cha64-0823m mafunso ndi mayankho vgrdownload.branham.org/pdf/cha/cha64-0823m questions and answers...

83
MAFUNSO NDI MAYANKHO Tiyeni titsalire titayima kwa mphindi yokha pamene ife tikuweramitsa mitu yathu kwa pemphero. Atate Mulungu Achisomo, ife tikukuthokozani Inu mmawa uno kuchokera mu kuya kwa mtima wathu, chifukwa Inu ndinu okhoza ndi kulolera kuti muyankhe mapemphero athu. Ndipo ife tikupemphera kuti Inu mulandire kupereka mathokozo kwathu chifukwa cha zimene Inu mwatichitira kale ife. Ife tikuyembekezera ndi chiyembekezo chachikulu kuti Inu mutithandize ife mmawa uno, ndipo pamene ife tizichoka pa makonde a nyumba ino, mulole ife tituluke pano tiri munthu wosinthika kuposa momwe ife tinaliri pamene ife timabwera muno. Mulole Mzimu Woyera utiwumbe ife mmawa uno, makhalidwe athu, ndi kutipanga ife kukhala omvera a mu Ufumu Wanu pakuti ife tikupempha izi mu Dzina la Yesu. Ameni. (Mukhoza kukhala pansi.) 2 Ndikupepesa basi kuti ndachedwerapo pang’ono pokha, koma ine ndinali ndi zinthu zingapo ndithu zoti ndichite, ndiponso anthu odwala ambiri ndi oyankhulana nawo ine ndisanafike mu—ku nyumbayi pafupifupi. 3 Ndipo kotero, ife tiri okondwa kuti tiri pano mmawa uno ndi kukuwonani anthu abwino nonsenu. Ndipo ine ndikufuna kuti ndiwathokoze aja—anthu awo amene anatitumizira ife zinthu zabwino zija, mphatso ya kwa mkazanga ndi kwa— ndi—m’bale amene ananditumizira ine mfuti yake ya agwape. Ambuye amudalitse iye. Iye—anati iye wayamba kukalamba ndipo sakanafuna kuti aziigwiritsanso iyo ntchito panonso, ndipo iye wafuna kuti ine ndikhale nayo iyo; kotero i—ine ndine woyamikira ndithudi kwa izo—chifukwa cha izo. Utali wonse pamene ine ndikhale wamoyo, m’bale, momwe ine ndingathe kudzithandizira ndekha, ine ndikhala ndiri nayo iyo. Ine sindimaiyika konse iyo mu dzanja langa kupatula ine nditaganizira za inu ndi kukupemphererani inu. 4 Tsopano, ife tiri…Zinthu zochuluka kwambiri zoti zichitidwe lero, ine ndimaganiza mwinamwake pamene ine ndiri kuno ine ndikhale ndi mafunso ena ndi kupeza chimene chinali pa mtima wa mpingo wanga—osiyana awo. Ine ndithudi ndinaterodi! Ine ndiri ndi mafunso okwanira oti akhoza kunditengera ine mpaka Zakachikwi zidzayambike! Ine sindimadziwa kuti analipo ochuluka chotero amene akanakhoza kupezedwa. I—ine ndiri nawo zana ena pano, ndipo alipo zana kapena kupitirirapo amene abwera muno mmawa uno. Kotero ine sinditha konse kuwayankha iwo, ine ndikulingalira,

Upload: vodat

Post on 26-Mar-2018

390 views

Category:

Documents


23 download

TRANSCRIPT

MAFUNSO NDI MAYANKHO

Tiyeni titsalire titayima kwa mphindi yokha pamene ifetikuweramitsa mitu yathu kwa pemphero.

Atate Mulungu Achisomo, ife tikukuthokozani Inu mmawauno kuchokera mu kuya kwa mtima wathu, chifukwa Inu ndinuokhoza ndi kulolera kuti muyankhe mapemphero athu. Ndipoife tikupemphera kuti Inu mulandire kupereka mathokozokwathu chifukwa cha zimene Inu mwatichitira kale ife.Ife tikuyembekezera ndi chiyembekezo chachikulu kuti Inumutithandize ife mmawa uno, ndipo pamene ife tizichokapa makonde a nyumba ino, mulole ife tituluke pano tirimunthu wosinthika kuposa momwe ife tinaliri pamene ifetimabwera muno. Mulole Mzimu Woyera utiwumbe ife mmawauno, makhalidwe athu, ndi kutipanga ife kukhala omvera amu Ufumu Wanu pakuti ife tikupempha izi mu Dzina la Yesu.Ameni. (Mukhoza kukhala pansi.)

2 Ndikupepesa basi kuti ndachedwerapo pang’ono pokha,koma ine ndinali ndi zinthu zingapo ndithu zoti ndichite,ndiponso anthu odwala ambiri ndi oyankhulana nawo inendisanafike mu—ku nyumbayi pafupifupi.

3 Ndipo kotero, ife tiri okondwa kuti tiri pano mmawa unondi kukuwonani anthu abwino nonsenu. Ndipo ine ndikufunakuti ndiwathokoze aja—anthu awo amene anatitumizira ifezinthu zabwino zija, mphatso ya kwa mkazanga ndi kwa—ndi—m’bale amene ananditumizira ine mfuti yake ya agwape.Ambuye amudalitse iye. Iye—anati iye wayamba kukalambandipo sakanafuna kuti aziigwiritsanso iyo ntchito panonso,ndipo iye wafuna kuti ine ndikhale nayo iyo; kotero i—inendine woyamikira ndithudi kwa izo—chifukwa cha izo. Utaliwonse pamene ine ndikhale wamoyo, m’bale, momwe inendingathe kudzithandizira ndekha, ine ndikhala ndiri nayoiyo. Ine sindimaiyika konse iyo mu dzanja langa kupatula inenditaganizira za inu ndi kukupemphererani inu.

4 Tsopano, ife tiri…Zinthu zochuluka kwambiri zotizichitidwe lero, ine ndimaganiza mwinamwake pamene inendiri kuno ine ndikhale ndi mafunso ena ndi kupeza chimenechinali pa mtima wa mpingo wanga—osiyana awo. Ine ndithudindinaterodi! Ine ndiri ndi mafunso okwanira oti akhozakunditengera ine mpaka Zakachikwi zidzayambike! Inesindimadziwa kuti analipo ochuluka chotero amene akanakhozakupezedwa. I—ine ndiri nawo zana ena pano, ndipo alipozana kapena kupitirirapo amene abwera muno mmawa uno.Kotero ine sinditha konse kuwayankha iwo, ine ndikulingalira,

1002 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

molondola, chifukwa…Ndipo i—iwo ndi mafunso abwino,abwino kwenikweni.5 Tsopano, ena a iwo sangati awerengedwe apa pomwemu chigulu, kotero inu mukudziwa, ine ndawafunsa iwo…Ngati zimene ine sindingathe kuziika pamenepa…Ndimavuto a m’banja ndipo…inu mukumvetsa. Ndipo i—inendawapempha kuti ndikhale nawo onse mwamuna ndi mkazakepa kuyankhulana kwapadera, chotero ine ndithe kuyankhulananawo iwo mwamseri pa nkhani zimenezi. Si zinthu zoipa; ndizinthu zoti zikuyenera kuthetsedwamu banja, kungoti chibadwacha umunthu ndi mtundu umene ife…nthawi imene ife tirinkukhalamo ndi zina zotero nzimene zikubweretsa zinthu iziapo, ndipo awo ndimavuto amene amapita ku banja la umunthu;ndipo iwo ayenera kuti ayankhidwe. Ndipo kotero, ine ndichitachirichonse chimene ine ndingathe kuti ndiwayankhe iwo mwanjira yopambana.6 Nthawizina poyankha mafunso, izo zimakhala ngatizimatenga nthawi yaitali; ndipo ine sindikufuna kuti ndiphonyelirilonse la iwo. Ine nditenga lirilonse mwapafupi basi momweine ndingathere. Tsopano, iwo basi—ine ndinangowalongezaiwo mu thumba pano, ndiwayankha iwo, ndipo—ndiikapoLemba ine ndikakhala ndiri nalo ilo, n—ndi kuzibwezeretsaizo. Ndiye ine ndinali tsiku lonse dzulo, ndi gawo lalikulu lausiku wausiku watha, ndipo chiyambireni kutangocha pang’onommawa uno…Ndipo ine ndiri nazo pafupi kawiri kwa zimenezinabwera mmawa uno. Kotero, ine ndikuganiza zimene ifetiti tichite, Ambuye akalola, ine ndiwayankha iwo mpaka—momwe ine ndingathere mpaka pafupi dzuwa paliwombo,ndiyeno nkubalalitsa, ndiyeno nkukabwerera kachiwiri usikuuno n—ndi kuyesera kuti titsirizitse ochuluka momwe inendingathere usikuuno, ndi kuwona ngati ine ndingathekutenga—kuwatsiriza iwo apo. Ndipo mwinamwake inesindichita kuti ndikulangeni inumotalika choteromu kukomanakumodzi kwakutali kwambiri. Ndipo ine ndikuganiza izozingakupatseni inu nthawi kuti mupite panja, ndi kukapumula,ndi kupezanso mphamvu pang’ono, kukausa pang’ono kapenachinachake, ndi kubwereranso ngati inu mungathe. Ngati inusimungathe, bwanji, M’bale Fred Sothmann, ine ndikulingalira,ali kujambula izi. Kodi izi zikujambulidwa? Chabwino, izoziri bwino. Eya, iwo ali mu chipindamo akujambula izo, n—ndipo tepi iyi mwina—ngati ziri zabwino—inu mukhoza kukhalanayo tepiyo; iyo ingasungidwe ndipo izitchedwa Mafunso ndiMayankho, chifukwa muli mafunso ena olimba kwenikwenimkati umu ndi chinachake…Ambiri a iwo ali pa chiphunzitsocha mpingowu.7 Tsopano, ine ndikufuna kuti anthu adziwe kuti nthawizinapoyankha mafunso awa, ndi zovuta. Zimatengera chisomochochuluka kuti uyime pano, ngati inu mutadziwa chikondi

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1003

chimene ine ndiri nacho pa anthu inu. Ine sindingathekuchifotokoza icho. Ine sindimachifotokoza nkomwe icho kwaana anga; ine sindimachifotokozera nkomwe—chikondi changachakuya kwa mkazi wanga momwe ine ndimayenera kutindizichitira, chifukwa nd—ndine wopsyamtima, ndipo inendimangopita mu mzere umodzi wowongoka. Pali chinthuchimodzi chokha chimene ine ndingafotokozereko chikondichanga kwa icho: ndiko kwaMulunguWamphamvuzonse. Ndipoi—ine ndimangomukonda Iye poyambirira pa zonse. Anthuena ine ndimawakonda, koma i—ine sindikufuna kuti ndifike—ine sindikufuna kuti ndiwononge chikondi icho chimene inendiri nacho kwa Iye; kulola icho kukhala choyambirira.Kotero chotero, pamene ine ndikuyankha mafunso anu, inendikuwayankha iwo ndi chikondi mu mtima mwanga kwa inu;koma chinthu chimodzi chiri patsogolo panga nthawizonse:chimenecho ndi Yesu Khristu (mwaona?), mwa njira yomwe Iyeakanayankhira izo.8 Nthawizina ine ndingati ndiyankhe…Izo zingatizipweteke, zingati zikande, ndipo i—ine sindikutanthauzakuti izo zikhale mwanjira imeneyo. Ine ndikuyankha izondi cholinga chimodzi, monga ine ndinanenera, Khristupatsogolo panga. Ndipo ine ndikuyenera kuti ndizikumbukirakuti Ali Iyeyo amene i…Ine ndidzati ndidzakayankhireko.Kotero chikondi changa choyamba chiri kwa Iye; chikondichanga chachiwiri chiri kwa inu anthu, ndipo kotero i…Mpingo Wake umene Iye anawugula ndi Magazi Ake omwe.Ndipo Iye amakukondani kwenikweni inu kuposa momwe Iyeamadzikondera Iyeyekha, chifukwa Iye anadzipereka Iyeyekhapofuna inu. Ndinu ogulidwa a Magazi Ake, ndipo i—inendikuzigwira izi mosamalitsa basi ndi moonamtima momweine ndikudziwira kutero. Komano, pochita izo nthawizinainu mumaganiza, “Uko kunali kuyankhula kwa mwano zediine…pafupi… Izo ziri zosathwa kwambiri ndi zosabisa.” Inendikuchita izo ndiri naye Iye mu malingaliro anga (mwaona?)kuti ndiyesere kupanga—kuti ena a—aliyense awone basi kuti izoziyenera kumakhala mwanjira imeneyi. Izo si chi—chirichonsechoti chipweteke kapena osatinso kuposa kungoti nditsimikizekuti anthu azimvetsa izo, ndipo ine ndikuyembekeza aliyenseazilandira izo mwa njira imeneyo. Ndipo tsopano, mkati umu ifetikupeza zomwe ziri mumalingaliro anu.9 Ndipo pamene ine ndikukuwonani inu nonse mutasonkhanammawa uno ndi chirichonse chitadzazidwa pozungulira, ndipoine ndikuganiza tiri ndi khamu losefukira m—mu mpingo wina.Mpingo wapaubale watenga—wailesi kapena china chonga—kulumikiza kwa lamya. Ndizo…Kusefukira kuli mu mpingoumenewo mmawa uno, ine ndamvetsedwa. M’bale…Kapenam’bale wina ali ndi—mpingo umene uli ndi kusefukira kumenekwasamutsidwa kuchokera kuno kupita ku mpingo umenewo.

1004 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Izo ziri chomwecho kuti inu musachite kuyima pamapazi a winandi mzake ndi zinthumutazungulira khoma.10 Tsopano usikuuno, Ambuye akalola, ife tikhala ndi—ifetiyambamolawirira usikuuno. Ine ndikufuna kuti ndimupemphem’busa ndi—borodi ngati iwo angathe…Tiyeni tiyambemolawirira pang’ono pokha usikuuno, chifukwa cha anthu, enaa iwo ali pano, ndipo iwo akhala ndi kuyendetsa kwakutali.Ndipo ine ndikanafuna kuti ndiyambe molawirira ndi orausikuuno, ngati ife tingathe, ndi kutsirizitsa izo. Kotero inu…Mwamsanga basi inu mukakhala ndi chakudya chanu ikadutsasikisi koloko kapena nthawi iliyonse, ndiye, ine ndiyamba.Mwaona? Kuti, inu kawirikawiri mumayamba pa hafu pasitiseveni sichoncho inu? Tiyeni tidzakhale, tiyeni, mulole inendidzakhale pa nsanja pofika seveni koloko. Mwaona? Ndipopamenepo pofika eyiti koloko kapena hafu pasiti eyiti, kapenachinachake monga choncho, izo zikupatsani inu nthawi k—kutimupite ku makwanu ndi kukakonzekera ntchito ya mawa, ngatimawa liripo.11 Tsopano, Ambuye akhale nanu ndi kukudalitsani inumochulukitsa, ndipo ine ndipita mwamsanga pamenemsonkhano uno utha ndi kukawatenga mafunso ena awa ndikuyesera kuti ndiwayankhe iwo. Ine ndingolemba pa iwo,pang’ono pokha—zidutswa pang’ono za zolemba ndi zinazotero, zimene ine ndingathe—ine ndingathe…Zimakhalangati ndingaiwale Malembawo. Ndiye pamene ine ndikakhalamu chipindacho ndikuwerenga, ndiye ine (ine ndikufunakumalozeranso kwa iwo penapake, ndipo ine ndiri nazo izopano) ndipo—ndangozilemba izo pa chidutswa cha pepala.Ndipo kotero, ngati izo ziri mu—bukhu lolongosola inendikuyenera kuti ndikazitenge izo, kapena kufotokoza kwinakwa mawu, kapena dzina, ine ndikhale nditazilemba izopatsogolo panga. Ine sindikusowa kuti ndichite kubweretsachimulu chachikulu cha mabuku ndi zina zotero; ine ndikhalenazo izo pamenepo.12 Tsopano, ngati funsolo simunakhutitsidwe nalo inuyo,chabwino, ndiye i—mwinamwake ine ndalakwitsa. Mwaona?I—i—ine mwinamwake ndingakhale nditalakwitsa, chifukwazinthu izi ziri basi mwa kupambana kwa kumvetsakwanga. Ndipo ine ndikufuna—atumiki amene angakhale ndiosonkhana awo, kapena osonkhana a mpingo winawake ameneangamamvetsere kwa mafunso amenewa…Ine sindikufunaizi…Ngati izo ziri ndi chinyezimiritso chirichonse pachiphunzitso chanu ndi o—o—osonkhana anu, ine ndikufunaosonkhanawo kuti amvetse bwino bwino kuti uku ndikuphunzitsa kwathu basi pa kachisi pano. Ine sindirindikuyesera kuti ndizikakamizire izo pa magulu ena onsea anthu. Ndipo i—i—ine ndikufuna kuti ndikhale Mkhristum—mu mtima mwanga, kuti ine ndiziphunzitsa zimene ine

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1005

ndimazikhulupirira. Ine ndikuima pa kukhudzidwa kwanga.Ngati ine ndinyengerera pa izo, ndine waupandu kwa Khristundi wachinyengo kwa inu; ndipo i—ine ndiyenera kuimamomvera pa zimene ine ndikuzikhulupirira kuti ziri Choonadi.Koma munthu wina aliyense ali nawo ufulu kuti azichitamofanana. Mulungu ndiWoweruza wa ife tonse.13 Tsopano, basi ife tisanayambe, ine ndimaganiza kutinditchulepo za wambiriyakale wabwino, Paul Boyd. Ambiria inu mukumudziwa iye; iye amabwera kuno ku kachisi.Iye wabwerera kumene kuchokera ku Yerusalemu ndipoanakakhala nawo pa Chiwonetsero cha pa Dziko. Iye alimochuluka kwambiri m—mphunzitsi wa uneneri, ndipo iye ndiwazambiriyakale, mmodzi wa abwino kwambiri. Iye ndi m’balewa Chimennonite—iye anali—ndipo iye analandira ubatizo waMzimu Woyera. Ndipo kotero iye anakhala mzanga wapafupikwambiri wanga. Ndipo iye nthawizonse amayang’ana ndikumasamalitsa chirichonse chimene ine ndinena chokhudzaza uneneri, kuti ayang’anire ndi kuwona ngati izo ziti zifikepokwaniritsidwa.14 Ndipo tsopano, iye wandilembera ine apa (pamene iyeali kuno mu States kachiwiri tsopano), ndipo izo ziri pabolodi lazolengeza, ine ndikuganiza, mmawa uno. Ndipo iyewalemba apa cholembedwa chimene iye wachiika mu imodziya mapepala kapena chinachake kapena imzake, zokhudzamauneneri opambana. Ndipo iye watchula chinthu chachisanu,ine ndikuganiza icho chiri, chimene ine ndinachiwonazaka sate-firii zapitazo chokhudza kupindula kwa—kupitapatsogolo, maka, kwa sayansi. Ndipo aliyense wa inu amenemukukumbukira, inu munazilemba izo. Ine ndiri nazo izo mumabuku anga. Ndi chirichonse chimene Ambuye ananena…amandiuza ine, ine ndimazilemba izo, icho ndi chachikulucho-…kapena chinthu chimene ine ndingawauze anthu.15 Ndipo ine ndimaganizammawa uno, ife tisanayambe ichi…Uwu si ulaliki, koma ife tiri pano kuti tikhale palimodzikuti tiphunzire kuchokera kwa wina ndi mzake zimene ziripa mitima yathu. Tiyeni tizipese bwino zinthu izi tsopano,pamene ife tikubwera chotsika kudutsa muMibadwo ya Mpingondi zina zotero. Ine ndikuganiza ndi chabwino kuima ndikukhala ndi msonkhano kapena iwiri, ndi kufufuzapo, ndikupeza zimene ziri pa mtima wa anthu, ndiyeno nkumapitirirakuchokera pamenepono. Inu mukuona? Ndiye nkubwererammbuyo kachiwiri ndi—kupita mu ndi mndandanda w—wa mautumiki. Ngati Ambuye alola, ine ndikufuna kutindidzakhale nazo izo pano pa kachisi pasanapite nthawi,mndandanda wautali basi wa mautumiki; inu mukudziwachimene ine ndikutanthauza, w—wamongamaphunziro osiyana;ndi kumapitirira nazo basi mpaka Iye andidzere ine kapena inendipite kukakomana naye Iye, limodzi. Mukuona?

1006 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

16 Paul Boyd walemba apa zokhudza zinthu zisanu ndiziwiri zija zimene ine ndinaziwona mu 1933, zomwe zinalizoti zidzachitika. Ndipo iye akuziyang’ana izo mwatcherubasi, mwaukatswiri, momwe iye angathere, chifukwa iyendi wazambiriyakale. Ndipo iye amaziyang’anitsitsa izo,ndendende basi zimene iwe unena. Ndipo iye anawona zinthuzija zimene zinanenedwa zaka zambiri zapitazo: za momweMussolini…ndi zomwe zikanadzamuchitikira iye, ndi Hitler,ndi zomwe zikanadzakhala za iye; ndi momwe Chikominisichikanati chidzatenge zonse chi Fascism ndi zonse izi; ndimomwe—Mzere wa Siegfried ukanati udzamangidwire, ndimomwe kuti Amereka akanati adzakamenyeredwere kumeneko(ndipo iwo sakanati avomereze konse izo mpaka pafupizaka ziwiri zapitazo, ndipo iwo anatenga zithunzi za kuGerman za kuzingidwa kumeneko; ndipo iwo analandirakumenyedwa kwenikwenidi. Iwo monga…Iwo anakatayaankhondo awo pafupifupi kumeneko); ndi zinthu zonse izozimene zinachitidwa.17 Ndipo tsopano, izo zinanenedwa aponso, “Ndipo zidzafikapochitika, kuti asanafike mathero a nthawi, kuti magalimotoadzatenga maumbidwe a dzira, kukhala mochuluka ngatidzira.” Ndipo ine ndinawona banja la Chimereka likuyendetsamu msewu mu galimoto imene…Iwo anali atakhalaakuyang’anizana wina ndi mzake, ndipo iwo anali ndi gome,ndipo anali, ankawoneka ngati, akusewera njuga kapenamakhadi. Ndipo iwo analibe chiwongolero chirichonse mugalimotoyo. Ndipo iyo inali kulamulidwa ndi mphamvuinayake popanda chiwongolero. Ndi angati akukumbukira inendikunenera izo (mwaona?), izo zakhala ziri kuno?18 Tsopano, pa Chiwonetsero cha Padziko iwo ali nayokale galimotoyo pa msika. Apa pali…Iyo ikugulitsidwatsopano; kampani yaikulu inayake yatenga ambiri a iwo. Ndipogalimoto iyi, ndi iyi apa. Paul Boyd anakumbukira uneneriwo,anakayang’ana mu bukhu lake zimene ine ndinanena, ndipoanatengera chithunzicho mmenemo. Ndipo ndi iyo apo,ndendende mwa maumbidwe a dzira, ili ndi mipando iwiriitayikidwa mbali iyo, ndi iwiri itayikidwa mbali iyi, ndigome litayikidwa pakati kuti azisewera makhadi ndi zinthu,ndendende basi.19 Mawu a Ambuye ndi olondola mwangwiro. Izo zinalimu 1933. Izo zingakhale ziri…Tiyeni tiwone, kodi zimenezozingakhale chiani? Zaka sate-thuu zapitapo, si choncho izo?Ichi ndi 1964. Eya, sate…Eya, zaka sate-wani zapitapo. Zakasate-wani zapitapo Ambuye anandiuza ine zimenezo, ndipo ndiiyi pano. Ndipo kampaniyo ili kuno imene yawaodetsa kaleiwo; n—ndipo makampani a magalimoto akatundu ndi zinthuakugula magalimoto akatundu opangidwa monga amenewo.Iwo akhoza kumawalamulira iwo kuchokera ku malikulu

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1007

awo monga choncho, sakusowa ngakhale kuti azikhala ndiwoyendetsa mmenemo. Ndipo pano iyo yapangidwa kale,ndipo apo ziri ndi magalimotowo. Tsopano, izo ziri pa bolodila zolengeza kumbuyoko, ndipo inu mukhoza kuwerengauneneriwo ndipo mungawone kulondola kwake Mulungu wathualiri, momwe Mawu Ake…Iye anati, “Miyamba ndi dzikolapansi zidzachoka, komaMawuAnga sadzalephera konse.”20 Tangoyang’anani, zaka sate-firii zapitapo. Inu mukudziwachomwe—chomwe ya 1931, kapena chirichonse chomwechinali, mtundu wa galimotozo momwe zinkawonekera; iyoinkawoneka ngati chidina. Iwo anati, “Iyo izidzawonekamonga ngati dzira, idzakhala ngati dzira.” Ndithudi, palibewina muno, ine ndikupeneka, amene ali moyo lero kapenapakati pathu amene anandimva ine ndikunena zimenezo.Ndi…Inu mwandimvapo ine ndikuneza zimenezi kudutsammibadwo, koma…Eya, apo pali mkazi ali pano. Bwanji,Akazi a Wilson, ine sindimakuwonani inu pamenepo. Inumukukumbukira pamene izo zinkachitika. Apo ndi pameneiye anachiritsidwa, akufa ndi TB (mayiyo, mwamuna wakendi mwana wake wamkazi anabwera nandiitana ine kutindipite ndikamupempherere iye) mpaka iye ankawukha magazimpaka—pangodya panali patadzaza n—ndi mapilo ndi zinthuzomwe iye ankawukhizirapo. Ndipo adokotala anati, “Palibenjira yoti iye angafike pakuti akhale moyo konse,” ndipongakhale…Iye anali kuyesera kuti anene chinachake kwa ineasanafe, ndipo magazi ankakhoza kukhavukira pa mabulangetindi nsalu zofunda pamene iye anali pamenepo, pamene iyeankayesera kuti akhosomole. Ndipo ine ndinamuchotsa iye pakama ameneyo, ndipo ndinamutengera iye ku mtsinje wozizirakuno, ndi madzi achisanu, ndipo ndinamubatiza iye mu Dzinala Yesu Khristu. Ndipo izo zakhala ziri zaka sate-firii zapitapo,ndipo ndi uyu wakhala apayu lero, akadali ndi moyobe, pameneana aakulu, athanzi, ambiri a iwo apita kale. Ndi inu apo.“Chisomo chododometsa, kukoma kwake kuchimva, chimenechinapulumutsa wopanda pake ngati ine!” Izo zikungosonyezamomwe zimakhalira zangwiro pamene zifika pochitika ndiPAKUTI ATERO AMBUYE.21 [Mkazi ayankhula kwa M’bale Branham kuchokeramwa osonkhana—Mkonzi.] Inde, uko nkulondola, Mlongo.Inde, bwana! Akazi…Ine ndinati akazi adzakhala opandamakhalidwe kwambiri mu…Tsopano, inu mukudziwa zakasate zapitazo momwe iwo ankavalira. Ndinati iwo akukhalaopanda makhalidwe kwambiri, mpaka iwo akumayenda mumsewu atangovala chokhala ngati zovala zawo zamkati. Ndipoine ndinati, “Ndiye zidzafika pochitika, kuti iwo adzakhalangakhalenso ochititsa manyazi kwambiri, mpaka iwo azidzavalachinachake chinkawoneka ngati tsamba la nkhuyu.” Inendinaziwona izo, ndipo iwo ali nazo izo; ndipo iwo akuzivala

1008 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

izo. Basi—kupanda makhalidwe kwa akazi kudzafika potsikakwambiri ndimopanda ulemu! Ife sitingathe kutsika kuposa apotsopano; inu simungathe kupita moipirapo. Iye ali pa mapeto!Mukuona, iwo sadzakhala ali kwathunthu amaliseche. Ayi,iwo…22 Ine ndalalikirapo kwa anthu, akazi mwa makumi a zikwiamene amakhala alibe chidutswa chimodzi cha zovala pa iwo(mwaona?), amuna aang’ono, ndi akazi aang’ono, ndi onse, komaiwo asakudziwa kuti ali maliseche.Mwaona? Iwo samadziwa izo.Ndipo momwe akazi akuchitira lero…23 Ine ndinali kuyankhula usiku wina kwa amzanga enaa ine pamene ife tinali kutali komwe uko mmapiri, ndipom—mkazi wachichepere…ine ndinali nditamupemphererakumene mwana wake; iye anali ndi khunyu; ndipo mwanayoali bwino. Ndipo banja laling’ono, losawuka, kutali komweuko ku phompho, kamunda kakang’ono ka fodya kachikalemozungulira nyumbayo—ndi pafupi zipinda ziwiri mmenemo—ndi ana seveni kapena eyiti…Mkazi ameneyo amagwira ntchito(o, mai!)—ali ndi nkhwangwa yaikulu kunja uko, akuwazankhuni ndi zinthu, n—ndi kumalima mminda, ndi kumalongezazinthu. Ndipo ine ndinayang’ana pa mkazi wosawukayo—diresi yomweyo imene iye wakhala akuvala kwa chaka kapenaziwiri, ndipo yonse itagawanika ndi chirichonse…Ndipo inendinali kuyesera kuti ndipeze ena mwa madiresi a Meda kutindiwatengere uko kwa iye sabata yotsatira.24 N—ndipo ife tinazindikira titaima pamenepo, abaleangapo ndi ine, donayo akumuyamwitsa mwana wake. Iyeanangotulutsa bere lake k—k—kuchokera mu diresi lake ndikuyamba kumamuyamwitsa mwanayo; ndipo izo zinakhalangati zododometsa kwa miniti; umo ndi momwe amayi angaankandiyamwitsira ine! Ndizo kulondola ndendende.25 Ine ndiri nawo ulemu kwa mkazi ngati ameneyo kuposamomwe ine ndimachitira kwa akazi enawa amene amaikakachingwe kakang’ono pansi pawo kuti azidziponyera okhakunja. Samawoneka nkomwe ngati anthu okhalapo. Iwo alinacho cholinga pa kuchita zimenezo; izo ndi zachigololo,kupanda umulungu. Mkazi amayala zovala nthawizonsezambiri ndi kuyesera kuti adzipange yekha kumawoneka ngatichinachake chimene iye asali…ine…Bwanji, akazi s—salikwenikweni mwanjira imeneyo; uwo ndi mtundu winawakewa zinthu zaku Hollywood. Ndipo mzimu wa mdierekeziumafika pa akazi amenewo kuti uziwapangitsa iwo kutiaziyesa kukopa tcheru cha amuna kudzera mu kugonana.Mabere a mkazi anapatsidwa kwa iye kuti aziyamwitsiramwana. Ndiko kulondola ndendende. Mkaziyo ali mu mzerewakusatukuka, koma iye wadzifoletsa molondola. Ine ndirinako kulemekeza kochuluka kwa izo, kwa mkazi ameneyomonga choncho, chifukwa iye…Umo ndi momwe amayi ake

