli chonse tichipempha, tidziwa kuti tili nazo izi tizipempha kwa iye.” Ndikufunseni: Kodi kukwaniritsa ntchito yaikulu ziri mchimene Mulumgu akuchifuna? INDE! INDE! INDE!!!! Kodi Yesu ali ndi Mphamvu pa kukwaniritsa ntchito yaikulu? INDE! INDE! INDE!!!! Kodi adzakwaniritsa bwanji? Kuzera mu mphavu pa kukwaniritsa ntchito yake yomwe ikugwiridwa mwa inu komanso kuzera mwa INU!!!FUNSO LOKAMBIRANA: N’chifukwa chiyani nthawi zonse timaadalira kuthekera kwathu, mphatso ndi !! luso lathu pogwira ntchito yomwe Mulungu adatiitanira?!!!Pemphero, tsono, ndiye chida chathu champhvu. Pemphero limaonetsa kizichepetsa kwathu pakudalira mphamvu ya Mulungu. Pemphero limaonetsa kuzichepetsa kwathu pakudalira mphamvu ya Mulungu. Pemphero limaonetsa kudalira kwathu pa ulemerero wake ndi mphamvu yake pa kukwaniritsa zokhumba zake. Kudzera m’pemphero, timafitikoza kuthokoza kwathu pa ntchito yomwe khristu adaimaliza pa mtanda, zoyenera zake ndi ntchito yake m’miyoyo yathu, komanso timapeza njira yomwe tingalemekezereee pa kupanga ophunzira ochulukitsa ndi kuphunzitsa okhulupirira atsopano kukula mwa khristu.!!Mbali iliyonse ya utumiki wathu ndi miyoyo yathu zikuyenera kuchitika mwa pemphero. Taperekeka ku pemphero, koma ichi sichitanthauza kuti pemphero ndiye zonse zomwe tingachite sitikuLIchimbika mtima kuti iye adzatsogolera ntchito zathu.!!

�32

FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi nchito zanji zomwe mukuzimva kuti mukufunika kuzipatsa yambiri !! yozipempherera?!!!Limodzi mwa mapemphero ofunika kwambiri kupemphera pamodzi ndi kupempherera “antchito otuta.” M’buku la Luka 10:2-3, Yesu akuudza ophunzira ake, “Dzinthu zichuluka, koma antchito achepa, potero pemphani mwini dzinthu, kuti akankhe antchito kukututa kwake. Makani, taonani, ine ndifuna inu ngati ana ankhosa pakati pa mimbulu.” Amaudza omtsatira iye kuti apemphe antchito ambiri, komanso kuti akuwafuna iwo TSOPANO! Timapempha antchito, koma sitimadikira kuti afike tisanapite ku kholola. Makamaka, kuti Ntchito yayikulu ikwaniritsidwe, antchito okakolola adzachokera m’khololalo! . lingalirani ichi kwa kamphindi. Anchito ambiri omwe adzatenge nawo mbali yokwaniritsa ntchito yayikulu sanamkhulupirire Yesu pa chipulumutso chawo! Choncho, tikapempha Ambuye kuti apereka antchito, tikupempha kuti ophunzira ochulukitsa apangidwe! LIMODZI ngati gulu, TAYENERA KUPEMPHA! Tikuyenera kupeza chitsogozo kuchokera kwa Atate! Tikuyenera kugwira ntchito Mphamvu yake, osati yathu. TIKUYENERA KUDZIPEREKA KU KUPEMPHERA LIMODZI! Membala aliyense m’banja la Strategic Impact adakhazikitsa kupemphelera antchito ku kukolora. (10:02) mmawa tsiku ndi tsiku kuti azitikumbutsa kupemphelera antchito ku kukolora (10:02 m’mawa ikutanthauza Luka 10:2)!!FUNSO LOKAMBIRANA: Imani tsopano kuti aliyense atchere nthawi yake kapena foni yake alamu pa !! 10:02 m’mawa. Pemphererani antchito panthawiyi kukukolora.!!!!Yesu ali ndi mphamvu kumwamba ndi pa dziko lapansi. Iye adalonjeza kukhala nafe mpaka ku mathero. Tapatsidwa mphamvu ndi yokwaniritsa ntchito yayikulu. Pemphani Ambuye wa kholola kuti afune antchito ku kukolola! Zoona, ndi Mulungu zinthu zonse ndi zotheka. (Mateyu 19:26)!!!!PHUNZIRO LALIKULU: PEMPHERO LAYENERA KUMANGA UTUMIKI WATHU OPAANGA !! OPHUNZIRA OCHULUKITSA ENA.! !!!!!!!!!!!!!!!

�33

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: M’sabatayi, pempherani tsiku ndi tsiku kuti Ambuye apereke antchito pa nthawi ya !! 10:02 mmawa. Chongani m’bokosi pamene mwamaliza kupemphera tsiku lililonse.!!� Lamulungu � Lolemba � Lachiwiri � Lachitatu � Lachinayi � Lachisanu � Loweruka!!!

� Tsiku 2: Konzani nthawi sabata liliyonse kuti gulu lanu lidzisonkhana ndi kupemphera !! PAMODZI kuti ufumu wa Mulungu upitepa tsogolo.‘‘ antchito akolola,’’ kuti Ntchito yaikulu !! ikwaniritsidwe, mwayi wolalikira uthenga wabwino, kupempherera anthu otaika powatchula !! maina, kupempherera ntchito yomwe ikubwera ya kulalikira kwa mpingo. !!! Dera: _____________________ Tsiku pa Sabata: _____________ Nthawi:_________!!!!!� Tsiku 3: Khazikitsani nthawi yochitira mapemphero angapo omwe achitidwe ndi gulu lanu. !! Yenderani dera lokuzungulirani komwe mukubzala mpingo ndi kupemphera kuti Ambuye !! atsegule mitima ya anthu ndi kupemphereranso zosowa za deralo. !!! Dera: _____________________ Tsiku: _______________ Nthawi:_________!!! Dera: _____________________ Tsiku: _______________ Nthawi:_________!!! Dera: _____________________ Tsiku: _______________ Nthawi:_________!!! Dera: _____________________ Tsiku: _______________ Nthawi:_________!!!� Tsiku 4: Kodi ndi njira zina ziti zomwe mungawatsogolere anthu anu kukhala anthu a !! pemphero?!!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�34

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 7 - “MUNTHU WA MAWU A MULUNGU”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Madziko a moyo wa chikhristu chopambana ndi utumiki wopambana ndi kudziwa ndi kumvera Baibulo. Mulungu adatipatsa mawu ake “kuti munthu wa Mulungu akhale woyenera, wokonzeka kuchita ntchito ili yonse yabwino” (2 Timoteyo 3:16-17). Sitingakule m’chikhulupiriro ndi kutumikira kwa ena pokhapokha titadzadza maganizo athu, mitima yathu ndi moyo wathu choonadi cha Baibulo. Ndiye, kodi tingakhale okonzeka bwino motani kuchokera m’baibulo? Baibulo limafotokoza njira zisanu ndi imodzi za momwe tingadzadzire kuganiza kwathu ndi moyo wathu ndi choonadi chake.!!Choyamba, tiyenera KUMVETSETSA malembo. Gulu lonse la Israeli lidamvetsera malembo pamene amawerengedwa (Yoswa 8:34-35). Paulo adauza Timoteo kuwerenga poyera kapena pagulu malembo (1 Timoteo 4:13). Tonse tikuyenera kumvetsera mawu a Mulungu. Kawirikawiri tidzimvetsera ena akumawerenga malembo. Sinthani powerenga Baibulo m’banja lanu.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi njira ziti zomwe mwapeza kukhala zothandiza powerenga !! malembo?!!!!Chachiwiri, tikuyenera kuwerenga Baibulo. Mfumu ili yonse ya Israeli imaudzidwa kulemba kope layokha la malembo kuti “idziwerenga masiku onse a moyo wake”, (Deutoronomo 17:18-19). Mpingo ukulamulidwa kuwerenga makalata a chipangano chatsopano (Akolose 4:16).Tikuyenera kuwerenga kosalekeza ndi mobwereza bwereza Baibulo lonse.Tikukulimbikitsani kuti mudziwerenga kawirikawiri machaputala osachepera 25 mpaka 30 a Baibulo sabata lililonse.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi phindu lanji lomwe mungapeze ngati inu kapena ena mumpingo !! wanu mukuwerenga machaputala 25 kapena 30 a Baibulo sabata lililonse (machaputala 3 !! mpaka 5 pa tsiku?). Kodi iyi ndi ntchito yovuta?!!!!Chachitatu, tikuyenera kuphunzira Baibulo.Ezara “adazipereka yekha ku kuphunzira ndi kudzukuta chilamulo cha Ambuye,” (Ezara 7:10). Munthu wa Mulungu akuyenera kudzukuta, kutanthauzira ndi kugwiritsa ntchito malembomosamala kuti amvetsetse chomwe akuphunzitsa, kuti tiphunzire kukhala mmoyo wolungama (2 Timoteo 3:16-17). Tikuyenera kawirikawiri ndi nthawi yodzipereka pakuphunzira malembo mwakhama.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi pali kusiyana kotani pakati pa kuwerenga Baibulo ndi kuphunzira !! Baibulo?! !!!!

�35

Chachinayi, tikuyenera kulowedza malembo. Mnyamata angayeretse mayandedwe ake posunga mawu a Mulungu mumtima mwake, (Masalimo 119:11). Yesu adasusana ndi mayesero aakulu a satana pogwiritsa ntchito mawu omwe adalankhulidwa kale omwe adawaloweza iye. (Mateyu 4:4-7, 10). Tikukulimbikitsaninso kuloweza ndime zosachepera imodzi pa sabata. Njira yomwe idayesedwa yochitira izi ndi kuwerenga mokweza ndimeyo kasanu ndi kawiri pa tsiku kwa masiku asanu ndi awiri.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Ziperekeni poloweza Yoswa 1:8 sabata ino. Werengani ndimeyi mokweza !! limodzi kasanu ndi kawiri tsopano!!!!!Chachisanu, tikuyenera kulingalira malembo.Ambuye adawuza Yoswa kulingalira mawu a Mulungu usana ndi usiku (Yoswa 1:8). Masalimo 1 imati moyo wobereka ndi wochuluka umadza pamene tikulingalira malembo.Kulingalira kumatanthauza kuganizira mosamala za tanthauzo la malembo ndi momwe tingawagwiritsire ntchito pa moyo wathu.Kulingalira ndi kuloweza zimayendera limodzi.!!Chachisanu n’chimodzi, tikuyenera kugwiritsa ntchito ndi kumvera Baibulo.Mulungu adatipatsa mawu ake kuti absinthe miyoyo yathu. Njira iliyonse m’mwambamu yaikidwa kwa ife kuti tiphunzire mosamala kukhala m’choonadi cha malembo (werenganinso ndime iliyonse kuti muone izi). Ngati sitikugwiritsa ntchito choonadi cha Baibulo, yakobo adati tikuzinyenga tokha. (Yakobo 1:22-25)!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi malembo ati omwe Mulungu akukutsimikizira kuwachita tsopano?!!!!!!!!Chithunzi chabwino chokuthandizani kukumbukira njira zisanu ndi ziwirizi ndi dzanja lanu.Chala chilichonse chikuimira njira zisanu zoyamba, pamene dzanja likuimira, kugwiritsa ndi kumvera Baibulo.Ngati tichita njira iliyonse mwa zisanu ndi chimodzi tidzakhala ogwira Baibulo zolimba.!!!!!!!!!!!!PHUNZIRO LALIKULU: MADZIKO A MOYO WA CHIKHRISTU NDI UTUMIKI NDI KUDZIWA NDI !! KUMVERA MALEMBO. TITHA KUKULA M’KUMVERA, POMVETSERA, KUWERENGA, !! KUPHUNZIRA KULOWEZA, KULINGALIRA NDI KUGWIRITSA NTCHITO MALEMBO.!

�36

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Ziperekeni pogwiritsa ntchito dzanja lanu tsiku lililonse kuti mukumbukire ndi kuloweza !! njira zisanu ndi imodzi za kagwiritsidwe ka Baibulo. !! Chongani m’bokosi pamene mwamaliza tsiku lililonse. !!� Lamulungu � Lolemba � Lachiwiri � Lachitatu � Lachinayi � Lachisanu � Loweruka!!!