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1009

anamulerera iye; umo ndimomwe…I—iwo—samapereka chidwichirichonse kwa izo. Mwanayo anayamwitsidwa apo pomwemonga chithunzi cha Madonna chimene inu mungachiwone.Ndipo ngati anthu atangokhazikitsa malingaliro awo mongachoncho, izo zikanakhala zosiyana.26 Koma pamene inu mufika popita kunja ndipo mwinamwakekuvala zosachuluka ngati bulauzi kapena zina zotero, ndiyenonkuzinyamulira mmwamba nokha kunja uko ndi ngolekera ndizinthu, zimene zimawoneka zopanda umulungu ndi zopangitsaamuna…Kodi inu mukuzindikira kuti umenewo ndi mzimu wamdierekezi uli pa inu? Kotero inu simukufuna kuti muzichitazimenezo, mlongo. Musati inu muzichita zimenezo; zimenezondi zopangitsidwa ndi Hollywood ndi msampha wa mdierekezi!Pamene inu muchita zimenezo, inu mumawapangitsa amunakuganizira chinthu cholakwika pa inu; ndipo pamene inumuchita izo, ndiye inu muli wolakwa pa kuchita chigololo ndimwamuna ameneyo, chifukwa inu munadziwonetsera nokhamwanjira imeneyo kwa iye. Inu simungachitire mwina momweinu munawumbidwira, koma zingopitani ndi kumakakhalamomwe Mulungu anakupangirani inu. Mukuona? Musatimuzidziyesera kudzipanga nokha chinachake chimene inusimuli. Zingokhalani anthu anthu. Izo si zoipa? Chabwinomwinamwake izo zayankhamafunso ena awinawake aponso.27 Atate athu, ife tikukuthokoza Inu lero chifukwa chaYesu Khristu ndi chifukwa cha kuwongoka kwa Mawuuku. Monga ine ndikukuwonerani Inu mwangwiro kwambirimukuwapangitsa mawu amenewo kufika pokwaniritsidwa,izo zikundipangitsa ine kukhala wotsimikiza mochuluka kutindikhalabe ndi Choonadi ndi mawu aliwonse a Choonadi.Kotero ine ndikupemphera, Atate, kuti Inu mutidalitse ifemmawa uno, anthu okondeka awa. Ndipo podziwa kutitepi iyi ikupita mu malo osiyana kumene ati akaimve iyongakhale ndemanga imene yangopangidwa kumene ija…inesindinati—izo sindinazichite mokonzekera; Inu mukudziwamtima wanga. Izo zinangobwera apo mu malingaliro anga,ndipo ine ndikukhulupirira Inu mumafuna kuti ine ndineneizo. Ndipo ine ndazinena izo, ndipo izo zatha tsopano. N—ndipo izo ziri ndendende kukhudzidwa kwanga ndi zimene inendikukhulupirira kuti Inumwandipangitsa ine kuzinena.28 Mulole mkazi aliyense amene adzamva izo kudutsa mumaiko ndi kuzungulira fukoli ndi padziko; iye atakadzichitirayekha manyazi ndi kuwona zimene zachitika, ndi kumakazivekayekha ngati dona ndiye, kuti iye asakhale ndi mlandu wachigololo. Cholengedwa chokongola, chokondeka monga Inumwachipereka, gawo la mwamuna, kuti akhale mwanjiraimeneyo k—k—kuti azikakopera tcheru cha mwamunayo kwaiye, awiriwo azikhala mmodzi, chifukwa iye anachokeramwa mwamunayo. Ine ndikupemphera, Mulungu, kuti mkazi

1010 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

azindikire kuti kukongola kwake ndi chimene iye ali, kulikongoperekedwa kwa mwamuna wake yekha. Perekani izi,Atate.

29 Ife tikupempha kuti Inumutithandize ife tsopano pamene ifetikuyesera kuti tiwafotokoze mafunso awa. Ndife osakwanirapa zinthu izi, koma mulole Mzimu Wanu wawukulu ubwere,Ambuye, umene uli chotikwaniritsa chathu; ndipo Iwoutayankha funso mu mitima yambiri. Ife tikukuthokozaniInu pa zimene Inu mwatipatsa ife: Mibadwo ya Mpingo, ndiZisindikizo, ndi…O, momwe Inu mwachitira nafe mu zinthuzazikulu zamphamvu zomwe zakhala zazikulu kwa ife, Ambuye,chifukwa ife tikuwona nthawi yamapeto ikuyandikira.

30 Tsopano, n—ndimaganiza kuti zinali zopindulitsa kapenazikanakhala zopindulitsa kwa Ufumu Wanu ngati inendikanafufuza pa anthu. Nthawi zambiri pansi pa kuzindikiraza mmitima ndi kuwona zinthu zambiri zosiyana, ndipo iwesungathe kusamalira pa chimodzi cha izo; kotero poganiza—inendinangowalola iwo kuti alembapo zimene iwo amaganiza pamtima wawo. Ndiyeno ine ndikhoza kulongosola malingaliroawo kuchokera pa chidutswa cha pepala chimene iwoalembapo, ndiyeno Inu mutipatsa ife yankho loyenera. Ife tonsetikudikirira, Ambuye. Bwerani mu kukhalapo kwathu, Ambuye,ndipo yendani chokwera ndi chotsika mu mipita, ndi kuchitanaye aliyense molingana ndi chifuniro Chanu. Ife tikupemphamu Dzina la Yesu. Ameni.

[Malo osajambulidwa pa tepi—Mkonzi.] Terry, kodiine…Kodi izo zikubwerabe, kumeneko pa m’bale-…inendinakhudza…Kodi ichi chikuzimitsa izo, kapena chirichonse?Icho sichikuvutitsa. Ine ndinakhudza icho ndi dzanja langa. Inesindimadziwa.

31 Tsopano, pamene ine ndikunena mobwereza tsopano,pamene ife tikuyamba, kwa—atumiki awo kapena anthu mumagawo osiyana a dziko, kapena amene ati adzamvere tepiyi,i—inu ndi (ngati tepiyi ili bwino bwino)—awa ndi mafunso apa mitima ya anthu amene ali akuno pa kachisi uyu, kumeneife tiribe chipembedzo, timangokhala ndi chiyanjano wina ndimzake. Ndipo ine ndikudalira kuti izo zikhala ziri z—zichotsamaganizo athu, kuti ife tidziwa zoti tizichita ndi kudziwamomwe tingamakhalire bwinoko mafunso athu akayankhidwa.Ine ndikudziwa, pa kungowawerenga iwo, iwo anali mdalitsokwa ine.

32 Tsopano, ine ndangowawunjika iwo apa mu mulu, ndipoine ndiziyang’ana ndipo pafupi maminiti faifi kuti ikwane 12,ine ndibalalitsa. Ndiyeno, nkubwereranso madzulo ano pa hafupasiti sikisi.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1011

Funso loyamba limene ine ndiri nalo, ine ndikukhulupirirakuti ndi mafunso asanu mondondana, olembedwa motaipa pakachidutswa ka pepala kachikasu.

236. Kodi izi zikutanthauza chiani? Mateyu 24:19: “Tsokakwa iwo amene ali ndi mwana, ndi kwa iwo ameneazidzayamwitsa mu masiku amenewo!”Mwachilendo, posadziwa kuti, ine ndinena izi pokhudza

mkazi, ndipo ndi izi mu nthawi ino, funso loyamba.33 Tsopano, Mateyu 24:19. Yesu anali atafunsidwa mafunsoatatu. Mu mafunso amenewa munali zakuti: Ndi liti pomweiti idzakhale nthawiyo pamene sipadzakhala mwala umodziutasiyidwa pa umzake? ndi, Nchiani chiti chidzakhalechizindikiro cha kutha kwa dziko? n—ndi mafunso atatu osiyanaIye anali—Iye anafunsidwa. Ndipo Iye akuyankha izo mwa njirazitatu zosiyana, akuyankha funso lirilonse. Kodi zidzakhalaliti pamene sipadzakhala mwana umodzi pa umzake? Ndipochidzakhala chiani chizindikiro cha kudza Kwanu? Ndipo ndichiani chomwe chiri chizindikiro cha kutha kwa dziko? NdipoIye akuyankha izo mwa njira zitatu zosiyana. Iye akuwauzaiwo pamene nthawi iti idzafike pamene sipadzakhala mwalaumodzi pa umzake; chomwe chiti chidzakhale chizindikiro chakudza Kwake; ndiyeno, pa kutha kwa dziko. Ndipo nthawizambiri, ngati inu simungati muyang’anitsitse mwatcheru,tsopano, momwe Iye akuyankhira (mwaona?), inu mungatengeizo mosokonezedwa ndi kuziponyera izo zonse mu nthawiimodzi; ndiye inu mwasokonezeka yense.34 Tsopano, mopanda kunyozetsa kwathu—kwa abale athuachi Adventist amene amazitenga izi momwe ziriri kuti ndi zamtsogolo. Polowa mu phunziro ilo la tsiku lachisanu ndi chiwiri:“Pempherani ndiponso kuti kuthawa kwanu kusadzakhale munthawi yachisanu kapena pa tsiku la Sabata,” anati (mwaona?),iwo adzakhala akusunga apobe Sabata. Si kuwaponyerakumbali abale amenewo, izo sizikanakhala monga-Mkhristukuti ndichite zimenezo, koma pongolinga kuti ndiziwongole izoapo. Mukuona?35 Zingatheke bwanji kuti dziko lonse la Chikhristulidzasonkhane mkati mwa khoma, ndipo makomawo salikutsegulidwa ndi kutsekedwa monga iwo ankachitira apo.Mwaona? Ndi kusiyana kwanji komwe izo zikanati zidzapange,kuti kaya itakhala nthawi ya chisanu kapena nthawi yachirimwe kwa anthu amene amakhala mudera lotentha.Mukuona? Izo zinali basi kwa Israeli yekha. Ndizo pansi panthawi pamene sipakanadzakhala mwala umodzi utasiyidwapa umzake. “Tsoka kwa iwo amene ali ndi mwana, ndi kwa iwoamene adzakhala akuyamwitsa mumasiku amenewo,” chifukwamayi amene ali ndi mwana (mukuona?), zikanakhala ziri zovutakuti iye athamange, ndi kwa iwo amene ali kuyamwitsa kwa ana

1012 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

awo kuti awanyamule iwo, chifukwa iwo akanati achokere kuYerusalemu kutuluka mu mzinda kupita mu—mpaka mu mapiria Yudea.36 Ndipo tsopano, ine ndikhoza kungokhala mmawa wonsepa chinthu chimodzi icho pamenepo, kungoti ndichipangeicho kumveka; koma ine ndingoyesera kuti ndigunde maloapamwamba amene ine ndingathe, mpaka izo zifike kwa anthu,ndiyeno nkupita ku funso lotsatira.37 Tsopano, Yesu anali atawauza iwo kuti iwo a… “Pameneinu mudzawona Yerusalemu atazingidwa ndi ankhondo, ndiyesiyani iye amene ali mmunda, asati abwererenso mu mzindakuti adzatenge chikhotho chake, kukatenga china chirichonsekuchokera mnyumba mwake; asati abwererenso mu mzindawokonse, koma athawire mu Yudea, pakuti iyo idzakhala ili nthawiyavuto siinakhalepo chiyambireni cha dziko.” Ndipo zonse izozinafika pochitika mu masiku pamene mkulu wankhondo waChiroma, Tito, anazinga Yerusalemu, anawutentha mzindawo,ndipo uko kunali kokha—ndipo anawapha anthuwo mpakamagazi anataikira pa zipata ndi kuyenderera k—kupitammisewu. Iye anawuzinga iwo. Ine sindikudziwa basi zakazingati zomwe zinali, zomwe iye anangowatenga ankhondo akendipo anabwera uko ndi kudzangomanga msasa kuzunguliramzindawo. Ndipo ngakhale anthuwo, akazi, ankawawiritsaana awo omwe ndi kumawadya iwo, kudya makungwa nathapa mitengo, maudzu nkutha pa nthaka. Izo zinali chifukwa chakuwakanaMawu.Ndi zimene zinachititsa izo. Ndiyeno…38 Tsopano, awo amene anali atawalandira Mawu, mongaJosephus, wazambiriyakale wamkulu akulembera…Iyeanawatcha iwo okudya nyama ya anthu, anati iwo ankadya thupila Mwamuna wotchedwa Yesu waku Nazareti, amene Pilatoanamupachika; ndipo iwo anabwera usiku ndipo anadzalibamothupi Lake, ndipo anthu awa analitengera ilo kwina ndipoankalidula ilo mzidutswa ndi kumalidya ilo. (Iwo anali kutengaMgonero, inu mukuona. Iwo sanali kudziwa.) Izo zinangokhalazoyankhulidwa zinkapita mozungulira, momwe iwo aliri nazolero za ife ndi Akhristu ena onse. Inu mukuona? Iwo amanenazinthu zimenezo, koma…39 Tsopano, anthu awo amene anali…Chifukwa, “Pempheranikuti kuthawa kwanu kusadzakhale mu nthawi ya chisanu,”Yudea anali kuchita chisanu. Mukuona, Khrisimasi? Tsopano,Yesu anabadwa chotani kumeneko ndiye mu mapiri ochitachisanu awo? “Pempherani kuti kuthawa kwanu kusadzakhalemu nthawi ya chisanu, ngakhalenso pa tsiku la Sabata,”mwaona, chifukwa pa tsiku la Sabata zipata zinali kutsekedwa,ndipo iwo akanati adzagwidwe mu msampha wawo womwe.Ngati Tito anakafika uko l—l—Lachisanu madzulo, iwo akanatiazingidwe mkati umo chifukwa cha Sabata, chifukwa zitsekozinali kutsekedwa. Zipata zinali kutsekedwa pa Sabata ndipo

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1013

sanali kuzitsegula. Uko kunalibe kulowa umo ndi kupita kunjakwa mzindawo pa tsiku la Sabata.40 Ndipo tsopano, inu mukuona zimene zinachitika? NdiyeIye anati, “Tsoka kwa iwo amene ali oyembekezera, ndi kwaiwo amene adzakhala akuyamwitsa mu masiku amenewo,”(mukuona?) chifukwa kuthawa ndi kuthamanga…Ndipomalingana ndi mbiriyakale, uko kunalibe mmodzi wa iwo ameneankakhulupiriramwaYesu nawakhulupiriraMawu koma ameneanali kuyang’anira kuti izo zichitike. Ndipo iwo anathawa, ndipoanapita kuchokera ku Yerusalemu kupita ku Yudea, n—ndipoanathawitsa miyoyo yawo, ndipo palibe mmodzi wa iwo…chifukwa iwo anachenjezedwa ndi M’busa wawo ndipo analikuyang’anira ora limenelo kuti libwere. Pamene iwo anamvakuti Tito anali kubwera iwo anachokako, anathawitsa miyoyoyawo, ndipo anatulukamomumzindawo.

Tsopano, funso lina likutsatiralo.237. Mateyu 24:24: “Ndipo pamenepo adzawuka aneneri

abodza—ndi akhristu abodza, ndi aneneri abodza, ndipoazidzawonetsa zizindikiro zazikulu ndi zodabwitsa.” Kodiife tidzawazindikira bwanji iwo?

41 “Pamenepo adzauka…” Mmenemo tsopano inumukubwera mpaka mu m’badwo wina. Mwaona? “…padzaukaakhristu abodza ndi aneneri abodza.” Khristu wabodza ndiwodzozedwa mwabodza, chifukwa Khristu ndi Wodzozedwayo.Ndi angati akudziwa kuti Khristu amatanthauza “Wodzozedwauyo”? Padzakhala pali odzozedwa mwabodzawo, ndipo iwoazidzadzitcha okha aneneri. Koma kodi inumuzidzawazindikirachotani iwo? Mwa Mawu; ndi momwe inu mumawaziwira iwo,mwa Mawu, ngati iwo akulondola. Kodi ife tidzawazindikirachotani iwo? Zidzakhala mwa Mawu. Ngati iwo ali…Ngatiiwo akunena kuti iwo ali nawo Mawu, ndiyeno nkumawakanaMawu, ndiye kulibe chirichonse kwa izo, ziribe kanthu zomweiwo akuchita. Iwo akhoza kumachiza odwala; iwo akhozakumatsegula maso a akhungu; ndipo nkumawakana Mawu,khalani kutali kwa izo. Musasamale chomwe izo ziri, khalanindi Mawu amenewo mosasamala zina (mwaona?), chifukwanthawi zambiri ine ndawonapo vuduu ndi mitundu yonse yazinthu zikuchitika pansi—pansi pa machiritso.42 Apa pali M’bale Sidney Jackson, Mlongo Jackson mmawauno ochokera ku South Africa. Iye akhoza kuima pano ndikutenga phunziro limenelo ndi kukuuzani inu kwenikwenizinthu zina za zimenezo kumeneko. Bwanji zedi, anthuamabwera kwa mafano ndipo amachiritsidwa. Mukuona,chifukwa chiani?43 Monga momwe Dr. Hegre anandinenera ine nthawi ijayi,zakuti ine ndimanena kuti mdierekezi sangathe kuchiza. Ndipoiye anati, “Munthu amene umaima pamaso pa anthu ochuluka

1014 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

momwe iwe umachitira, ndi fioloje yoperewera choncho,” anati,“kumanena kuti mdierekezi sangathe kuchiza.” Anati, “Ife tirinaye mkazi mwa oyandikana nafe momwe amavala apuronipa iye, ndipo amapita kumeneko; ndipo anthu amabweramomuzungulira iye ndipo amayenera kuti aziponyera ndalamamu apuroni iyo; ndiyeno iye amawasisita iwo ndi kuthotholatsitsi pa mutu wake ndi magazi kuchokera mu misempha yawon—ndi kuziika izo pa tsitsi ndipo amaziponyera izo kumbuyokwake; ndipo iye akakakamizidwa kuti atembenukire mmbuyo,matendawo amabwereranso kwa anthuwo. Ndipo,” anati, “satepa zana a iwo amakhala bwino. Ndiyeno iwe ukuti mdierekezisangathe kuchiza?”44 Ndipo ine ndinaganiza, “O, mai!” Ine ndinamulembera iyemomuyankha, ndipo ine ndinati, “Wokondedwa bwana:” Inendinati, “Ndi chinthu chachirendo kwa ine kuti mphunzitsi wasukulu yaukachenjede ya Chilutera angakhazikitse fioloje yakepa chomuchitikira mmalo mwa Mawu a Mulungu.” Mwaona?“Mawu a Mulungu amanena kuti Satana sangathe kutulutsaSatana. Izo zikukhazikitsa izo; Yesu ananena chomwecho.”Ngati Satana…Ndinati, “Ndiye inumukhoza kudabwamomweanthu awa amachiritsidwira podzera mzimenezo, mfiti imeneyo,ndi chifukwa chakuti anthuwo eniakewo amaganiza kutiiwo akufikira kwa Mulungu podzera mwa mfiti imeneyo.Ndipo machiritso amakhazikitsidwira pa chikhulupiriro, osatipa momwe iwe uliri wolungama, momwe uliri wabwino,kuchuluka kwa momwe iwe umasungira malamulo, kapenachirichonse chimene chiri, iwo amakhazikitsidwira kwathunthupa chikhulupiriro. ‘Zinthu zonse ndi zotheka kwa iwo ameneakhulupirira!’ Mwaona? Izo siziri pamaziko a momwe iwe uliriwabwino. Ine ndawawonapo achiwerewere akubwera pa guwandi kuchiritsidwa nthawi yomweyo ndipomkazi woyera kudutsapa nsanjayo nkuwaphonya iwo. Zedi, iwo ali pa maziko achikhulupiriro, ‘Ngati inu mungati mukhulupirire,’ osati pakulungama.”45 Yang’anani kumusi uku mu France kumene iwo amapita kuguwa lija la mkazi uja, amapita mmenemo ali mu zikuku ndipoamatulukako akuyenda, osati pa chinachake koma zamatsengamwangwiro, ngati chiri chirichonse, zamizimu—pa kupembedzamunthu wakufa. Mwaona? Ndipo komabe iwo amachiritsidwa,chifukwa iwo amaganiza kuti iwo akufikira kwa Mulungu.Tsopano, sikuti ndikuwanyozetsa anthu Achikatolika, inendikunyozetsa kachitidwe ka Chikatolika, monga momwe inendikuchitira ndi kachitidwe ka Chiprotestanti (mwaona?),zinthu zonse izi.46 Tsopano, atumiki, ine ndikudziwa kuti izi ziyambakukung’ambani inu, koma ine ndikuyankha mafunso; ndipoine ndiku—ine ndikufuna kuti inu mumvetse kuti (mwaona?)ine ndikungo—ndikungokuuzani inu Choonadi kuchokera

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1015

mu mtima wanga; Khristu patsogolo panga mwakukhozakwa kudziwa kwanga. Mwaona? Ndi kachitidwe konseko,ndipo kachitidwe kameneko kawapiringiza anthu ngati…Anthu amapita ndi kukajowina Chimethodisti, Chibaptisti,Chiprebateria, Chipentekoste, Chikatolika; ndipo iwoamaganiza kuti iwo akufikira kwa Mulungu pamene iwoakungopita kudutsa mu kachitidwe. Mulungu amalemekeza izonthawizina ndipo amawachotsera—matenda awo kuwachotsakwa iwo kudzera mu mafano. Chabwino, uko komwe kwaAkafula aku Afrika iwo analandira machiritso ndi mafanondi zina zotero (mwaona?), koma iwo amaganiza kuti akufikirakwa Mulungu.47 Inu mukuganiza kuti nani wa Chikatolika amapitandi kukajowina—unani wa Chikatolika chifukwa kuti iyeakufuna kuti akhale mkazi woipa? Iye amakajowina unaniumenewo chifukwa kuti iye akufuna kuti akhale mkaziwabwino. Mwamuna samapita kukajowina mpingo waKatolika basi kuti akhale mwamuna woipa; iye amapitakumeneko kukajowina kuti akhale mwamuna wabwino. Inusimuma…Kuti, “Chabwino, ndi chiani ichocho?” Ngakhalensoawo—ngakhalenso Amwenye aku India, kapena Achihindusamajowina Chihindu kuti akhale munthuwoipa.48 Pamene ine ndinapita mu kachisi w—wa Chijaini, kumeneine ndinafunsidwa kumeneko ndi wansembe—wonga papaatakhala pa pilo wamkulu, mapazi ake atapiringizidwira pansipake, atagwira zala zake za kuphazi—ndi kupenya koterokomwakuti iye amalemba chofanizitsa ndi Lemba la Masalmo23 ndi maso ake akuyang’ana apoyera pa chidutswa chachitsulo chimene chinali chochepera kuposa—chosakula kuposakotala la inchi. Tsopano, ndipo izo ndi zopitirira kulingalirakwa umunthu kulikonse kuti alembe zimenezo, ndipo iyeanazizokota izo pamenepo ndi maso ake achibadwa; ndipo iyeanali mwamuna wa usinkhu wa zaka forte kapena kupitirira.Mwaona?49 Bwanji zedi, i—inu mumangokhala mozungulira apa,mumangomvera za Amethodisti, Abaptisti, Apresbateria; inumukuyenera kuti muzituluka ndi kupita ku minda ya umishoninthawi ina. Kukawona zinthu zoti zikutseguleni maso anu!Mwaona?50 Tsopano, inu mukuganiza kuti masisitere onse aja atakhalauko; iwo samati nkomwe—iwo samaphika; iwo samadya; iwoamachita kupempha chirichonse chimene iwo amalandira. Iwosangati—iwo amakonza zikolopa zazing’ono ndi manja awo kutiazikolopera nyerere ndi zinthu kuzichotsa pa msewu, chifukwaiwo amakhulupirira kusintha kwa cholengedwa; iwo akhozakukhala akuponda pa wachibale wawo. Samaponda pa nyerere,samapha ntchentche, kapena kalikonse; samatenthetsa nkomwempeni kuti achite opareshoni pa chala. Amamusiya munthuyo

1016 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kuti afe, chifukwa iwo akapha jeremu; iyo ikhoza kukhalaili w—wachibale wawo wina atabwereranso. Mwaona? Iweumapitirira kukhala bwinoko, ndi bwinoko, bwinoko; potsirizaiwe umadzakhala munthu wokhalapo, munthu wokhalapowabwinoko, ndipo popitirira pitirira monga, mpaka iweumadzakhala kamulungu. Kumangopitirira pitirira pitirira, ndi,kumasintha, kumakhala wabwinoko ndi bwinoko.51 Tsopano, iwo samachita zimenezo kuti akakhale anthuoyipa. Iwo amachita zimenezo ndi kuonamtima, koma inumukuona, “Pali njira imene imawoneka yolondola kwamunthu.” Pali chinthu chimodzi chokha, anthu, chimene inendikudziwa kuti ndikuuzeni inu ng—ngati kalasi mmawa uno pamafunso amenewa, ndicho Mawu, Mawu a Mulungu. Ndiye inumuzikhulupirira kuti Yesu Khristu ali Mawu amenewo, ndipoMawu amenewo apangidwa thupi pakali pano pakati pathu,kukwaniritsa ndendende zimene Iye anati Iye akanadzachitamu m’badwo uno. Chabwino.

Tsopano, umo ndi momwe inu mumawadziwira iwo, osatimwa mpingo wawo, osati mwa kachikhulupiriro kawo, osatimwa chizindikiro chawo, osati mwa zipembedzo zawo, osatimwa machiritso aliwonse, osati mwa chirichonse, koma mwaMawu. Mwaona?238. Mateyu 24:26 (lotsatira) akuyankhula za “chipinda

chinachake” ndi “mu malo a mchipululu.” Kodi izizikutanthauza chiani?

52 Izo zikutanthauza kuti kudzakhala kuli wotsutsakhristu,wotsutsa-kudzoza, zina zotero. Ndipo kodi anti ndi chiani?Anti-ndi “kutsutsa.” Zidzakhala zolengedwa izi zomwe zikuwatsutsaMawu. Ndipo izo zidzakakhala ziri ku chipululu ndi mu zipindazobisika.” Ndiye Iye anati, “Musati muzipita mozidzatsatira izo.Zikhalani kutali ndi izo.” Mwaona?

Tsopano, funso lachinai:239. Mateyu 24:28: (Munthuyo akubwera nazo ndithu

mmusi. Iwo sanalembepo dzina apo; inde iwo atero.Ine ndikhululukireni. Ine sinditchula maina amenewa,chifukwa si zofunikira. Mukuona?) Mateyu 24:28: “Pakutikulikonse kumene kwafa nyama, kumeneko mphunguzimadzasonkhana palimodzi.” Kodi nyamayo ndi ndanindipo mphunguzo ndi ndani?

53 Tsopano, limenelo ndi funso labwino, palibe cholakwikandi zimenezo! Kodi nyamayo ndi chiani? Nyama ndi chomwemphungu zimadyapo. Tsopano, mphungu imatengedwa muBaibulo, mneneri. Mneneri ndi mphungu. Mulungu—Mulunguamadzitcha Iyemwini mphungu, ndipo ife ndi “timphungu”ndiye, o—okhulupirira. Inu mukuona? Ndipo kodi nyama ndichiani imene iwo amadyapoyo? Iyo ndi Mawu. Kulikonsekumene kuli Mawu, chikhalidwe choona cha mbalame

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1017

chimadziwonetserako chokha. Mwaona? Mphungu, imeneimafuna nyama yatsopano, iye amayenera kukhala ndi nyamayake yatsopano. Iye si k—khungubwe (mwaona?), iye ndimphungu. Inu simungatengere zinthu zachipembedzo kwaiye; iye amayenera kukhala ndi chakudya cha mphungu;imeneyo ndiyo nyama yatsopano kwambiri, osati zimene Moseanazichita, osati zimene winawakenso anachita, osati zimeneSankey, Finney, Knox, Kalvin, koma pakali pano, Nyamaimene yaphedwera kwa tsiku lino. Ndipo limenelo ndilo gawola Khristu amene anafera kuti awapangitse Mawu awa kutiatsimikizidwire. Ndi chimene iwo amadya pa icho. Mukumvetsazimenezo? Onani, mwaona?54 Osati zimene Nowa anachita, zimene Mose anachita, izozinali zitsanzo; ife timawona ndi kuwerenga zimene iwoanachita, koma ndi zimene Iye analonjeza kuti azichita tsopano.Iye anali Mawu kumbuyo uko; imeneyo inali Nyama ya tsikulimenelo. Tsiku l—laWesile panali nyama ya tsiku limenelo; tsikula Lutera panali nyama ya tsiku limenelo; koma iwo sabwererammbuyo kwa iyo. Imeneyo yavunda kale. Zimene zinasiyidwaziyenera kuti ziziwotchedwa, monga za Mgonero ngakhalenso;musati muzisiyira izo kwakam’badwo kotsatira. Baibulo linatipamene inu mutenga Mgonero, zimene zatsalira za iwo, musatingakhale muzisiye izo mpakammawa; muziziwotcha izo. Koterotizilozera mmbuyo kwa izo? Ayi, bwana! Ife tiri ndi Chakudyachatsopano lero; amenewo ndi Mawu amene alonjezedwerakwa ora lino, akhale akuwonetseredwa mu ora lino. Ndikokumene mphungu ziri—kumene kuli nyama. Ife tikanakhozakukhala nthawi yaitali pa zimenezo, koma ine ndikutsimikizainumukumvetsa zimene ine ndikutanthauza.

Chabwino, funso lachisanu:240. Kodi Mkwatibwi adzasonkhanitsidwa palimodzi mu

malo amodzi pa mkwatulo, ndipo kodi izo zidzakakhalaKumadzulo?

55 Ayi, sizikusowa kuchita kukakhala kumeneko. Eya,Mkwatibwi adzasonkhana palimodzi mu malo amodzi. Izondi zoona, koma osati chisanachitike chiukitsiro. Mwaona?“Pakuti ife amene tiri amoyo ndipo titatsalira mpaka kukudza kwa Ambuye…” Aefeso—ll Atesalonika mutu wa 5, inendikukhulupirira ndi pamene pali. “Ife amene tiri amoyo ndipotitatsalira mpaka pa kudza kwa Ambuye sitidzawalepheretsa(kapena kuwatchinga) iwo amene akugona (konsekonse); pakutilipenga la Mulungu lidzawombedwa, ndipo akufa mwa Khristuadzauka, ndipo ife tidzakwatulidwira mmwamba palimodzi ndiiwo kukakomana nawo Ambuye mu mlengalenga.” Chotero,Mkwatibwi yense adzakhala palimodzi pamene Iye akupitakukakomana nawo Ambuye. Mwaona? Iye adzakhala palimodzi,koma izo sizikutanthauza kwenikweni kuti ife—iwo onseadzakhala ali mu malo amodzi monga chonchi; chifukwa

1018 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Mkwatibwi akugona mu fumbi la dziko lapansi kuzunguliramdziko, kuchokera kozizira mpaka kotentha, ndiponso k—kuchokera kummawa mpaka kumadzulo, kuchokera kumpotompaka kummwera.56 Yesu anati, “Pamene Mwana wa munthu ati adzawonekere,”pakuti anati, “izo zidzakhala monga kuwala kumene kumawalakuchokera kummawa ngakhale mpaka kumadzulo.” Chinthuchonsecho, apo padzakhala pali chiukitsiro, mkwatulo, ndipokutali Iye adzapita. Ndipo Iye asanapite konse mmwambakukakomana naye Iye…57 Tapenyani nzeru ya Ambuye. Tsopano, tiyeni tinene, mwachitsanzo, poyankhula izi…ine ndikunena izi kudzera mumalingaliro a chisomo ndi chikhulupiriro mu Mawu, pameneine ndikuti “ife.” Ine ndikudziponyera ndekha mmenemo ndiinu nonse ndipo ine—ndi Thupi lonse la Khristu, konsekonse. I—ine ndikukhulupirira zimenezo. Pamene ine ndikuti “ife” ndiye,ine ndikutanthauza, mwa chisomo i—ine ndikuzikhulupirirazimenezo. Mwa chikhulupiriro ine ndikukhulupirira izo mwachisomoChake, kuti ife tidzakhala tiri pakati pa anthu amenewoamene ati adzakwatulidwire mmwamba.58 Tsopano, chinthu choyamba chimene chikuchitika pameneife taukitsidwa…Iwo amene ali amoyo adzakhala basialipobe…Chiukitsiro chidzakhalapo umo poyamba, chiukitsirocha iwo amene akugona. Padzakhala pali nthawi yogalamuka,ndipo iwo amene ali kugona mu fumbi tsopano, osatiiwo amene akugona mu tchimo, chifukwa iwo azidzagonamopitirirabe. Iwo sakuuka mpaka zaka chikwi zina. Komaiwo amene ali—amene akugona mu fumbi adzazutsidwapoyamba, ndipo iwo adza—matupi achivundi awa adzavalachisavundi mu chisomo chokwatulitsa cha Ambuye. Ndiyenoife tonse tidzabwera palimodzi. Ndipo pamene iwo adzayambakubwera palimodzi, ndiye ife amene tiri amoyo ndipo titatsaliratidzasinthidwa. Matupi achivundi awa sadzawona imfa, komabasi mwadzidzidzi, padzangokhala ngati kusesa kwapita pa ife,ndipo inu mudzasintha. Inu mudzasintha nkubwerera mongaAbrahamu anachitira, kuchokera ku mwamuna wachikulirekukhala mwamuna wamng’ono, kuchoka ku mkazi wachikulirekukhalamkazi wamng’ono. Nchiani kusintha kwadzidzidzi uku?Ndipo pakapita kanthawi i—inu mukuyenda ngati lingaliro,ndipo inu mukutha kuwawona awo ndiye iwo awukitsidwakale. O, ora lakelo! Ndiye ife tidzasonkhana limodzi nawondiyeno nkukhala titakwatulidwira mmwamba limodzi nawokukakomana nawo Ambuyemumlengalenga.59 Si zofunikira ayi, ngati amalume ako anaikidwa ukokummwera kwa Kentucky, ngati iwo ali woti abweretsedwe muIndiana, kapena ataikidwa mu Indiana kuchita kutengedwerakummwera kwa Kentucky. Ziribe kanthu kumene iwo ali…Iwo amene anafera mnyanja adzauka kuchokera mu nyanja. Iwo

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1019

amene anawonongedwa mu bwalo lija nadyedwa kwathunthundi mikango, iwo amene anaponyedwera mu ng’anjo yamoto ndipo palibe ngakhale mafupa adzakhale atasiyidwakapena fumbi, iwo adzawuka apobe! Kaya iwo anali kuRoma, kapena bwalo la ku Roma, kapena kaya iwo analiku nkhalango zotentha za Kummwera, kapena mu zigawozachisanu za Kumpoto, iwo adzawuka kuchokera kwa akufandi kusinthidwa ndi kuwukitsidwa; ndipo amoyo adzasinthidwamu kamphindi, mkuthwanima kwa diso ndi kukwatulidwirammwamba palimodzi.

60 Tayang’anani pa amishonare amene anafera uko mu mindaya ku Afrika. Tayang’anani pa iwo amene anafera uko m—mu—zigawo zachisanu za Kumpoto. Tayang’anani pa iwo ameneanafera mu bwalo, konsekonse mdziko monse, ku Congo, ndikonse kuzungulira dziko. Iwo anafera kulikonse, China, Japan,kuzungulira dziko; ndipo kudza kwa Ambuye kudzakhala kwakonsekonse, mkwatulo uwu udzatero.

61 Penyani kusinthako. “Adzakhala ali awiri mu kama;ine ndidzatengapo mmodzi ndi kusiyapo mmodzi,” mphindiyomweyo, “Adzakhala ali awiri mmunda; ine ndidzatengammodzi ndi kusiya mmodzi,” mmodzi kumbali yamdima yadziko ndi wina ku mbali yowala ya dziko. Mwaona? Iwoudzakhala mkwatulo wa konsekonse. Inde, Mpingo wonseudzakhala uli palimodzi, koma chitachitika, chitachitikachiukitsiro ndipo mkwatulo utalowamo.

62 Tsopano, ngati umo si momwe inu mukuziwonera izo,bwanji, zonse ziri bwino tsopano. Ine sindiri kuyankhulandendende pamene ine ndikunena izo; ife tikujambula izi.Inu mukuona? Ndipo pakhoza kukhala atumiki ena ameneakutsutsana nazo izo. Zonse ziri bwino.

241. Wokondedwa M’bale Branham, funso langa liri paubatizo. Ndi liti pamene munthu amapulumutsidwa?Ine ndamvapo kuti ndi pamene munthuyo akhulupirira.Ena amanena kuti pamene iwe walandira MzimuWoyera iwe wapulumutsidwa, ngakhale kuti iweusanabatizidwe mu madzi, monga momwe zinaliri ndiKorneliyo pa Machitidwe 10:47. Ena amanena kuti Pauloanapulumutsidwa pa njira yaku Damasiko, koma muMachitidwe 22:16, amanena kuti iye anali akadali nawomachimo ake masiku atatu pambuyo pake. Kodi munthuangabatizidwe mwa Mzimu Woyera momwe Korneliyoanachitira, ndi kukhala nawobe machimo ake, pakuti iyeanali asanalandire ubatizo wa madzi, pa—kapena kodimunthu samakhala ndi njira yopitira Kumwamba mpakaiye atalandira ubatizo wa madzi, ngakhale kuti iye alinawo Mzimu Woyera?

1020 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

63 Tsopano, mzanga wofunika…Tsopano, m’bale uyuwalembapo dzina lake; ine sindikumudziwa iye, koma iyewalembapo dzina lake. Koma i—ine sinditchula maina ake,chifukwa izo si zofunikira; chifukwa anthu ena azifika kwaiwo nkumati, “Chabwino, i—ine sindikugwirizana nanu pa izindi izo.” Mukuona? Ndipo ine sindimatchula basi maina ayi.Zambiri za izi ziri nawo maina, koma i—ndi za kwa ine basi.Mwaona? Ine ndikuzibwezera izi mkati umu, kuti ine ndithekuzisunga izo. Kotero ndi zolemba za buluu chotero; zina za izondi zotaipidwa ndi njira zosiyana.64 Tsopano, funso pano poyamba linali: “Ndi liti pamene iweumapulumutsidwa?” Ndipo lotsa—lotsatira ili, “Kodi machimoangachotsedwe kunja kwa ubatizo wa madzi, pakuti Kornelioanalandira Mzimu Woyera—iye ndi apa banja ake—ndipo analiasanabatizidwe apobe mu madzi.” Ndipo Paulo anali asana—iye atakomana nacho chomuchitikira chake p—pa njira yakuDamasiko, iye, nayenso, anali akadali nawo machimo akepa iye mpaka iye atabatizidwa; chifukwa iwo amati (inendawawerenga Malemba onsewa modutsa aponso kuti ndikhalewotsimikiza)…Ndipo kotero izo zinali…Iye anati, “Uka ndipopita pomwepa molunjika ndi kukabatizidwa, kumatchula paDzina la Ambuye—ukabatizidwe, ukhale kuti machimo akoakhululukidwe (achotsedwe), n—ndi kumapita ukutchula paDzina la Ambuye.”65 Ndiyeno, “Kodi ubatizo wa Mzimu Woyera…munthuakhoza kubatizidwa ndi Iwo ndi kukhala uli nawobe machimoawo ndipo kusa—ndi kusabatizidwamumadzi.”66 “Kodi njira ya munthu yotsimikizika kuti akupitaKumwamba pamene wabatizidwa, ngakhale iwo atakhala alinawo Mzimu Woyera; komabe iwo ayenera kuti abatizidwemu madzi, njira yawo isanakhale yotsimikizika kupitaKumwamba?” Tsopano, ine ndikukhulupirira…Tsopano, inesindi—ine sindikumudziwa m’bale uyu, ndipo ilo ndi labwinokwambiri ndi funso la luntha. Ndipo ilo liyenera kuchitidwanalo motalika, chifukwa ndi zofunikira kuti ife tizidziwa zinthuzimenezi. Mwaona?67 Tsopano, ine ndikukhala ngati ndikukhulupirira kutim’baleyu mwina akunena kwa ine kapena akundipangitsa inekuti ndinene izo (kapena mwinamwake iyeyo amakhulupiriramu zimenezo, ine sindikudziwa) ndi—za chinachake chimeneine ndiri kuganiza kuti chiri basi—pang’ono pokha mosiyanakwa chenicheni, chikhulupiriro choona mu Mawu. I…Izizikumveka ngati kuti m’baleyu akuti…Tsopano, zomweziri zabwino bwino, M’bale; mukhoza kukhala muli pano;ndipo zimenezo ndi zabwino. I—ine ndikuganiza zimenezo ndizabwino…Ine ndikukondwa kwambiri kuti inu munaziyikaizo pamenepo. Tsopano, mwaona? Koma ine sindimakhulupiriramu kubatizidwa mmadzi kuti usinthike (mwaona?), chifukwa

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1021

pamene iwe utero, izo zimawadumpha Magazi. Mwaona? Iweumabatizidwa mu madzi kuti uwonetsere kuti kusinthikakwachitika. Mwaona? Izo ndi zakunja chabe—chiphiphiritsocha kusinthika. Chinthu chonsecho chimakhazikika mwaulemupa kukonzedweratu. Mwaona? Koma ife sitimadziwa ameneali ndi amene asali; chotero, ife timalalikira Uthenga. Mwachikhulupiriro ife timangopita tikulalikira.68 Koma pa kusinthika tsopano, apo ndi pamene inendimasiyana ndi abale aumodzi. Ndipo inu abale aumodziamene mukumvetsera tepi iyi ya mafunso, ngati iyoingadzagwere mu ofesi yanu, kapena mu nyumba mwanu,kapena pakati pa inu anthu amene muli anthu aumodzi, musatimundimvetse molakwika ine, tsopano, kuti i—i—basi chifukwachakuti ife sitigwirizana.69 Ine ndi mkazi wanga sitigwirizana; zedi ife timatero. Inendimamuuza iye kuti ine ndimamukonda iye, ndipo iye amatisakukhulupirira kuti ine ndiri. Kotero nd—kotero ndiye ifendithudi sitimagwirizana, koma ine ndikukuuzani inu, ifendithudi timapitirira limodzi bwino bwino.70 Tsopano zindikirani. Mwinamwake ine sindimasonyezazizindikiro zokwanira kwa iye, zimene ine ndimachita.Koma ine ndimakhala kunja ndikulalikira, ndiye ndikabwerakunyumba ndipo ndimatenga ndodo yanga yowezera ndi kupitakukawedza. Mukuona? Koma pansi mu mtima mwanga inendimamukonda iye; ine ndimangoyenera kuti ndikakhale kutalindi iye, ndizo zonse.71 Tsopano, zindikirani mu izi…Tsopano, ngati ifesitigwirizana, zonse ziri bwino; koma inu mukuona, madzisamachotsa machimo; ndi kuyankhira kwa ku chikumbumtimachako chabwino.72 Tsopano, ine ndikukhulupirira chifukwa chimenePaulo anayenera kuti abatizidwe pamenepo, chifukwa zirimovomerezeka ndi zofunikira mu Baibulo kuti ife tizibatizidwa.Chifukwa ine nditenge mobwerera mmbuyo momwe kwa ichindiye: pamene wakuba anali atapachikidwa pa mtanda…Ndipo iye anafa wopanda kubatizidwa konse, ndipo komabeali ndi lonjezo kuti Yesu akanati akakomane naye iye muParadiso tsiku limenelo—muParadiso, osati muMadera a otaika,chifukwa inali nthawi yoyamba yomwemwayiwo unaperekedwakwa iye.73 Ndipo ine ndikukhulupirira zikhalidwe zomwezo zinali ndimitima imeneyo ya aku nyumba ya Kornelio pamene iwoanali atalandira Mawu a Mulungu ndi kukondwera. NdipoMzimu Woyera ndiwo Mawu amenewo akapatsidwa moyo,ndipo Iwo anali atapatsidwira moyo kwa iwo. Ndicho chifukwaMzimu Woyera unayamba kuyankhula mu malirime ena ndi

1022 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kumalosera. Inali mitima yolandira ya anthu imene Mawuanagweramo, powona zauzimu zonsezo.74 Ndi zimene zimandidodometsa ine lero mu ora ili limeneife tiri kukhalamo. Pambuyo pakuti gulu lija la Aromalinali lita—ndi Agriki, monga iwo anali, anali atangowonakuwonetseredwa kwa masomphenya kukutsimikiziridwa,Mzimu Woyera unadzidzimutsa kwambiri mitima imeneyompaka pamene Petro anali chiyankhulire mawu awa, MzimuWoyera unagwera pa iwo. Mwaona?75 Monga ngati…Onani, Kornelio anati, “Pitaukamuitane…” Iye anali kenturio, ndipo izo zikuchokera ku“sentare” ndi zochokera ku zana. Iye anali woyang’anira amunazana. Iye ndi senturio wa Chiroma; ndipo iye i—iye anawonamasomphenya pamene iye anali akupemphera, ndipo Mngeloanabwera kwa iye. Iye anali mwamunawabwino. Iye anati, “Pitauko ku Yopa. Simoni wina, wofufuta zikopa, ndipo kuli winawotchedwa Simoni Petro. Iye ali pamwamba…Iwe ukamupezaiye kumeneko, ndipo iye abwera adzakuuze iweMawu.”76 Chabwino, iye anaganiza kuti masomphenya awo analiowoneka enieni kwambiri. “Ine sikuti ndinali ndikugona;ine ndinali ndikuyang’ana kumene pa—Mngelo.” Kotero iyeanawatumiza asilikari ake ena okhulupirika kumeneko.77 Ndipo ali kumeneko, Mulungu anali akumukonzekeretsamtumwiyo ku mapeto ena a mzere awo. Ndipo Iye anati,“Tsopano, dzuka.” Iye anati…Powona kuti iye analipamwamba pa nyumba apo akuyembekezera—Mayi Simonikuti akonze chakudya. Ndipo pamene iye anali pamenepo…Iyeanali wa njala, mwinamwake pakuyenda, atumwi, kudutsa—muzipululu. N—ndipo anali atagona pamwamba apo panyumbachisanafike chakudyacho, pamwamba pa nyumba, mongachinali chizolowezi. Akumachitabe chinthu chomwecho,amagona pamwamba pa denga apo, ndipo iwo amapita pansi ndimakwerero ndipo nthawizina masitepe ndi zinthu, kuchokera padengalo—kukhala pamwamba apomu chisisira chamadzulo.78 Koma mtumwiyo anagona tulo, ndipo pamene iyeanali akugona, iye anapita mopyola kugonako nalowa muchizimbwizimbwi; ndiyeno iye anawona chinsalu chikubwerapansi chiri ndi zodetsedwa zonse ndi zinthu mmenemo, ndipoiye anamva Liwu likuti, “Dzuka, ipha ndi kuzidya.”

Iye anati, “Si choncho, Ambuye, palibe kanthu kanayambakalowamkamwamwanga kali kodetsedwa.”79 Tsopano, onani, awo ndi masomphenya. Tsopano, penyani!Zimenezo zikuyenera kuti zitanthauziridwe. Tsopano, izozikuwoneka ngati Petro apita paulendo wokasaka ndipoakapeza mtundu wina wa nyama imene iye sanayambe wadyapokale ndi kudzayesera kuti ayidye iyo. Iye anati, “Si choncho,

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1023

Ambuye, i—ine sindinayambe ndakhala ndi chirichonsechosayera chinabwera mumilomo yanga.”80 Iye anati, “Usati uzitche izo zoyera zimene ine ndazipanga—zosayera zimene ine ndazipanga kuyera.” Anati, “Dzuka, kuliamuna akukudikirira iwe pa chipata. Pita, usati ukaikirekalikonse.” Nthawi yomweyo iwo anali akugogoda pa chitseko.[M’bale Branham agogoda pa guwa—Mkonzi.]81 Tsopano, mwaona? Ndiyeno pamene iye anamupezamwamuna uyu pamenepo, asilikari okhulupirika awa, basimogwirizana ndi masomphenya…Ndipo apa iwo anabwererandi mwamuna yemweyo amene Mulungu anali atamunena mumasomphenya—munthu wosadziwika, nsodzi wamng’ono basiwosadziwika. Koma pakati pa gulu laling’ono ilo, izo zinalizodziwika kwambiri kuti iye anamupeza nsodzi wamng’ono uyu.Ndipo ndi uyu apa akubwera kuno kudzalowa mu nyumbayitsopano, malo omwewo amene iye anawona masomphenya.Kornelio anawasonkhanitsa anthu onse palimodzi nati, “Pakuti,ziri ndendende basi momwe ine ndinaziwonera izo.” NdiyenoPetro anaimirira apo ndipo anayamba kuyankhula momweiwo analandirira Mzimu Woyera, ndipo pamene iye analichiyankhulire…! Iwo anawona chirichonse mwangwirokwambiri mu dongosolo la masomphenya amodzi. Gulu laanthu amene anali Amitundu, amene anawaona masomphenyaamodzi akuwonetseredwa, ndipo iwo anamva Mawu a Choonadia momwe iwo akanati alandirire Moyo; ndipo Mzimu Woyeraunagwa pa iwo asanabatizidwe nkomwe.82 Kodi izo zikuyenera kuchita chiani kwa kachisi uyu mmawauno? Odwala, osautsika, akhungu, ogontha, osayankhula,w—wochimwa, chirichonse…Tangoganizani, kuchokeramwa zinthu zikwi khumi, palibe nthawi imodzi zinayambazalepherapo dontho limodzi! Bwanji, izo zikuyenera kuyatsamitima yathu lawilawi!83 Tsopano, tsopano, iye apobe, pamene anali chiyankhuliremawu awa, Mzimu Woyera unagwa. Ndiye Petro anati, “Kodiife tingaletse madzi, powona kuti awa alandira Mzimu Woyeramonga ife tinachitira.” Ine ndikukhulupirira machimo awo analiatapita kale, pakuti Mzimu Woyera sukanati ubwere mkatimo;ndipo Iye sakanati abwere umo kupatula ngati chikanakhalachotengera chokonzedweratu. Iye ankadziwa kuti iwo akanatiatsatire. Iye ankadziwa…84 Ine ndikukhulupirira Paulo, chifukwa chimene iyeankayenera kuti abatizidwe kachiwiri chinali, iye analiatawazunza Akhristu. Ndiko kulondola. Ndipo Iye, Mulunguankadziwa, chifukwa Iye anati, “Ine ndamusankha iye,” Iyeanatero kwa Anania, mneneri. Pamene Iye anadziwa kuti Sauloanali kumeneko mu chipinda, nkhope itadetsedwa ndi masoatadetsedwa, ndipo i—iye anali atapemphera molimba kwambiri

1024 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ndi fumbi paliponse pa iye, ndipo iye anachititsidwa khungukuchokera ku Lawi la Moto limene linawonekera kwa iye panjira wa kumeneko; ndipo Iye anati, “Ine ndamusankha iyechida cha kwa Amitundu.” Mulungu ankadziwa zimenezo—kuti Anania akanati akhoze kumubatiza iye mu Dzina la YesuKhristu mu Mtsinje wa Damasiko masiku atatu patsogolopake. Koma ine ndikukhulupirira kuti machimo ake analiatakhululukidwa kale, koma iye ankayenera kuti achite izikuti asonyezere kwa dziko. Ndipo ine ndikukhulupirira kutiicho ndi chifukwa chake ife timayenera kuti tizibatizidwa muDzina la Yesu Khristu. Ndipo ine ndikukhulupirira kuti mbewuyokonzedweratu idzatha kuziwona zimenezo, ndipo ndi iwookha ati adzaziwone izo.85 Tsopano, abale a chikhulupiriro chautatu, ine sindirikuponyera izi kumbali kwa inu, m’bale wanga wokondedwa,ine ndikungoyankha mafunso. Ine ndikungopereka malingaliroanga owona a izo. Tepi iyi ikhoza nthawi ina kukathera muAfrika. Ine ndikukhulupirira kuti ife tiri mu mithunzi ya kudzaKwake. Ife tonse tikukhulupirira zimenezo.

Ine ndiri nawo abwenzi ofunika, a DuPlessis ndi aSchoeman, ndi onse, Yeager, ndipo iwo abale abwino m—mu South Afrika. Koma nthawizonse pali winawake ameneamangoima bwino bwino mu moyo wa munthu. Ndipo mwaanthu onse amene—ndipo ine ndimawakonda iwo mokondekabasi momwe ine ndimamukondera m’bale uyu, mofunikira basi,koma M’bale Jackson ndi mkazi wake nthawizonse ankaimabwino mumoyo wanga. Ine sindimatha basi kumvetsa zimenezo;i—iye ankaima bwino. Tsopano, kumeneko kuli JustusDuPlessis,mzanga wapachifuwa, ndipo o, ochuluka kwambiri a amenewoabwino, abale abwino Achiafrikani ndi alongo.86 Chabwino, chifukwa chiani M’bale Jackson ndi mkaziwake anali kundiimira bwino ine? Chifukwa iye anali msaki?Ayi! Chifukwa ine ndiri nawo abwenzi ambiri abwino osakakumeneko. Koma nchifukwa chiani iye amaima bwino? Ndipobwanji? Ngati inu mukanati mungodziwa chinsinsi cha kuserikwa zonse izi. Koma ine sindimawauza anthu zinsinsi zonsezimene ine ndimazidziwa. Pakuti, chifukwa chiani izo zinalikuti pa ora lomwelo limene Ambuye anati, “Uyankhulanendi Sidney Jackson ku South Afrika,” Ambuye anayankhulakwa Sidney Jackson kuti abwere kuno? Lamlungu lapitaloiye anabatizidwa, iye ndi mkazi wake, mu Dzina la YesuKhristu, komwe kuno mu nthawi ya mwamthunziyi. Onani,okonzedweratu ku cholingacho. Mwaona?87 Tsopano, ine ndikukhulupirira kuti iwe—uma—pulumutsidwa pa kumulandira Yesu Khristu. Ndipo ubatizowa madzi ndi kuwonetsera kwa kunja koti usonyeze kutichinachake mkatimo chachitika, chifukwa madzi alibe ukoma;

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1025

ndi choyimira chabe. Ndipo ine ndikukhulupirira kuti iweumapulumutsidwa pamene iwe…88 Tsopano, pali anthu ambiri (ndiroleni ine ndiziwongoleizi kwa m’baleyu)…Pali anthu ambiri amene ali—amati iwoanapulumutsidwa; ambiri amabatizidwa mu Dzina la Yesu;ambiri amayankhula mu malirime, ndipo ali ndi mitunduyonse ya zisonyezo za Mzimu Woyera, ndipo apobe asaliatapulumutsidwa nkomwe. Uko nkulondola. “Ambiri adzadzakwa Ine mu tsiku limenelo nati, ‘Ambuye, kodi ine sindinakhalendikulosera mu Dzina Lanu?’—mlaliki—‘Kodi ine sindinali muDzina Lanu kutulutsa ziwanda ndi kuchita ntchito zambirizamphamvu.’” Iye adzati, “Chokani kwa Ine, inu ochitamwa kusaweruzika; Ine sindinali kukudziwani nkomwe inu.”Mwaona? Kotero zinthu zonse izo, komabe i—i—izo ndiMulungu;izo ziri mmanjaMwake. Koma pamene ine ndiwona izo…89 Inu mukuti, “Chabwino ndiye, nchifukwa chiani inumumawaitaniranso anthu kuti adzabatizidwenso?” Ndichifukwa chakuti ine ndikutsatira ndondomeko ya pachiyambi.Ife sitingathe kutaya ndondomeko imeneyo.90 Tsopano, ife timutenge mtumwi Paulo pamene iyeanawapeza ophunzira ena ake amene anali anthu odabwitsa.Ine ndikukhulupirira iwo anali opulumutsidwa, ndipo komabeiwo anali asanabatizidwe mu Dzina la Yesu Khristu, ngakhaleiwo anali atabatizidwa (Machitidwe 19). Paulo podutsa kumaikoa gombe la kumtunda kwaAefeso; iye anawapeza ophunzira ena.Ndipo iye anati kwa iwo, “Kodi inu munalandira MzimuWoyerachikhulupirireni chanu?”

Ndipo iwo anati kwa iye, “Ife sitikudziwa za MzimuWoyera,ngati kuli MzimuWoyera uliwonse.”