� Tsiku 2: Mwa njira zisanu ndi imodzi izi zogwiritsira ntchito malembo, kodi ndi njira iti yomwe !! mukufunitsitsa mutaisintha?!!!!! Kodi mudzatani poisintha?!!!!!!!!!� Tsiku 3: Sankhani ndi kuchita njira imodzi momwe mungamachitire njira zisanu ndi imodzi za !! kumvetsetsa Baibulo.!!! ! Njira #1:!!!! ! Njira #2:!!!! ! Njira #3:!!!! ! Njira #4:!!!! ! Njira #5:!!!! ! Njira #6:!!!!!� Tsiku 4: Lowezani Yoswa 1:8.!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�37

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 8 - “KUPANGA OPHUNZIRA OCHULUKITSA ENA”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Ntchito yaikulu ya Khristu kwa ife ilipo mpaka iye adzabwere, ichi ndi chomveka bwino; “Pitani ndi kupanga ophunzira a mitundu yonse.” Mateyu 28:19. Kupanga ophunzira ndi lamulo lofunika tikuyenera kumvera ngati tikufuna kukwaniritsa ntchito ya Khristu.kulalikira kokha sikokwanira. lamulo la Khristu ndi kupanga ophunzira omwe adzahulukitsa ndi kupanga ophunzira ena. Pamene tikupanga ophunzira, zotsatira zake ndi mipingo.Titha kumaganiza kuti titha kubzala mipingo yatsopano ndi kuti tikhale ndi ophunzira omvera.Izi sizikhala choncho nthawi zones. Mipingo yambiri ili ndi Akhristu osachitachita komanso nthawi zina osamvera omwe samachita kanthu koma kungosonkhana ku mpingo. Komabe tikuyenera kuika maganizo anthu onse pa kupanga ophunzira ochulukitsa, kenaka mipingo idzakhazikitsidwa.!!Izi zimabweretsa funso lofunika kwambiri lomwe tikuyenera kuliyankha ngati tikufuna kumvera lamulo la Khristu. “kodi ophunzira wophunzitsika bwino amaoneka bwanji?’ chipangano chatsopano chimaonetsa magawo anayi a kukula pamene munthu akupanga ophunzira.!!!!Gawo loyamba ndi kumpanga munthu kukhulupirira Yesu.Wophunzira amayamba kukhulupirira Khristu (Werengani 1 Yohane 5:11; 1 Atesalonika 1:7-8). Timayamba kuwauza ena uthenga wabwino ndi kuwathandiza kuika chikhulupiriro chawo mwa Khristu. Mwachisoni, komabe, apa ndi pamene nthai zambiri timauza anthu kukika chikhulupiriro chawo mwa Khristu kenaka timawayitanira ku mpingo ndi kungochita nawo zochepa chabe. Timawapempha kuti akhale mamembala a mpingo, koma sitiwathandiza kukula m’chikhulupiliro chawo chatsopano. Mapeto ake amene anena poyera za chikhulupiriro chawo mwa Yesu samapitilira kukula. Okhulupilira atsopano amafuna chisamaliro ndi chithandizo kuti akule1 amakhala ngati ana mwa Khristu! (1 Akorinto 3; 1-2). Amafuna mkaka wauzimu ndi chithandizo chapadera.!!Udindo waukulu kwa wophunzitsa ndi kuyanjana nawo. Izi ndi zomwe Yesu adachita ndi omwe adaika chikhulupiliro chawo mwa iye. Iye amangokhala nawo. (Onani Yohane 1:35-42). Ifenso, tikuyenera kupita komwe okhulupilira atsopano ali ndi kukakhala nawo.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi pali kuopsa kotani kungomusogolera munthu kukhulupilira Yesu !! osamuthandiza kuti akule m’chikhulupiliro chake? Kambiranani ndi gulu lanu momwe !! mudalimbikitsidwira ndi wina pamene mudangokhulupilira kumene.!!!!Mugawo lachiwiri la kupanga ophunzira timamthandiza wokhulupilira watsopano kukhala wotsatira Khristu (Werengani Marko 1:17; Yohane 1:43; Akolose 2:6-7). Wotsatira Khristu amadziwa ndikumvetsetsa choonadi chofunikila m’chikhulupiliro chawo chatsopano mwa Khristu, zinthu monga chitsimikizo cha chipulumutso chawo, momwe angawerengere ndi kumvetsetsa Baibulo, angayanjane bwanji ndi Mzimu Woyera, kufunika kwa ubatizo ndi mpingo, angavomereze bwanji machismo, angapemphere bwanji. Ndikofunika kumachita nawo maphunziro a Baibulo, monga

�38

amene akupezeka kumbuyo kwa chipangizo cholalikirira cha SI ndi chipangizo chophunzitsira cha SI (Onani Ntchito 9). Ndi kofunika kwambiri kukhala nawo kuwaonetsa momwe angamachitire zomwe tikuwaphunzitsa.Izi zikuyenera kuchitika pa nthawi yoikika pamene mukukomana ngati gulu kudzaphunzira Baibulo komanso pa nthawi yosakhazikitsa yokhala nawo limodzi. Amayenera akuoneni momwe mumakhalira pa moyo wa chikhristu.!!Udindo wamkulu kwa wophunzitsa pa gawo ili ndi KUONETSERA iwo momwe angatsatire Khristu, (Werengani 1 Akorinto 11:1-2; 2 Timoteo 3: 10-12). Ophunzira a Yesu oyambilira adaphunzira pakumuonera iye. Adaphunzira kupemphera, kuchitira umboni kwa ena, kusamalira odwala ndi osowa, kusamala mawu a Mulungu. Ifenso tikuyenera kulangiza ndi kuonetsera otsatira Khristu momwe angakhalire moyo wa chikhristu ndi kutumikira Khristu.!!FUNSO LOKAMBIRANA: N’chifukwa chiyani ndi kofunika kuonetsa ena momwe angakhalire m’moyo !! wa chikhristu osati kungowauza kokha? Kodi ndi njira zina ziti zomwe mungachite !! powonetsera moyo wa chikhristu kwa ophunzira anu? !!!!Pamene okhulupirira akuphunzira kutsatira Yesu, amasuntha kupita pa gawo lachitatu la kupanga ophunzira. Wotsatira Khristu akuyenera kuphunzira kukhala wantchito wa Khristu, (Werengani Aefeso 4:12). Mulungu amafuna omtsatira ake adzitumikira mu ufumu wake. Yesu adati kwa ophunzira ake, “Munditsate ndipo ndidzakupangani kukhala asodza a anthu,” Marko 1:17.!!Wotsatira Khristu tanthauzo lake ndi msodzi wa anthu. Aefeso 4:12 imati oyera mtima aliyense ayenera kuphunzitsidwa kukagwira ntchito ya utumuki.Wokhulupilira aliyense akuyenera kuphunzira kukonda ndi kutumikira okhulupilira ena mu mpingo.Otsatira Khristu onse akuyenera kuphunzira momwe angagawire uthenga wabwino ndi kuthandiza Akhristu atsopano kuyamba moyo wawo watsopano mwa Khristu.tikuyenera kuwaphunzitsa ndi kuwaonetsera momwe angamagwiritsire zipangizo za SI zolalikirira ndi zophunzitsira.Ayitaneni kuti apite nanu ku utumiki/kotumikira.!!Udindo waukulu wa antchito pa gawo ili ndi KUDZIPEREKA.Yesu adapereka ntchito ya utumiki ndi mwayi kwa ophunzira ake pamene iye amawaonerera ndi kuwaphunzitsa, (Onani Mateyu 10; Luka 10).!!FUNSO LOKAMBIRANA: N’chifukwa ninji kuli kofunika kuti wotsatira khristu aliyense adzitenga nawo !! gawo pa kutumikira ena ndi kugawana chikhulupiriro chawo. Kodi pali kuopsa kotani ngati !! sachita izi?!!!! !Gawo lachinayi la kupanga ophunzira ndi kuthandiza watchito kukhala obereka mwa khristu (Mateyu 9:36-37; 28:18-20; Yohane 15:5, 16). Utumiki ochulutsa ndiye chimake cha chokhumba chathu.Osati mpaka omwe mwawaphunzitsa akuphunzitsa ena. Kodi kuphunzitsa kwa m’chipangano chatsopano kwachitika (Werengani 2 Timoteo 2:2) izi ndi zomwe yesu adachita kwa ophunzira ake. Asadabwerere kumwamba adapatsa mphamvu ophunzira kupita ndi kukapanga ophunzira ena (Mateyu 28:18-20).Cholinga chathu ndi kupanga okhwima ndi odalilika omwe adzapanganso amzawo.Mudzayenera kupitiliza kulimbikitsa ndi kuwathandiza, koma tsopano ndi oyenera pa ntchito yopanga ophunzira ena. Sitikuyenera kukhutitsidwa mpaka anthu omwe lidawapindula kukhulupirira mwaKhristu akupindula ndi kupanga ophunzira ena mdera lozungulira kwawo, kuphunzitsa ena ndi kuwathandiza kuyambitsa mipingo yatsopano ndi pokhapo pomwe tinganene kuti tapambana (Onani Machitidwe 6:1,7).!

�39

Udindo wanu waukulu ndi ochulutsa ena ndi KUCHULUTSA. N’chifukwa kulikofunika kwa inu kuti musangotenga nawo mbali musukulu yochulutsa odzala mipingo komanso phunzitsani ena kugwiritsa ntchito chipangizochi.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi ati omwe mukuwatsogolera kudutsa mgawo loyamba la sukulu !! yochulutsa obzala mipingo, kapena kodi ndi anthu ati omwe ali nako kuthekera kuti !! muwaphunzitse kuchulukitsa kudzera m’sukuluyi? Kodi mungatchule maina a omwe !! mudawaphunzitsa ndi tsopano akuphunzitsa ena? !!!!Mudongosolo la kupanga ophunzira tikupemphera ndi kugwira ntchito kuti tione OKHULUPILIRA akukhala OTSATIRA omwe adzakhale ANTCHITO omwe adzakhale OCHULUTSA ENA (Akolose 1:28-29). Chonde ganizirani, koma, kuti magawo onsewa akuchitika motsatana.Tisamaganize kuti zimachitika gawo lina litatha ayi. Wokhulupilira amayenera kutsatira ndi kutumikira ndi kuchulutsa zones nthawiimodzi. Pamene okhulupilira atsopano akukula m’chikhulupiliro, musakayikirezowalora kutumikila ndi kuchulutsa! Nthawi zambiri okhulupilira atsopano ndi omwe amachita bwino kwambiri popanga ena kukhulupilira mwa Khristu! Pamene dongosolo ili likubwerezedwa, padzakhala zochita zambiri zomwe zidzalowerere m’dera lonse, dziko lonse ndi chigawo chonse. Zotsatira ndimipingo ndiponso ntchito yaikulu idzakwaniritsidwa.!!!!!!PHUNZIRO LALIKULU: DONGOSOLO LOPANGA OPHUNZIRA SILIMATHERA PA KULALIKIRA. !! LIMAPITILIRA M’MAGAWO A OKHULUPIRIRA, OTSATIRA. ANTCHITO NDI !! WOCHULUKITSA.!!!!!ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Onaninso dongosolo la magawo anayi a kupanga ophunzira ochulukitsa. Kodi ndi !! gawo liti lomwe mwakhala mukulikana mu utumiki wanu?!!!!!!!!!!!!!!!!

�40

� Tsiku 2: lembani ndondomeko yanu ya momwe mungagwilitsire ntchito dongosolo ili mu !! utumiki wanu wopanga ophunzira.!!!!!!!!!!!! Khalani odziwa mwatsatanetsatane komanso kutha kugwiritsa ntchito chipangizo !! chophunzitsira cha SI (Onani Ntchito 9)!!!!!!!!!!� Tsiku 3: lembani maina a omwe mukuwaphunzitsa panopa. Kodi aliyense ali pa gawo liti? !! Kodi mukuyenera kutani kuti muwathandiza kupita pa gawo la pa tsogolo?!!! ! DZINA! ! GAWO! ! ! ZOMWE MUCHITE! ! ! !!!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Werengani ndi kuphunzira 2 Timoteo 2:2. Kodi ndi mibadwo ingati yomwe ikutchulidwa !! m’ndime imeneyi? Mungatchule maina a anthu mu utumiki wanu wopanga ophunzira omwe !! ali mum’badwo wachitatu? Musakhutitsidwe mpaka mutatha.!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�41

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 9 - “KUMVETSERA KWA MULUNGU”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Ngati mudzakhale zaka 100, sipadzapezeka tsiku limodzi la moyo wanu lomwe Mulungu sakufuna kukupatsani VUMBULUTSO LATSOPANO la pamtima pake kupita pa mtima wanu.!!! ! “Ambuye Yehova wandipatsa ine lilime la ophunzira, !! ! kuti ndidziwe kunena mawuakuchirikiza iye amene ali wolema. !! ! Iye andigalamutsa m’mawa ndi m’mawa, !! ! nagalamutsa khutu langa kuti limve monga ophunzira.” !! - Yesaya 50:4!!FUNSO LOKAMBIRANA: Mulungu akuyankhula tsiku ndi tsikula moyo wanu. Mukumumvetsera?!! Motani?!!!!Chikhalidwe cha Mulungu n’chamavumbulutso. Amafuna kuzivumbulutsa yekha za iye mwini kwa aliyense wa ana ake. Kulengedwa kwa dziko lapansi ndi vumbulutso la Mulungu kwa munthu. (Onani Aroma 1:20). Baibulo ndi VUMBULUTSO LAYEKHA la Mulungu kwa ife. Mulungu ndi munthu ndipo chifukwa cha ichi, iye amayankhula.!!Yesu adafanizira pa kuzivumbulutsa yekha kwa ife:!! ! “Nkhosa zanga zimamva mawu angan ndipo ndimazidziwa.” - Yohane 10.27!!!Moyo woyenera wa chikhristu ndi ubale woyenera m’mene kulumikizana kumakhala kukuchitika pakati pa anthu awiri okondana. Makamaka, zingakhale zosayenera kusalumikizana kwa mbali ziwiri mu ubale wabwino.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi zotchinga zanji zomwe zimakulepheretsani kumvetsera Mulungu !! nthawi zambiri?!!!!!Apa pali chotikumbutsa cha lonjezo labwino kuchokera kwa Yesu Khristu mwini:!! ! “Iye wakukhala nawo malamulo anga, ndi kuwasunga, iyeyo ndiye wandikonda ine; !! koma wandikonda ineadzakondedwa ndi atate anga, !! ndipo ine ndidzamkonda, ndipo ndidzadziwonetsa ndekha kwa iye.” - Yohane 14:21!!!KUMVERA KWATHU KWA MALAMULO A KHRISTU:!!

1. Kumaonetsera chikondi chathu pa Khristu; “Iye wakukhala nawo malamulo anga, ndi wakusunga, iyeyu ndiye wandikonda ine.”!!

2. Kumatithandiza kuona chikondi cha Atate; “Ndipo iye wondikonda ine adzakondedwanso ndi Atate wanga.”!

�42

3. Kumatsatira mkudziwonetsera yekha kozama kuchokera bpa mtima pa Khristu kupita ku mitima yathu; “Ndidzamkonda ndi KUDZIWONETSERA NDEKHA kwa iye.”!!

FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi udindo wa kumvera ndi wotani poyikira mtima pa kuthekera kwathu pa !! kumvera Mulungu?!!!!Kodi mukufuna Mulungu aziyankhula nanu kwambiri?! Mverani zomwe adakuwudzani kuti muchite, ndipo adzadzionetsera yekha kwa inu mochuluka.!!Mbaliyi ndiyovuta kuimvetsa: Mulungu wa mphamvu, amene ADAYANKHULA pa dziko lapansi ndi kupezeka, ANJALA ndi kudziwidwa. Amakhumba abale WOKONDANA ndi inu. Kukondana kumafana kulumikizana. Kulumikizana kumafana kuyankhula.!!Lingalirani za ichi: kodi ndi ubale wa mtundu wanji umene mungakhale nawo ndi mzanu wapamtima amene simunalumikizane naye? Sipangakhalenso ubale ayi!!!Nthawi zambiri, timafunsa Mulungu CHANI! “Kodi ndi CHANI chomwe mukufuna kuti ine ndichite?”!!Koma choonadi ndi ichi, nthawi zambiri, iye amafuna kuyankhula ndi ife za NDANI:!!! “Ndisungeni monga kamwana ka m’diso.” (Masalimo 17:8)!! “Ndiwe mwana wanga wokondedwa, mwa iye ndikondwera.” (Mateyu 3:17)!! “Pokhala iwe ndi wamtengo wapatali, pamaso panga, ndi wolemekezeka, ndipo !! ! ndakukonda iwe.” (Yesaya 43:4)!!! !