Iye anati, “Ndiye inumunabatizidwira ku chiani?”Iwo anati, “Ife tinabatizidwa kale. Yohane anatibatiza ife,

mwamuna yemweyo amene anamubatiza Yesu.” Umenewo ndiubatizo wabwino ndithu.91 Mupenyeni mtumwi wolimba uyu. Iye anati, “Koma Yohaneankangobatiza kuloza ku kulapa,” osati kwa kukhululukidwakwa machimo, chifukwa Nsembe inali isanaphedwe apo,kubatizidwira kwa iko…Ndipo pamene iwo anamva ichi, iwoanabatizidwanso mu Dzina la Yesu Khristu, ndipo MzimuWoyera unabwera pa iwo.92 Tsopano, kodi ichi chinachita chiani? Zinasonyeza kutianthu awa amene anali okonzedweratu ku Moyo, mwamsangapamene iwo anawona Choonadi cha Mwamalemba, iwoanayenda mu Choonadi ndipo analandira mphotho yawokhulupirira: Mzimu Woyera unabwera pa iwo, ndipo iwoanayankhula mu malirime, analosera, anamukuza Mulungu.Inu mukumvetsa zimenezo tsopano? Mwaona? Iwo anachita

1026 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

zimenezo iwo atakhala nacho kale chisangalalo chachikulu,kufuula, ndi kumutamandaMulungu.93 Mu Baibulo iwo anali naye mlaliki wa Chibaptistikumeneko; iye anabatizidwa nayenso. Koma iye anali, ndipo iyeanali—ankatsimikizira n—ndi Baibulo kuti Yesu anali Khristu.Ndipo anthu anali ndi chisangalalo chachikulu, ndipo iwoanali okondwa kwambiri basi pa chimenecho; ndipo apobeiwo anali opanda Mzimu Woyera! Iwo anachita kubatizidwansokachiwiri. Ndipo Paulo ananenamuAgalatia 1:8, “Ngati Mngelowochokera Kumwamba angabwere nadzalalikira uthengawina uliwonse wosiyana ndi uwu umene ine ndaulalikira kwainu, musiyeni iye akhale wotembereredwa.” Sanali kusamalachimene icho chikanakhala chiri.94 Chotero, podziwa zinthu izi…Mwinamwake inusimukuzidziwa izo, abale anga; koma podziwa zinthu izi,ndiye ine ndiri wokakamizidwa ndi kumangikira pa ntchitokwa Mulungu kuti ndizichita dongosolo la maziko oyambirira,chifukwa palibe munthu wina amene angaike maziko enaaliwonse kuposa awo amene anaikidwa kale; amenewondiwo atumwi ndi aneneri. Aneneri ananeneratu izo, ndipoatumwi ankazichita izo; ndipo ife tikuyenera kuti tizipitirirakumazichita izompaka chimangochi chitsirizidwe.95 Tsopano, ine ndikukhulupirira ndiye, kuti munthuamapulumutsidwa pamene iye akhulupirira pa Ambuye YesuKhristu ndi mtima wake wonse, ndipo kuchokera mu mtimamwake, osati kuchokera ku chikumbumtima chake chakunjatsopano…96 Onani, inu—ndinu munthu wapawiri—anthu atatu mwammodzi, solo, thupi, ndi mzimu. Tsopano, ine ndikukhulupiriramphamvu zanu zakunja, s—solo yanu kuchokera-osati soloyanu, koma chikumbumtima chanu chakunja, mphamvuzanu…Pamene inu muli maso, mwa kuyankhula kwina, i—inu mumagwiritsidwa ntchito ndi mphamvu zisanu: kuwona,kulawa, kukhudza, kununkhiza, ndi kumva. Zimenezozinangopatsidwa kwa inu kuti muzikhudzira kwanu kwapansipano; ndipo i—izo sizinapatsidwe kwa inu kuti muzikhudzirakwanu kwa kumwamba. Pali mochitika mphamvu zisanu ndiimodzi mu thupi laumunthu, chifukwa iye ndi wa chiwerengerocha chisanu ndi chimodzi mu Baibulo. Iye analengedwa pa tsikulachisanu ndi chimodzi, ndipo iye ndi wa chiwerengero chachisanu ndi chimodzi—munthu ali. Ndipo iye ali nako kuwona,kulawa, kukhudza, kununkhiza, kumvera, ndi chikhulupiriro.Chikhulupiriro chake chimakhazikitsa kumene iye akupita,kumene iye walunjikako.97 Tsopano, chikhulupiriro ndi thunthu la zinthuzoyembekezeredwa, umboni wa zinthu zimene inusimukuziwona, kulawa, kuzikhudza, kununkhiza, kapena

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1027

kuzimva. Koma mwa chikhulupiriro, pamene iye awagwiraMawu, Iwo amamutumiza iye mu dera (mwaona?) izozimawapangitsa Iwo kukhala enieni kwambiri kwa iye, mpakaiye amangokhala basi ngati kuti iye ali nazo izo mu dzanja lake.Iye amadziwa kuti izo zichitika.98 Tsopano, apo pali chinthu chomwecho pa funso ili panopa ubatizo wa madzi. Mwaona? Mulungu ankadziwa kutianthu awa akanati abatizidwenso mu Dzina la Yesu Khristu.Ndipo Paulo, iye anaika neno lakuti palibe munthu, ngakhaleMngelo wochokera Kumwamba, asamaphunzitse chiphunzitsochina chirichonse chosiyana ndi chimene iye anali ataphunzitsa;kotero choncho, ngati ine ndibwera ngati mlaliki; ngati mtumiki,ngati mneneri, kapena chirichonse chimene ine ndingakhalendiri, kapena ngakhale Mngelo kutsika pansi, ndi kuphunzitsachinachake chosiyana kwa chimenemtumwi uyu anachita, ndipoine ndikapanda kuwalamulira anthu kuti azibatizidwanso muDzina la Yesu Khristu, ine ndikanadzapezeka mwa Baibulomboni yabodza ya chinthu chimene ine ndikudzinenera kutindikuchikhulupirira.99 Kotero ine ndikukhulupirira kuti ndondomeko yayalidwakale. Munthu aliyense mu Baibulo anali kubatizidwa muDzina la Yesu Khristu. Panalibe nthawi imodzi pamenealiyense anayamba wabatizidwapo mu dzina la Atate,Mwana, Mzimu Woyera. Mwaona? Panalibe aliyense anayambawakonkhedwapo; iwo onse ankamizidwa.100 Kotero ine ndikukhulupirira kuti pamene iwe mochitika…Kwa funso lanu, m’bale wofunika, ine ndikukhulupirira kutipamene Mulungu adziwa mtima wako…Padzakhala zikwi ukoamene anabatizidwa mu Dzina la Yesu. Iwe umangopita pansiwochimwa wowuma ndi kutulukamo uli wonyowa. Mukuona,mwaona? Koma monga wokhulupirira weniweni, woona, ameneiwe ukuyenera kuti uziyenda mu chikhulupiriro chonse ndichikumbumtima chabwino kwa Mulungu, pamene iwe uziwonaizo, iwe umabatizidwa! Koma ine ndikukhulupirira kuti izozimangokhala kuwonetsera kwakunja kusonyezera kuti ntchitoyamkati ya chisomo yachitidwa.101 Chimodzimodzi basi momwe Mulungu anamangira chombo.Anati, “Nowa, kalowe mu icho, iwe ndi banja lako ndiapanyumba ako.” Ndipo iwo anakalowammenemo. Tsopano, inendikukhulupirira kuti ngati apo pakanati pasakhale chombo,Mulungu akanamulola Nowa kuti akhale pa chipika kapenakuyenda pa madzi. Mwaona? Koma Iye anapanga chombo kutiiye alowemo, ndipo iyo inali njira yochitira zimenezo; imeneyoinali njira yoperekedwa ndi Mulungu. Ine ndikukhulupirira kutiMulungu amamupulumutsa munthu mwa chisomo. Mu Dzina laYesu Khristu kudzera mu kuwonetsera kwa kunja ndiyo njiraya Mulungu yoperekedwa yoti ulowere mu zimenezo, pakuti iwoonse ankabatizidwamwanjira imeneyo.

1028 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

102 Ine sindiri kumuweruza munthu winayo, koma izo ndibasi…ine ndikuganiza kuti ndi chimene izo ziri. Madzisamamupulumutsa munthu, iwo amangosonyeza kuti iyewapulumutsidwa; icho ndi chofotokozera mwakunja. Tsopano,izo zikhoza kusakhala zolondola, m’bale. Ngati izo siziri,chabwino, ife tidzazitenga izo nthawi inayake kapena…Chabwino.242. Mu Genesis 6:4, chitachitika chigumula, kodi zimphona

zinachokera kuti?103 Limenelo ndi labwino, labwino kwambiri. Limenelondi funso lanzeru. Kodi zimphona izi zinachokera kuti?Adamu sanali chimphona monga momwe ife tikudziwira,chifukwa ngati izo zikanakhala, Baibulo likanakhala litanenachomwecho. Iye anali munthu wamba chabe. Kodi iwoanachokera kuti? T—tsopano, uwu ndi mtsutso wawukulu, ndipoichi changoperekedwa kwa ine. Izo ziri pa pepala lalikulu,lakuda, ndipo izo ndi—kapena zilembo zazikulu, zakuda pachidutswa cha pepala loyera.104 Tsopano, zimphona izi…ine ndikukhulupirira anali wina—winawake kuno osati kale…Iye ayenera kuti anali Josephus.Ine si—ine sindikunena izo tsopano, abale otumikira, kutianali Josephus. Koma izo zikuwoneka kwa ine kuti akhozakukhala kuti anali iyeyo, kapena Dr, Scofield, kapena enaa iwo, amene ananena kuti zimphona izi zimene zinali mudzikolo zinali makamaka mizimu yokugwa ya Mulungu imeneinamvera k—ku nthano za Satana, pamene iye anazinena ku—cha Kumwambako…Ndipo anali Mikaeli…Ankayesera kutiayambitse nkhondo ndi Mikaeli Kumwamba…anaponyedwerapansi…Kuti ana amuna a Mulungu awa anawaona ana aakazia anthu, ndi kuti zimphona izi zinali mu dzikolo pa nthawiimeneyo, kuti iyo inadzikanikizira yokha mu thupi laumunthu.Ngati inu muchita zimenezo, inu mumupanga Satana kukhalamlengi. Inu simungati muchite zimenezo.105 Mosachuluka kuposa Dr. Smith, ku Seventh Day Adventistpa mbuzi yansembe. Iye anati mbuzi imodzi imene inali…Iwo ankapha mbuzi ziwiri pa—tsiku la nsembe—Tsikula Chitetezero, ndipo mbuzi imodzi inkaphedwa ndipoinayo inkamasulidwa ipite. Ndiyeno iye anati mbuzi imeneinkaphedwa inkaimira Yesu, wonyamula machimo athu ameneanafa; koma mbuzi imene inkamasulidwa inkaimira mdierekezi,amene amanyamula machimo athu ndipo amapita kutali kumuyaya ndi iwo. Tsopano, inu mukuona, aliyense…Kwalingaliro langa…Ngati izi ziti zidzakafikenso konse kwam’balewa Adventisti, ine sindikunena kanthu pa munthu wamkuluuyo, Dr. Smith. O, iye anali munthu wophunzira, waluntha,wabwino, Mkhristu wotukuka, wokhulupirira; koma kwa ine,inu mukuona, izo sizikupanga nzeru. Pamene inu muchitazimenezo, inu mukupereka nsembe kwa mdierekezi ndiye. Izo

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1029

zonse zinkaimira Khristu kufa, kuikidwa, ndi chiukitsiro. Iyeaponso anafera machimo athu ndipo anawanyamulira machimoathu kutalitali; zonse izo zinali Khristu.106 Kotero zimphona sizinabwere pa kudzikanikizira yokhammenemo. Zimphona izi zinali ana a Kaini, amene bambo wawoanali serpenti, amene ankawonekamwamawonekedwe aliwonsendendende monga munthu, koma anali munthu wamkulu,kwambiri, wamkulupo kuposa munthu. Ndipo uko ndi kumeneana amenewo anachokera, chifukwa iwo anali ana a Kaini,nchifukwa iwo anali Akanani mu dziko la Kanani, kumeneiwo anachokerako; ndipo uko nndi kumene Kaini anapitako.Ndipo izo zinali…Mukuona, izonso zikutsimikizira mbewu yaserpenti. Iwo unali mtundu wa anthu wosiyana mwapalimodzi.Zimenezo zinali mbewu za serpenti. Mwaona?107 Tsopano, f—funso la mbewu ya serpenti ilo liri mkati umu,kotero i—ife tifika kwa ilo, ndipo ine ndikufuna kuti inumukhalenazo izi mu malingaliro. Mwaona? Tsopano, kuti ndingoperekamaziko awa.108 Mukuona, iwo anali—iwo anali Akanani, zimphona izi;ndipo iwo anali ana a Kaini, amene anali mwana waserpenti. Ndipo serpenti anali chimphona cha munthu, munthuwamkulu, wokhala ngati mwachinyama, osati chokwawa konse,wokongola. Iye anali wochenjera kwambiri mwa zinyama zonseza kuthengo. Ndipo iye anali yekhayo…109 Onani, m—majini ochokera kwa chinyama kupita mwaakazi sangabale konse. Iwo aziyesera izo mobwereza bwereza;ndi zosabereka kwa ukazi wa mkazi. Ndipo tsopano, iwoakulephera kuti achipeze icho. Kutenga chimpanzi, iye ndichinthu chapafupi kwambiri chimene iwo angathe kuchipezakwa munthu, kapena gorila, kapena zina za izo zoyandikirapokwa munthu. Monga Mulungu mu kusintha kwake kwachirengedwe kwakukulu anayamba kupanga nsomba; ndiyenoIye anapanga mbalame; ndipo kenako Iye anapanga zinthuzinazo, zinyama, ndipo izo zinakhala zikubwerabe chokwera,mpaka china chinabwerapo mpaka kwa chimpanzi, ndi kwanyani, ndi kumapitirira mpaka kwa gorila, ndiyeno mpakaku mawonekedwe a serpenti, ndiyeno kuchokera kwa serpentikufika kwa munthu.110 Ndipo mtundu wa anthu wayesera kuti afufuze, sayansi,kuyesera kuti apeze mafupa, chimene chinyama ichi chinalichomwe chinali chapafupi kwa umunthu. Ndipo umunthu ndichinyama.Munthu, gawo lamnofulo ndi mnofu wa chinyama; ifetikudziwa zimenezo. Ife ndife zinyama, chimene chiri chinyamacha magazi ofunda; ife tikudziwa zimenezo! Koma nchianichimapangitsa kusiyanako? Chinyama sichimakhala nayo soloyamkati iyo, koma umunthu uli nayo. Icho sichimadziwachabwino kusiyanitsa ndi choipa.

1030 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

111 Galu wamng’ono wamkazi iye samadziwa kuti akuyenerakumavala diresi, ndipo ine sindikukhulupirira kuti iye angavaleakabudula ngati iye akanati—akanamvetsa. Ngakhalensonkhumba siikanatero, koma ndi mtundu wokugwa wa umunthu.Mwaona?112 Tsopano, u—uko ndi kumene izo zinachokera. Uko ndikumene zimphona izi zinachokera. Iwo anali ana a serpenti.113 Ndipo onani, pamene iye anamuwona Eva ali muchikhalidwe ichi, i—Satana analowa mwa iye ndipoanamupangitsa iye kuti…Mukuona, Adamu analiasanazizindikire izo apobe. I—ine sindikudziwa momwendingagwiritsire ntchito mawu awa. Izo zikhala zabwino bwinonanu inu nonse pano, koma winawake amazitsutsa kwambirizimenezo. Inu mukudziwa, iwo nthawizonse amayesera kutiatole chinachake. Koma onani, Adamu anali asanamudziwekonse Eva, mkazi wake. Iye anali asanafike konse pa maloamenewo, ndipo Satana anamutsogolera iye pamenepo.Mwaona? Ndiyeno pamene iye anakhala ndi pakati, ndiye iyeanamudziwa iye. Ife tifika kwa izo pa funso lotsatira ili kapenalimodzi la mafunso awa. Ine sindikudziwa kuti liri pati; ife—inendinangoliwona ilo mkati umu. Tsopano, koma uko ndi kumenezimphona zinachokera.

243. Wokondedwa M’bale Branham, kodi ana onse aamunandi aakazi a okhulupirira owona, obadwa mwatsopanoadzapulumutsidwa?

114 Ayi, m’bale; ayi, iwo ndithudi sadzati. Onani, monga ine—monga ine ndinamutengera David DuPlessis pa ndemangaiyi, “Mulungu alibe zidzukulu (mwaona?), ana aamuna ndiaakazi okha.” Mukuona, iwo adzayenera kuti adzabadwechimodzimodzi basi monga abambo awo ndi amayi anabadwiranao Mzimu. Mwaona? Icho ndi chimene chimamupangamunthu kukhala munthu watsopano, ndi chifukwa chakuti iyewabadwa kachiwiri, kubadwanso. Kubadwa kwake koyambakumamubweretsa iye munthu wachibadwa pa dziko lapansi;kubadwa kwake kwachiwiri kumamubweretsa iye munthuwauzimu wa Kumwamba. Mwaona? Izo zimamusintha iye,solo yake, osati chikumbumtima chake chakunja, mapangidweake akunja, mphamvu zake; iye amamverera apobe, ndikununkhizabe, kulawa, ndi kumva; koma magawo ake amkati,zokhumba zake, zimene zimamupangitsa iye, zasinthidwira kwaMulungu. Mwaona?115 Tsopano, kumbukirani, njira yokha yomwe izi zingachitikireingati ikhale iyi: monga momwe izo zinaliri mu nthawi yakenturio wa Chiroma. Paulo anamuuza wa Chiromayo, iyendi Sila, pamene iye ankafuna kuti asolole lupanga lakendi kudzipha yekha, chifukwa Mulungu anali ataigwedezerandendeyo pansi ndi chivomezi; iye anati, “Usati udzipweteke

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1031

wekha, powona kuti ife tonse tiri muno. Dzuka!” Ndipoankafuna kuti adziwe chimene iye akanati achite. Iye anati,“Dzuka ndi kukabatizidwa, ukutchula p—pa Dzina la Ambuye,ndipo iwe ndi a pa nyumba yako mupulumutsidwa.” Mwaona?Mwa kuyankhula kwina, “Khulupirira paAmbuye YesuKhristu,iwe ndi nyumba yako mupulumutsidwa.”116 Tsopano, motani? Ngati nyumba yako ikhulupirira mwanjira yomweyo imene iwe ukukhulupirira. Mwaona? Inupempherani ndi kumawapereka ana anu kwa Mulungu ndikugwiritsitsabe kwa Mulungu, mukukhulupirira kuti iwoadzapulumutsidwa.117 Ine ndangodutsa kumene mu chondichitikira ndi Rebekahwanga. Mwaona? Kungozipereka izo kwa Mulungu. Pameneiye anafika pokhala “wa mmateni,” ndipo iye anali kuyendandi mtsikana wina pamene ife tinapita koyamba kumeneko,amapita—kuthamangira ku nyumba ya mtsikana winawakekumakatengamaphunziro a zoyimba…Ndipomtsikana uyu…Ine ndinadzera uko tsiku lina, ndipo apa mtsikana uyu analiatakhala pa limba akusewera roko ndi rolo. Chabwino, zimenezozinali zokwanira basi kwa ine! Kotero ine ndinamuuza iyekuti asadzapitenso kumeneko. Mwaona? Ndiyeno iye anati,“Chabwino, awo ndi malo okha kumene ine ndikuyenera kutindingamapite kukaphunzira zazoyimbira.” (Inu mukudziwamomwe “amzaka za mmateni” amachitira.)118 Ndipo ine ndinati…Mwana aliyense amayenera kudutsamu zimenezo. Mwakuchitika aliyense amadutsa mu usinkhuumenewo. Inu munatero; ine ndinatero. Ndipo ife tikuyenerakumaganiza maganizo awo.119 Kotero ndiye, masiku angapo zitachitika zimenezo amayiake anamutsatira iye chifukwa cha chinachake, ndipo iyeanawazazira iwo. Tsopano, ameneyo si Rebekah konse.Anachokapo ndipo anamenyetsa chitseko, ndi pafupifupi kutiakanagwetsa zinthu zinali pakhoma, napita ku sukulu.120 Tsopano, ine ndimayenera kuti, zimawoneka choncho,ndingovula lamba wanga, ndi kumamutsatira iye mu bwalo, ndindikumubweza iye ndi zikwapu zikumukulunga iye. Mwaona?Koma ine ndinaganiza, “Dikira miniti, ine ndinayambakuganiza malingaliro a wausinkhu wa zaka eyitini.” Mwaona?“Tsopano,” ine ndinati, “Mayi, ine ndikudziwa izo…” Iyeanayamba kulira, Meda. Ine ndinati, “Ine ndikudziwa kuti iwewachita zonse zomwe iwe ukanatha kuzichita; ine ndachitazonse zimene ine ndikanatha kuchita. Tsopano, ngati izozatipulumuka mmanja athu, ife tiyenera kuti titenge sitepeyotsatira.”121 Monga dona wina mokoma analemba tsiku lina (ziri mulimodzi la mafunso awa pano), anati, “M’bale Branham, inu siMesiya, kodi muli?”

1032 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Ine ndinati, “Ayi, mayi.”Iye anati, “Ife timakukhulupirirani inu kuti ndinu m’busa

wathu, koma inu nthawizonse mumatilozera ife kwa M’busaWamkulu.”

Ine ndinati, “Uko ndiye kulondola; uko ndiye kulondola.”Mwaona?122 Ine ndinati, “Chabwino penya, Wokondedwa, tsopano, iweukuyenera kuti umvetsere kwa ine. Ndi zovuta kuti iweungachite izi; ine ndine mwamuna wako. Koma anthu amayendakudutsa mafuko ndi kozungulira kuti adzangopeza mawuochepa a malangizo. Tsopano, ngati iwe…Ine ndinayankhulakwa iye tsiku lina, ndipo iye anangochokapo kwa ine.”123 Tsopano, Becky sanachitepo konse zimenezo kwa ine.Mwaona? Ndipo pamene amayi ake ananena chinachake pa izo,iye anamenyetsa chitseko ndi kuti, “Inu mukuyembekeza kutiine ndizingokhala pano ndi kungokhala maluwa a pakhomamoyo wanga wonse?” Ndi kupsyonya! Iye anamenyetsa chitsekondipo anapita kunja. Ameneyo anali mdierekezi.124 Ine ndikukumbukira, zaka ziwiri zoyambirira za moyo wakeiye ankalira. Ife tikapita ku malo odyera ndi kumadya; inendimamuyendetsa iye mumsewu pameneMeda akudya, ndiyenoiye amayenda naye iye mu msewu pamene ine ndimadya.Ankangolira lira. Ndipo tsiku lina tiri uko ku Canada, analirausiku wonse, ndipo ine sindinathe kupuma ndi chirichonse; inenditaima pamenepo…Tsopano. Ndipo Chinachake chinanenakwa ine, “Ndimdierekezi akulowamu utumiki wako.”125 Ine ndinati, “Ndipatse ine mwana ameneyo.” Ine ndinati,“Satana, mu Dzina la Yesu Khristu, iwe chotsa manja akopa iye.” Iye anatonthola apo pomwe ndipo sanalire konsemoonjezera. Iye ndi mwana wa bata kwambiri amene ine ndirinaye. Kuchokera pa ora ilo lomwe izo zinachoka. Iwe umayenerakuti uchipeze icho…Iwe umayenera kuti ukhale uli nachochimenechomwa iwe basibe, iwe usanachichite icho!

Ndiyeno pamene iye—ndiyeno izo—iye anayamba zimenezo.Ndipo ine ndinamutenga Meda pafupi ora. Ine ndinati, “Meda,chotsapo manja ako.”

“Ine? Ameneyo ndi mwana wanga!”126 Ine ndinati, “Kodi iye si wanganso?” Chabwino. Inendinati, “Ngati iye akanakhala akufa mmawa uno, iwe ukanatiumupereke iye kwa Mulungu pofuna kopita kwake kwamuyaya.Bwanji ife sitikumupereka iye kwa Mulungu tsopano pofuna zaulendo wake wa pansipa?”

Ndipo iye anati, “Chabwino, ameneyo ndimwanawanga!”Ine ndinati, “Ameneyo ndi wanga inenso.”Ine ndinati, “Tsopano, kodi iwe ungatenge ako…”

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1033

“Ine osanena kanthu kwa iye?”127 Ine ndinati, “Ine sindinanene konse zimenezo. Ife tisiyekumuzazira iye, tizingomulangiza iye. Iye akusowamzake, ndipoiwe ndi amene ukuyenera kukhala uli mzake, iwe ndi ine. Ife ndimakolo ake.”128 Ana awa lero akusowa mzawo. Ngati iwo akanakhalanawo amayi ndi abambo amene akanamakhala panyumba ndikumawasamalira iwo, mmalo mopita kunja uku mu chipindachogulitsira mowa kuthamangathamanga usiku wonse ndizinthu monga izo, sitikanati—sitikanati tikhale ndi kupandamakhalidwe kwa ana. Mwaona?129 Iwo achoka ku Baibulo; iwo onse amapita ku tchalitchindi kumakapanga masewero a banko ndi zinthu mongaizo ndi…Mwaona? Inu mukuyesera kuzipukuta izo momweSatana wakhazikitsira uko mu Hollywood. Inu simungatikonse muibweretse Hollywood mu mpingo, inu muyenera k—ine ndikutanthauza kuwubweretsa mpingo mu Hollywood,inu mukuyenera kumubweretsa Hollywood ku mabwalo anu.Mwaona? Osati kupita mu mabwalo awo, asiyeni iwo azibwerakunoko. Ife tiri nacho chinachake chimene iwo sakudziwakanthu za icho.130 Kotero ife pamenepo ife tinagwada pa mawondo athu ndipotinazipereka izo kwa Mulungu. Ine ndinati, “Ine ndikudziwaiye ali usinkhu wa zaka eyitini—akhala mu masiku pang’ono,ndipo iye—ndipo msungwana wa usinkhu umenewo amaganizaza amzake achimuna, ndipo ife timamusunga iye mkati.”Ine ndinati, “I—ine sindimafuna konse kuti ndidzamuwoneiye akukwatiwa. Ine ndikufuna kuti ndimuike iye mu ofesikuno, azichita ntchitoyo. Ine ndikufuna ndidzamuwone iyeatadzazidwa ndi Mzimu n—n—ndi kumakhala moyo mongachoncho.”

Ndipo i…Chabwino, ife tonse tinkafuna zimenezo. Iyeanati, “Chabwino, ife sitingathe kuzichita izo.” Anati, “Iye basisamvera kwa zimenezo.”131 Ine ndinati, “Dikira miniti! Ife tamulera iye monse momweife tingathere, tsopano timuike iye mmanja a Mulungu—timupereke iye.” Ndipo ine ndinati, “Ndiye iye akamachitachirichonse tiziti, ‘Becky, wokondedwa, amayi, sakufuna kutiiwe uzichita zimenezo, koma ine ndi bambo wako; inendikhalabe pafupi nawe.’ Mwaona? Kumulola Iye adziwekuti iwe ukumukonda iye. Iye ayenera kupeza wina wotiazimukonda iye, ndipo uyo akhoza kukhala mkazi wolakwika.”Mwaona? Ine ndinati, “Iwe ukhale mkaziyo amene azichitakukondako.” Ine ndinati, “Wokondedwa, zimenezo zikumvekangati zopanda pake, koma anthu amabwera kulikonse, ndipoamakhala pa zokambirana za payekha, ndi zinthu.” Ine ndinati,“Ndine wawamba kwambiri; ndife awamba wina kwa mzake,

1034 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

chifukwa ndife mwamuna ndi mkazake, koma tisamalole izokuti zizichitika. Iwe uyenera kuti uzikumbukira, izi ziri muDzina la Ambuye!”

Kotero iye anati, “Chabwino.”Ife tinagwada pa maondo athu ndipo tinamupereka iye kwa

Mulungu. Tinati ife tikuchotsamanja athu pa icho.Madzulo amenewo iye anabwera umo; iye anati, “Chabwino,

ine ndikulingalira inu panobe mukuti ine ndisamapitekumeneko!”132 Meda anati, “Ayi, ine sindinanene kanthu za izo.” Anati,“Iwe ukudziwa, Amayi sakufuna kuti iwe uzichita zimenezo;ndipo iwe ukudziwa kuti zinakhala ngati ziwaphe abambo akopamene iwo anakumva iwe ukusewera nyimbo za bugi wugizija, chirichonse chimene izo zinali, ndi msungwana ujayu.”Anati, “Tsopano, iwo sakufuna kuti iwe uzichita zimenezo,ndipo ife sitikufuna kuti iwe uzichita zimenezo, Becky, komaife tinangozipereka izo kwa Ambuye. Ine ndikufuna iwe udziwekuti ife tikukukonda iwe. Chirichonse chimene iwe uti uchite, ifetikukukondabe iwe.”

Iye anafuula, nati, “Ine ndikupitabemulimonse!”Anati, “Chabwino, Wokondedwa.” Kotero anapitirira nazo.

Anati, “Chabwino, ine ndikonzeratu chakudya pamene iweuzibwerera.” Iye sanapite konse! Ayi, iye sanapitenso kuyambirapamenepo. Mwaona?133 Si motalika zitachitika zimenezo iye anakomana ndi George;George ndiMkhristu. I—izo zinakhazikitsa icho ndiye.134 Iye anali kuyesera kuwauza Akazi a Wood za izo tsiku lina.Iye anati, “O, ine ndinafika polusa moyipa.” Anati, “Adadindi Amayi anandipereka ine kwa Ambuye.” Anati, “Ndinalusamoyipa.” Koma i—izo zinali kulusa kwa ife; ife sitikufunakukhala ndi kulusa kulikonse koposa kumeneko. Mwaona?Kungozisiya izo kuti zipitemonga choncho. Chabwino.244. M’bale Branham, kodi inu mukuganiza chiani za athu…

(O, o! Ine ndikukumbukira ndinaliwerenga ili. Inesindinali…Ine ndinati ndilisunge ilo mmbuyo mochedwa,koma ine ndikuganiza ine ndikhoza kungoliwerenga ilo.Zolemba za mkazi wina. Iye ayenera kukhala wochokeraku Kentucky, chifukwa ali ndi—tikiti ya Kosmos PortlandCement apa.) M’bale Branham, kodi inu mukuganizachiani za alongo athu mu mpingo akuvala madiresi aafupichoterowa? Kodi izo sizikuipitsa umboni wathu ndi kuikachitsanzo cholakwika kwa anthu athu aang’onomumpingowathu uno? Izo zikuwoneka mwakuti-…kumuwonawamng’ono—kumuwona mkazi wachikulire atavala diresilalifupi kwambiri mpaka ilo limawonetsa mawondo akepamene iye akuyenda.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1035

135 Aliyense yemwe inu muli, Mulongo kapena M’bale, aliyenseamene muli, ine ndikugwirizana nanu zana pa zana. Ndichamanyazi, koma ndiuzeni ine choti ndichite nazo izo!Ine ndalalikira izo molimba basi momwe ine ndikudziwirakulalikira kwake kwa izo; iwo akumachita izo chomwechobe.Kotero ndi chiweruzo chawo, chifukwa Mawu apitapo.Inde, ine ndithudi ndimatsutsana nato timadiresi tating’onotogwira thupi timene timawoneka ngati…Ine mowirikizandimawakalipira ana anga, Becky ndi Sarah. Ine sindikusamalamomwe iwo aliri aang’ono, i…izo…ine ndimangowakalipiraiwo nthawi zonse. Ine ndikuganiza iwo amavala ngakhalemadiresi aja…Meda amamutengera Becky pambali tsikulirilonse pa izo. Mwaona? Madiresi olekezera kupitirira…Ndithudi ana, inu mukhoza kuyembekezera zimenezo mwa ana,ndipo inu mumayenera kuti muziwakonza iwo; koma zikafikakwamzimayi, pali chinachake cholakwika pamenepo.Mwaona?136 Ndisati ndipweteke kumverera tsopano, inendikungoyankha mafunso. Inu mwandifunsa ine kuchokeramu mtima mwanu; ine ndikukuzani inu kuchokera mu mtimawanga. Ngati inu mwapeza kukonza kwake, c—chonde bweranimudzandiuze ine, ine ndithudi ndichita zimenezo, ngati inendingathe kuchita chirichonse pa izo.137 Monga winawake ananena tsiku lina, iye anati, “Chabwino,ine ndikuuzeni inu, M’bale Branham,” anati, “Ine ndikuuzaniinu zimene Adamu ndi Eva…” Anati, “Izo zinali ndendendebasi; iwo anali ndi apulo!” Ndipo ine ndazindikira kuti iwoasintha zimenezo tsopano; iwo akuti iwo anali ndi chiani?Ine ndikukhulupirira icho chinali kutchedwa chinachake?[Mwamuna mwa osonkhana ayankha, “Apurikoti”—Mkonzi.]Apurikoti, eya, inali apurikoti imene iwo anadya. Chabwino, ndinthawi yoti tigawenso maapurikoti ngati iwo angawapangitseiwo kumazindikira kuti iwo ali maliseche. Mwaona?245. M’bale Branham, ine ndawulandira Uthenga wa Mulungu

wa lero, ndiponso mwana wathu wamwamuna. Ndipo ifetonse tinabatizidwa mu Dzina la Ambuye Yesu Khristu.Mwamuna wanga—mwamuna wanga sanaulandireUthengawu ndipo akumenyana nawo Uthenga uwu.Ndipo iye wamukopa mwana wathu wamwamunandipo akumamutengera iye ku mpingo wa Methodisti.Iye akufuna kuti ine ndizipita naye ku mpingowopamene ife sitiri mu utumiki kuno ku kachisi. Kodi izozingakhale zoyenera kuti ine ndizipita naye iye kapenakodi izo zingakhale bwinoko kuti ndizikhala kunja kwachipembedzo chimenecho?

138 Chabwino tsopano, Mlongo wokondedwa…Iyesanalembepo dzina ayi, koma mwinamwake inu mukumvetserakwa funso lanu; ngati inu simukumvetsera, inu mudzalimvailo pa tepi. Zipitani ndi mwamuna wanu, koma musati

1036 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

mukhale ochita nawo a—a zimene iwo akuchita. Mukuona, inumukuyenera kuti muziwakonda amuna anuwo, ndipo chikondindi chimene chimachititsa izo. Inu mungokhala muli wamcherekwenikweni; iye ayamba ludzu ngatimuli chirichonsemwa iye.139 Musati mujowine chipembedzo chakecho. Iye anati,“Inu mukhale kutali ndi chipembedzo chimenecho.” Musatimuchijowine icho; zipitani kumeneko. Ngati inu simungapezemkate wamphumphu, zipezani watheka; mukapanda kupezawatheka, ingopezani kachidutswa. Mukuona, mwaona? Komaumo ndi momwe inu muti muwapindulire amuna anu, pakuchitazimenezo. Musati mukhale amwano, ndiye iye adziwa kuti iyeali nazonso zochuluka momwe inu muliri nazo. Mwaona? Komapamene inu muzisonyeza chinachake chimene inu muli nachochimene iye alibe, zimenezo zimupangitsa iye kukhala waludzukuti akhale monga inu. Mkazi woyeretsedwa amamuyeretsamwamuna wake.140 Limenelo linali langizo chabe. Kotero i—ine ndingati nditayenthawi yaitali pa zimenezo, koma ife tikungofuna kuti tidutsemu ochuluka momwe ife tingathere, chifukwa ine ndikuwonakuti ine ndangotsala ndi pafupi maminiti twente-thuu ndiye.Chabwino.

246. M’bale Branham, ine ndikukhulupirira Uthenga umeneinu mukuphunzitsawu ndi mtima wanga wonse. Iwoumakondoweza moyo wanga; komabe, mkazi wanga ndimwana wanga wamwamuna samasangalala mu Mawu.Iwo sali kukhumba kuti adzilekanitse okha ku zinaza zizolowezi zawo zachidziko. Inu munanena kuti ifetizidzitengera athu—tizidzitengera mabanja athu. Inendikupeza izo zikundivuta kuti ndizichite, zikuwonekakuti iwo sakukhalira moyo Mawu kapena mu Mawu. Kodinjira yanga ndi iti, bwana? Kodi ine ndidzitengere iwo ndikumakhulupirira, kapena kodi ine ndizipemphera, “Atate,chifuniro Chanu chizichitidwa,” ndi kumakhutitsidwa muchikhalidwe chimene ine ndadzipeza ndekha ndirimomu?Ine ndikanayamikira kundilondolera kwanu, M’baleBranham.

141 Mulungu akudalitseni inu, M’bale wanga kapenaMlongo, aliyense yemwe inu mungakhale muli. I—inendikanangowapereka iwo kwa Ambuye. I…Mukuona,chifukwa, “Onse amene Atate anandipatsa Ine adzadza kwaIne.” Mwaona? Tsopano, chinthu chokha choti inu anthumuzichita…142 Izo zinapangitsa mtima wanga kufufuma ndi chisangalalotsiku lina ndikupita kutunda ndi kumusi ndikuwawona amunaa mamotelo awo. I…ine ndinapita uko kwa Bambo Becker. Iyeanati, “Billy, iwe ukudziwa chiani? Ine ndimadyetsa osonkhanaanu onse Lamlungu lirilonse”—pamene Blue Boar imadyetsa

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1037

mazana atatu pafupifupi Lamlungu lirilonse! Mwaona? Ndipoine ndinatuluka panja ndipo mnyamata uyu kumeneko, njondaiyi kumeneku—kuRanchHouse,munthuwabwino kwambiri. Inendinakomana naye; iye anati…

Ine ndinati, “Chabwino, izo zinali zabwino kwenikweni.” Inendinati, “Ine ndikuyamikira inu pochotsa zinthu zonse zija kunjakuja—kuchita mopitiriza konse kunja kuja.”

Iye anati, “Inde, bwana, M’bale Branham.”Ine ndinati, “Iye wandidziwa bwanji ine?” Mwaona? Ine

ndinati, “Inu mwandidziwa bwanji ine?”Iye anati, “Ine ndikukudziwani inu,” Anati, “Ine

ndimadyetsa osonkhana anu onse Lamlungu lirilonse pa…Chabwino,” iye anati, “ndipo ine ndikufuna kuti ndikuuzeni inuchinachake: iwo ndi anthu abwino. Iwo ndi anthu abwino!”143 Tsopano onani, izo zinandipanga ine kumverera bwino.Inu ndi ana anga. Mwaona? Pamene ine ndimva kuti anaanga akuchita bwino ndi kukhala abwino, izo zimawapangaAbaba kumverera bwino kwenikweni. Mwaona? Kotero inumukumvetsa.144 Tsopano, tsopano, Amayi, pamene…Mlongo Wanga, ngatiamuna anu akufuna kuti inumuzipita kumpingo waMethodisti,inu zipitani nawo. Inu mwina simukapezako mtanda wonse wamkate, koma ngati iwo ngakhale atati iwo amakhulupirira kutiYesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu, inu mukakhulupirirezimenezo, chifukwa ife timatero nafenso. Tsopano, ngati iwoapambukira pa zolunditsa zina ndi zinthu, basi—zingowasiyaniiwo kuti azipitirira nazo, koma inu muzidya mkate wochulukachoterowo. Mwaona? Ndipo mmenemo, inu muzingosonyezamwa kukoma kwa moyo wanu ndi kulingalira bwino kwanupa ena…Ndipo ngati inu mulibe izo, wokondedwa Mlongo,pempherani mpaka izo zibwere kwa inu, kuti inu musamachitekudzipangitsa chirichonse chongopeka, chifukwa pamene inumuchita zimenezo, izo si zenizeni. Mwamuna wanu akhozakudziwa zimenezo. Koma inu—pamene inu mwapempherazenizeni mpaka pa malo pamene moyo wanu uli wodzaza ndimchere wa Mpulumutsi, izo zipanga kukhudzako. “Ngati inenditi ndikwezedwe mmwamba, ine ndikokera anthu onse kwaIne.” Ine ndikanamapita; zikhalani osamala kwenikweni. Musatimukajowine mpingowo apobe! Chonde musati mukachitezimenezo; inu musati mukajowine mpingo wawo, koma zipitaninawo!247. M’bale Branham, apa pali funso limene lakhala ngati

lododometsa kwa angapo a ife pano. Mmodzi—p—pa (pepani ine)—pa matepi ena inu mumayankhulaza Ayuda okha kukhala akupulumutsidwa Mkwatibwiatakwatulidwa kaye. (Ndipo padutsa mzere.) Chondefotokozani kwathunthu za Amitundu amene sati apite

1038 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

mu mkwatulo. Ine ndimaganiza inu munanena kutiAmitundu amene anasiyidwa anadutsa mu chisautsondipo anapereka miyoyo yawo mwa umboni wa Yesu.Pamene Iye akubwerera kuchokera kwa Amitundu kupitakwa Ayuda—pamene Iye akupotoloka nachoka kwaAmitundu kupita kwaAyuda, ndiye apo palibemwayi winauliwonse kuti Amitundu apulumutsidwe, Amitundu okhaamene anapulumutsidwa kale, koma amene sanalandireChoonadi cha tsiku lawo lotsiriza adzapita mu nthawiya chisautso ndiyeno nkudzapulumutsidwa pa mapeto.Kodi uku nkulondola? Chonde longosolani, chifukwainu munanena kuti uko kudzangokhala chiwerengerochaching’ono chokha chopita mu mkwatulo. Nanga bwanjianthu amene anakhulupirira pa Ambuye—akukhulupirirapa Ambuye tsopano ndi momwe—ndipo sakukhulupiriramomwe inu mumalalikirira Uthenga wa tsiku la nthawiyotsiriza uwu? Kodi iwo adzapulumutsidwa? Ndiyenomlongoyo walemba dzina lake.

145 Tsopano, funso labwino kwambiri. Tsopano, malo oyamba,kusokoneza kwake kuli, kuli zimene ine ndanenapo za masikua Amitundu kuti adzatha pamene chisautso—mu chisautso.Tsopano, ine sindimawawona Amitundu mu Baibulo…Mkwatibwi wa Amitundu, Mkwatibwi, osati mpingo waAmitundu tsopano, mpingo wa Amitundu udzadutsa munthawi ya chisautso (mwaona?), koma osati kwa…Mukuona,Mkwatibwi ndi Wosankhidwa; Iwo sali kudutsa mu chirichonsekoma mkwatulo. Iwo adzangosinthidwa ndi kuchotsedwamu dziko. Mwaona? Tsopano, ine ndifotokoza zimenezo mufunso lamtsogolo pano, ndizibweretsa izo kuchokera kwaLutera mmwamba, ndipo inu muwona ndiye chimene izozikutanthauza; uko ndi kukhwima kwaThupilo.Mwaona?146 Tsopano zindikirani. Tsopano, Ayuda amene akutsala ndiamene ati adzalalikidwire ndi aneneri awiri, Eliya ndiMose.147 Tsopano, awa ndi malingaliro anga anga, abale otumikira,njira yanga yanga yomwe ine ndikumverera kuti Mzimu Woyerawaziwululira kwa ine.148 Tsopano, chinthu chotsatira choti chichitike ndiAchiyuda—kapena Mkwatibwi wosankhidwa wa Amitundukuti akwatulidwe palimodzi ndi Mkwatibwi wina yensewosankhidwa wa Amitundu amene wakhala ali mmusimokudutsa mmibadwo—adzakwatulidwira mmwamba muKukhalapo kwa Khristu mmiyamba. Akufa akuuka; ameneali amoyo ndipo atatsalira akusinthidwa; ndipo iwoakukwatulidwira mmwamba palimodzi mu mlengalengakukakomana nawoAmbuye. Ndiye, chifukwa…149 Pambuyo pa mwambo wa Chikwati mu Ulemerero, Yesu—iwo akadzati akwatulidwirammwamba kupita mumlengalenga,

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1039

Yesu akubwerera pa dziko lapansi ndi kudzadzidziwitsa Yekhakwa anthu Ake, mwa choimira monga Yosefe anadzidziwitsayekha kwa abale ake. Ndipo mkazi wake, palibe Wamitunduamene analipo, palibe wina aliyense koma Yosefe yekha, pameneiye anakadzidziwitsa yekha kwa abale ake. Nonse mukumvetsazimenezo tsopano?150 Iye anatumiza…Ngakhale mkazi wake anali ali munyumba yachifumu, choimira kuti Mkwatibwi adzakakhala alimu nyumba yachifumu mu Ulemerero pa nthawi imeneyo.Ndiye Yesu akudzidziwitsa Yekha kwa Ayuda (mwaona?)ukadzachitika mwambowa Chikwati, zaka 3½, n—n—ndi vuto laYakobo, zaka 3½ zija, kutha kwa sabata lachisevente la Daniele.Mesiya ndi woti adulidwe mkati mwa…Ndipo Iye ananenerazaka 3½ ndipo anadulidwa nachotsedwapo. Ndiye pali zaka 3½zatsalirabe kwa aneneri awo, Mose ndi Eliya, ndiyeno pa kuthapa masiku sevente awo monga zinawerengedwera pa anthuwo,momwe Daniele ananenera; ndiye pa kutha kwa masiku seventeamenewo, Yesu ali woti akadzidziwitse Yekha kwa iwo. Iyendiye Kalonga uyo amene akuyenera kuti abwere kwa Ayuda.Mwaona?151 Tsopano, ndiyeno pa nthawi imeneyo…Onani, Mkwatibwiwa Amitundu ali Kumwamba, ndipo anamwali opusa, namwaliwa Amitundu, si woti adzapulumutsidwe pa nthawi imeneyo; iyeali wopulumutsidwa kale, koma wakanidwa mwa Mkwatibwi.Ndipo iye akungodutsa mu nthawi ya chisautso kwa nthawiya chiyeretso, chifukwa iye wamukana Khristu, Mawu, oti iyeayeretsedwe nayo. Ndiye iye ayenera kumva kuwawa chifukwacha zochita zake, koma Mkwatibwi amene wasandulikaMawu, chitetezero chathunthu chinapangidwa ndi Khristu,chifukwa Iye ali Mawu. Thupi limenelo linang’ambidwa, ndipopamene thupi limenelo linang’ambidwa, Mkwatibwi anali muthupi limenelo, chifukwa ilo Lonse liri Mawu! Ameni! Inumukuziwona zimenezo?152 Pamene Yesu anamva kuwawa mu thupi limenelo, Iyeanamva kuwawa…Chifukwa mwamuna ndi mkazi ali munthummodzi. Eva anatengedwa kuchokera kwa Adamu, Mpingo…Nchiani chinachitika? Mulungu anatsegula mbali y—yaAdamu ndipo anatenga kuchokera mmenemo womuthandizira,mkwatibwi. Ndipo Mulungu anatsegula mbali ya Yesu paKalvare ndipo anamutulutsamo Mkwatibwi. Mwaona? Ndipopamene Yesu ankafa pa Kalvare…Kumbukirani, Mkwatibwisanatengedwe kuchokera mu thupi mpakana thupilo litafa. Iyeanali atafa kale, ndipo iwo ankati athyole miyendo Yake. Ndipomneneri anati, “Sipadzakhala fupa limodzi liti lidzaswedwe.”Kotero iwo anali atakokela mmbuyo kale nyundo kuti athyolemiyendoyo, ndipo mwamuna anapita apo ndi nthungo ndipoanaithimbiriza iyo kupyoza mtima Wake; ndipo madzi ndimagazi zinatulukamo; Iye anali atafa kale. Mkwatibwi anali

1040 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

atawomboledwa kale mu thupi mwa imfa Yakeyo, koteropalibenso kuvutika mu nthawi ya chisautso kwa Mkwatibwi.Mwaona? Iye akupita kukalowa. Koma mpingo wa Amitunduumene unangokhulupirira pa Iye ndi kumatenga tizikhulupirirotachipembedzo ndi zina zotero ndipo apobe…153 Monga munthu wosauka uyu anati: “Mwamuna wanga ndimwana wamwamuna, iwo akukondabe zinthu za mdziko ndizinthu monga choncho”…Mukuona, iwo sanakuvomerezekuwombola kumeneko, pakuti pamene iwe utero, izozimakutsuka iwe mwazokha. “Iye amene wabadwa mwaMulungu samachita tchimo.” Sipamakhalanso chikhumbo,mulibe kanthumwa iye ka zinthu za mdziko.154 Yesu anati, “Iye amene akonda dziko (Kosmos tsopano),kapena zinthu za mdziko, chikondi cha Mulungu sichirinkomwe mwa iye.” Iye sali mu chikondi ndi Mkwati. Mwaona?Choncho, iye ayenera kuti adzalipire chilango chimenecho,ndipo osati…Iye sali kudzapulumutsidwa mu nthawi imeneyo;iye ali kupulumutsidwa tsopano kuchokera ku imfa yamuyaya;koma iye adzayenera kuti adzadutse mu nthawi ya chisautsokuti adzayeretsedwe. Mukuona chimene ine ndikutanthauza?Tsopano, tsopano, izo—ine ndikukhulupirira izo zikukhazikitsafunso limenelo. Tiyeni tiwone, pali chinachakenso apa.155 “Chonde tafotokozani, chifukwa inu munanena kutipadzakhala pali chiwerengero chapang’ono chokha chidzapitemu mkwatulo.” Amene ali awa pa dziko lapansi amene atiadzasinthidwe. Yesu anati, “Khwalala ndiro chipata ndiponjirayo ndi yopapatiza, koma apang’ono adzakhalapo ameneati adzaipeze iyo.”156 “Nanga bwanji anthu amene akukhulupirira mwa Ambuyetsopano ndipo sali—ndipo osati momwe inu mukulalikirira?”Iwo sakusowa kuti akhulupirire izi. Iwo sakusowa kutiachite kukhulupirira momwe ine ndimalalikirira izo. Mwaona?Sakusowa kuti achite kukhulupirira izo. “…kwa Uthengawa tsiku lotsiriza. Kodi iwo adzapulumutsidwa?” Inde, ngatiiwo akhulupirira Ambuye. Mwaona? Ndipo ngati iwo—ngatiiwo azitsutsa ndi kumati, “Ine sindikukhulupirira kuti Iyeali Mawu. Ine sindikukhulupirira kuti izi ndi zolondola.Ine sindikukhulupirira mu ubatizo wa Mzimu Woyera,” izozikusonyeza kumene iwo ali nkupita, nthawi ya chisautso. Komaiwo amene angawalandire Mawu mu chidzalo Chake, osati inendikuwalalikira Iwo, chifukwa Liri Baibulo likunena choncholo.Awo amene akuvomereza izo ali mfulu, chifukwa iwo—Mawuanaweruzidwa kale.157 Tsopano, kodi Woweruza wolungama angamuweruzemunthu kawiri pa chinthu chirichonse ngati chilangochochinalipiridwa? Ngati ine ndikanakhala ndiri mu sitolo yapinyolo, ndipo inu nkubwera uko ndipo mukanati, “Ine

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1041

ndikuti ndimuwombole iye”; ndipo inu mukanalowa umondipo mukanalipira mtengo wa kuwomboledwa kwanga(ndipo icho ndi chilango changa cha kukhala ndiri musitolo ya pinyoloyo), ndipo inu munalipira chiwombolochanga, ndiye wopinyolitsayo anganditengenso ine kachiwirichotani? Kupatula ine nditagulitsidwanso kachiwiri. Ndi inupamenepo. Pamene ine ndinakana Chidzalo cha Mawu, ndiyeine ndinabwereranso mu sitolo ya pinyolo kachiwiri. Mukuona,mwaona? Ndiye ndimenyeretu njira yanga yotulukira mmenemondiye, ngati ine ndingathe. Koma Iye anandiwombola ine.Chabwino. Ine ndikuyembekeza kuti izo…ine—ndangokhalanazo zochuluka kwambiri pano ine ndikufuna kuti ndizitenge izizimene…[Kutha kwa mbali yoyamba ya tepi. Mbali yachiwiriikuyamba ndi gawo la funso likusowapo zina—Mkonzi.]

248. …Chikoka Chachitatu ichi ndipo chiri kuyankhulaMawu. Izo zikuwoneka kwathunthu zotheka kwa iwe kutiuyankhule mawu ndipo wina akhoza kubwezeretsedwakwathunthu ndi modzaza, nkuikidwa mwamphumphumokonzekera mkwatulo mu chiukitsiro, Mwana wamunthu. Izi ziri chomwecho, kapena kodi izo sizirichoncho? Ndipo iwe ungachite izi ngati iwe utapsyinjikabwino bwino, kodi iwe “Sungathawe ayi zinthu zonsezi(pali kubwereza pamenepo)—kuthawa zinthu zonse izi ndikukaima pamaso pa Mwana wa munthu”? (Luka 21:36)

158 Tsopano, m—mzanga wokondedwa. Mwaona? Tsopano,ine ndikuganiza apa kuti i—i—inu muli—inu muli ndimaneno abwino. Inde, bwana! Inde, bwana! Tsopano, izozingakhale chomwecho. Inu munati, “M’bale Branham…”Mwakuyankhula kwina, ndi ichi chimene ine ndiri…Inesindikuganiza izo ziri…ine ndingati…ine ndikukhulupirirai…Sikuti ndikupukuta zimene inu munanena, koma inendikukhulupirira ine nditha kuzipangitsa izo kuti zimvekepobwino pang’ono kwa anthu. Mwaona? Inu mukukhulupirira,chifukwa cha Mawu Oyankhulidwa ndi zinthu zonga izo zimeneIye anazikamba. Ndipo nonse inu pano munachitirapo umboniagologolo ndi zinthu zina zonse izi zimene zachitidwa. Komakodi inu munazindikira, kuti zimenezo zinaperekedwa mwaKuchitakwayekha! Ine sindinamupemphe konse Iye, “Ambuye,ndiroleni ine kuti ndichite izi, ndiyankhule zinthu izi mongachoncho, ndichite zinthu izi pamenepo.” Ine sindinamupemphekonse Iye zimenezo. Iye mwa chifuniro Chake cha Umulunguanabwera kwa ine ndipo anati, “Iwe pita ukachite izi.”Mwaona?Ine sindinali kupempha chinthu chimodzi cha izo. Mosesanapemphe konse kuti apite mu Igupto kuja, koma analiMulungu amene anamutumiza iye ku Igupto kuja.Mwaona?159 Tsopano, ine ndikukhulupirira kuti Mzimu Woyeraungabwere kwa ine ndi kunena mu masomphenya, “Pitaukamuuze munthu wakuti, wakuti kuti iwo sali—iwo akuyesera

1042 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kuti agonjetse chinthu chinachake, ndipo iwo sangathe kuchitaicho. (Ndipo iwo akusuta; iwo akumwa; iwo akunama, akuba,kapena akuchita chigololo, chirichonse chimene chingakhalechiri; kapena iwo ali ndi mzimuwachisiliro.) Ndipo iwe ungopitakulikonse kumene iwo ali ndi kukati, ‘Iwe mzimu, tulukammenemo; ine ndikumumasula wamumsinga uyu paufulu.’”Kodi izo zingachitike? Mwamtheradi! Inde, ndithudi, izomwamtheradi zingatero; izo zingachitike. Koma tsopano, pakupenekera kwanga kwanga…Tsopano, kupenekera ndipo—kumatanthauza “kuchitapo wopanda ulamuliro.” Mwaona? Inendingapite kumeneko kuti ndikamuthandize munthu ameneyu;ine ndikungopenekera kuti izo zikhala ziri bwino bwino.Mwaona? Ndiye ine sindikudziwa; ine ndikhoza kutchuliraDzina la Ambuye pa iwo; ine ndikhoza kuwapempherera iwo,kuchita chirichonse chimene ine ndikukhumba kuchichita.160 Ngati ine ndikanakhala nayo njira yanga yanga mmawauno…i—ine ndinangokhala ndi kuyankhulana ndi donawamng’ono uyu amene wakhala mu chikuku ichi. Kuti abwereku msonkhano uno lero, iwo anachita kubweretsa ozimitsamoto kuti akamuchotse iye mu nyumba yake ku Chicago; ndipoanthu amakhala patsidya la msewuwu ndipo samabwera kumisonkhano. Mwaona?161 Kodi ine ndikanachita chiani? Ngati izo zikanakhala mumphamvu yanga…Izo ziri mu…Ine ndiri nawo ulamulirowoti ndichitire izo, koma ine ndimayenera kuti ndizidikirirakulamuliridwa kuti ndichite zimenezo. Mwaona? Ine ndiri nawoulamuliro wochokera kwa Mulungu kuti ndizichita izo; komatsopano, pamene Iye ati apereke kulamulirako, iye akhozakubwerera kwawo ali bwino. Mwaona? Ine ndikudziwa kuti izondi zoona. Mwaona? Ine ndikanangokhala wololera kuti ndifemmawa uno pa izomomwe i—ine ndikanakhalira pa chirichonse.Mwaona? Zimenezo ndi zoona.162 Koma poyamba, inu mukuona, ndi zonse zimenezo…Palibemmodzi, ngakhale Yesu Mwiniwake ankati, “Mwana sangathekuchita kanthu mwa Iyeyekha, koma zimene Iye awaona Atateakuchita, zimenezo Mwana amazichita chimodzimodzi.” Ifetikudziwa zimenezo. Yohane Woyera 5:19. Chabwino. “Mwanasamachita kanthu mwa Iyeyekha, koma zimene Iye awawonaAtate akuchita, zimenezo Mwana azichita chimodzimodzi.”Chabwino.

249. Kodi masomphenya amene munali nawo zaka zapitazoa chozizwitsa chachikulu choti chidzachitike pafupi ndiCorydon, Indiana, anafika pochitika konse?