Mulungu akuyankhula nthawi zonse.!!Amafuna kunduonetsera yekha kwa inu.!!

Sipadakhale tsiku lomwe Mulungu sakuyankhula.!!Kodi mukumvetsera?!!!!

Khalani ndi nthawi tsopano yakumfunsa Mulungu funso limodzi: “Kodi mumaganiza chiyani za ine?”!!! Ndikukulonjezani adzayankhula nanu tsopano, ngati MUNGAMVETSERE kwa iye.!!!! Lonjezani kumvera kwanu kwa Mulungu kuti chilichonse chomwe iye angayankhule kwa inu, !! ! yankho lanu likhale “inde!”!!!!PHUNZIRO LALIKULU: TIKUYENERA KUMVETSERA MOSAMALA CHIMENE MULUNGU !! AKUYANKHULA KWA IFE, NDI KUMUYANKHA NTHAWI YOMWEYO.!!!!!!

�43

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Kumvetsera kwa Mulungu ndi kophweka – Iye akufunitsitsa kulumikizana ndi ife, koma !! ife timachitenga kukhala zosafunika ndi zovuta. Kodi zina mwa zovuta zomwe !! zimakulepheretsani kumvetsera kwa Mulungu nthawi zambiri? Kodi mudzathetsa bwanji !! zovutazo?!!!!!!!!!!� Tsiku 2: Khalani ndi nthawi tsopano khazikitsani bata mtima wanu ndi kumvetsera kwa !! Ambuye. Kodi mukumva chiyani chomwe Ambuye akuyankhula nanu?!!!!!!!!� Tsiku 3: Khalani ndi mphindi ziwiri kapena zitatu m’mawa uliwonse, yomvetsera kwa Ambuye, !! ngati nthawi yanu yokomana ndi Ambuye, Kodi Mulungu akulankhula chiyani?!!!!!!!!!� Tsiku 4: Pangani zolemba za pempero pa zolinga ziwiri:!!

1. Lembani mawu omwe Mulungu amalankhula nanu.!!2. Lembani maina a anthu a m’banja lanu:!!

! ! Mfunseni Ambuye momwe akufunira kuti mupempherere aliyense wa iwo payekha !! ! payekha. Mvetserani pempherani chilichonse chomwe Ambuye akuyankhula nanu.!!!! ! Lolani mzimu woyera apemphere mwa inu.Zoona awa ndi mapemphero !! ! otsogozedwa ndi mzimu woyera.!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�44

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 10 - “TINGAPHUNZITSE BWANJI ENA MWA NTCHITO”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Ngati gulu werengani chipangizo chophunzitsira chotsatirachi limodzi.Onetsetsani kuti mwadzidziwa mwa tsatanetsatane ndi zam’kati mwake ndi kumvetsetsa momwe mungagwiritsire ntchito.!!!

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!CHIPANGIZO: PANGANI OPHUNZIRA OCHULUKITSA!!!

Maitanidwe athu ngati otsatira Khristu ndi kupanga ophunzira ochulukitsa ena zimene zotsatira zake ndi kuchulukitsidwa kwa mipingo.!!Pamene mukugawa uthenga wabwino mokhulupilika kwa anthu, ena adzavomera ndi kukhulupirira mwa Yesu Khristu ngati mpulumutsi wawo.!!Ndi kofunika kwambiri kuwakhazikitsa okhulupirira atsopano m’chikhulupiliro chawo chatsopano.Ndikuwathandiza kuti akule ndi kukhwima ndi kukhala ochulukitsa ophunzira.!!Pofuna kuchita izi ndi kofunika kuwayendera komwe ali – m’makomo mwawo, ku malo awo antchito kapena kukhala nawo m’moyo wawo wa tsiku ndu tsiku. Yambani kuphunzitsa okhulupirira atsopanowo paokhapaokha kapena m’magulu a anthu atatu kapena asanu.!!Ngati m’kotheka muyendereni koyamba wokhulupirira watsopano asanathe maola 48 pamene aika chikhulupiriro chawo mwa Khristu.Osalora kuti pathe nthawi yaitali musanawayendere kuwakhazikitsa m’chikhulupiliro chawo chatsopano.Okhulipirira atsopano ayenera kumumvetsetsa Mulungu m’mawu ake.Ngati n’kotheka, yambani nawo ndi buku la Yohane la uthenga wabwino. Gwiritsani ntchito mawu otsogolera ndi mitu 4 pa kuwayendera kanayi kuchokera mu uthenga wabwino wa Yohane umene ukupezeka kumbuyo kwa chipangizo cholalikiracha SI. Mutatha kukomana nawo koyamba, pangani tsiku lomwe mudzakomananso nawo m’sabata imodzi yomweyo, ndipo kenaka pafupipafupi sabata iliyonse mpaka mutamaliza kukomana nawo kanayi.!!!!!!!!!!!!!

�45

Kufunika Koyendera Ndi Zipangizo Zophunzitsira!!Kodi mudzathandiza bwanji okhulupilira atsopano kukhala ophunzira ochulukitsa?Pali maphunziro a Baibulo abwino komanso ndondomeko zopangira ophunzira zomwe zikupezeka. Koma kuphunzitsa ena kumaposa kungophunzira Baibulo! Zotsatirazi ndi zipangizo zofunika kwambiri:!!

1. Baibulo: Gwiritsani ntchito mawu a Mulungu pophunzitsira okhulupilira atsopano. Ili ndi dongosolo la maphunziro lofunika kwambiri lomwe mungagwiritse ntchito! (2 Timoteo 3:16-17)!

2. Pemphero: Pemphererani ndi kupemphera nawo okhulupirira atsopano mokhulupirika. (Aefeso 1:15-23)!

3. Mzimu Woyera: Dalirani ndi kuwalimbikitsa okhulupilira atsopano kuti aphunzire kudalira pa mzimu woyera kuti awasinthe ndi kukhala m’chikhulupiliro cha Khristu. (2 Akorinto 3:17-18)!

4. Inu! Kukhuzidwa kwanu ndi kunyengetsa kwanu okhulupilira atsopano ndi kofunika kwambiri. Kupanga ophunzila ndi dongosolo la moyo pa moyo. Khalani ndi nthawi yambiri ndi a Khristu atsopano.Pezeranipo mwayi pa miyoyo yawo kupatula kungokhala ndi maphunziro a Baibulo.Atengeni pamene mukupita koyendera ena kapena kolalikira. Khalanawoni ngakhale pa nthawi yomwe simunaikonze.Idyani nawo pamodzi. Aloleni kuti “akuoneni” mukumtsatira Yesu mmoyo wanu wa tsiku ndi tsiku. (2 Timothy 3:10-11)!!!

Mutamaliza maulendo anayi oyambirira kuwayendera, apatseni mphatso ya chipangano chatsopano ya kumaliza maphunziro, ngati adali okhulupilika ndi inu komanso kuzipeleka. Kenaka afunseni kupitiliza kukumana nanu kwa maulendo 20 kuti muwathandize kukula ndi kukhala ochulukitsa ophunzira.!!Pamene mukukhala ndi ophunzira atsopano:!

• Athandizeni kuphunzira Baibulo ndi momwe angamtsatire Yesu. (kukula)!• Aonetseni momwe angauzira ena za Yesu. (Umboni)!• Alimbikitseni kuyamba kugwiritsa ntchito zipangizo izi pa kuphunzitsa amzawo ndi apabanja

pawo. (kuphunzitsa ena)!!!Chokhumba chanu sikungopanga ophunzira kukula mwa Yesu, koma ndi kupanga ophunzira ochuluka ena. Apa ndi pamtima pa ntchito yaikulu ndi kuitana kwa Mulungu pa moyo wanu.Ndi chinthu chofunika kwambiri chomwe mungachite pa kutumikira Khristu.!!M’musimu muli mitu yaikulu kuchokera m’mawu a Mulungu kwa inu pa kuthandiza ophunzira anu kumvetsetsa ndi kugwiritsa ntchito m’miyoyo yawo. Inde, pali zinthu zina zambiri zofunika pa Mkhristu, koma izi ndi maziko a moyo wokodweretsa Mulungu. Chonde komanani pafupipafupi sabata iliyonse ndi gwiritsani mawu a Mulungu pophunzira zinthu izi:!!Kodi ndi chiyani chomwe muchite pamene mukukomana?!!!!!!!!!

�46

PAMENE MUKUKOMANA TSATIRANI DONGOSOLO LA MAGAWO ASANU ILI!!1. YANJANITSA: Afunseni momwe akuchitira ndi kupeza zomwe zakhala zikuchitika mmiyoyo

yawo kuchokera pamene mudakomana.!!2. LIMBIKITSA: Yambani nthawi yanu mogwirizana poyankha mafunso olimbikitsa: !

A. Kodi mudakhala ndi nthawi nokha ndi Mulungu m’mawu ake ndi pemphero tsiku ndi tsiku kuchokera pamene tidakomana?!

B. Kodi mwayenda m’chikondi mu ubale wanu wabwino ndi ena m’baja lanu, komanso amzanu, oyandikana nawo ndi mpingo?!

C. Kodi mwatenga nawo mbali m’chizolowezi choipa?!D. Kodi mudamalizitsa zomwe mudapangana kuchokera m’maphunziro a Baibulo apitawa?

Motani?!!3. KAMBIRANA: Werengani ndi kukambirana ndime za m’Baibulo zogwiriza ndi phunziro la tsiku

limenero pogwiritsa ntchito ka funsidwe ka mafunso 6 m’musimu:!!! Pezani munthu winaawerenge ndime mokweza pamene ena akumvetsera kapena !! kuwerenga motsatira m’maBaibulo awo! !!! Funsani mafunso awiri oyambirira ndi kulola anthu akambirane:!

1. Kodi ndi chiyani chomwe mukufuna pa nkhani imeneyi?!2. Kodi ndi chiyani simudachikonde, kapena chakusokonezani m’nkhani imeneyi?!!!

! Patatha nthawi yokambirana, pezani wina kutiawerengenso nkhani mokweza ndipo kenaka !! kambiranani mafunso awiri otsatira:!

3. Kodi mwaphunzira chiyani za anthu m’nkhaniyi?!4. Kodi mwaphunzira chiyani za Mulungu?!!Patatha nthawi yokambirana, pezani wina awerenge nkhani mokweza kachitatu ndipo!kenaka kambiranani mafunso atatu otsiriza:!5. Malingana ndi nkhaniyi moyo wanu udzasintha bwanji m’sabatayi? (Dziwani: lembani

mayankho a anthu ndi kuwafunsa poyamba kukomana m’sabata ikubwerayo)!6. Kodi ndi ndani yemwe mudzamuwuza za Yesu m’sabatayi kapena ndi ndani yemwe

mudzaphunzitsa pogwiritsa chipangizochi? (atchule munthu ndi chifukwa chake ndi tsiku lomwe mudzamuuza iye, kawirinso, lembani dzina la yemwe aliyense wathula kuti akufuna kulankhula naye ndi kuwafunsa podzakomana sabata ikudzayi)!!!

4. KONZEKERA: Kambiranani za ndime ya malembo yomwe mudzawerenga m’sabata imeneyo. (Mitu itatu pa tsiku ndi yomwe yayerekezedwa).!!

5. PEMPHERA: Malizani nthawi yanu popempherera wina ndi mzake limodzi ndi zomwe mwagwirizana kuchita kuchokera mafunso 5 ndi 6.!!!!!!!

�47

Mitu Ndi Ndime Za M’Baibulo Zopangira Ophunzira!!MAZIKO - kumbuyo kwa chipangizo cha SI cholalikira ndi mafunso 6 komanso ndime zofunika kuchokera mu uthenga wabwino wa Yohane:!!

1. Dziwani Yesu? Yohane 1:1-18!!2. Mvetsetsani kubadwa kwanu kwa topano, Yohane 3:1-18!!3. Tsimikizani chipulumutso chanu, Yohane 10:27-30!!4. Khalani mwa Yesu, Yohane 15:1-11!!!

KUKULA - sonkhanani pafupifupi pa sabata kamodzi kudzakambirana nkhani ndi mitu imeneyi:!!5. Pemphero, Mateyu 6:5-15!!6. Vomerezani machismo anu, 1 Yohane 1:5-2:2!!7. Umboni wanu: auzeni ena momwe Yesu adakusinthirani, Machitidwe 26!

a. a.!Gwiritsani ntchito mfundo zitatu powathandiza kuganizira za umboni wawo:!i. Moyo wanga udali wotani ndisanamukhulupilire Yesu.!ii. Kodi ndinakomana bwanji ndi Yesu.!iii. Kusintha komwe Yesu adapanga m’moyo wanu kuchokera pomwe ndidaika

chikhulupiliro mwa iye.!b. a.!Aloleni kupeleka umboni wawo kwa wina musadakomane sabata ya mawa.!!

8. Kuchitira umboni: uzani ena za Yesu, Machitidwe 1:1-11 (2 Akorinto 5:16-21).!a. Aphunzitseni momwe angagwiritsirae chipangizo cha SI.!b. Pitani limodzi iwo kukauza wina za Yesu pogwiritsa ntchito chipangizocho.!c. Dziwani: ngati adamtsogolera wina kwa Khristu athandizeni momwe angagwiritsire bukuli

pophunzitsa okhulupilira atsopano!!!9. Yanjanani ndi ophunzira ena mu mpingo, Machitidwe 2:40-47 (Ahebri 10:19-25).!

a. a.! Itanani ophunzira wanu abwere kuselo yanu!b. Thandizanu ophunzira wanu kuzipereka pa kutenga. nawo mbali pa selo yatsopano.!!