163 Ine ndinayang’ana mu bukhu langa pamene ine ndinapezaili ndipo ndinaikapo chizindikiro chofunsira. Tsopano, panalipokuti padzakhale nthawi imene ine ndinali—ndimayenerakumadzayang’ana kumene mitengo ya mikunguza iyo…

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1043

Basi pamene iwe uyamba kutsika phirilo kumeneko, kumbaliinayo, kupita mmusi chaku Corydon, utachoka pamwamba paphirilo ku New Albany, ine ndinali woti ndisamale mitengoya mikunguza chifukwa cha ngozi yowopsya imene inendikanadzakhala nayo. Ndipo mwa chisomo cha Mulungu,ine ndinapulumuka kwa iyo pamene msungwana wamng’ono,akumwa botolo la mowa, anaphedwa—khosi lake linadulidwaapo pomwe ndi botolo limene iye anali nalo mkamwamwake, msungwana wa usinkhu wa zaka sikisitini, ndipo inendikanakhala ndiri apo pomwe pa nthawi imeneyo. Mwaona?Tsopano, izo mwina zikhoza kukhala zimene inu mumazinena.Ine ndinaziwerenga zimenezo.164 Ndiyeno aponso, pamene ine ndinali ndi msonkhano uwumwa M’bale Beanblossom…Izo zikhoza kukhala ziri zimenezo.Izo zikhoza kukhala kuti anali Georgie Carter. Mwaona? Iyoinali ina imene inachitika kumeneko. Ndiyeno pali anai kapenaasanu a iwo pamenepo…ine sindinawone kalikonse komakamene kanachitika. Ng—ngati munthu amene analemba iziangalembenso izo kachiwiri ndi kundiuza ine zimene inendinanena pa nthawi imeneyo, ndiye ine ndikaziyang’anaizo. Mwaona? Ngati inu mutangondiuza ine zimene inendinanena, masomphenyawo…Chifukwa ine ndinazindikiramumasomphenyawo uko zinthu zimene ine ndinaika mu bukhu,ndipo ndi izi apa pamene izo zinachitika monga chonchi. Inendinalibe kalikonse kataikidwamo, kamene ine ndinkadziwa,chinthu chotsimikizika chirichonse kunja kwa icho.165 Ndiyeno apo panali chinthu china; icho chinali kutembenukakwa Omar Price kumusi uko panthawi imeneyo pamene iyeanali wotsutsa kwambiri kwa ine. Ndipo inu mukudziwa, iyeanabwera ku kachisi ndipo anadzabatizidwa mu Dzina laAmbuye Yesu. O, iye ankamenyana nane molimba kwambiripa zimenezo; ndipo ine ndinakhala limodzi naye pa nthawiya usiku. Ine ndinangopitirira kumukonda iye, ndinangokhalapomwepo chimodzimodzi basi; koma potsiriza iye anabwera,chifukwa Ambuye anandiuza ine kuti iye akanati abwere, ndipokotero i—ine ndinangokhala nazo izo. Mwaona?166 Chinthu chofanana ndi mlaliki wamng’ono wakhalakumbuyo kwangaku pano. Ine ndinapita uko ku Clarksvillekuti ndikayankhule naye iye nthawi ina, kukamuyankhuliraiye mu mpingo wa Methodisti, ndipo iye anali wa Methodistimwathunthu ndi mwathunthu—chimene ine ndikutanthauza.Ine ndinabwerera kuno; ine ndinati, “Tsiku lina inendidzamubatiza iye mu Dzina la Ambuye Yesu Khristu.” Ndipoine ndinatero; ameneyo ndi M’bale Neville!250. Ngati kuli kolakwika kuti ine kuti—kodi ndi zolakwika

kuti ine ndiziyendetsa—sitolo ya zokongoletsa? Ine ndinewokongoletsa ndipo ine sindimakhulupirira kuti Akhristuazidula tsitsi lawo, koma ine ndimawadula ena ndipo

1044 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

(ine ndikulingalira kuti ndi k-u-l-o-c-h-a, kulocha, izozikutanthauza mitundu, ine ndikuganiza, sichoncho izo?)Kuika mitundu naponso.

167 Mlongo wokondedwa, ine ndikanati—ine sindikanadziwachoti ndikuuzeni inu. Mvetserani, ine sindingathe kunena kwaakazi za zimenezo, kuika mtundu mu tsitsi lawo. Ine ndiribeLemba lotsutsa zimenezo; ine ndingathe kumangokhala ndiLemba. Mwaona? Lemba silimanena kuti iwo asamachite izo.Lemba limanena kuti iye azikhala ndi tsitsi lalitali, ndipopambuyo pa izo, ine sindikudziwa koti ndipite. Mwaona? I—inesindikudziwa kanthu kena za zimenezo.168 Tsopano, mlaliki wamng’ono amene ali pano penapake inendikudziwa, bwenzi wokondeka wa ine, ife tinali kuyankhulanapalimodzi tsiku lina ku Blue Boar pamene ife tinali kulandirachakudya. Iye anati, “Mkazi wanga akukhala ngati akuchitamanyazi kuti abwere pamaso panu.”Mkazi wachiyero kwambiri,waumulungu, wachichepere, ndipo iye ndi—dona wamng’onowokongola, gogowamkazi, ndi…Koma iye ndi wabwino,waukhondo, kwenikweni…Mkaziwanga amatengeka naye basimkazi uyu, n—ndipo ine ndikuganiza iye ndi mkazi weniweni,mwenimweni. Iye…Ine sindikudziwa ngati iye ali muno; inendikulingalira iye ali muno. Ine ndikuganiza mwamuna wakeali muno. Ndipo iye anati kwa ine; iye anati, “Iye analisiyatsitsi lake kuti lizikula pambuyo pa kukumvani inumukulalikirandipo iye akuwona kuti izo zinali zoona, koma,” anati, “iyewakhala akugwiritsa ntchito mitundu ina mu tsitsi lake; ndipoiye akuyeseramwakukhoza kwake kuti apangitsemitundu yonseichokemo kuti likule iyeyo asanabwere pamene inumuli.”169 Tsopano penyani, Mlongo wokondeka, ine ndikulemekezamwapamwamba zimenezo. Ine ndiri nako kulemekeza kwamkazi amene angachite zimenezo. Kuti mkazi wina kutiangobwera apo ndi kulikonza tsitsi lake mulimonse, kapenakulavulira pa mapazi ako ndi kumayendayenda apo mwamwanondi mopanda kulemekeza konse, kumbukirani, Yesu anati,“Zimene inu muchitira kwa awa, inu mukuchitira izo kwa Ine.”Mwaona? Ndipo ine ndikulemekeza zimenezo mwa inu, ndipoMulungu akudalitsani inu chifukwa cha izo.170 Koma, Mlongo, za mtundu wa tsitsi kapena chinachakechonga izo, i—ine sindikudziwa. I—ine sindingathe kuziikirakumbuyo izo ndi Lemba, kotero i—izo ziri basi kwa inu.Inu mukuona? Inu, ngati inu mukufuna kuti muzichita izo,zimenezo ziri zangwiro bwino bwino ndi ine. Momwe inendikudziwira, mpingo ulibe mwambo woterowo. Ngati inumukufuna…Chirichonse chimene mulibe mu Baibulo ili,chabwino, inu basi…Zimenezo ziri kwa inu. Inu mukuona?Koma ine ndingangokupatsani inu langizo langa, inu mukuona,ndi momwe ine ndikanadziwira…Inu mukudziwa, basi ndi

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1045

chibadwa cha mkazi kuti aziwoneka wokongola; iye amayenerakuti azikhala mwanjira imeneyo.

171 Inu mukudziwa, mu moyo uliwonse umene ulipo,champhongo ndicho chokongoletsetsa, kupatula mtundu waumunthu. Mukatenga mbalame iliyonse, ng’ombe. Kutengagulu la ng’ombe. Nditi iti ili yokongoletsetsa, ng’ombeyokalamba ya nyanga-zokwinyika kapena nkhuzi yaikulu?Tengani gwape; ndi uti, wathazi kapena tonde? Tenganigulu la mbawala; yokongoletsetsa ndi iti, yatonde kapenayathazi? Insa, chirichonse chimene inu mukufuna kuti muchite.Tengani i—tengani izo mwa mbalame; tengani izo mwankhuku, tambala kapena nsoti? Tengani izo mwa mbalame,yaing’ono—yamphongo yaikulu yokongolayo kapena nsotiwawung’ono wamangamangawo, utakhala pa chisa chake ndikumautamira mazira ake? Mwaona? Chirichonse mu mtunduwonse, nthawizonse—champhongo ndicho chokongoletsetsa,koma wamkazi kwa umunthu. Bwanji? Iye anayambitsa kugwa.Satana anamusankha iye apo pomwe, ndipo kukongola ndi kwamdierekezi. Mwaona?

172 Satana anali mngelo wokongola kwambiri. Iye analimkerubi amene ankaphimba. Penyani kusiyana kwake momweakazi akukhalira. Ndi angati akumukumbukira Pearl—anawerenga za Pearl O’brien? Tiyeni tiwone manja anu, enaa inu anthu achikulire. Zedi. Mwaona? Akuyenera kuti analimkazi wokongola kwambiri mu Amereka. Msungwana wamu zaka khumi aliyense wonyang’ama pa msewu angakhalewokongola pawiri mwa momwe iye aliri tsopano. Bwanji?Ndizo ndendende basi zimene Baibulo linanena: “Pameneana a Mulungu anawawona ana aakazi a anthu kuti analiokongola…” Limenelo linali gulu la zigawenga limenelinapangitsa chigumula pamwamba pa dziko lapansi, kutiMulungu anawononga mtundu wonse wa umunthu. Mwaona?Ndizo ndendende. Ndipo lero chirichonse maziko ake ndiHollywood n—ndipo kukongola ndi zinthu monga zimenezo,pamene kukongola chiri chinthu chachinsinsi cha mtima(mwaona?) ndipo osati mawonekedwe akunja. Asiyeni iwoazidzikongoletsa okha, osati ndi mawonekedwe akunja,koma amkati, a kufatsa, mzimu woleza. Uyo—ameneyo ndiyeMkhristu.

Kotero tsopano, pa funso lanu, Mlongo, ine sindikudziwabasi zoti ndikuuzeni inu.

Tsopano, ine ndikhoza kuima panali pano kapena kutengamaminiti ena sate ndiye, ndiyeno…Kodi maminiti sateangati…? Ndi angati angakhale alipobe maminiti ena sate,ndiyeno zimenezo zitipatsa ife kanthawi kowonjezera pang’onousikuuno. Chabwino, ine ndithamangamofulumira ndiye.

1046 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

251. M’bale Branham, kodi l Timoteo uyu 2:9 akutanthauza kutimkazi sangathe kuluka tsitsi lake? Kodi tsitsi “lotiwidwa”limatanthauza tsitsi “lolukidwa?”

173 Tsopano penyani, Mlongo, tsopano izi…I—inendikukondwa kuti ilo latsatira ili. Ine sindinachite kuliika ilopamenepo, koma basi i—ilo latsatiramwabwino chotero.

Zindikirani, tsitsi lolukidwa mu tsiku limenelo linalichisonyezo cha mkazi wamumsewu; izo ndi zimene iyeankachita, ankaliluka tsitsi lake. Ndipo Paulo ananenakwa Akhristu, “Tsopano, kakongoletsedwe, kasakhale kakuluka…” (kapena ‘kutiwa’ ndi ‘kuluka’ ndi chinthuchofanana)—kuluka tsitsi lawo, chifukwa izo zinkawoneka ngatidziko lina lonse.

174 Tsopano, inu simukuyenera kuti muziwoneka monga dzikokapena kumachita monga dziko! Mwaona? Akazi akuyenerakuti azikhala osiyana pamenepo. Mwaona? Ayi, tsopano, kulukatsitsi…Tsopano, lero tsitsi lolukidwa ndi lokongola, ndipo liriulendo wautali kuchokera ku fashoni ya mdziko. Tsopano, inumumawawona akazi, momwe iwo akuchitira ndi tsitsi lawolero…Muzingolisunga tsitsi lanu mu njira iliyonse; kungotimusamawoneke ngati dziko! Mwaona? Musati muziwonekakapena kuvala monga ilo! Ngati iwo akuvala akabudula, inumuzivala diresi. Ngati i—ngati iwo akuchita tsitsi lawo lonse—kulimeta ilo lonse ndi kulidula ilo, ndi kumachita izo konse…I—i—inumungolisiya lanu lokha. Mwaona?

175 Ndipo kuluka—koma lolukidwa…Funso linali: Kodi“lolukidwa” limatanthauza—“lotiwidwa” kutanthauza“lolukidwa”? Inde, uko nkulondola. Ndipo tsopano, pamsewu…

176 Tsopano, ine ndinaziyang’ana izo bwino kuti ndipezepo zakazapitazo chimene tsitsi “lolukidwa” linkatanthauza. Mwaona?Mkazi, mwakuchita, akazi akale, iwo ankangolikokera tsitsilawo mmbuyo ndipo ankalimanga ilo, mochuluka ngati nchirawa kavalo lero. Ndipo iwo ankayendayenda…Iwo ankakhalaatavala mikanjo monga choncho, koma akazi apa msewuankatenga tsitsi lawo ndipo ankaliluka ilo pa mitu yawoponse, ndi kulimanga ilo mozunguza monga choncho, ndikuika maluwa mu ulo ndi zinthu monga choncho, ndipoizo zinali ngati—wodzigwedeza pa msewu; monga momwe ifetingamuwone wodzigwedeza lero, momwe iye amavalira. Inendikuti wodzigwedeza, chifukwa inu mukudziwa ndine bambowachikulire; kotero icho ndi chimene iwo ankawatcha iwo mumasiku amenewo. Kodi iwo akuwatcha iwo chiani lero? I…Mai, ine sindikudziwa. Anapiye kapena chinachake kapenachimzake. Kotero…Chirichonse chimene icho chiri. Apatseniiwo dzina lamtundu uliwonse, iwo amalikonda ilo.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1047

252. M’bale Branham, inu munanena pa imodzi yamatepi kuti Nowa anapulumutsa apanyumba ake.Kodi izi zikutanthauza mayi akhoza kukhala ndichikhulupiriro chofanana kwa apanyumba ake? Ndipokodi izo zikutanthauza kuti aliyense wa pa banjapoadzapulumutsidwa ngati ife titakhulupirira izo?

177 Tsopano, izo ndi—eya, izo ndi zokhala ngati…Inumuyenerakusamala momwe ine nditi ndiyankhire ili tsopano. Mwaona?Choyamba, “Inu munati…(Tsopano, ndiloleni ine ndiwonebwino.) Inu munanena pa imodzi ya matepi anu kuti Nowaanawapulumutsa apanyumba ake.” Bwanji? Chifukwa iwoanakhulupirira. Ndi zimenezo, chifukwa iwo anakhulupirirauthenga wake.178 “Kodi izi zikutanthauza kuti mayi akhoza kukhala ndichikhulupiriro chofanana kwa apanyumba ake?” Inde, Mlongo!Ine ndikutha kuwona mtima wa mayi wamng’ono ukuliriraanthu ake. “Ndipo kodi izi zikutanthauza kuti aliyense wam’banjamo adzapulumutsidwa ngati ife tikhulupirira izo?” Inde,ngati iwo ati azivomereze izo. Ndiko kulondola.179 Kumbukirani wamndende waku Filipi. Khulupirira pakutiinu nonse…Ngati iwe uli nacho chikhulupiriro chokwanirakwa chipulumutso chako chako, kodi iwe sungathe kukhalanacho chikhulupiriro icho chomwe chimene chidzagwire ntchitopa anthu anu? Kodi chikhulupiriro ndi chiani? Ndi mphamvuyosawoneka. Mwaona? Ndi chiani—ndi chiani—ndi Mzimu.Mzimu Woyera umabweretsa chikhulupiriro. Mwaona? Ndimphamvu yosawoneka.180 Chifukwa chiani ine ndingamaike manja pa odwala?Mwaona? Ngati ine ndingathe kukhala ndi kukhudzana naokwandekha ndi mzimu umene uli mwa munthu ameneyopamenepo, chinachake chingachitike. Mwaona? Apa pamaimaMzimu Woyera; Iye amawulula zinsinsi za mu mtima. Iye achitandendende basi zimene Iye ananena kuti Iye adzachita mu tsikulotsiriza. Anthu amakhulupirira zimenezo; iwo amayang’ana paizo, “Inde, bwana, ine ndikuzikhulupirira izo.”181 Tsopano, ngati ine sindingati ndingokhala wawambakwambiri kwa inu (mwaona?)—kumakhala chinthu chawambachabe. Inu muzingothamanga kudutsapo tsiku lina ndikungothamanga kudutsapo tsiku lotsatiranso. Mwaona? U—uko ndiko kungotengerapo mwayi. Inu simuli kuzikhulupiriraizo pa kuyamba pomwe (mwaona?), chifukwa mwamsanga basipamene inu mukhulupirira kwenikweni izo…Mkazi uja anati,“Ngati ine ndingathe kukhudza chovala Chake, ine ndipangidwakukhala wamphumphu pa chidutswa chirichonse,” ndipo iyeanachita izo. Mwaona? Iye sananene kuti, “Siyani ine ndiyesereizo kachiwiri.” Mwaona? Iye anakhulupirira izo. Mwaona?Ndizo—ndizo…

1048 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

182 Tsopano, ngati inu mutati mungokhulupirira ndi zonsezimene ziri mwa inu kwa banja lanu…183 Tsopano, monga apa, nchiani chimandipangitsa ine? M—mphamvu iyi ndi chiani mu nkono wanga? Iyo ndithudi siakatumba anga, ndi mzimu wanga. Ndithudi, mukatulutsamomzimu umenewo, ndiyeno akatumba awa achita chiani? Iwoakhala okufa momwe iwo angakhalire. Mwaona? Iwo avunda,koma ndi…Mukuona, ndimzimu umene umalimbikitsa.184 Tayang’anani pa Samsoni wamng’ono. Ambiri a iwoankawona zitseko zinkawoneka ngati pakati pa mizati iwiriiyi apa. Bwanji, mwamuna wamkulu chotero angayambanenawo mkango ndi kuwukhadzula iwo mzidutswa, M’baleJackson.Mkango utalumphira pamwamunawonga ameneyo ndichitseko—wokhala ndimapewa onga chitseko cha barani, bwanjizedi, zimenezo sizikanakhala zozizwitsa ayi; koma chozizwitsachinali, iye anali basi kachiwala kakang’ono kwambiri kamutu wa tsitsi lotiwidwa, wamng’ono kwambiri, munthuwamkulu, pafupi—wachikazi pang’ono, mnyamata wamng’onowa amayi, mangongo asanu ndi awiri achikazi akulendewerakumbuyo kwake. Koma inu mukazindikira, iye anali wopandachomuthandiza monga chirichonse mpaka Mzimu wa Ambuyeutabwera pa iye. Ndipo pamene Mzimu wa Ambuye ubwerapa iye, mkango umenewo unathamanga ndipo unabangula, iyeanangowukhadzula iwomzidutswa. Uyo sanali Samsoniyo; Uwounali Mzimu wa Ambuye.185 Tsopano, iye angatenge bwanji fupa la chibwanu chabulu, limene linali liri ku chipululu kuja ndipo chitasulukakukhala loyera…Ndipo zipewa za Afilisti zimenezo zinalipafupi inchi kukandapala kwa mkuwa wolimba. Chabwino, inumukatenga chibwanu chimenecho ndi kuchimenyetsa icho pachimodzi cha zipewa zimenezo, icho chingapite mu zidutswachikwi. Inu mukudziwa zimenezo. Iwo akanamenya, chibwanochakale chowuma icho…Koma penyani pamenepo, iye anaimapamenepo ali ndi fupa la chibwano icho mdzanja lake ndipoanawakanthira pansi Afilisti chikwi; ena onse a iwo anathawiraku mathanthwe. Iye anati, “Zibwerani kuno, inu mukufuna zinaza izonso?” A—apobe atagwirizira icho! Kodi chinali chiani icho?Mzimuwa Ambuye unadza pa iye. Mwaona?186 Choncho, Uwo ndi Mzimu wa Ambuye. Ndipo pamene inumuli nawo Mzimu wa Ambuye mwa inu kuti mukukhulupirirakwa chipulumutso chanu chomwe, chiikeni icho pa banjalanu. Kuti, “Ine ndikudzitengera iwo mu Dzina la YesuKhristu; ine ndikudzitengera ilo! Mulungu, ine sindikudziwamomwe Inu muti mupangire kuti iye achite izo, ndi momweInu muti mumupangitsire iye kuti achite izo, koma inendikukhulupirira izo. Ine ndikukhulupirira izo, Ambuye!Thandizani kusakhulupirira kwanga.” Dzitengereni izo ndipopenyani zomwe ziti zichitike. Icho chichita izo.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1049

253. Kodi Mkwatibwi—kodi Mkwatibwi asanabwere Yesu, kodiIye adzakhala nazo mphamvu zonse za Mzimu Woyerakuti azidzachita zozizwitsa, kuwukitsa akufa, ndi zinazotero monga mu mvula ya masika—kapena kodi mvulaiyi ya masika ndi ya kwa Ayuda 144,000? Kodi atumikionse adzakhala nazo izi, kodi ife—kapena kodi ifetikuyembekezera kudzako kokhako?

187 Inde. Ukuona, mzanga, i—i—ine sindine wafioloje. Inesindinewafioloje; choncho, ine ndimayenera kuti ndiziphunzitsazonse zimene ine ndikudziwa za Baibulo kuchokera kumithunzi ndi zoimira. Inu mumakhala ngati mumanditcha inewofanizitsa. Koma ngati ine ndingayang’ane pa khoma ilo, ndipoine ndisanayambe ndadziwonapo ndekha; ndipo ine poyang’ana,ndipo ine ndingathe kuwona kuti ine ndiri nawo mutu, ndimakutu, ndimanja, ndipo—ine ndidziwa chinachake chamomweine nditi ndidzawoneke monga ngati ine nditi ndidzaziwonendekha konse. Mwaona? Ngati ine ndiwona kuwonekera kwangapa kalilole, ine ndidziwa momwe ine ndikanaonekera ngati inendikanatha kuyima pambali ndi kudziyang’ana pa ndekha.188 Tsopano, umo ndi momwe ine ndimaganizira za Baibulo.“Zinthu zonse izi,” Aroma 26 anati, “zinachitika kwa zitsanzozathu.” Ife tikhoza kumayang’ana mmbuyo ndi kuwona zomweizo zinali, monga mwezi kunyezimiritsa dzuwa. Ife tidziwachimene dzuwa liti lidzakhale pamene—ngati ife sitinayambetaliwonapo dzuwa; ife tikhoza kuwuwona mwezi, ndi kuwonakuti ilo lidzakhala lopambana kuposa uwo. Chabwino, pameneinu muwona zimene zinkachitika mu Chipangano Chakale, ndichinyezimiritso basi cha zimene zikuchitikamuChatsopano.189 Tsopano, mkati umu, ine ndikukhulupirira ndi mtimawangawonse i—ife tiri, kapenamasiku ano…Ngati ife sitiri, winawakeali; izo zikuyenera kukhala ziri. Nthawi yatha; ife tiri pamapeto!190 Yense…Dziko…Mulungu anapanga dziko mu zaka zikwizisanu ndi chimodzi, ndipo chikwi chachisanu ndi chiwiri Iyeanapuma. Iye anati munthu sadzakhala konse moyo nthawiimeneyo nkuitsiriza—c—chaka—kapena—kapena tsiku—“tsikulimene iwe udzadye, tsiku limenelo iwe udzafa.” Adamu—kapena Metusela anali munthu wamkulu kwambiri ameneanayamba wakhalapo moyo mu Baibulo, ndipo iye analiwausinkhu wa zaka 969; ndipo iye sanakhale moyo konse zakaChikwi zija. Koma munthu amene ati adzakhale moyo kupyolamu Zakachikwi, zaka chikwi chimodzi, nkuti asonyeze k—kuti chilango chinalipiridwa kale…Munthu akukhala moyokwanthawizonse; tsiku latha; nthawi yatha; iwo alimumuyaya.191 Tiri chiyankhulire, ine ndalandira makalata ochulukakwambiri pa uthenga wanga wa ma Lamlungu awiri kapenaatatu apitawo pa—Kwawo Kwa Mtsogolo kwa Mkwatibwi ndi

1050 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Mkwati.Zimenezo ndithudi zinawakhudza pamalo ambiri a iwo.I…Izo zinatero kwa ine aponso. Ine sindinafike pondithera izo.192 Tsopano, zindikirani. Pa izi (mwaona?), Abrahamuanawona…Tsopano, monga Iye ankachitira naye Abrahamu,chomwechonso Iye akuchita ndi mbewu yake. Tsopano, limodzila masiku awa pamene ine ndidzabwerera nthawi ina, inendikufuna kuti ndidzatenge izo pafupi mochuluka pang’ono ndikudzakuwonetsani inu ndendende malo a moyo wa Abrahamu.Zinali ndendende ndi Lutera, Wesile, ndipo mpaka mmusikufika kuno, ndendende basi momwe Iye anachitira ndi mipingomonga Iye ankachitira ndi Abrahamu; momwe Iye anawonekera;momwe kuti apo pamene Iye anatsimikizira pangano kwa iyepansi pa magazi okhetsedwa, uwo unali m’badwo wa Filadefia.Inde, bwana, umenewo unali m’badwo wa magazi, Lutera—m’badwo wa Wesile.193 Komano penyani m’badwo wa Chipentekoste. Iye atafikakale kumeneko, Iye anapanga lonjezo la El Shaddai, “yamwakuchokera kwa Ine.” Funso ndi lakuti: Kodi inu mungayamwe?Izo zinabweretsedwa pamaso pa Achipentekoste. Mwaona?Kodi inu mungayamwe? Koma iwo sanachite izo; iwoanambwandira awo—mabere a ku chipembedzo kumene iwoanatulukako. Komano Mbewu, Mbewu yeniyeni, inabwera apokuti idzayamwe mabere amenewo.194 Ndipo kodi chizindikiro chotsiriza chimene iwo anali nachochinali chiani, asanafike mwana wolonjezedwa uja amene analiatamudikirira zaka zonse izi, pamene Iye anabwerera? Iyeanali Mulungu ataima mu mawonekedwe a Munthu ndipoankakhoza kuzindikira maganizo amene anali mu mtima waSarah (Sarah pokhala Mpingo, woimira Mpingo)—kuzindikiramaganizo amene ali muMpingo umene unali ngakhale kumbuyokwa Iye. Ndi kulondola uko? Ndipo mwamsanga zitachitikazimenezo, iye anasintha nabwerera ku utsikana ndi iyemnyamata; ndipo Isaki anabweretsedwa powonekera, mwanawolonjezedwayo.195 Ine ndikukhulupirira kuti inu mukuwona chinthu chotsirizachimene chiti chichitike kwa Mpingo usanachitike mkwatulo.Ndizo ndendende. Ine ndikukhulupirira zimenezo. Mvula yatha.Ingowerengani mitu itatu yoyamba ya Chivumbulutso ndipoinu muwona zimene zalonjezedwa kwa Mpingo. Izo ndi zimenezinalonjezedwa,Mpingo, apo pomwe—mibadwo yampingo.196 Inu munazindikira tsiku lina pamene ife tinayambamalipenga aja, Mzimu Woyera unati, “Zimenezo si za kuno.”Mukuona, mwaona?197 Tsopano, mvula ya masiku, Ayuda 144,000, ayi, izo sizimenezo—i—iwo sadzati—izo—ndi pamene Eliya ndi Mose…uko ndi kumene zozizwitsa ziti zikachitike. Zinthu zimene anthuakhala akuziyembekezera, Achipentekoste, pofuna zozizwitsa,

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1051

uko ndi kumene izo ziti zidzachitikire mmenemo—pansi pa iwo.Mukuona, umenewo ndiwaEliya ndiMose. Iwo akukantha dzikolapansi ndi matemberero mowirikiza momwe iwo afunira; iwoakutseka miyamba kuti isavumbe mu masiku a uneneri wawo.Ndipo Mulungu adzaima ndi kumawamenyera iwo monga Iyeanachitira, ndipo Iye adzawatulutsamo iwo pansi pa dzanjalamphamvu chimodzimodzi basi monga Iye anachitira ku Igupto(mwaona?), kuwachotsa ku “machitidwe” awa a mdziko. NdipoIye adzachita zimenezo, koma zimenezo sindizo…198 Ife tiri woti tizingodikirira pa kudza kwa Ambuye.Zingodikirirani; sungani nyali zanu zitakonzedwa, zonse zikhalezodzazamafuta. Zipempherani ora lirilonse, osati tsiku lirilonse,ora lirilonse. Muzingokhala okonzeka; khalani okonzeka,khalani okoma, ndi kuyang’anira…

O, tikudikirira kudza kwa tsiku lokondwa laZakachikwi ilo.

Pamene Ambuye wathu odala ati adzabwerendi kudzamutengera Mkwatibwi Wakewoyembekezera napita.

O, mai—o, mtima wanga wadzadza ndimkwatulo pamene ine ndikuvutikira,kudikirira, ndi kupemphera,

Pakuti Ambuye wathu akubweranso padzikokachiwiri.

Ndi zimenezotu; ndicho chiyembekezo chaMpingo ora lino.254. Kodi Dzina la “Yesu Khristu” ndi labwino kwa ubatizo,

kapena kodi izo zimayenera kumakhala mu Dzina la“Ambuye Yesu Khristu”?

199 Liri lonselo. Ine ndimatenga la Ambuye Yesu Khristu(mwaona?), chifukwa ine ndikuganiza Iye ndi Ambuye wathu.Tsopano, Dzina la Yesu chabe, monga ena mwa abale athuamabatizira, i—ine ndimasiyana nawo pamenepo (mwaona?),chifukwa ine ndikudziwa ine ndiri nawo abwenzi ambiri dzinalawoYesu, ochuluka a—ochuluka a amzanga olalikira kuMexico,n—ndi Italy, ndi ena otero. Iwo amawatcha iwo Yesu, ndipokoteroYesu si zokwanira. Iye anabadwa ali KhristuMpulumutsi,monga Iye anabadwa ali Mpulumutsi, Khristu, wodzozedwayo.Ndipo masiku asanu ndi atatu kenako Iye anapatsidwa dzinala Yesu. Mwaona? Ndiye Iye anali Ambuye Yesu Khristu. Ndichimene Iye anali. Chabwino.255. M’bale Branham, kodi Ambuye angakulolezeni inu kuti

mutilangize ife pa funso la chikwati ndi chilekano panthawi ino? Funso: Kodi mwamuna angakwatire mkazindi kusudzulidwa ndi iye ndiyeno nkukwatira winanso?Ngati onse a iwo akwatira wina, kodi iwo onse akuchitachigololo? Inu munatchula kuti izo zidzalumikizana mumbewu ya serpenti. Mmotani izo?