10.Batizidwani, Machitidwe 8:26-38 (onaninso Mateyu 28:19; Machitidwe 2:40-41)!a. a.! Itanani okhulupilira watsopano kuto abatizidwe.!b. Muudzeni aitane abale ndi amzake (makamaka amene mwina sakumdziwa Yesu)

kudzachitira umboni kubatizidwa kwake.!!11. Mgonero, Luka 22:14-20!

a. Muitaneni okhulupilirs watsopano kudzachita nanu mgonero ndi ina.!!12.Kumvera, Yohane 14:15-21!

a. Afunseni zomwe akumva m’moyo wawo kuti Ambuye akuwafunsa kuchita.!!!!�48

13.Nthawi yokomana ndi mulungu, werengani ndi kuphunzira Baibulo. Masalmo 1 (Luka 5:15-16)!a. Udzani okhulupilira watsopano kukhala ndi nthawi tsiku ndi tsiku yowerenga Baibulo ndi

kupemphera.!!14.Khululukirani ena, Mateyu 18:21-35!

a. Afunseni ndi ndaniyemwe akuyenera kumkhululukira.!!15.Ziperekeni ku Umbuye wa Khristu, kuzipereka kwa Mulungu wopambana. Aroma 14:5-12.!!16.Cholinga cha Mulungu pa moyo wanu, Mateyu 28:18-20 (2 Akorinto 5:17-21)!!17.Kodi uthenga wabwino ndi chiyani? 1 Akorinto 15:1-8 !!18.Ukwati ndi banja, Aefeso 5:22-6:4.!!19.Yendani ndi mzimu woyera, Agalatia 5:16-26!!20.Kufanana ndi Khristu, Aroma 6!!21.Chikondi choyambirira, 1 Yohane 4:7-21!!22.Mphamvu ya mawu a Mulungu, 2 Timoteo 3:14-17!!23.Kasamalidwe ka moyo, Luka 19:10-27!!24.Nkhondo ya uzimu, Aefeso 6:10-18.!!!

Chulutzani Ophunzira Anu!!Pa nthawi yophunzitsa okhulupilira atsopano kuti akhwime ndi kuchulukitsa, athandizani: !

• Kukhala mbali imodzi ya mpingo watsopano!• Kuyamba kuchitira umboni ena!• Kuyamba kuphunzitsa okhulupilira ena atsopano amene awapindule mwa Khristu ndi

kuwaitanira ku selo yatsopano.!!Mukamaliza mitu 24, mudzapeza amuna ndi akazi okhulupilika anjala ndi Mulungu, omwe m’chikhulupilirochatsopano, komanso omwe akuwina anthu ena ndi kuphunzitsa ena. Ngati mupeza ophunzira okhulupirika, auzeni omwe ali ndi kuthekera kwakukulu kulowa msukulu yochulutsa abzala mipingo ndi kuwatengera dongosolo lomweli; kuphunzira ndi kukhala ntchito yaikulu!!!!Mutatha kuwerenga chipangizochi limodzi, gwiritsani ntchito mafunso 6 okambirana za Baibulo pokambirana Yohane 15:1-7 limodzi.!!!PHUNZIRO LALIKULU: KUMBUKIRANI, CHOLINGA CHANU CHACHIKULU NDI KUPANGA !! OPHUNZIRA OCHULUKITSA ENA OMWE ADZAYAMBITSE ZOCHITIKA ZA KUBZALA !! MIPINGO!!!

�49

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Werengani mafunso 6 okambirana za Baibulo kawiri ndipo onetsetsani kuti !! mwamvetsetsa mwatsatanetsatane momwe mungagwiritsire ntchito!!!!!!!!!!� Tsiku 2: Konzekerani Mafunso 7 okambirana za Baibulopogwiritsa ntchito ndime imodzi !! kuchokera m’Baibulo ndi munthu wina.!!!!!!!!!!� Tsiku 3: Pempherani ndi kulemba maina a omwe angakhale nanu kuyambira pa mutu wa !! Maziko kapena kukula limodzi.!!!!!!!!!� Tsiku 4: Aafunseni omwe mwawalemba kuyamba kukomana nanu pophunzira mituyo limodzi. !! Khazikitsani nthawi yoyambira.!!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!!

�50

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 11 - “PEMPHERANI!”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!

WERENGANI: Mateyu 6:5-15!!Pemphero ndi njira yachindunji yolumikizana ndi Mulung. Ngati okhulupilira,mwapatsidwa mphamvu,mwayindi lamulo lofika pamaso pa Mlengi wa zonse, wolamula wamkulu wa dziko lonse lapansi, mwini wa zachilengedwe zones. Pemphero ndi lofunika pamoyowanu ngati Mkhristu ndi utumiki monga wophunzira wochulukitsa. Potimmalembo mulimalangizo a momwe tingapempherere, pali njira yoyenerakomanso yosayenera pamomwe tingamfikire Mulungu m’pemphero. Yesu adatiuza mwachindunjimomwe tingapempherere. Pa Mateyu 6: 5-8anapereka enamwamalangizo papemphero, pa Mateyu 6:9-13. Anapereka chitsanzochapemphero, ndipopaMateyu 6:4-15 akuzindikiritsa choonadi pa momwemapemphero athu ayenera kukhala nacho.!!MALANGIZO TISANAPEMPHERE:!Mateyu 6 :5 -6akuti tisapemphere ngati‘‘onyenga ’’momwe amachitira. Simumapemphera ndi cholinga kuti mumvedwe ayi.Simumapemphera ndi cholinga kuti mumvedwe ayi. Simumapemphera kuti musangalatse ena ndi momwemungalankhulire mawuokongola.anthu ambiri akhala akulakwitsa pochita izinthawi zina,kumangodikilirampata basi wotitipemphere pa gulu kuti ena aziganiza kutindife auzimu. Pamene choona chake ndi choti mtima wathu wakhadzikika pa ulemelero wathu, tadzaonetsera kuti siife auzimu.!!Pitani malo anokha ndi kupemphera.Mulungu amakumvaningakhale muli malo a chinsinsi.kodiizi zikutanthauza kuti musadzapemphere pagulu? Kodi zingamatani?Pemphero lachitsanzo pa ndime 7 -13 linapempheredwa pamaso paomwe Yesu amawaphunzitsa.Pali zifukwa zambiri zopempherera pagulum’chipangano chatsopano chonse.Ayi, sitchimo kupempherapagulu, koma ndi tchimo kupempherangati onyenga- kupemphera kuti anthu atidziwe.Ngati simungapemphere pa gulu osagwa m’mayesero amenewo, ndiye muzipemphera pa inu nokha.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi tingaziyang’anire bwanji popewa kupemphera kuti tisangalatse ena?!!!Chachiwiri, tisamapemphere ngati momwe amachitira “Amitundu” kupemphera ndi mawu opanda kanthu.izi zikutanthauza kupemphera mumchitidwe wosachokera pansi pa mtima komanso osalumikizidwa.Nthawi zambiri timangoloweza pemphero ndi kepempheramwa chizolowezi; osaganizira tanthauzo kapena cholinga cha mawuwo.Mwachisoni pemphero lachitsanzo la Khristu lakhala pemphero la mtundu umenewu. Mawu ake akhala opanda tanthauzo kwa anthu angapo. Akhristu sakuyenera kumapemphera ngati nyimbo nthawi ndi nthawi,kuonjezera mawu kuti Mulungu amve. Ayi! Ndime 8 ikuti Mulungu amadziwa zomwe tifuna. Atate amadziwa kalezosowa zathutisanapemphere kwaiye! Mulungu ndi wopambana, ndiye pamene tikupemphera, sitimabweretsa uthengawatsopano kwa iye.!

�51

FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi tingapewe bwanji mapemphero obwerezabwereza opanda tanthauzo !! ndi a chizolowezi omwe Yesu adachenjezapo?!!!!Poti Mulungu amadziwiratu zosowa athu, n’chifukwa chiyani timapemphera? Pali zifukwa zingapo zomwe zimatipangitsa kupemphera: 1) Tachita kulamulidwa kutero- timachita pa chifukwa chomvera. 2) Limaonetsera zinthuzathuzopambana chifukwa choti timaonetsera nthawi pa kupemphera ndipo zinthuzomwe timapempherera zimaonetsera zinthu zopambana za pamtimawathu, chomwe ndi chofunik kwambiri kwa ife. 3) Limaonetsa kudalira- ngatitimpemphaMulungu, timatsimikiza kuti timamdalira Mulungu kwatunthu pazosowa zathu, chofunikaso kwambiri. 4) Limazamitsa ubalewathu ndi Mulungu. Ubwenzi wabwino umayamba chifukwa chokhalira limodzi. Kuchuluka kwa nthawi yomwe chokhalira limodzi. Kuchuluka kwa nthawi yomwe timalumikizana ndi Mulungundi pakuwerengamawu ake, mochulukanso timayandikira kwa iye. Ndipomwensotimamdziwa bwino. !!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi kupempherakwakuthandizani motanipokuza ubale wanu ndi Mulungu?!!!!!PEMPHERO LACHITSANZO:!Pa Mayetu 6 :7-13, Yesu akutipatsa chitsanzocha pemphero. Timapeza zofunikira zambiri pamomwe ndi chomwe Yesu amapempherera. Tiyeni tiyambe ndi momwe. CHOYAMBA, Amapemphera mwaubale, osatikwa milungu ina, komakwa Mlengi wachikondi, Atate! koma osati Atate wamba, koma Atate omwe ndi kumwamba. CHACHIWIRI, Amapemphera m’deralomwelo. Nthawi zonse amagwiritsa ntchitomawu aunyinji monga “athu,” “ife”. Amazipempherera yekha, komanso okhulupilira amnzake pa nthawi yomweyo.akulumikizidwanso ndi ana a Mulungu m’pemphero ili. CHACHITATU, adapemphera ZAZIKULU! Zinthu zomwe zikutchulidwam’pempheroli ndi zomwe zingachokere kwa Mulungu basi.!!Tsopano pa CHOMWE Yesu akupanga zopempha zisanu ndi chimodzim’pemphero lake. Zitatu ndi zounikira Mulungu(Dzina la Mulungu kuti liyeretsedwe, ufumu wa Mulungu kuti udze, chifunirochaMulungu kuti chichitike pa dziko lapansi) ndipo tsiku ndi tsiku, kukhululukira pamene takhululukira, chitetezo ndi kupulumutsidwa).Dziwani zopemphazounikira Mulungu ndi zoyambirira.!

• Kuyeretsedwakwa dzina la Mulungundi choyamba ndime 9.!• Chachiwiri ndi kukula kwa Ufumu wa Mulungu ndiyekuti,kukulakwaokhulupirira ndikukhala

mchifuniro cha Khristu ndi kutengerauthengawabwinokwa onseomwe sadamvepo, ndime 10a.!• Chachitatu,kutikufuna kwa Mulungu kuchitidwe m’dziko lochimwali monga kumwamba, kuti

Mulungu amveredwe ndi kuti zokhumba zake zichitidwe pano tsopano, monga momwe zimachitikira kumwamba, ndime 10b. !!!!!!

�52

KENAKA Yesu akupita ku zoyambirira zachiwiri: !• Kuperekedwa kwa zosowa za tsiku ndi tsiku, ndime11.!• Akupemphereranso chikhululukiro PAMENEtikukhululukira ena, ndime 12, ichi chikufotokozera

chidwi chakuyenda muumodzi. Khristu akutionetsakufuna chiyanjano chosasweka ndi Mulungu kuzera m’kulapa, komansozikutionetsera kufuna chiyanjanochosasweka ndi abale athu mwa Khristu.powakhululukira pamene atichimwira.!

• Chomaliza, Yesuakupempherera chitetezo ndi chipulumutso kumayesero ndi zoipa,kwa adani enieni komanso oopsa, ndime 13.!!

FUNSO LOKAMBIRANA: kodi tingagwiritse bwanji ntchito pemphero la chitsanzoli kutsogolera !! mapemohero athu osangoti kubwereza mawu opanda tanthauzo?!!!!Chinthu chomaliza ndi chofunika chomwe tingachione ndi choti yesu amapemphera. Samangochiyankhulaayi. samangopereka malangizo a momwe tingamapempherere. AMAPEMPHERA, AMAPEMPHERA NDITHU. Ndi chinyengo ngati Abusa ndi atsogoleri akulangiza ena kupemphera ndipo kenaka osakhala ndinthawi yopemphera patokha. Sitikuyenera kukhala achinyengo.sitikuyenera kumangokamba za pemphero. Tikuyenera kupemphera! ngati tikufuna kutsatira Yesu,pemphero ndi gawo lofunika m’tsiku lathu.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Gawanani ndi ena chomwe chidakuthandizani kukhala ndi moyo !! wapempheroosasinthikakomanso wotheka.!!!!!PHUNZIRO LALIKULU: TIKUYENERA KUPEMPHERA MOSASINTHASINTHA KOMANSO !! MOSASINTHASINTHA KOMANSOMOYEMBEKEZA KWA ATATE WATHUPOGWIRITSA !! NTCHITO MAWUOTSOGOLERA OMWE YESU ADATIPATSA.!!!ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Fufuzani momwe moyo wanu wa pemphero umakhalira. !!! Kodi mumapemphera kawirikawiri bwanji?!!!!!! Kodi mfundo zenizeni za mapemphero anu ndi chiyani?!!!!!!!!

�53

! Kodi ena mwa mawu anu siali opanda kanthu chifukwa chowayankhula kawirikawiri ? !!!!!!!!!� Tsiku 2: Ikani chidwi chanu papemphero m’sabatayi ya utumiki popemphera mamawa, masana !! ndi madzulo. Kodi mudzachita motani?!!!!!!!!!!!!!� Tsiku 3: M’mapemphero anu, pemphanizokhudz Mulungu ndizokhudza munthu.!! Pempherani ndi mzimuwanu. (1 Akorinto 14:15)!!!!!!!!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Pempherani tsiku ndi tsiku ‘‘antchito kukutita’’(Luka 10:2) komanso mwayi !! wogawachiyembekezo chauthenga wabwino ndikupanga ophunzira. Gulu la Strategic Impact !! lidakhazikitsaalamu ya wotchi kapena fonizawopa 10:02 m’mawa tsiku ndi !!! tsikukutiiziwakumbutsa kupempherera atchito kukakolola. Tcherani nthawi yanu tsopano !! kuti muzilumikizana ndi ife m’mapemphero.!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!!

�54

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 12 - “SANKHANI MALO OMWE MUTSEGULE SELO YATSOPANO”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!

Masomphenya a Yesukwa anthu ake ndi: 1) Kukuza okhulupilira kukhala okhwima ndi ochulukitsaophunzira, 2) Kupitilira kukula ndikufikiramaderaomwe sadamvepo uthenga wabwino (Machitidwe 1: 8; 8:1; 11:19-21; Aroma 15 :20). Pamene Mulungu akutsogolera gulu lanu kukwaniritsa ntchito yaikulu , adzakupatsani gulu la ophunzira lomwe lingakuthandizeni kutengera uthenga wabwino kumadera atsopano ndi kubzala mipingo yatsopano.!!Ndipofunika kwambiri kutsatira lamulo ili mu utumikiwanu. Mulungu samafuna anthu kupita ku Mpingo, mofanana ndi momwe amafunirakuti Mpingoupite kwa anthu. AmafunaMpingo wake kukhala pa cholinga, ndipo zikutanthauza kuti kukhala wokhulupirika pamene muli komanso kukhala pa ulendo wokafikira maderaatsopano ndi magulu a anthu atsopano ndi uthenga wabwino.!!Kusankha malo osiyanasiyana kukabzala Mipingo yatsopano zimayambandi pemphero. Popemphera mukuyenera kudziwa komwe Ambuye akukutsogolerani kukafikako.Zithakukhala deralomwe simukalidziwa.Litha kukhala dera lokuzungulirani komwe iye akukutsogolerani kuti mukafikeko.Utha kukhala mudzi kapeni tawuni yoyandikana nanu-ngakhaledziko lina komwe iye akufuna kuti mutengerekouthenga wabwino.!!Kukuza kwanu kusangokhala kosankha malo, koma chikhalidwe. Litha kukhala gulu a anthu lomwe Mulungu akukufulumizitsani kufikira- mtundu wa anthu wosiyana ndi inu, Chidwi chanu chofikira ena chitha kukhala pagululina lakelaanthu kapena gululinalake mumzindawanukapenadera monga ophunzira m’sukulu za ukachenjede, kapenamtundu wina wa anthu kapena anthu akunjaomwe akukhala mdera lanu. Posatengera momwe malo atsopano alili, mukayenera kukhala osamala pa MOMWE ndi KOMWE Mulungu akukutsogolerani.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi midzi yoyandikana nayo iti komwe sadamvepo uthenga wabwino?!! Kodi ndi gulu liti la anthu m’chigawo chanu anangomva popang’ono kapena alibe mwayi !! womva uthenga wabwino? Lembani maina m’magulu awa: !!!!!Ndiye, gawo loyamba la kudzindikira komwe Mulungu akufuna kuti mupiteko ndi kupemphera ndi kufunsa mzimu woyera kuti akutsogolereni.Izi ndi zomwe Paulo amachita pakuti amakhudzidwa ndi kutengera uthenga wabwino ku malo atsopano. (Werengani Machitidwe 16:6-11) Paulo ndi gulu lakeamaziperekapotengera uthenga wabwino ku chigawo chatsopano. Adayetsetsa kulowa mzigawo zachiroma, zaku Asiya ndi betinia komamalingaliro awo opambanawa Mzimuwa Mulunguadawaletsakupita ku malo amenewa.Pomaliza, Paulo adaona m’masomphenya munthu waku Makedomia akupempha chithandizo ndipo adazindikira kuti awaadali malo omwe Ambuye amafuna kuti apiteko. Iye ndi gulu lake adaona chofuna cha Mulungu ndi iye adawatsogolera ku Filipi komwe adakalandira ndi kuyamba Mpingo waku Filipi, umene udakhala Mpingo umodzi mwa Mipingo ya mphamvu komanso yomwe idathandiza utumiki wamtsogolo wa Paulo.!Timaphunzira mfundo zofunika kuchokera ku chochitika ichi chotitsogolera mwa pemphero kuzindikira komwe Ambuye akufuna kuti tifikireko.!

�55

Choyamba, tipeze njira yokuzira ndi kufikira ku dera latsopano. Paulo ndi gulu lake adali ndi chidwi pa kutengera uthenga wabwino ku malo atsopano ndi magulu a anthu atsopano.Anali achangu muzochita zawo. Adawatsogolera ku malo enieni kumene iye amafuna kuti iwo apite. Mipingo yambiri ndi yogona – sikutenga udindo wokuza ndi kufikira madera atsopano.!Mutha kuyembekeza kuti Ambuye akutsogolereni ku malo atsopano pamene mukuyambapo kufikira ena.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi tingachulutse motani cholinga cha Mipingo yathu m’kupititsa uthenga !! wabwino ku madera atsopano ndi magulu atsopano a anthu? !!!!!Chachiwiri, khalani tcheru ku kutsogodzedwa ndi mzimu woyera. Ngakhale sitikudziwa bwinobwino momwe Mzimu woyera adaletsera Paulo ndi gulu lake kupita ku Asiya ndi ku betinia, titha kutsimikiza kuti amuna awa amatchera khutu ku utsogoleri wa Mzimu woyera ndi komwe angapite. Kutanthauza kuti tikuyenera kupemphera ndi kumvetsera kwa Ambuye pamene tikufufuza komwe iye akufuna kuti tipite. Inu ndi gulu lanu mufunika kukhala ndi nthawi yopemphera kumfunsa Mulungu akutsogolereni. Khalani ndi nyengo zapadera za mapemphero kuti muchite izi:!!Chachitatu, pitani komwe kuli chosowa.Kodi ndi kuti komwe anthu thandizo lanu? Mkutheka pali gulu la anyhu lomwe limayenda mtunda wautali ndi kumapemphera ku Mpingo wanu ndipo mukuyenera kuyambitsa Mpingo watsopanokudera lawo. Kodi pali gulu la anthu kapena dera limene mukufulumizidwa mwapadera kulifikira? !!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi zosowa zazikulu ziti zakuthupi ndi uzimu mdera lanu?!! Kodi ndi pati pomwe zosowa zo zakula?!!!!!Chachinayi, fufuzani mavuto apa dera ndi zosowa za anthu a mderali (werengani Machitidwe 16:13-22). Kodi anthu kumeneko akumasonkhana pa zifukwa zauzimu?Kodi kuli ‘‘mwamuna’’ kapena mkazi wa mtendere,’’monga Lidiya, amene angakhale munthu wofunika pa ntchito yatsopanoyi.kodi kuli khomo kapena malo opembezera omwe mungadzayambepo konsonkhana?Kodi kuli zolimba kapena zovuta za uzimu zomwe mungadzayambepo kusonkhana?Kodi kuli zolimba kapena zovuta za uzimu zomwe mungakumane nazo ndi kuzithetsa? Yambani kuchita ubale ndi kufunsa anthu zosowa kapena kuzitsegula kwa uzimu pakati pawo. ( onani m’munsimu).!!!Chomaliza, khazikitsani tsiku ndi kukhadzikitsa ntchito, pitani! Ndi kuyembekeza Mulungu! !!Apa pali zochita za gulu lanu ndi inu kuti muziganizire pamene mukusankha malo a Mpingo watsopano:!!

1.Bzalani selo ya Mpingo watsopano komwe kulibe Mipingo (kapena kuli yochepa). Ngakhale kulibe Mipingo wanu kapena gulu m’dera lomwe mukuliganizira, kutha kukhala Mipingo ina ya Chikristu. Pitani komwe kuli chosowa cha uthenga wabwino!!!!

�56

2.Ganizirani kuyamba Mpingo watsopano komwe anthu ochokera mumpingo wanu kapena gulu lanu akukhala, kugwira ntchito kapena kukhala ndi abale. Nkutheka wina akuyenda ulendo wautali kupita ku “Mpingo wanu” ndipo pali chosowa cha pingo watsopano pafupi pawo. Nkutheka wina ali mgulu la anthu amene akusowa Mpingo. Funsani kodi ndani yemwe akusowa kukhala ndi Mpingo pafupi ndi iwo?!!

3.Fufuzani “ Anthu a mtendere” komwe mukufuna kukayamba Mpingo watsopano (Luka 10: 5-7). Munthu wa mtendere ndi munthu wochereza ndi kukalandireni komanso ali ndi kuthekera mderalo kolumikizana ndi ena. (onani zitsanzo za mzimayi waku Samariya pa Yohane 4, Koneliya pa Machitidwe 10, ndi Lidia pa Machitidwe 16:11-15).!!

4.Yendani ndi mapemphero mderalo. Anthu a mgulu lanu kapena mpingo atha kuyenda m’dera lozungulira kapena tawuni ndi kuona zomwe zikuchitika. Imani ndi kupemphera zomwe mwaziona.Pempherani anthu omwe mwawaona.Tsekerani deralo komanso anthu amderali ndi mpemphero. !!

5.Osaganiza kuti mukuyenera kukhala ndi nyumba yopemphereramo kuti mukhale ndi Mpingo wabwino. Yang’anirani khomo kapena dera komwe Mpingo watsopano uyambe kukomana. Apangeni kukhala malo odziwika bwino komanso anthu athe kuwapeza mosavuta. Mutha kufuna kuyamba ndi maselo m’makomo kapena m’madera amderalo musanayambe kuwabweretsa onse pamodzi (ngati mwina mukufuna kuchita izi). Kumbukirani, Mpingo si nyumba yomangidwa kapena yooneka ndi maso. Mpingo ndi thupi la Khristu ,lokhala ndi okhulupilira… ndiye kuti, Mpingo ndi anthu! Choncho sikofunika kugula kapena ngakhale kuchita lendi nyumba kuti mukhale ndi Mpingo. Mmalo mopemphera, “ Kodi ndi nyumba ya mtundu wanji yomwe ingakope anthu? “Pemphani”,kodi ndi chiyani chomwe chingandithandize kwambiri kupanga ophunzira?” Mpingo woyamba umasonkhana pali ponse pomwe angathe ndi nthawi yomwe akuyenera kutero kuti apange ophunzira ndi kuwaphunzitsa kuti akule. Amasonkhana m’kachisi (Machitidwe 3:1; 5:20-21, 42) Amasonkhana m’masunagoge (Machitidwe 18:27-28; 20:20). Amasonkhana mnumba zichitiramo misonkhano ( Machitidwe 19: 9-10). Amasonkhana mnyumba mnyumba (Machitidwe 5:42; 20:20) komanso amasonkhana mnyumba zapaderadera (Aroma 16:3-5; Akolose 4:15; Filimoni 1:1-3) kwambiri, awa adali malo okhazikika kapena chikonzero chokhazikika… zoona zake, uku kunali kupezekapingo kwa zaka 300 zoyambilira za kupezeka kwake!inali nthawi yomwe uthenga wabwino udafalikira pa dziko lonse lapansi! Madongosolo omanga omwe mpingo woyamba udakhudzidwa nazo ndi: 1) Kumanga ufumu wa Mulungu ndi okhulupirira atsopano. 2) Kumanga okhulupirira atsopano kuti ankhwime.!!!!

Mfundo ndi iyi: Sizitengera kuti ndi kuti komwe musonkhane,koma zimatengera kuti inu mukusonkhana.Muyenera kusankha malo osonkhana oyera mtima ndiye aliyense amadziwa komwe apite,malo alionse osankhika kuchoka pa mtengo wina wake kupita pa malo oyimitsa malimoto,kupita kunyumba. Choona ndi ichi,Mulungu sakhala mnyumba yomangidwa ndi manja. Werengani: Machitidwe 7:48-50. Iye azakhale mmitima ya oyera mtima ake. (Akorinto 3:16) Iye adapereka mzimu wake mmtima yathu (2 Akorinto 1:21-22, Agalatia 4:4-7, 2 Timoteo 1:14)!!!Ndibwerezanso: Sititengera kuti mukusonkhana kuti koma zimatengera kuti inu mukusonkhana.!!!

�57

MUSALORE WINA akupeputseni chifukwa mulibe kanthu kapena simunachite lendi nyumba yosonkhanamo,ngati mukupanga opunzira ochulukitsa ena ndi kuwakuza, mukupambana mu ufumu wa Mulungu! Zoona tadzionapo kuti kuika chidwi pa chenicheni chopanga ndi kukuza ophunzira ndi kudzala mipingo.Ngati mukupanga (Osati mwangopanga kumene )ophunzira ochulukitsa omwe akudzala mipingo yochulukitsa, NDINU OPAMBANA PAMASO PA MULUNGU-kaya muli ndi nyumba yopemphereramo kapena ayi.!!!MUSALORE KUTI KUSOWA KWA MALO OSONKHANA” ABWINO” KUKULEPHELETSENI KUDZALA MIPINGO YATSOPANO! Sankhani paliponse pomwe mukufuna ndi nthawi iliyonse yomwe mukufuna kuti mupange ophunzira achulukitsa ndi kuwakuza mu utsogoleri wa nkhristu.!!

1. Zindikirani nthawi ya bwino kuti muzdisonkhana mdziko la chipangano chatsopano la mulungu ,tsiku loyamba la sabata,lidali tsiku la ntchito kwa anthu ambiri,pamene mpingo sankasonkhana pa kawirikawiri pa tsiku limeneli mosafana,mpingo umasonkhana mmakomo atatha ntchito kuti adye ndipo kenaka kupembeza limodzi. Lolani zovuta za anthu zitsimikizire nthawi yabwino ya kusonkhana kwa selo yanu yatsopano .Mkutheka dongosolo la nthawi yak u ntchito likudzindikiritseni kapena maudindo a anthu akazindikiritseni nthawi yabwino ndi tsiku losonkhana pa sabata.!!

2. Inu ndi gulu lanu mudzayenera kuyankha amafunso otsatirawa pamene mukuyamba selo ya mpingo yatsopano:!a. Kodi atsogolere ndani kupembeza? Kodi mudzasowa zida zoimbira?!b. Kodi aphuzitse ndani kapena kutsogolera zokambirana za Baibulo?!c. Kodi mudzachita chiyani ndi ana? Awasamale ndani!d. Kodi mudzakhala ndi chopereka? Ndani akhale ndi udindo pa izi?Kodi chopereka

mudzagwiritsa ntchito yanji?!e. Kodi ndi zipangizo zanji zomwe mukusowa (Baibulo, Mipando, Mabuku anyimbo, ndi zina).!!!!!!