1052 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

200 Tsopano, pano—pano pali limodzi la mafunso ovutitsitsakwambiri amene ife tiri nawo mu mulu uwu, ndipo ilo ndilofunsidwa kwambiri m—m—mu dziko lero. Tsopano, ndimveniine, ndipo ine ndiri nacho chifukwa cha izi. Ngati inendikanabweretsa kwenikweni kwa mpingo uno ndi pa tepi iyimmawa uno, chinthu cholondola cha pa chikwati ndi chilekano,izo zingaphwasule mpingo uliwonse mu dzikoli, ngati iwoatamvetsera kwa izo. Mwaona? Ndiko kulondola.201 Tsopano, kotero ndithandizeni ine, apa pali Baibulopatsogolo panga, ine ndiri naye pa funso limenelo, PAKUTIATERO AMBUYE! Ndipo mbali zonse zimene zikutsutsanazoziri kulakwitsa. Onse amene amakwatitsanso wokwatiwayo ndizina zotero, iwo onse akulakwitsa pa zimene iwo akuchita, komapakati pakepo pali Choonadi, pakati pa msewu. Ine sindikufunakuti…Ine ndipanga tepi kaya ngati chinachake chindichitikiraine, ndiye abale akhoza kumaisewera iyo ine nditapita kale(mwaona?) kwa mipingo. Koma i—ine ndikufuna kuti ndipangetepi pa izo ndi kungokusonyezani inu pamene izo ziri; komampaka ine nditi ndimverere kutsogozedwa ndi Ambuye, inesindinena kalikonse za izo. Koma ine ndikumverera kuti pazinthu izi kuti ine ndikuyenera kumatsogozedwa ndi Ambuye;ngati ine sinditero, ine ndichita zowononga kwambiri kuposammene ndingachitire bwino. Mwaona?202 Tsopano, ine ndikufuna kuti inu muzindikire ichi. Funso:“Kodi mwamuna angakwatire mkazi ndi kusudzulidwa naye iyendiyeno mkukwatira wina; ndipo ngati onse a iwo akwatirawina, kodi onsewo akuchita chigololo?” Tsopano, bwenziwanga, ine sindikufuna kuti ndivulaze kumverera kwanu, komazimenezo ndi Choonadi. Yesu anati, “Aliyense amene akwatirauyo amene wachotsedwayo achita chigololo.” Mwaona? I—ine sindikufuna basi kuti ndinene zimenezo, koma icho ndiChoonadi.203 “Inu munanena kuti izi zidzalumikizira mu mbewu yaserpenti.” Mwaona? Ine sindikukumbukira kuti ndinanenazimenezo, koma mwinamwake ine ndinatero penapake,ndinanena chinachake cha izo.204 Monga tsiku lina, ine ndinasakaniza chinachake, inendinapezeka kuti ndinamvetsera izo, ndipo izo…inendinazigwira izo apo pomwe; ndipo izo ziri pa tepi, ndipoi—ine mwinamwake ndizimva kuchokera pamenepo. Pameneine ndinali kuyankhula za Malipenga Asanu ndi awiri,ine ndinanena kuti anali malipenga asanu ndi awiri. Inendimalozera ku phwando la Chipentekoste. Kuchokera paphwando la Chipentekoste mpaka asanu ndi awiri—mpaka—Malipenga, apo panali Masabata asanu ndi awiri. Masabataasanu ndi awiri anali pakati pa Phwando la Paskha kukafikapa Pentekoste (inu mukuona?), zimene zinkapanga masikufifite. Mukuona? Koma chimene ine ndinali kulozera kwa

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1053

icho, pokhala kuti, ine ndinati, “Izo zikutanthauza Mibadwoya Mpingo Isanu ndi iwiri.”205 Pa tepi imeneyo (ngati inu mudzapezeka mutsaipezaiyo kapena chirichonse)—pa tepi imeneyo ziyenera kukhala,kuti mwezi wachisanu ndi chiwiri zitachitika kuti zimenezozinkabweretsa umo p—Phwando la Malipenga, limenelinkatanthauza Mibadwo ya Mpingo Isanu ndi iwiri—miyeziisanu ndi iwiri, osati Masabata asanu ndi awiri. Masabata asanundi awiri anapita kwa…Ine ndinafotokoza izo pamenepo. Inendinati Masabata asanu ndi awiri, monga choncho, komanoine ndinapitirira nalo lingaliro lomwelo mopitiriza, pamene ulimwezi wachisanu ndi chiwiri litachitika Phwando la Paskha—kapena Phwando l—la Pentekoste, ndiye pamabwera phwandolo,mtolo utabweretsedwa umo, utaweyulidwa. Inu mukuonand—ndiye…Kumbukirani pamenepo, mtolowo ukusandulikakukhala mtanda wa mkate itatha nthawi imeneyo. Mwaona?Pamene—mtolo w—mtolo umodzi, ndiye wonsewo ukupita mumtanda umodzi. O, ndi kuphunzitsa kwakukulu pamenepo;ine sindinakhudze mphepete mwa zimenezo. Koma ngatizichitika kuti inu mwazigwira izo pa tepi yanu, kumbukirani,kayang’aneni mu Baibulo. Inu mukawona, iyo ndi miyezi isanundi iwiri zitatha zimenezo. Kuwerenga miyezi isanu ndi iwiri:Januwale, Feburuwale, Malichi, Epulo, Meyi, Juni, ndi Julayi—angakhale ali Julayi, miyezi isanu ndi iwiri, imene ikuimiraMibadwo ya Mpingo Isanu ndi iwiri yamphumphu. Mtumikiwina akhoza kuzitola zimenezo, ndiye inu mukhoza kukhalanazo izo, inumukaziwona pamenepo. Chabwino.206 Tsopano, pa izi apa, t—t—tiyeni tingokhala ngati…Inu…Izi ndi zimene ine ndikunena. Ndiroleni ine ndinene izi, siAmbuye, ndiroleni ine ndinene izi. Ngati inu muli wokwatirapa nthawi ino, ndipo inu nonse ndinu opulumutsidwa, ndipondinu odzazidwa nao Mzimu Woyera, ndipo inu mukukondanawina ndi mzake, ndipo inu muli nao ana aang’ono (tsopano,kumbukirani uyu ndi ine, osati Ambuye. Mwaona?), pitiriraninazo kumakakhala limodzi; khalani okondwa; chifukwa inusimunathe kukhala naye mkazi wanu woyamba kapena inusimukanati mukwatire. Ndiye ngati inu muti mumusiye uyundi kubwerera kwa woyamba wanu, inu mukuchita moyipitsakuposa momwe inu munachitira pamalo oyambawo. Mwaona?Kotero inu mukuwona, inu mwangodzisokoneza yense; apopalibe njira yochokera kwa zimenezo. Pangakhale njira imodziyokha moona imene ine ndingainene kuchokera mu Baibulo:nonse inu kukhala mbeta. Mwaona?207 Tsopano, koma…Iyo ndi njira yokha imene ine ndingathekuinena pakali pano, koma pali chinthu china mmenemo,chimene i—ine sindingathe kukuuzani inu tsopano, ndipochifukwa chimene ine ndikuti, “Si ine, koma Ambuye,zipitirirani nazo.” Ngati inu mudzazibweretse izo konse kwa

1054 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

tepi, ndipo tsiku lina, ngati ine ndidzazibweretsa konse izo,inu mudzakumbukire momwe ine ndanenera izo. Ngati inumukanakhala anzeru, inu mukanatha kuzigwira izo apo(mwaona?), pa momwe ine ndinanenera izo pamenepo, ndiyenoinu mukanadziwa.

256. M’bale Branham kodi ife tizipita ku mipingo ina ngakhalepamene iwo akutsutsana nanu?

208 Zedi, inde! Yesu ankatero pamene iwo ankatsutsana nayeIye. Pitirirani kutero. Ife tikuzindikira apa, akuti, “Kodi ifetizipita ku mpingo wina umene amatsutsana ndi inu?” Zedi,ine sindikuti…Ine sindine nsangalabwi yokha pa doko, inumukudziwa. P—pali amuna ena aumulungu kulikonse; inendikuyembekeza ndine mmodzi wa iwo. Mwaona? Koma musatikonse muzifika kumusi kuno…209 Ine ndinaitanidwira mu chinachake chonga ichi tsiku lina.G—gulumuArizona linaitanira tcheru changa kwa izo.Mwaona?Gulu la atumiki linati, “Chinthu chokha chimene ife tiri nachomotsutsana ndi inu, M’bale Branham, ndi (chimodzi cha zinthu)anthu amene amabwera kuno ndi inu, ife timalephera kutitiwapangitse iwo kuti azipita ku tchalitchi kulikonse.” Anati,“Iwo ali ndi ana ndi chirichonse; iwo samapita ku tchalitchi.”Ndipo anati, “Chabwino, ife tinawauza iwo kuti iwo analiolandiridwa kuti azibwera—azibwera ku tchalitchi chathu.”210 Tsopano, ine ndikudziwa iwo amaika kupanikiza pa inundipo amafuna kuti inu muwajowine, koma inu simukusowakuti muwajowine; koma ayikeni ana amenewo mu Sandesukulu kwinakwake! Ndipo inu muzipita ku tchalitchi; musatimuzikhala kunyumba, kumapita kokawedza, ndi kukasaka, ndizinthu monga zimenezo Lamlungu.

Inumukuti, “Chabwino, ine sindinewamwamalamulo.”

Chabwino, inu kulibwino mukhale mu chikhalidwechimenecho kwa kanthawi, kusalemekeza chiukitsiro chaKhristu. Inumuzipita ku tchalitchi kwinakwake!211 Ngati i—ngati ine ndikanapita…Ngati ine sindikanathakupeza…Ngati ine ndikanapita ku mpingo winawakeumene ine ndikudziwa kuti pali chinthu chimodzi chokhachimene anthu amenewo anayamba anenapo chimene inendikuchikhulupirira—iwo atati iwo amakhulupirira Yesu ndiMwana wa Mulungu. Iwo atanena zimenezo (ine ndikukaikiraizo), koma ine ndingamapite kumeneko kumakawamvera iwoakunena zimenezo. Mwinamwake inu mukuti…Umenewondi mpingo uwu, mwinamwake mpingo winawo ungakhalechinachake monga wa Baptisti. Iwo amati, “Eya, inendikukhulupirira kuti iwe uyenera kukhala ndi chokuchitikira.”Ine ndinga—ine ndingamapite nawo iwo pa izo. Ndiye inendikukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu;

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1055

ine ndikukhulupirira kuti iwe umayenera kukhala ndichokuchitikira. Chabwino.212 Ndiye mwinamwake pali a Assemblies of God. Tsopano, iwoamakhulupirira…Mwaona, ine—tsopano ine ndikhoza kudyamwina pafupi zidutswa zitatu kapena zinai za mkate ndi iwo(mwaona?), chifukwa iwo akukhoza kukhulupirira…213 Monga tsiku lina, munthu uyu yemwe anaimba ndipoamafuna kuti adziwe za zimenezo, ndipo anati, “Inu munati…”(Mtumiki uyu kunja uko, munthu uyu kumusi uko ameneankafuna kuti tikambirane zimenezo. M’bale wosauka, iyeali mu chisokeletso chotero.) Iye anati, “Chabwino, M’baleBranham,” mukuona, iye anati, “iye akutsutsana ndi inu kuAssemblies of God.” Ndipo ngati mtumiki wa Assembly apezekaatatenga tepi iyi, ine ndikufuna kuti inu mundiuze ine ndiliti pamene ine ndinayamba ndatsutsanapo ndi munthu waAssembly of God kapena munthu wina aliyense! Nchifukwachiani kuti, pamene malikulu anu omwe akuvomereza kutiine ndakutumizirani inu firii kotala ya milioni ya ana angaamene ine ndawabalira kwa Khristu? Ine ndikutsutsananawo chotani a Assemblies of God? Chifukwa chiani inendikutsutsana nawo aumodzi? Ine sindikutsutsana nawoaumodzi, Assemblies of God, Mpingo wa Mulungu, kapenamunthu aliyense! Ine ndikutsutsana ndi kachitidwe kalikonsekamene kamawalekanitsa anthu.214 Penyani, ine ndawatumizira aAssemblies, mwa kuwerengerakwawo komwe, firi kotala ya milioni ya ana anga omwe. Ngatiiwo ali oyipa chomwecho, bwanji ine ndinachita zimenezo?Bwanji? Ine ndikuganiza kuti ndi opambana omwe alipomu dziko kuti ndiwatumizeko iwo—kaya aumodzi kapena—ena a chikhulupiriro cha Chipentekoste, chifukwa iwoamakhulupirira mu machiritso Auzimu; iwo amakhulupirira muzauzimu; iwo amakhulupirira mu ubatizo wa Mzimu Woyera.Ndizo zopambana…I—ine sindingathe kuwabweretsa iwoonse komwe kuno; iwo ali konsekonse mdzikomu. Ine ndirinawo abwenzi konse konse mdziko, ana amene ndawabalirakwa Khristu. Ine ndimawatumiza iwo kwa opambana…Kodiinu munayamba mwandimvapo ine pamene ine ndikupangakuitanira ku guwa? Ine ndimati…Pamene ine ndimawatengeraiwo pamwamba apo ndi kuwafikitsa iwo populumutsidwa,ine ndimati, “Tsopano, inu muzipita ku mpingo winawabwino wa Uthenga Wamphumphu ndipo inu mukazipezerempingo wa kwanu.” Ndi angati anayamba andimvapo inendikunena zimenezo? Zedi, zedi. Chabwino, nchifukwa chianindiye chomwe ine ndimawatumiza iwo kumeneko? Kodi inendikanakhala wachinyengo kuti ndiziwatumiza ana anga omweku imfa? Izo zikhale kutali kwa ine. Ayi, bwana!215 Ngati inu simungathe kupita…Ngati inu simungathekumabwera kuno ku kachisi, kapezeni mpingo wina

1056 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kwinakwake; zipitani kwa iwo. Inu simukusowa kuti mukachitekutengera zonse zimene iwo amachita. Gawo la mkate limeneiwo akugawa, inu muzigawa mkatewo. Pamene iwo ali ndigaliki, potero, inu mungozisiya izo zokha. Mukuona? Ndikokulondola. Ine sindingathe kuwapangitsa iwo kuti azikachitazimenezo, koma ndizo ndendende…Zedi, inu muzipita kumpingo. Kulikonse kumene chitseko cha mpingo chatsegulidwa,inu muzinyamuka nkupita mwamphamvu momwe inumungapitire. Ngati iwo samakhulupirira, chabwino…Tsopano,inu simukusowa kuti muzikachita nawo. Musati mukawajowineiwo, musati mukajowine uliwonse wa mipingo imeneyo; komazipitani kwa iyo; zikayanjanani ndi iwo. Kodi inu mukudziwabwanji kuti si Ambuye? Iye anati Iye azipangitsa chirichonsekumagwira ntchito palimodzi kwa ubwino!Ndipomwinamwakekuli moyo kumeneko umene ukuyenera kuti upulumutsidwe,ndipo inu mungati mukaunikire Kuwala kwa iwo. Mukuona?Zipitanibe kumeneko. Musati muzipita mwamwano, zipitanimokoma; ndipo anthu akayamba kumati, “Ameneyo ndi mkaziwa Chikhristu chotero, ndi banja la Chikhristu; uyo ndimnyamata kapena msungwana wa Chikhristu chotero. Mai,ine ndimakonda izo…Mnyamata, iwo akuchitadi ngati iwo alindi chinachake.”Mukuona? Ndi kuti, “Ndi chiani icho?”

“Ndi izi apa.” Ndiye awuze iwo. Koma kangokhalaniamchere, ndipo iwowo azikakhala aludzu.

257. Wokondedwa M’bale Branham: Kodi inu mukukhulupirirakuti zizindikiro ziziwatsatira onse amene ali nao MzimuWoyera?

Yesu ananena choncho, Marko 16.

Ngati ziri choncho, nanga bwanji anthu ameneamakhulupirira Uthenga ndi zonse zimene ziri mkati mwawo,komabe iwo alibe zizindikiro izi? Kodi iwo ndi osakhulupirirakapena kodi iwo akusowa Mzimu Woyera? Ngati ziri choncho,chonde tilangizeni ife lero, momwe tingalandirire MzimuWoyera. Ife tikukhulupirira inu ndinu kamwa ya Mulungu yatsiku lathu. M’bale wanu.

216 Zikomo inu, m’bale wanga, chifukwa chonditenga ine ngatiwanu—m’bale wanu, ndipo ine ndikuganiza limenelo ndi funsolabwino kwambiri. Abwenzi, inde, ilo ndi lochedwa pang’ono.Ine ndikanafuna kuti ndichite motalika pang’ono pa ilo ngatiine ndikanatha. Mukuona? Ilo lachedwa. Penyani! Ena ainu…Mukuona? Pamene—inu simungathe kulandira ubatizowa Mzimu Woyera popanda kukhala ndi chokuchitikiranipamene izo zikuchitika…Tsopano, ngati inu mukukhulupirira“chidutswa chirichonse cha Mawu,” inu mukuti…Inu mukutimumakhulupirira chidutswa chirichonse cha Iwo, ndiye Mawuali chikhalireni pamenepo kuyembekezera Mzimu Woyera kuti

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1057

uwayike Iwo pogwira ntchito; koma izo zimatengera kuyatsakwa kandulo.217 Apa pali kandulo ndi chingwe mwa iyo, ndipo ndizonse—mafuta, ndi chirichonse chimene iyo ili nacho chotichikhale mu kandulo iyo; koma mpaka moto ubwere pa iyo,iyo siingawalitse kuwala kulikonse. Ziribe kanthu momwekanduloyo iliri yangwiro, ndi momwe iyo ingayakiremwangwirondi chirichonse, iyo iyenera kuti iyatsidwe, ndiyeno iyo imayaka.Ndipo pamene inu mukhulupirira ndipo mwapangidwa ndimalangizo a chimene Mzimu Woyera uli, chikondi, chimwemwe,mtendere, kupirira motalika, ubwino—zipatso zimene Iwoumabalapo, mpakaMzimuWoyera ndi chokuchitikirani choyakatsikani ndi kudzayatsa kandulo imeneyo, ndiye inu—inu—inusimunawulandire Mzimu Woyera. Mukuona? Inu mukuyenerakukhala ndi chokuchitikirani kutimukhale naoMzimuWoyera.

258. Ndine wa mgwirizano wa apa ntchito. Kodiizi ndi zolakwika kwa Mkhristu? Mawu amati,“Musamalumbire—musamalumbire.” Ife timayenerakulumbira kuti tizisamalira chikhazikitso cha apa ntchito.Ine sindinatenge gawo lolimbikira kuyambira pamenendinakhala Mkhristu, koma ine ndimalipira panobezopereka zanga.

259. Kodi dzina la Yudasi Iskarioti linafufutidwa pa Bukhu laMoyowaMwanawankhosa, kapena kodi ilo linali pa Bukhula Moyo wa Mwanawankhosa?

218 Chabwino. Zokhudza mgwirizano wa apa ntchito, inendikudziwa kuti inu ogwira ntchito…Anthu inu mulindi migwirizano ya apa ntchito ndi zinthu zimene inu…Ngati iwe ukufuna kuti uzigwira ntchito, iwe umayenerakuti ukhale wa mu zimenezo. Ndiko kulondola ndendende.Iwe umayenera kuti uchite zimenezo. Koma samalani izo(mwaona?), chifukwa izo zidzachokera ku ntchitozo kufikaku chipembedzo limodzi la masiku amenewa. Mukuona?Tsopano, inu muzingomakumbukira, izo ndi zotsogolera kudzakwa chirichonse chodzakhala mwamgwirizano. Iwe sungathekugwira ntchito; iwo sangakulole iwe kuti ukhale pa ntchito;iwe—ndiwe “wachabe,” kupatula iwe—kupatula iwe ukhale wamu mgwirizano uwu.219 Tsopano kumbukirani, inu achinyamata, mudzakumbukirezimene M’bale Branham akunena. Ndipo mulole mawu angaazokotedwe ndi cholembera cha chitsulo p—p—pa phiri lachitsulo! PAKUTI ATERO AMBUYE, chinthu chomwechochidzachitika mu chipembedzo. Inu mudzakhala a chipembedzocha mtundu wina, kapena inu simungathe kugula kapenakugulitsa. Kotero khalani osamalitsa kwenikweni, M’bale.Siyani izo zizingothera pa za ntchito zokha. Samalirani izo; ilondi chenjezo!

1058 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

220 “Kodi dzina la Yudasi Iskarioti linafufutidwa kuchokera muBukhu la Moyo waMwanawankhosa, kapena kodi ilo linayambalakhalapo pa Ilo?” Inde, ilo linali pa Ilo ndipo ilo linafutidwapo.Mukuona? Chifukwa mu Mateyu mutu wa 10, Yesu anamuitanaYudasi ndi onse a iwo, ndipo anawapatsa iwo mphamvumotsutsana ndi mizimu yosayera. Iwo anapita namakatulutsaziwanda, ndipo Yesu anati, “Ine ndinamuwona ngakhale Satanaakugwa kuchokera Kumwamba.” Uko ndi kulondola? Ndipo iwoanabwererako, ophunzira onsewo palimodzi, ndipo iwo analiakusangalala; ndipo Iye anati, “Musati muzisangalala k—kutiziwanda zimakumverani inu, koma zisangalalani kuti dzina lanulinalembedwa pa Bukhu la Moyo.” Mukuona? Ndiko kulondola.Ndipo Yudasi anali kumene ndi iwo!Mukuona?221 Kotero kumbukirani, pa chiweruzo, penyani, pa mpandowa chiweruzo, “Chiweruzo chinakhazikitsidwa; mabukuanatsegulidwa; ndipo Bukhu lina linatsegulidwa, limenelinali Bukhu la Moyo, ndipo munthu aliyense anaweruzidwachomwecho.”222 Tsopano, ndi inu apo, kwa funso la kanthawi kapitako.Mukuona? Pa mpando wa chiweruzo. Yesu, Mpingo, Mkwatibwi,anakwatulidwa, anapita mmwamba ku Ulemerero, ndipo analikumwamba uko ndipo anakwatiwa, anadzabwereranso padziko lapansi, ndipo anadzakhala zaka chikwi. Pa kutha kwazaka chikwi Satana anamasulidwa ku ndende yake, kumeneanamangidwa ndi Mngelo ndi unyolo, osati unyolo wachipika,koma unyolo wa zochitika; omumvera ake onse anali mu hade.Onse amene anaukitsidwa pa dziko lapansi anawomboledwandi Yesu limodzi nawo. Iye sakanatha kugwira ntchito pachirichonse; koma pa mapeto a zaka chikwi, chiukitsirochachiwiri… “Wodala ndi woyera ali iye amene ali nalogawo mu chiukitsiro choyamba pa omwe imfa yachiwiri ilibemphamvu.”223 Tsopano zindikirani, mu chiukitsiro chachiwiri ichi, pameneiwo akubwera apo, ndiye Satana akumasulidwa kuchokeramu ndende yake kwa kanyengo kakang’ono; ndiye chiweruzochikuyambika. Tsopano penyani, Yesu ndi Mkwatibwi, mongaMfumu ndi Mfumukazi, atakhala pa mpando wachifumu,Mpandowachifumu Woyera wa chiweruzo; ndipo mabukuanatsegulidwa, mabuku a ochimwa. Ndipo Bukhu linalinatsegulidwa, limene linali Bukhu la Moyo; ndipo munthualiyense anaweruzidwa chomwecho ndi Mkwatibwi. “Kodi inusimukudziwa (pakutengera nkhani zazing’ono izi pamaso paalamulo)—kodi inu simukudziwa kuti oyera adzaweruza dzikolapansi?” Mwaona, mwaona? Chabwino.

260. Kodi chonde inu mungafotokoze omwe gulu laChivumbulutso 20:4 ali? Kodi iwo ali gawo la Mkwatibwiwakale kapena mtsogolo?

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1059

224 Iwo ndiwo Mkwatibwi kwathunthu, onse wakale ndiatsopano. Iwo ndiwo Mkwatibwi kwathunthu, chifukwa iwoakukhala mu Zakachikwi. Chabwino.261. Kodi chonde inu mungafotokoze (Chabwino, ndi

ndendende funso lomwelo.)…Chivumbulutso 20:4, kodiiwo ali miyoyo ya odulidwa mitu chifukwa cha umboniwa Khristu amene sanalambire chirombo ngakhalekulandira chilemba chake mu (O, ine ndikuwona kumeneiwo akupita tsopano. Ili langopatsidwa kumene kwaine, langoperekedwa kumene kwa ine.)…pakuti akutianakhala moyo ndipo ankalamulira limodzi ndi Khristukwa zaka chikwi? Kotero izo ndi zododometsa, chifukwacha kuzunzidwa kwa Mkwatibwi, koma kodi iwoangakhalenso ndani ndi kumalamulira ndi Khristu zakachikwi? Kodi i—i—kodi iwo angakhale 144,000?Ayi, ayi! Iwo ndiwo Mkwatibwi. Tsopano, kumbukirani,

kumbukiranai, iwo…225 Inu munati, “Pamene iwo akudulidwa mitu chifukwa chaumboni…” Tsopano, inu mukuti, “Pakuti—sali kulambirachirombo…” Zedi! Inu mukuti, “Chirombo ndi chotichidzabwerabe.”226 Chirombo chakhala chiripo nthawi yonseyi; chirombochinali chimene chinkawadyetsa iwo ku makola a mikangoaja, chikawadyetsanso iwo mmbuyo umo mu mabwalo uko muRoma. Ameneyo anali wotsutsakhristu; icho chinali chirombouko komwe, anayambitsa mawonekedwe a chipembedzo.Ndendende basi monga—pafupifupi ndondomekoyo. Mpingowa Roma unatengedwa kuchokera mu Baibulo, ndiyeno…Chimene iwo anachita pa izo, iwo anapanga bungwe chinthuchondipo anapanga chikhazikitso ndipo anapanga—mpingo wakonsekonse kuchokera mu zimenezo, ndipo onse amenesamagwadira kwa izo ankayenera kuti aziwonongedwa.Mukuona? Izo zinali.227 Ndipo iwo a mu gawo la Thupi amene linali apo…Tsopano, Thupi lakula chimodzimodzi monga mtengo mpakaIzo zikubwera ku Mutu. Mukuona? Ndipo onse, onse ofera, ndiozunzidwa, ndi ena otero…228 Koma Yesu watipatsa ife mtendere mbali ino ya mtsinje,monga momwe Iye anachitira kwa mafuko amene…uko(mukuona?) sanawolokere kwinako. Tsopano.262. Kodi ine ndiwachitire chiani iwo? Kodi ine ndipitirize

(O!) kuwasamalira Adadi ku munda? Kodi ine ndichitechiani…kuti akhale—nazo moyo…? Ndipo walembapodzina lake.Inde, m’bale wanga…Izo—walemba apa. Ine sindikudziwa

kuti ndi ndani…Ilo likuti, “M’bale Branham…” Ilolikungoyamba ndi, “Kodi ine ndiwachitire chiani iwo?”

1060 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

229 Tsopano, mwinamwake mnyamata wina kwa abambo ake.Penya, M’bale wanga wokondedwa, wodala uli iwe pameneiwe ukuwasamalira abambo ako, chifukwa abambo akoanakusamalira iwe pamene iwe sunkatha kudzisamalira wekha.Ndipo lamulo loyamba lokhala ndi lonjezo, lamulo loyambalokhala ndi lonjezo: “Lemekezeza abambo ako ndi amai akochimene chingatalikitse masiku pa dziko lapansi amene AmbuyeMulungu wako anakupatsa iwe.” Mukuona? Eya, ziwasamaliraabambo ako mwanjira iliyonse yomwe iwe ungathere. Uziwonakuti iwo akulandira zopambana kwambiri.

263. Inu munanena kuti Kaini anali wa mbewu ya serpenti.Nchifukwa chiani Eva anati, “Ine ndalandira munthukuchokera kwa Ambuye”?Tiyeni nazoni. Ine kulibwino ndidikire mpaka chakudya

pa ili. Eya, ine ndiyembekezera mpaka chakudya pa ilo. O,izo zingatenge pafupi kanthawi pang’ono kuti ndifotokozezimenezo. Chabwino.

264. Wokondedwa M’bale Branham: Kodi inu mungafotokozendime iyi kwa ine, Yesaya 2:2: “Ndipo kudzachitika kutimumasiku otsiriza, kuti phiri la Ambuye—pa phiri la Ambuyenyumba idzakhazikitsidwa pamwamba pa mapiri, ndipoidzakwezedwa pamwamba pa mapiri; ndipo mafuko onseadzakhamukira ku iyo.”

230 Inde, ine ndinatero, Lamlungu lisanafike lathali. Mukuona?N—nyumba ya Ambuye idzakhazikitsidwa pamwamba pamapiri, ndipo mafuko onse azidzakhamukira kwa iyo.Lalikulu…Ngati inu mulibe…Ngati inu muli nayo tepiya Kwawo Kwa Mtsogolo Kwa Mkwatibwi ndi Mkwati, iyoikufotokoza izo ndendende basi mwanjira imeneyo.

O, mai! Ine mwina ndibwino ndingolekeza pakali pano,chifukwa mai, o, mai, m’bale, ife sitingate kutsiriza zonse iziapa. Fyuu!

265. M’bale Branham, ndi…(Tiyeni tiwone chomwe ili liri.)M’bale Branham, zikukhulupiriridwa mwawamba ndiambiri amene akutsatira Uthenga wanu kuti inu ndinuMesiya wa tsiku lino. Kodi izo ziri choncho?

231 Ayi, bwana!

Mwapoyera tatiuzani ife, M’bale Branham. Inumukuwonekangatimukudodomapozidziwitsa nokha, ndipo ife tikudziwa kutindi utumiki woterewu wonga womwe Mulungu wakupatsaniinu, inumukuyenera kuzindikiritsidwamuMalemba penapake.