PHUNZIRO LALIKULU: MAPEMPHERO SANKHANI MALO A SELO YA MPINGO WANU !! YATSOPANO POFUFUZA DERA LATSOPANO KUPEMPHA NDI KUMVETSERA KWA !! MZIMU WOYERA,NDI KUPITA KOMWE KULI CHOSOWA,KENAKA PITANI NDI KUKAONA !! MULUNGU AKUGWIRA NTCHITO!!!!!!!!!!!!!!!!

�58

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: pempherani ndi gulu lanu kuti Mulungu avumbulutse komwe ndi kwa anthu omwe inu !! ndi gulu lanu mupite ndi uthenga wabwino kwa otayika ndi kudzala mpingo watsopano. !!!!� Tsiku 2: Lembani zosowa za thupi ndi zauzimu za deralo kapena anthu ndi kupemphera kuti ! !! Mulungu akutsogoleleni pothandiza osowawo ndi mitima yotsegukira uthenga wabwinowo.!!!!!!!!!� Tsiku 3: Pitani ku deralo kapena kwa anthu pemphererani kuzindikira pamene mukuyenda !! pemphererani otayika.Komanani ndi anthu okhala komweko ndi kuwadziwa yang’anani anthu !! a mtendere. Kodi zotsatira zake zidali zotani? !!!!!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Khazikitsani tsiku pasanathe masiku 30, kuti muyambe ntchito yolalikira mdera latsopano kapena kwa anthun atsopano.!!! ! ! Tsiku: ________________________ Nthawi: ________________!! ! ! Zomwe Muchite:!!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!

�59

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 13 - “KUVOMEREZA MACHIMO NDI KUYANJANA NDI MULUNGU NDI ENA”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!

WERENGANI: 1 Yohane 1:5-10!!Kuyanjana ndi Mulungu ndi okhulupirira ena ndi kofunika kwambiri pa moyo wa chi khristu. 1 Peter 3:18 imatiuza kuti khristu adatifera kuti”akatifikitse kwa Mulungu, kutifikitsa m’chiyanjano ndi iye. Yohane 13:35 imatiuza kuti”anthu onse adzadziwe kuti ndinu ophunzira anga, ngati mukondana wina ndi nzake kweni kweni yesu akupereka chilolezo ku dziko lapansi choweruza ngati tili ophunzira ake pakuyang’ana pachiyanjano chathu win ndi nzake.!!FUNSO LOKAMBIRANA: kodi chiyanjano chimenechi chimapezedwa bwanji? Kodi chiyanjano !! chimenechi chimasungidwa motani? Kodi zotsatira za kukhala ndi kupitiriza kukhalabe pa !! ubale wabwino ndi mulungu komanso okhulupirira amzathu ndizotani?!!!!Werengani 1 Yohane 1:5-10 kawiri. Aapa tikuona zinthu ziwiri zosiyana zikuperekedwa: !(1) Kuyenda mkuunika kukusiyanitsidwa ndi kuyenda mmdima ndipo (2) Kuvomereza machismo athu kukusiyanitsidwa ndi kukana kuti tachimwa, pali zovuta ziwiri pa chilichonse. !!!KUYENDA MKUUNIKA!Mulungu ndi woyera,Mulungu ndi kuunika Sali ngati ife,Poti iye ndi kuunika sadakhalepo mumdima (Kuimirira tchimo) Poti mdima ndi kusowa kwa kuunuka. Ndiye tinganene bwanji ngati tili mchiyanjano ndi Mulungu? Poyang’ana momwe tikuyendera, kodi miyoyo yathu I imadziwika ndi chikhalidwe chotani? Kodi zomwe timakonda kuchita ndi zotani? Kodi zomwe tomakonda kuchita ndi zotani? Ndime 6 ikuonetsa kuti chiyanjano chathu ndi Mulungu sichimaonetsedwa ndi mawu athu. Koma zomwe tikuchita.Ngati tikayenda mumdima sitili mchiyanjano ndi mulungu koma ngati tikuyenda nkuunika, poti Mulungu ali mkuunika, sitingokhala ndi chiyanjano ndi wina ndi mzake ndipo machismo athu akhululukidwe.!!Mutha kufunsa, “Ngati tikuyenda mkuunika,ndiye machismo athu akuyenerakukhulukidwa?” Limenelo ndi funso labwino! Kuyenda mkuunika sikutanthauza kulungama kukutanthauza kudziwika ndi chilungamo. Ngati tikuyenda mkuunika chikhalidwe chathu ndi kukhala olungama nthawi ina, tidzatha kugwa mumdima ndi kuchimva koma sitikhalabe momwemo.Timavomereza machismo athu ndi kubwerera m’kuyenda mkuunika,komwe kumatitsogolera muchosiyanitsa chachiwiri.! !FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi Kudziwidwa Ndi Chilungamo Kumasiyana Bwanji ndi kukhala !! wolungama ndi wopanda tchimo? Kodi kuyenda m’kuunika kumaoneka ngati chiyani !! m’moyo wanu? Kodi munganene bwanji ngati mwapita ku kuyenda mumdima, mmoyo wanu?!!!!KUVOMEREZA KUTI TACHIMWA!Malemba akufotokoza bwino kuti “onse adachimwa ndi kuperewera pa ulemerero wa Mulungu” (Aroma 3:23). “Onse” ndithu sikutanthauza kuti “ONSE” zikutanthauza ine komanso inu. Kudzera mmwazi wa khristu.timavomereza machismo athu ndipo timabwezeretsa ku yanjana ndi Mulungu ndi wina ndi mzake. Mwazi wa yesu ndi wa mphamvu kwambiri kuti iye atha kukhululukira tchimo lililonse lomwe lavomerezedwa. Mulungu yemwe ndi kuunika, ali ndi mphamvu zambiri kuti atha kugonjetsa mdima.!

�60

Koma titatha kuyenda mkuunika kwa kanthawi, titha kuiwala chosowa cha mwezi wa khristu. Titha kukhala ozilungamitsa tokha ndi kunyada. Kudalira ubwino wathu kopopsa mwazi wa khristu. Titha kukhala ozilungamitsa tokha ndi kunyada, kudalira ubwino wathu koposa mwazi wa khristu. Titha kufika pa mulingo sitingakane machismo athu atsopano okha, komanso ngakhale kukana machismo omwe takhala tikuchimwapo. Izi makamaka ndi zoopsa kwa abusa komanso atsogoleri a chikhristu, pamene tikumatchulidwa kuti” Munthu wa Mulungu” ndi kumachimva kuti ndi kofunika kuteteza udindo wathu choona ndi choti abusa ndi mamembala a mpingo onse amadalira mofanana mwazi wa khristu pa kukhululukidwa. Tikuyenera kukhala osamala ndi tchimo pa miyoyo yathu. Tikuyeneranso kuyenda mkuzichepetsa ndi kukumbukira momwe mulungu adatipulumutsira ndi kukondwera m’chipulumutso chake! Iye watikhululukira ndi adzatikhululukira pa tchimo lomwe tingakhale nalo, ngati tilivomeleza. Ngati tikukana kuchimwa, ndiye tikumutcha Mulungu ngati wabodza, ndipo mawu ake Sali ndi ife. Tikuyenera nthawi zonse mosasintha kuvomereza (kuvomera ndi Mulungu) za machismo athu.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi m’busa kapena mtsogoleri angaonetse bwino bwanji kuzichepetsa !! pakati pa anthu ake?Alipo madera ena autchimo obisika kwa omwe mukusowa !! kuwavomereza kwa mulungu tsopano?!!!!ZOTSATIRA!Kuyanjana ndi Mulungu komanso wina ndi mzake ndi kokondweretsa kwambiri kukuyenera kukhala pa mtima pa miyoyo yathu ndi utumiki wtahu. Kuononga chiyanjano chimenecho ndi kuzipweteka tokha. Ndiye tikuyenera kusamala posungabe chiyanjano poyenda mkuunika ndi kuvomereza tchimo lililonse pamene tagwa mumdima. Ngati sititero, ndiye sitingakhulupiriridwe, chifukwa tikunama ndi kusachita choonadi. Koposa apa tilibenso chiyembekezo chogawa khristu kwa otayika.!!M’chitidwe wabwinowu wovomereza ndi chifukwa chiyani kufunsa ndi kuyankha moona mafunso osintha moyo nthawi zones pomwe gulu lanu likusonkhana ndi ofunika kwambiri. Pamene tikukhala okhulupirika kwa mulungu ndi kwa wina ndi nzake, timakula m’chisomo chake ndi kuona ubale wokoma ndi Mulungu komanso wina ndi mzake mwa khristu.!!Umboni wa moyo wosinthika umaonetsera kuti uthenga wabwino uli ndi mphamvu! Izi zimaonetsedwa bwino ndi munthu yemwe amayenda mumdima. Koma tsopano akuyenda m’kuunika! Sitikuonetsa kwa ena kuti ndife olungama ndiopanda tchiomo. Mmalo mwake tikuyenera kunena kuti takhululukidwa mwa ufulu mwa chisomo cha mulungu ndi kuti tikupitirizabe kukula m’moyo wathu wa chi khristu ndi chikhulupiriro mwa chifundo chake. Koma ngati tikane kuti tachimwa, kapena ngati tingayerekeze kubisa machismo athu osawavomeleza, tikuphwanya chiyanjano ndi Mulungu komanso wina ndi mzake. Tikuyenda m’chilungamo cha ife tokha ndi kupereka ulemelero kwa ife tokha osati kwa khristu mpulumutsi wathu.!!Tikavomereza poyera machismo athu kwa Mulungu apa pali lonjezo: Mulungu ndi wokhulupilika. Ife ndi wolungama. Adzatikhululukira ngati tidzavomereza. Timakhala mu ntchito yake osati yathu. Zimatengera pa kukumbukira chisomo cha Mulungu kwa ife kuti timakhululukira ena akatichimwira. Plandira chikhulukiro kwa mulungu ndi pokhapo pomwe timakhululukira ndi kuonetsela chikondi wina ndi mzake. Dziko lapansi likuyang’ana kuti lione ngati mwazi wa khristu ndi wa mphanvu yochititsa kuti wochimwa ayende mkuunika. Dziko lapansi likuyang’ana kuti liwone ngati tingakhululukire monga tikhululukidwa. Dziko lapansi likuyang’ana kuti lione ngati ndithu timakondwa m’chiyanjano ndi Mulungu ndi wina ndi nzake.!!!

DZIKO LAPANSI: LIKUYANG’ANA… KODI MUKUONETSA CHIYANI?!!!PHUNZIRO LALIKULU: KUMAONETSERA KUDZICHEPETSA NDI CHIKONDIMNDIPONSO !! NDIKOFUNIKA PAKUSUNGABE CHIYANJANO NDI MULUNGU NDI OKHULUPIRIRA ENA.!

�61

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Lowezani 1 Yohane 1:9. Onaninso ndimeneyi tsiku ndi tsiku m’sabatayi kuti !! zikuthandizeni kuiloweza.!!!!� Tsiku 2: Chitani 1 Yohane 1:9. Mwapemphero mfunseni Mulungu akavumbulitsireni matchimo !! osavomerezedwa omwe angakhale m’moyo wanu nthawi ino. Lembani tchimo lililonse ndi !! kugwirizana ndi Mulungu kuti ndi kenaka funsani chikhulupiliro chake ndipo kenaka !! ng’ambano pepalayo. Kondwererani kuti iye ndi ‘wokhulupirika ndi wolungama kukhululukira !! machismo athu ndi kutichotsera chosalungama chilli chonse.’!!!!!!!!!� Tsiku 3: Chitani 1 Yohane 1:9. Pakutha pa tsiku lililonse msabatayi,onani mumtima mwanu !! ndi moyo wanu ndi kuvomereza tchimo ngati mwachimwa tsiku limenelo. Phunzirani !! kuvomereza tchimo tsiku ndi tsiku.!!!!!!!!!!� Tsiku 4: Ngati mwachimwira munthu wina khululukiranani: Tchimo nthawi zonse limatanthauza !! kuti tamvulaza wina ndi ntchito zathu kapena mawu. Yesu akutiuza kuti tisanampembeze !! ndi kuntumikira Mulungu, tikuyenera kukonza zolakwika ndi m’bale wanu yemwe !! wakuchimwirani (Mateyu 5:23-24). Yakobo akutiuza kuti tikuyenera kuvomereza machismo !! athu ngati tachimwirana (Yakobo 5:16). Ngati mwachimwira wina,pitani kwa munthuyo ndi !! kukhululukirana. Tisapemphe kwa Mulungu kokha chikhululukiro, komanso kwa yemwe !! tamchimwira. Chitani zoyenera kuti mubwezeretse ubale, ngati nkotheka. Aroma 12:18 !! imatiuza, kuti ngati nkotheka khalani ndi mtendere ndi aliyense. Onetsetsani kuti mukukhala !! olumikizana ndi ena pa kuyankha mafunso osintha moyo.!!!!!!!!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.! !

�62

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

NTCHITO 14 - “KODI MPINGO NDI CHIYANI NANGA MPINGO UMATANI?”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!!

Inu ndi gulu lanu mukukhudzidwa ndi dongosolo lobzala pafupipafupi selo ya mpingo yatsopano imodzi; Pamene mukuyamba mpingo watsopano kumeneko pali zinthu zingapo ndi mafunso kuti muzilingalire:!!KODI MPINGO NDI CHIYANI?!Strategic impact ilipo kuphunzitsa atsogoleri kupanga ophunzira ochulukitsa ena kuyambitsa zochita zobzala mipingo. Pamene mukuphunzitsa okhulupirira atsopano molimbikira mudzawasonkhanitsa kupanga selo ya mpingo yatsopano.Kusonkhanako kutha kukhala mnyumba, pamalo pofika anthu onse. Poimitsa galimoto kapena pochitira masewero, pansi pa mtengo, mu ofesi, kapena mnyumba yopemphereramo. Sizimatengera kuti ndi pati pomwe okhulupirira akasonkhana. MALO OMWE OKHULUPIRIRA ANGASONKHANE SAKUTANTHAUZA CHOMWE MPINGO ULI – ANTHU NDIYE MPINGO! Mpingo woyamba ku yerusalemu amasonkhana tsiku ndi tsiku mkachitsi wa chiyuda ndi m’makomo (Machitidwe 2:46). Kachisi ndi pa nyumba sizidali mpingo. Mpingo udali kusonkhana kwa okhulupirira pamodzi.!!Nthawi zambiri timasokoneza mpingo wa Kristu ndi nyumba yomwe mpingo umasonkhana. Timakamba za “kupita ku Tchalichi” pamene zoona zake tikukamba za kupita ku “nyumba ya mpingo”. Ena amenena za kubzala mpingo koma makamaka amaganiza za Kumanga nyumba yopemphereramo. Angakhale abusa ndi atsogoleri amasokoneza Kumanga mpingo waukulu ndi kutolera ndalama zomangira nyumba yaikulu ndi kudzadza ndi anthu.!!M’chipangano chatsopano simukupezeka mawu oti nyumba ya mpingo! Fufuzani Simudzapeza. Koma pali maumboni ambiri a mipingo yokhala m’mizinda: ku Roma, Efenso, Korinto, Filipi kapena Kolose. Kodi mipingo imeneyi imasonkhana kuti? Nthawi zambiri amasonkhana m’nyumba za anthu. Iyi imatchulidwa kuti mipingo ya mnyumba, (onani Aroma 16:5; 1 Akorinto 16:19; Akolose 4:15 ; Filimoni 2). Nyumba ndi malo opambana pa kusonkhana kwa okhulupirira. Kugwiritsa ntchito nyumba kumathandiza mpingo kuika ndalama zake ndi chuma chake pa kutumikira anthu ndi kufalitsa uthenga wabwino. Komanso ndi zopezekeratu pa kugwiritsa ntchito paliponse.Baibulo limaphunzitsa momveka bwino kuti imodzi mwa njira zochulukitsira mipingo ndi kukhazikitsa mipingom’nyumba za anthu.!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ena mwa maubwino ochulukitsa mipingo kudzera mkubzala mipingo !! ya mnyumba ndi wotani?!!!!Kodi izi zikuthanthauza kuti tisamakhale ndi nyumba zopempherermo? Ayi, koma mipingo yabwino ndi yochulukitsa simadalira nyumba! Kungoti, nthawi zina mipingo yokhala ndi nyumba zopemphereramo simakhala bwino kapena kuchulukitsa. Lamulo la ntchito yaikulu ndi “kupanga ophunzira” a Yesu khristu (Mateyu 28:18-20). Ophunzira ochulukitsa ndi yemwe wakhulupirira uthenga wabwino, akuphunzira njira za Yesu monga zidaphunzitsidwa m’baibulo, wofuna kutsatira Yesu m’moyo wa tsiku ndi tsiku ndi kumtsatira iye. Ngakhale nyumba itha kukhala yothandiza,

�63

mutha kupanga mazana ndi zikwi za ophunzira ochulukitsa a Yesu Khristu popanda kukhala ndi nyumba. Mipingo ya bwino ndi yochulukitsa ndi yomwe imaika maganizo onse kupanga ophunzira ochulukitsa omwe adzakwanitsa ntchito yaikulu pochulukitsa ophunzira omwe adzabzala mipingoyochulukitsa. Mipingo ya ntchito yaikulu yolalikirayi itha kupezeka paliponse – mmakomo, poima galimoto, pansi pa mtengo, pochitira malonda, komanso nthawi zina mnyumba zo pemphereramo – koma simafotokozedwa potengera nyumba kapena dongosolo lomwe ili nazo.!!NDIYE, MPINGO NDI GULU LA AKHRISTU OMWE AMASONKHANA PAFUPIPAFUPI PA NTHAWI INA YAKE NDI MALO ENA AKE.!!Komabe, pamene mpingo wasonkhana pamodzi, amasonkhana pa cholinga chinachake. Izi zikutitsogolera ku funso lachiwiri:!!!!WHAT DOES A CHURCH DO?!!FUNSO LOKAMBIRANA: Werengani Machitidwe 2:42-47 ndi kugawana maganizo anu pa zomwe !! ‘Mpingo woyamba’ umachita pamene wasonkhana.!!!Anthu amapita ku mpingo akayakhidwa pa zosowa zawo.Nthawi zonse amafuna dongosolo losangalatsa pa ana awo ndi achinyamata. Amafuna mpingo uwathandize pa zachuma, kupeza ntchito, kupeza zovala zabwino, kupeza malo abwino okhala, kuwathandiza kuthana ndi mavuto onse a munthu komanso banja lawo. Pamene ndipofunika kuwonetsa Chikondi ndi zosowa zawo zenizeni, atsogoleri a mpingo asamalote kuti zosowa za m’miyoyo ya anthu zisakwire zinthu zofunika kwambiri. (onani Machitidwe 6:1-7).!!M’chipangano chatsopano timapeza mautumiki awiri ofunika kwambiri a mpingo:!!

1. Amasonkhana pamodzi kuthandiza wina ndi mzake kudziwa ndi kukonda Mulungu (Machitidwe 2: 42-47; Aefeso 4; 11-16). Ichi chimatchedwa “kamangidwe” zochita zambiri za okhulupirira zakhazikika pa: kupembeza, kutamanda, pemphero, chiphunzitso, kupanga ophunzira, kukomana ndi zosowa za lathupi, kuthana ndi tchimo ndi zolimba ndi zina zambiri. Izi zimachitika pomwe mpingo wasonkhana.!!

2. Amapita kunja ndi kukanena za Yesu kwa otayika (Machitidwe 2:47; 5:42; 8:1, 4; 19:10) izi zikutchedwa “kulalikira”. Pamene okhulupirira amakhala moyo wawo wa tsiku ndi tsiku amalalikira uthenga wabwino kwa ena. Ena ankapita ku malo atsopano ndi mizinda yatsopano kukalalikira uthenga wabwino ndi kuyamba mipingo yatsopano. Izi zimachitika pamene mpingo wamwazika.!!

Ndiye tithe kupitiriza kuthanthauzira mpingo motere: Gulu lo Akhristu omwe amasokhana kuthandiza aliens kudziwa mdi kukonda Mulungu mdi kumwazika kukauza otaika za Yesu.!!Tikuyenera kuyang’ananso chilichonse tikuchita mumpingo mwa zolinga zazikulu ziwiri izi:!!

1. Kodi zikukwaniritsa kamangidwe? !!2. Kodi zikukwaniritsa kualikira? !!

�64

FUNSO LOKAMBIRANA: Pamene mukuyang’ana mpingo wanu, zilipo zochitika zina zomwe !! sizikukwaniritsa kamangidwe kapena kulalikira anthu otaika?!!

(chonde onani chipangizo chomwe chilli mbakali chomwe mungathe kuchigwiritsa ntchitopamene selo yanu yatsopano yampingo ikukomana).!!

Pamene ina ndi ena mukupanga ophunzira omwe adzabzala mipingo, adzakulamwachikhalidwe ndi kuchukitsa. Icichikutitsogolera ku funso lachitatu lokudza Mpingo.!!!KODI NDI KAONEKEDWE KAPENA NDONDOMEKO ZA MITUNDU WANJI ZOMWE MPINGO UNGAKHALE NAZO?!!Chipangano chatsopano chimafotokoza Mpingo ndi kukula, mitundu, kachitidwe ndi chikhalidwe zosiyanasiyana.!!Monga momwe taonera,mipingo yambiri yotchulidwa m’makalata a m’chipangano chatsopano imafanizidwa ndi selo kapena Mpingo wa mnyumba. Mwachitsanzo, Paulo akulemba mu 1 Akorinto 16:19, “Mipingo yak u Asiyaikupatsani moni, akupatseni moni ndithu mwa Ambuye, Akula ndi Priska, pamodzi ndi Mpingo wa mnyumba mwawo” Mu ndime iyi Paulo kutchula Mpingo wonse umasonkhana mnyumba pansi pa utsogoleri wa Akula ndi Priska. (onaninso Aroma 16:3-5; Akolose 4:15; Filimoni 2; 1 Akorinto 16:15)!!M’madera ena kumaoneka kukhala kulumikizana kwa selokapena mipingo ya mnyumba ndi m’busa/ambiri. Mwachitsano, Aroma 16: 3-5 imatchula Mpingo wina wake wa mnyumba komanso imatchula “mipingo ya amitundu” pamene Pauloakulembera Akhristu aku Kolose, akuyankhula kwa okhulupirira angapokomaakutchula Mpingo wa mnyumba umodzi (Akolose 4:15). Ichi chikuonetsa kuti kunali Mpingo mdera lina lake wopangidwa ndi Mipingo ingapo ya mnyumba.!!Timapezanso chomwe chitha kufotokozedwa ngati gulu la Mipingo lokhala ndi abusa ochuluka ndi atsogoleri mu Antiyokea (Machitidwe11:28-30;13:1-2). Mpingowuudapangidwa ndi “gulu lalikululaokhulipilira mwa Ambuye,” (Machitidwe 11:21). Pamene Baranaba adawatumikira, ambiri adaonjezedwa pagululo (Machitidwe 11:24). Ndi chithandizo cha Paulo limodzi “ankaphunzitsa gulu la anthu lalikulu” (Machitidwe 11:26) kenaka tikuona gulula aneneri ndi aphunzitsi omwe adatsogoleraMpingowu (Machitidwe 13:1). Sitikudziwa bwino bwino ngati Mpingowu udalindi gulu la Mipingoyamnyumba kapena ayi, komazikuoneka kutionse amasonkhana pamodzi ochuluka panthawi yopmbedzandi chiphunzitso. Amakambirana ngati Mpingo ndi kusonkhanitsa ndalama ndikutumiza thandizo ku Yerusalemu (Machitidwe 1:27-30) Mpingo waku Antiokea ndi gulu locheperapo la okhulupilira omwe amasonkhana pamodzi pansi pa atsogoleri angapo.!!Ndipo kenaka kudali Mpingo woyamba omwe umayamba mu Yerusalemu, omwe udayambika patsiku la pentekostendi anthu osachepera 3,000 atsopano! Werengani: Machitidwe 2:40-47. Mpingo wa ku Yerusalemuudali Mpingo waukulu wokhala ndi zikwi za znthu omwe amasonkhana pamodzi ngatiumodzikomanso magulu ang;onoang;ono. !!!FUNSO LOKAMBIRANA: Kodi ndi mapatani ati a Mpingo omwe akufotokoza bwino za Mpingo !! womwemuli? 1) Mpingo wa mnyumba 2) Kulumikizana kwa Mipingo ya mnyumba !! 3) Mpingo wokhala ndimipingo yambiri kapena 4) Mpingo wautali? !! Kodi ndi ndondomeko iti imene mukukhulupilira kuti ndiyabwino? N’chifukwa chiyani?!!

�65

Nkutheka Mpingo wanu ndi mbali imodzi ya Mpingo woima paokha kapena uli ndi dongosolo losiyana. Kuchokera mkufotokozera kwa mitundu ya Mipingo m’chipangano chatsopano zikuoneka kuti palibe “ubwino” kapena “kuipa” kosiya mipingo m’magulu.!!Komabe, zilibe kanthu kuti Mpingo uli ndi diongosolo lanji, komayonse inatsatira mfundo zofunikira zofanana:!!

• Atsogoleri a umulungu pomwe amaphunzitsa okhulupilira kukula m’kuyenda kwawo ndikutumikira Khristu. Atsogoleri amenewa nthawi zambiri amatchedwa maovasiya, abishopu ndi madikoni (Afilipi 1:1; 1 Timoteyo 3:1; 4:14; 5:17; Tito 1:5) Aefeso 4;11, imatengaatsogoleri a Mpingo ngati atumiki, aneneri, alalikindi abusa /aphunzitsi.muli monse momwe Mpingo wanu ukutchulira atsogoleri, kofunika kwambiri kuti pakhale atsogoleri a umulungu ndi wokhwima.!!

• Okhulupirira onse amene aku tumikilana wina ndi Mzache  mu Mpingo kapena mdela Lao.!!• Okhulupilira onse achitira umboni kwa otayika kuti apindule anthu kukhulupirira mwa Yesu.!!• Ophunzira ochulukitsa omwe achulukitse Mipingo yatsopano.!!!

Zilibe kanthu kaya ndi mtundu wanji kapena dongosolo lanji, mpingowo ukuyenera kukumbatira zolinga zoyambirirazo ndi zochita motsogozedwa ndi atsogoleri aumulungu. Mipingo yambirinthawi zambiri imaikachidwikwambiripa kukula, nyumba, zochita, ogwira ntchito ndindondomeko yakagwiritsidwe ntchito ka ndalama zomwe zimathera pakungokhala bungwe la chipembezo! Chofunika kwambiri ndikukonza ndondomeko yomwe mutha kumapanga ophunzira ochulikitsa omwe adzayambitsa mipingo yochulikitsa!!FUNSO LOKAMBIRANA: Mkati mwa dongosolo lanu ndi ndondomeko yanu, kodi mukusunga motani !! cholinga chofunikira chikupanga ophunzira ochulukitsa ena ndi kuchulukitsa mipingo? !!!!!!!!!!PHUNZIRO LALIKULU: MPINGO NDI GULU LA AKHRISTU LOTSOGOZEDWA NDI ATSOGOLERI !! AUMULUNGU OMWE AMASONKHANA PAMODZI KUTI AKULE MU UBALE WAWO NDI !! SKHRISTU NDI KUMWAZIKA POFALITSA UTHENGA WABWINO.!!!!!!!!!!

�66

ZOCHITA M’sabatayi:!!� Tsiku 1: Ganizirani malo ndi nthawi yomwe mudzasonkhanitsa okhulupilira mu selo yanu !! ya Mpingo yatsopano. !!! Mudzasonkhana kuti? _______________________________________________________!!! Ndi nthawi yanji yomwe mudzsonkhane nanga kwa nthawi yotalika bwanji? !! !! _________________________________________________________________________ !!! Kodi mudzasonkhana koyamba liti (ngati simudayambepo)?!!! _________________________________________________________________________!!� Tsiku 2: Lembani zochita muselo yaMpingo wanu zomwe mudzachitem poonetsetsa kuti ! ikukwaniritsa:!!! 1) Kulimbitsa okhulupirira:!!!! 2) Kufikira anthu otayika ndi uthenga wabwino:!!!!� Tsiku 3: Onaninso ndondomeko zinayi zomwe zafotokozedwe pamutuuno ndi kulemba !! zomwe mukumva kuti ndi zofunika ndi zosafunika za gawo lililonse.!!

!Kodi ndi ndondomeko yanji yomwe Mpingo wanu utsatile?Kodi mudzasunga bwanji cholinga chachikulu chopanga okhulupilira ochulukitsa omwe adzabzala mipingo yochulukitsa?!!!� Kulalikira: Gawani uthenga wabwino msabatayi kwa anthu osacheper m’modzi amene !! sakumdziwa Yesu Khristu.!!

NDondomeko ya Mpingo Ubwino Kuipa

Selo/Mpingo Wamnyumba !

Kulumukizana kwa melo/Mpingo yamnyumba

!

Mgwitizano wa Mipingo !

Mpingo Waukulu !

�67

STRATEGIC IMPACT SUKULU YOCHULUKITSA OBZALA MIPINGO!GAWO 1 “PHUNZIRANI NTCHITO YAIKULU”!

POOLOKERA GAWO 2 - “KHAZIKITSANI SELO YPTSOPANO YA MPINGO”!!Pamene mukumana pa gulu, pemphereranani wina ndi mzake ndi !

kufunsana Mafunso Osintha Moyo pa tsamba – kenako sonkhanani ndi kuwerenga ntchito yotsatira kambiranani mafunso limodzi.!!

Pa nthawi iyi, pafupifupi mwamaliza Gawo 1 ya Sukulu Yochulukitsa Obzala Mipingo.!Mwamaliza ntchito 14 – motsatana ndi zochita zake zofunika.Mwakhala mukusonkhana ndi kuyanjana ndi gulu lanu, kugwirana wina ndi mzake mchikondi choona. Mwakhala mukulalikiraYesu kwa otayika sabata iliyonse. Mwaphunzira ndi kuchita zambiri zomwe zakukuzani mwa Khristu ndi kukuza Ufumu wa Mulungu! Ntchito yabwino!!!Komanso: !

• Mwaphunzira ndi kukumbatira masomphenya a Mulungu opanga ophunzira ochulukitsa.!• Mwamvetsetsa kufunika kwa uthenga wabwino: chipulumutso mwachisomo kudzera

mkukhulupilra mwa yesu Khristu yekha. !• Mwakhudzidwa m’kupemphera limodzi kutintchito ya Ambuye ibale chipatso cauzimu. !• Mwatsogolera anthu ku chikhulupiliro pogwiritsa ntchitochipangizo cholalikira cha SI. !• Mwayamba kupanga ophunzira ochulukitsa pophunzitsa okhulupirira atsopano ku kukhwima

mwa Khristu pogwiritsa ntchitochipangano cha SI CHOPHUNZITSIRA!• Mwapemphera mwasankha malo a Seloyatsopano ya Mpingo!• Adazindikila dongosolo ndi lingo la Mpingo mdela lililonse. !!

Tsopano pakubwera ndime yofunika kwambiri kwa inu ndi gulu lanu: KUOLOKA kuchoka ku Gawo 1 ndim kupita Mgawo 2 – KUKHAZIKITSA Selo ya Mpingo yatsopano. Ndi nthawi yobweretsa maphunziro omwe mwakhala mukuwalandira ku mlingo wina wobereka chipatso chotsatira.!!Ngati simudachite ichi, pitani chitsogolo ndi KUKHAZIKITSA Selo ya Mpingo yatsopano ikuyenera kwambiri kupangidwa ndi okhulupirira atsopano omwe abwera m’chikhulupiliro kudzera m’ntchito yanu yolalikira komanso mudzasonkhana pa malo omwe mwasankha mu ntchito 12. Kumbukirani, Selo yatsopano ya Mpingo siikhala gulu lalikulu. Likuyenera kukhala lochepa la okhulupilira osonkhana pamodzi pa nthawiyi.Pitirizani kuwakudza okhulupilira atsopano m’chikhulupiliro chawo pogwiritsa ntchito chipangano chophunzitsira cha SI. Gwirani ntchito podzera m’mitu ndi malemba operekedwa mu phunziro 10.!!Pamene mwakhazikitsa Selo ya Mpingo yatsopano, funani omwe ndi okhulupirika ndi chipangizo cha SI cholalikira powathandiza kugawa Yesu ndi mabanja awo ndi amzawo omwe sakumdziwa yesu.!!Pamene Selo ya Mpingo yatspopano yakhazikitsidwa, chonde lembani maina a utumiki ndi kuchonga m’bokosi pambali pa maina a anthu omwe pa inu nokha mukuwaphunzitsa.!!POKHAPOKHA pamene mwakhazikitsa Selo ya Mpingo yatsopano, mutha kuputirira mu Gawo 2 ya sukulu yochulukitsa obzala Mipingo.Ngati simudakhazikitse selo yatsopano ya Mpingo ndi gulu lanu, MUSAPITILIRE NDI KUPHUNZITSA OKHULUPIRIRA ATSOPANO, KOMA MUSAPITIRIRE KU GAWO 2 MPAKA SELO YATSOPANO YA MPINGO ITAKHADZIKITSIDWA.!!!

�68

� !!! !!! !!!!!!!!!!!!!!!!!!

�69

� !

�70

� !

�71

NOTES!_____________________________________________!_____________________________________________!_____________________________________________!_______________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________!_____________________________________________!

�72

NOTES!_____________________________________________!_____________________________________________!_____________________________________________!_______________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________________!_____________________________________________!!

�73

� ! MAWU A CHIKHULUPIRIRO! !MULUNGU!Genesis 1:1; Dueteronomo 6:4; Mateyu 28:19; Yohane 4:24, 10:30; 2 Akorinto 13:14!Timakhulupirira kuti pali Mulungu m’modzi owona, oyera, wopezeka kosatha mwa atatu atate, mwana ndi Mzimu Woyera ali ndi ndi ziyeneretso zofanana za u Mulungu makhalidwe a umunthu. Pachiyambi Mulungu analenga popanda kanthu dziko lapansi ndi zinthu zonse ziri m’mwemo, kumeneko kuonetsera ulemelero wa mphamvu yake, nzeru ndi ukoma. Mwa mphamvu yake ya umulungu akupitiriza kukhazikitsa chilengedwe chake. Mwa kupereka kwake akugwira ntchito kudzera mu mbiri kukwaniritsa zolinga zake zakuombola.!!YESU KHRISTU!Mateyu 20:28; Machitidwe 4:12; Aroma 5:10; 2 Akorinto 5:18-19; 1 Yohane 2:2!Yesu Khristu ndi munthu wamuyaya wachiwiri wa utatu amene analumikizidwa kosatha ndi chibadwidwe cha munthu mwa kuima kodabwitsa mwa namwali. Anakhala moyo womvera kwathunthu kwa atate ndipo mwaulere anatetezera (analipira) machismo a onse pakufa pa mtanda ngati mlowam’malo wawo, kumeneko kukwaniritsa chilungamo cha kumwamba ndi kukwaniritsa chipulumutso ndi moyo wosatha wa onse amene akhulupirira mwa iye yekha. Anauka kwa akufa mu thupi lomwelo, ngakhale alemekezedwa, m’mene iye anakhala ndi moyo nafa anakwera kumwamba, nakhala pa dzanja lamanja la Mulungu la atate, komweko iye nakhala pakati pa Mulungu ndi munthu, akupitiriza kupembedzeraake a yekha. Adzabwera ku dziko lapansi, yekha maso ndi maso, kukwaniritsa zochitika zonse ndi dongolsolo losatha la Mulungu.!!MZIMU WOYERA mdi MOYO WA CHIKHRISTU!Yohane 15:26, 16:8-11!Mgwirizano wa chilengedwe wa kutumikira kwenikweni mu ubale ndi Yesu Khristu ndi moyo wa chiyero ndi kumvera, umapezedwa ndi okhulupirira pamene agonjera kwa M’zimu woyera, munthu wachitatu mu utatu. Anatumidwa pa dziko ndi atate ndimwana kuonetsera kwa munthu ntchito yopulumutsa ya Khristu. Amawalitsa maganizo a ochimwa, kuwatsutsa kuti azindikire kusowa kusowa kusowa kwawo mpulumutsi ndi kuwapatsa moyo watsopano . Pa mfundo ya chipulumutso amakhazikika mwa okhulupirira aliyense kukhala njira ya chitsimikizo, mphamvu ndi nzeru ndipo amaveka okhulupirira aliyense ndi mphatso kukumangirira thupi. M’zimu woyera amatsogolera okhulupirira mu kumvetsetsa malembo. Mphamvu yake ndi ulamuliro zimachitidwa mwa chikhulupiriro, kuzipanga zotheka kuti wokhulupirira akhale m’moyo wa chikhalidwe cha chikhristu bndikubereka chipatso kuulemelero wa Atate.!!BAIBULO!2 Timoteo 3:16; 2 Petro 1:21!Chiyambi ( maziko) a chikhulupiriro chathu ndi Baibulo, lapangidwa ndi mabuku 66 a chipangano chakale ndi chatsopano. Timakhulupirira kuti malemba (mau) onse anachokera kwa Mulungu ndi kuti anapatsidwa ku zotengera za anthu osankhika. Lemba limodzinthawi yomweyolimayankhula ndi ulamuliro wa Mulungu ndipo amawonetsera chiyambi, machitidwe ndi chilankhulo cha anthu olemba. Timagwiritsa kuti malemba salakwitsa, ndi opanda cholakwa kuchokera pachiyambi, ndi apadera, odzala ndi kukhala ndi ulamulirto omaliza pa nkhani zonse za chikhulupiriro ndi zochita, ndipo palibe zolembedwa zina zofanana mphavu ndi Mulungu.!

�74

!CHIPULUMUTSO!Aroma 3:23; 5:8; Aefeso 2:1, 8-9!Pachimake pa cholinga cha vumbulutso la Mulungu m’malembo ndi kuitana anthu onse ku chiyanjano cha mwini wake. Olengedwa pachiyambi kukhala m’chiyanjano ndi mulungu, muthu anipisa Mulungu nasankha kuyenda njira yayekha, ndip[o anlekanitsidwa kwa Mulungu navutika pa chivundi cha chibadwidwe, nalephera kukondweretsa Mulungu. Kugwa kwa munthu kunachitika pachiyambi pa mbiri ya munthu, ndipo pakuti wina aliyense wavutika ndi zotsatirazi ndipo akufuna chisomo chopulumutsa cha Mulungu. Chipulumutso cha munthu tsono, ndi ntchito ya thunthu ya chisomo chaulere ya Mulungu, osati zotsatira mu uphumphu kapena gawo la ntchito za munthu kapena ubwino, ndipo zoyenera kulandiridwa mwa chikhulupiriro yense payekha. Pamene Muluingu wayamba ntchito ya chipulumutso mu m’tima wa munthu aliyense, amapereka chitsimikizo m‘mawu ake kuti apitiriza kuwachita mpaka tsiku lake lakukwaniritsidwa.!!TSOGOLO LA MUNTHU!1 Atesalonika 4:16-17; Ahebri 9:27!Imfa ikusindikiza tsogolo losatha la munthu aliyense. Pakuti anthu onse, padzakhala kuuka kwa akufa kwa akufa matupi kku dziko lauzimu, ndi chiweruzo chimene chifotokoza zochita za aliyense. Pali kulanga kosatha pa osapulumuka ndi dalitso losatha pa opulumuka onse amene amakhulupirira Khristu adzalandiridwa mu chiyanjano chosatha ndi Mulungu ndipo adzapatsidwa mphoto pa ntchito yomwe anagwira m’moyo.!!MPINGO!Machitidwe 2:42; Aroma 12:1-6!Zotsatira za chiyanjano ndi Yesu Khristu ndi choti onse okhulupirira amakhala ziwalo za thupi lake, Mpingo. Pali mpingo umodzi owona dziko lonse, womangidwa ndi onse amene akhulupirira Yesu Khristu ngati mbuye ndi mpulumutsi wawo. Malemba akulamulira okhulupirira kusonkhana pamodzi kudzipereka okha ku kulambira, pemphero, chiphunzitso cha mawu, ubatizo ndi m’gonero monga zoikika zinakhazikitsidwa ndi Yesu Khristu, chiyanjano, kutumikirana ku thupi kudzera mu kutukulana ndi kugwiritsa ntchito maluso ndi mphatso ndi kufikira ku dziko lapansi. Kulikonse anthu a Mulungu akumana pafupipafupi mu kukwera lamuloli, pali kfotokozeka kwa mpingo. Pansi pa chisamaliro cha akuru ndi ma utsogoleri ena,, mamembala ake adzigwira ntchito pamodzi mu chikondi ndi umodzi, chifuniro pa cholinga chokweza Khristu ku ulemelero wa Mulungu ndi kukwaniritsa ntchito yaikulu ya Khristu.!!CHIKHULUPIRIRO mdi NTCHITO!1 Akorinto 10:24, 31; 2 Timoteo 3:16-17!Malemba ndi lamulo lomaliza mu ntchito zonse za chikhulupiriro. Tikudziwa kuti sangamange chikumbu mtima cha ena m’madera amene lemba lakhala chete. Komabe, wokhulupirira aliyense ayenera kutsogozedwa m’madera amenewo ndi Ambuye, kwa iye amene ali mdindo.!!!!!

�75

!VERSION UPDATE NOTES:!v2.0 (2014)!! - Complete revision of curriculum. !! - Addition of SMCP !! - Addition of Discipleship Tool!! !!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! !

STRATEGIC IMPACT!P.O. BOX 830337!

RICHARDSON, TX 75083!WWW.TOUCHINGEVERYNATION.COM!

© Zowonera, Strategic Impact.  Pasakhale kusintha kulikonse kwa bukhuli, !koma mukhoza kukopera mwaulere ndi kugawa osasintha kanthu.!!

© Copyright, Strategic Impact.  No changes may be made to this manual, but you!may freely copy and distribute without making changes to content.

�76