266. Lachiwiri: Inu munatiuza ife cholinga chanu chopitiraku Arizona nthawi yoyamba. Inu munatiuza ife chifukwachake, ndipo izo zinafika pochitika, koma inu simunatiuzeife chifukwa chimene inu munabwererakonso kachiwiri.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1061

232 Malo oyamba, ine sindine Mesiya! Mukuona? Mesiya ndiYesu Khristu, koma ife ndi “Tiamesiya,” mmodzi aliyense waife.Mesiya,Mesiya amatanthauza “Wodzozedwayo.” NdipomwaIye munkakhala chidzalo cha Umulungu mwathupi; mwa inemukukhala gawo la Mzimu Wake, womwewo umene umakhalamwa inu. Ine ndinapatsidwa mphatso k—kuti—ndizidziwazinthu zazing’ono ndi kuwoneratu zinthu. Izo zikundipangaine kukhalabe m’bale wanu. Mukuona? Ine sindiri—Mesiya ayi;ine ndine m’bale wanu (mukuona?), m’busa basi kwa gulu.Ndipo ngati ine ndikanakuuzani inu kuti ine ndinali Mesiya, inendikanakhala wabodza. Mukuona? Ndipo ine sindikufuna kutindikhale wabodza.233 “Tsopano, nchifukwa chiani ine ndinapita ku Arizonanthawi yoyamba?” Inu munamvetsa zimenezo. Ine ndinapitamu Dzina la Ambuye, chifukwa ine ndinatumidwa kumenekomwa masomphenya. Ine ndinabwereranso nthawi yachiwiripa cholinga. Ingozisiyani izo zokha. Ine ndikudziwa chimeneine ndinapitira uko; ine sindingathe kumakuuzani chirichonse.Pamene iwe—mdierekezi sakudziwa—sangathe kuzitenga izokuchokera mu mtima wanga. Ngati ine ndiziyankhula izonkuzitulutsa, ndiye iye akhoza kuzitenga izo, koma iye sa—iyesangathe kuzitenga izo pamene izo ziri mu mtima wanga. Ngatiine ndinganene, “Dikirani mpaka izo zifike pochitika!”…Ingokumbukirani, gwirani tepi iyi; ine ndinapita ku Arizonapa cholinga. Chonde pirirani nane. Mukuona? Inu muzingochitazimene ine ndikukuuzani inu kuti muzichita (mukuona?); basi—kuchitamomwe ine ndikunenera kutimuzichita.Mukuona?

267. M’bale Branham, ine ndiri ndi mafunso ena ameneine ndikukhumba kuti ndifunse—ndikufunseni inu. Inendawamva anthu akunena kuti inu mwawalangiza anthukuti agulitse zawo zonse…(Mwinamwake ine ndilisiye ilolokha nalonso. Tiyeni tiwone. Chabwino, ndi nthawi kaleyoti tizipita. Ife mwinamwake tidzalitenga ili pambuyopa chakudya, koma i—ine ndidzaliyankha ili kapenandidzayesera mwakukhoza kwanga. Ine sindikudziwa;ilo langoperekedwa kumene kwa ine. Mukuona? Billyanandibweretsera ine odzaza mdzanja apo pomwe—apopa khomo. Mukuona?) Ine ndawamva anthu akunenakuti inu mwawalangiza anthu kuti agulitse nyumba zawozonse ndi kuti akutsatireni inu ku Arizona k—kapena iwosadzakhala ali mu mkwatulo. Kodi izo ndi zoona?

234 Limenelo ndi bodza. Mukuona? U-nhu!

…kapena kodi ife tigulitse manyumba athu, kapena kodiinu munazinena konse izi?235 Ayi, bwana! Ine sindinazinene zimenezo! Ngati chirichonse,ine ndawalangiza anthu kuti asachite zimenezo. U-nhu!Kukumbukira, mukukumbukira loto la “Junie” Jackson nthawi

1062 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ija pamene ine ndinapita kumeneko? “Junie” analota kutiiye anaziwona izi…Ndi angati akukumbukira lotolo, ndimomwe Ambuye anaperekera kutanthauzira. Phiri lalikululija, ife tinali titaima pa ilo, ndi zilembo zakale zofufutikapamenepo; ndipo ine ndinali kuyesera kuti ndizitanthauzireizo, ndipo ine sindinali kutha kuchita izo. Ndipo i—ine ndinalikuzitanthauzira izo kwa iwo. Nditatha kutanthauzira zonsezo,zonsezo zitatanthauziridwa, ndiye ine ndinafikira pamwambandipo ndinatenga (mu loto lake tsopano) mtundu wina wa—chokhala ngati chitsulo ndipo ndinangodula pamwamba paphirilo ndipo ndinayang’ana mkati umo, ndipo umo monsemunali moyera-mwachipale, monga nsangalabwi. Koma umomunali mosalembedwa, ndipo ine ndinati, “Inu nonse mukhalekuno ndi kumayang’ana umu pa izi tsopano, pamene inendikupita kutali.”236 Ndipo “Junie”…Onse awo anapita pamwambapo ndipoabale onse ndi onse akuyang’ana pa iwo, wina…Iwo sankathakuzimvetsa; anati, “Chabwino, kodi inu mukudziwa chiani? Izosizinalembedwe nkomwe apa,” komabe iye anali akuwerengakunja kwake kwa izo. “Chifukwa chiani izo sizinalembedwemkati umu? Ife sitikutha kuzimvetsa.”237 Ndipo Junior anapotoloka pamenepo ndipo anayang’ana,ndipo iye anandiwona ine ndikupita cha kumadzulo, ndi kupitacha kolowera dzuwa, kupita pamwamba pa phiri limodzi, phirilina, mofulumira kwenikweni, kumangopita…Ndiyeno iwoanapotoloka nayang’ana ndipo anandiwona ine nditapita; gululalikulu lonse la iwo linachoka napita chaku njira imeneyo,ndipo iwo ankafuna kupita uku ndi kukachita izo, nditawauzaine kale kuti akhale pamenepo. Akhale pamenepo, akhalepomwe pano; malo ake ndi anowa.238 Ndiyeno, pamene ine ndinachita izo, ndiye—ndipo inendinapita ndendende basi; ndipo pang’ono pokha zitachitika izo,Mngelo wa Ambuye anawonekera kwa ine, nkuti, “Pita uko kuArizona kutaliko.” Ine ndinamva kuphulika kuja kukuchitikandipo ndinapita kumeneko, ndipo kodi chinali chiani icho?Mnyamata uyo analota loto limenelo molondola ndendende basi,ndipo Ambuye anapereka ufulu…Kumbukirani, ine ndinati,“Pali chinachake chimene ine ndikupitira kumeneko.” Ndipopamene ine ndinapita uko, icho chinali chinsinsi cha ZisindikizoZisanu ndi ziwiri, zimene zinasindikizidwa umo mkati mwaphiri lija la Ambuye. Ndinabwerera kuno komwe ndi kutsegulakwa Zisindikizo Zisanu ndi ziwiri. Mukuona?239 Ayi, inu musati muzichita zimenezo. Ngati inu mukufunakuti mupiteko, zimenezo ziri kwa inu. Chifukwa, ine sindiri…Mai, ine sindikusamala komwe inu mupita, koma kutimungochita zimenezo, mukuganiza kuti Mkwatibwi adzapitakuchokera kumeneko, inu mukulakwitsa.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1063

240 “Komanso ine ndamva izi…Ine ndiri (Ndirole i…Inendazitenga izo molakwika penapake apa. Tiyeni tiwone.)…mkwatulo. Kodi izi ndi zoona kapena kodi ife tigulitsemanyumba athu, kapena kodi inu munayamba mwanenapoizi?” Ayi, ine sindinanene konse zimenezo. Ine sindina…Inenthawizonse ndawalangiza anthu kuti muzikhala kumeneinu muli ndi kumapitiriza pitirizabe mpaka Yesu abwere.Ngati ine ndakuuzani inu nthawi zambiri, mulole tepi iyiikhale chikumbutso; mulole tsiku lino likhale chikumbutso;mulole mawu anga akhale chikumbutso; ine sindinayambe,pa nthawi imodzi, kumuuzapo konse aliyense, kubapo konseanthu, kuyesera konse kuti ndimutenge winawake kutiazibwera ku mpingo uno! Ine sindinachitepo…Kufika pakuwauza iwo kuti asiye mipingo yawo yomwe ndi kugulitsakatundu wawo ndi zinthu, Mulungu akudziwa kuti inenthawizonse ndimawalangiza anthu kuti akhalebe ali Akhristundi kumakhala kumene inumuli mpakaMulungu adzakuitaneniinu. Aliyense akudziwa zimenezo. Khalani uko komwe! Komatsopano, kuti ndiwauze anthu…Winawake akati, “Chabwino,ine ndikufuna kuti ndipite cha uku. Ine ndikufuna kutindizikakhala…” Inu pitani kulikonse kumene inu mukufunakuti mupiteko; izo zonse ziri bwino. Ine sindikusamala kumeneinumuti mupite; imeneyo si ntchito yanga pa izo.241 Koma tsopano, kuti muziganiza kuti…Onani, kodi ichochimachita chiani? Izo zimayambitsa kachiphunzitso kotsatiramunthu (mukuona?), ndiyeno ine ndilowa mu vuto. Iwo ali ndigulu kunja uko pakali pano limene liti likhale pa chithandizoposakhalitsapa.Ndiyeno kodi izo zidzakhala chiani? “Ife tadzerakuno pofuna mkwatulo wa Mkwatibwi.” Izo ndi basi zimenemanyuzipepala akuziyembekezera! Iwo akuyembekezera kutiatenge zimenezo pamene iwo ati agwere poti azithandizidwandipo sangathe kubwerera ku makwawo. Ndiye kodi iwoadzachita chiani?242 “Chabwino, ife tamutsatira M’bale Branham kuno.Amayenera kuti akhale…” Ndipo ine ndiri wosalakwabasi pa izo momwe ine ndingathe kukhalira ndiri. Anthuokondeka, okoma, i—iwo akudziwa kuti ine ndimawakonda iwo,ndipo ngakhale mu kulakwitsa kwawo. Ndipo iwo…Bwanji,a…Iwo…ine ndikuwakonda iwo mulimonsebe. Mukuona?Ine ndikuwakonda iwo; iwo ndi ana anga; koma basi iwosakundimvera ine, chimene ine ndikuyesera kuti ndiwauzeiwo. Ine ndikuyesera kuti ndichititse chinachake mu Dzinala Ambuye, ndipo iwo sakundilola ine kuti ndichichite icho.Mwaona? Iwo mwakuchita akupita motsutsana ndi ine mmalomokhala ndi ine. Iwo akuchita…243 Kodi ine sindinakuuzeni inu kuti ngati konse uthengaungati ulalikidwe, kwa kudzakhala kuli komwe kuno pakachisi uyu; chirichonse chimene ine ndikanati ndichichite,

1064 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ine ndikanamabwera kuno ndi kudzakuuzani inu poyamba,molunjika kumene kuchokera pa kachisi uno? Ilo ndi lonjezolanga!268. Ndiponso, ine ndamva kuti pali chiphunzitso chatuluka,

kuti bukhu limene inu munalilemba zaka zingapo zapitazolokamba za mkate wamoyo…Iwo akutanthauzira izo kutiife tonse tizikhala ndi inu kapena tiuphonya mkwatulo.

244 Chabwino, bukhulo liri kulakwa. Bukhu laMkate wa Moyo,ine ndikulikumbukira ilo tsopano. Uko kunali kudyetsa mpingokonsekonse, kulikonse. Mwaona, vuto lake liri…Tsopano,tsopano, anthu inu, inu ndi olimba inueni, koma iwe umayenerakukhala nazo izo. Izo zimatsatiramsonkhano uliwonse. A—a…

Ine ndinali kuwerenga za Marteni Lutera kuno osati kalelitali, si kudzifanizitsa tokha ndi izo; koma uku ndi kukonzansochimodzimodzi monga uko kunali. Ndipo—funso linali…A—azambiriyakale, iwo anati, “Ndi chinthu chopambana kuganizakuti Marteni Lutera akanatha kuwutsutsa mpingo wa Katolikandi kudutsa nazo izo. Icho chinali chinthu chodabwitsa, koma,”anati, “chinthu chodabwitsa kwambiri cha Marteni Luterasichinali chimenecho. Momwe iye akanathera kuugwira mutuwake pamwamba pa kutengeka konse kumene kunkatsatiramsonkhano wake ndi kukhalabe woona kwa Mawu, kuitanidwakwake…”Mukuona?245 Ayi, bwana! Musati muziika zanuzanu…Mwamunaaliyense kapena mkazi amene angaike chirichonse ku chimeneine ndikunena, Sali kukhulupirira zimene ine ndikunena. Iwosali…Iwo akuti…Iwo…269. Ndiponso za mabanja awa amene agulitsa zonse ndipo

asamukira ku Sierra Vista, Arizona, kumene iwoatanthauzira kuchokera mu imodzi ya matepi anuyotchedwa (miniti chabe) “Betelehemu Wamng’ono”—“Betelehemu Wamng’ono,” mkwatulo udzakachitikiramu Arizona. Kodi inu munawalangiza iwo kuti apitekumeneko?

246 Ine ndithudi sindinatero. Pamene iwo analemba kalata yazimenezo, winawake kuno mu Connecticut kapena chinachake,ine ndinayankha kalatayo mobwezera ndipo ndinati, “Inumukupanga kusuntha koipa kumene inu munayambamwakupangapo mu moyo wanu. Musati muzichita zinthumonga zimenezo.” Mwaona, inu simungathe…Chabwino,inu muzingokumbukira, anthu inu…Tsopano, inu nonsemukudziwa kuti ine sindikuwauza anthu amenewo kuti azichitazimenezo; ine ndikuwauza iwo kuti asachite zimenezo. Komainu mukuona, izo zikuyenera kutsatira msonkhano. Nchifukwachiani anthu amanditcha ine Mesiya? Nchifukwa chianianthu…? Iwo ali ndi kutenga…Chabwino, munthu winakunja uko anandiwonetsa ine tsiku lina, iye anali ndi kanthu

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1065

kakang’ono ndipo iye anali kupita—amapitiriza, ankafuna kutianthu onse azibatizidwa mu dzina langa. Izo zingandipangeine kukhala wotsutsakhristu! Koma ine sindine wofuna zinthuzimenezo, ndipo anthu nonse inu mukudziwa zimenezo. Komainu mukuona, izi ziyenera…Izo zikungouzindikiritsa kutiUthengawu ndi woona.247 Kodi iwo sanabwere ndi kudzayesa kumuuza Yohane, a—amene anatsogolera kudza koyamba kwa Khristu, “Kodi inusindinu Mesiya?”

Iye anati, “Ine sindiri! Ine sindine ngakhale woyenerakumasula nsapato Zake. Ine sindiri woyenera ngakhale kutindiyang’ane pa Iye.” Mukuona? Koma iye anati, “Iye ameneakudza pambuyo panga…”270. Tsopano, M’bale Branham, kodi ife tikuphonya pa

chinachake? Anthu awa akudzinenera kuti akukhulupiriramawu aliwonse amene inu mukuwanena kuti ndi owona.(Koma iwo sali! Iwo sali kukhulupirira izo. Zochitazawo zomwe zikutsimikizira kuti iwo sali.) Chondendiroleni ine ndidziwe yankho lanu lolunjika: indekapena ayi (Inu mwalipeza ilo! Chabwino.) za zinthuizi, ndipo ngati izo ziri zoona, ife tikufuna tikonzekerekuti tikalumikizane nawo ena onse a iwo kumeneko—onsea iwo. Ine ndikukuthokozani inu mochuluka kwambirichifukwa cha mayankho anu ku mafunso awa, pamene inendikhala ndikuyembekezera kuti ndiwamve iwo Lamlunguili, ngati Ambuye achedwa.

248 O, mai! Chabwino, M’bale, Mlongo, i—ine ndikuyembekezaizo zamveka (mukuona?) kuti ine sindinatero, sindikutero…Tsopano, ngati anthu…O, zedi, ngati inu mukufuna kutimubwere uko ku Arizona kumadzakhalako…Ndipo tsopano,ine ndidzakhala ndiri uko ku Arizona mwinamwake gawoloyamba ili. Ine ndidzayenera kuti ndidzabwererenso kuno.Ine ndidzayenera…I—ine ndikufuna ndikakhale kumeneko;ana ali athanziko ndi chirichonse. I—ine ndikufuna ndikakhalekumeneko kanthawi pang’ono, ndipo ine ndiri ndi cholinga.Kumbukirani tsopano, pa tepi, PAKUTI ATERO AMBUYE,ine ndiri ndi cholinga pochita zimene ine ndikuchitazi; inumukudziwa ine ndiri nacho; koma ine sindingathe kukuuzani inuzimenezo.249 Nchifukwa chiani ine ndikukuuzani inu kuti musagulitsemanyumba anu? Inu mudzakhala mukusowa, ndipo inumudzakhala muli ku mathero aafupi a chingwe. Musati muchitezimenezo. Ine sindikakhala kuArizona komakanthawi pang’onokokha. Bwanji? Ine sindingathe kuchita izo tsopano.250 Ngati ine ndiwalola anthu amenewo kuti azikakhalakumeneko ndi kumapitirira pa chithandizo, nchiani chitichidzachitike? Ndiye, izo ndizo ndendende basi zomwe

1066 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

zipembedzo ndi onse a iwo akuyembekezera. “Aha, inendinakuuzani inu zomwe zinali kumbuyo kwa iye, sukulu inaya aneneri kapena chinachake!” Mukuona? Ndi zimenezotu,izo ndi basi zimene iwo akuziyembekezera! Pambuyo pazonsezo, anthu amenewo, ine ndiri ndi chowayankhira paiwo; ngakhale iwo sanachite zimene ine ndinawauza iwo kutiachite, ndipo iwo achita ndendende…Inu mukuti, “Asiyeni iwoapite; i—iwo achita zimene inu munawauza iwo kuti asachite!”Zimenezo siziri mu mtima wanga. Ine ndikufunabe kuti ndipitekukawafuna iwo. Iwo ndi ana anga. Ine ndikhoza kudzawapatsaiwo kakhofi pang’ono pamene ine ndidzawabwezeko iwo, komai—koma i—ine ndithudi ndipita mowatsatira iwo. Ndipo kodi inendikachita motani kumeneko?251 Iwo anati, “Ife tabwera kudzatsatira Mawu.” Ine ndiribengakhale mpingo woti ndiziwatumizako iwo kumeneko. Mtunduwa mpingo komwe iwo azikapitako uko ndi mtundu womwewoumene inu mumawusiya ku malo ena, mwinanso moyipirapo.Mukuona? Ndipo iwo samapita ku mpingo mulimonse, ndipo inendiribe mpingo woti ndizikawalalikirako iwo. Ndiye ine ndiriwokakamizidwa mwamakhalidwe kuti ndiwachotseko ana angaku Arizonako, kumene…252 Ine ndikufunseni inu chinachake. Ine ndalalikirapokupitirira mauthenga sate mu mpingo uno chaka chathachi.Ndipo kwa zaka zisanu, nditachoka, kuyambira pamene inendakhala ndiri muArizona, ine ndalalikira ochulukamumpingouno mu chaka chimodzi kuposa momwe ine ndinachitirapo muzaka zisanu nthawi ina iliyonse (ndithudi!), muno mu mpingo.Kuno ndiye ku maziko a kwathu; kuno ndi ku likulu langa;kuno ndi kumene ife takhazikikako. Tsopano, gwirani izo mumalingaliro palibe kanthu chomwe chiti chichitike. Tsopano,ngati inu muli amzeru, inu mugwira chinachake. Ziribe kanthuchomwe chichitike, kuno ndi kulikulu kwathu, kuno komwe!Ndipo sungani zimenezo mu malingaliro ndipo mudzalozeremmbuyo ku tepi iyi tsiku lina, kuti inu munandimva inendikunenera. Chabwino, zikumbukirani zimenezo!253 Ngati inu mukufuna—ngati inu mukuyenera kuchoka ndikumabwera ku mpingo, musati mupite uko kuti mukaupezeiwo, chifukwa ine sindiri ngakhale kumeneko. Ine ndiribe malooti ndizipitako; ine ndiribe malo oti ndizikalalikirako. Iwosangandilole ine kuti ndizikalalikira mu mipingo yawo. Inendiribe ngakhale malo, ndipo ine ndinamulonjeza bamboyopamene ine ndinafika uko…Iwo onse ankachita manthakuti ine ndimabwera kumeneko ndi kudzamanga chinyumbachachikulu—nkuchotsa anthu mu mipingo. Koma chimenechosi cholinga changa cha moyo. Mukuona? I—ine ndimawafikitsaanthu populumutsidwa. Izo ziri kwa iwo. Monga Msamariyaanabwera uko ndipo anamutengera bambo uja ku nyumba yaalendo, ndiye nkuwasiya iwo kuti aziwasamalira iwo kuchokera

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1067

pamenepo mpakana. Ine sindiri kuno kuti ndidzaphwasulemipingo, ine ndiri kuno kuti nditengere otembenuka kwaKhristu! Mukuona? Ndipo izo zimandipangitsa ine kukhalawosamvetsedwa pakati pa anthu (mukuona?) p—pamene iwoakutanthauzira mwanjira yawo yawo ndipo osati—ndi—kunenazimene ine ndiri kunena. Mukuona?254 Kodi inu simukukumbukira masomphenya aja? Ndi angatiakukumbukira loto la Junior Jackson? Ndipo onse a iwoakutsatira izo ndendende basi. Kodi chinali chiani icho? Khalanikuno mpaka ine ndipite kutaliko! Mukuona? Ndi kukatengakutanthauzirako ndi kukabwererako.255 Tsopano, ine ndiri ndi chinachakenso mu mtima wangachimene ine ndachenjezedwa ndi Ambuye kuti ndichichite,kusuntha kwina koti ndikupange kokhudza za kachisi uyu,ndi tchalitchi ichi; kuti ine ndiyenera ndipite uko kapenakwinakwake kwa kanthawi pang’ono. Izo ndi za kwa cholinga,cholinga chachikulu, cholinga chimene inu simukudziwa kanthuka icho. Koma kumbukirani, ine sikuti “ndikungoyenda”mozungulira, chifukwa ine ndikuchita ngati ine ndiridi.Ine ndikugwira ntchito mu chifuniro cha Ambuye, utaliwonsewu momwe ine ndikudziwira kugwira kwake ntchitomu zimenezo. Mukuona? Ndicho chifukwa chake ngati inumukukhulupirira zimene ine ndikunena, ndiye inu zichitanizimene ine ndikunena kuti muzichita (mukuona?), ndiyemvetserani kwa ine ndi kundikhulupirira ine monga m’balewanu. Ngati inu mukundikhulupirira ine kuti ndine mneneri,musati muzitanthauzira molakwikamawu anga!256 Ngati pali chirichonse, kotero ndithandizeni ine, ngatipali chirichonse chimene inu mukuyenera kuti muchidziwechimene Mulungu angandiuze ine, Mulungu akudziwa inendikanati ndikuuzeni inu ndendende basi! Ndipo musatimuziwonjezera kwa izo kapena kuchotsa kwa izo; inumuzingochita izo mwanjira yomwe ine ndikuzinenera izo(mukuona?), chifukwa ine ndikukuuzani inu kuchokera mumtima wanga mwakupambana kumene ine ndikudziwira.Mukuona? Inu muzingokhulupirira zimenezo. Basi—muzitengaba—basi zimene ine ndikunena pa izo, ndi kungozisiya izo kutizipite monga choncho. Chabwino.257 Kotero tsopano, ine ndiyenera ndikawabweretse anaamenewo mobwerera kuno kuti azidzadya chinachake. Iwo aliuko mu chipululu akufa ndi njala.258 Mtumiki anabwera kwa ine tsiku lina, anati, “M’baleBranham, iwo akulowa mu kachiphunzitso kotsatiramunthu koipitsitsa kumusi uko kamene inu munayambamwakawonapo.” Anati, “Aliyense wa iwo, mmawa uliwonse,iwo amatuluka; ndipo iwo amati sapita kukagwira ntchito,tayandikira kwambiri ku mkwatulo.” Iwo sapita kukagwira

1068 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ntchito. Chabwino, izo zikungosonyeza kuti inu simukumvetsankomwe. Mukuona? Kulondola. (Tepi iyi ikupita kumeneko!)Kotero, inde, bwana! Inumuyenera kutenga phunziro kuchokerakwa chiswe, Baibulo limatero, inu mukudziwa. Ngati ichosichingagwire ntchito, icho sichingadye. Kotero izo zirindendende basi zolondola.

P—pano, ndangotola imodzi ya izi.

271. Ziri…(Ine sindikudziwa. Mwaona, izi ndi zina basi—ndizosiyana—ndi kulemba kwa dzanja losiyana ndi zinazi.Basi kuti ndikusonyezeni inu, ine ndikuganiza pali pafupieyiti kapena teni a awa mmenemo. Mukuona?) K—kodimpingo wangwiro kwambiri udzakakhala uli ku Tucson,Arizona? Ine ndikufuna kukhala mu chifuniro changwirocha Mulungu. Kodi ife tisamukire ku Tucson?

259 Si linanso konse—kulemba kwa dzanja lina. Ziri…ine…Kungoyang’ana mozungulira pano; ine ndingakusonyezeni inuangati amene alipo pa funso limodzi limenelo. Ine sindi…I—ine sindikanatha kuwapeza iwo, ine ndikuganiza. P—pano…ine ndiri nawo ena ndawalemba chizindikiro apa, “Inendikudziwitsani inu.”

272. M’bale Branham: Chonde…(Tiyeni tiwone.) Podziwakuti inu ndinu mneneri, ndipo ora limene ife tirikukhalamo, lidza—ndipo mneneri wa ora limene ife tirikukhalamoli (Ndicho chimene izo ziri.), kodi kudzafikanthawi pamene anthu aMulungu adzayenera kuti athawireku Arizona limodzi ndi inu? Ngati ziri choncho, kodi inumudzatidziwitsa ife pamene nthawiyo idzafika?

260 Zedi ndidzatero. Ine ndidzakuuzani inu. Ine ndidzakuuzaniinu. Tsopano onani, pali malembedwe a manja awiri osiyana,anthu awiri osiyana. Mukuona? Apo pali malembedwe a dzanjalimodzi, ndipo apo pali enanso. Mukuona? Izo ndi zimenezikuyenera kukhala, zimene ziri mu malingaliro a mpingo.Mukuona? Chabwino, tiyeni tingozitengera izi pokhazikitsidwa.Tiyeni tiwone ngati ine ndikanatha kupeza…Tiyeni tiwone.

273. M’bale Branham…(Pali limodzi lina, losiyana lonsekwathunthu.) M’bale Branham, ena anakumvetsaniinu kuti mumanena mu uthenga wanu wa “Kwawokwa Mtsogolo kwa Mkwatibwi ndi Mkwati” kunalikoti kudzakhala (Ayi, ili ndi losiyana.)—idzakhalamailosi fifitini handiredi kuchokera pa kachisiyu—mwamphwamphwa—seveni handiredi mbali iliyonse(Mwakuyakhula kwina, kachisi kukhala ali pakatipenipeni nkukhala seveni handiredi mbali iliyonse—zidzakhala mailosi fifitini handiredi.O!)—mbali iliyonse.Kodi izi ndi zoona? Ine ndikukhala kunja kwa dera ili; kodiine ndisamukire mmenemo?

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1069

261 Ayi, Wokondedwa, inu musati muchite zimenezo.Penyani! Tsopano, inu mukuona kuphweka kwake momweziriri kwa anthu? Ndi angati anali kuno pamene inendinkalalikira uthenga umenewo? Ine ndinanena kuti pameneine ndinkayeza Yerusalemu Watsopano, kuti iwo udzakhalauli wamphwamphwa mailosi fifitini handiredi. Ine ndinanenakuti iwo uzidzafikira pafupifupi kuchokera ku Maine mpakaku Florida, ndi mailosi sikisi handiredi kumadzulo kwaMississippi; izo zikanakhala mwamphwamphwa mailosi fifitinihandiredi. Ine ndinati Mzindawo, mwa kulingalira kwanga,udzakhala uli pa malo pomwepo pamene mneneri Abrahamuankawufunafuna Mzinda umenewo, kumene sikudzakhalakulinso nyanja. Baibulo linati sikudzakhala kulinso nyanja,chimene chiri pafupi magawo atatu pa anayi a dziko lapansiliri madzi. Ndipo uko sikudzakhala kulinso nyanja; kotero, iwosungati ukhale uli Mzinda wawukulu kwambiri utakhala mumalo monga amenewo. Ine ndikukhulupirira iwo udzakhalauli pa malo aang’ono amenewo pamene iwo akukangamiramochuluka kwambiri, ndipo Mulungu anabadwira, kumenekomu Betelehemu. Ine ndikukhulupirira uko kudzakhala ukokomwe ku Palestina, kumene iwo uti udzatukuke kuchokera padziko lapansi uko komwe ndi kudzakhala phiri limenelo.262 Koma, mzanga wokondedwa, izo ziribe kanthu kochita ndikachisi uyu. Mukuona? Abrahamu, Isaki, Yakobo, Paulo, oyeraonse, iwo anafa konse konse pa dziko lapansi, anawotchedwa,anamizidwa mmadzi, anadyedwa ndi mikango, ndi chinachirichonse; ndipo iwo adzatulukira kuchokera mu mng’aluuliwonse, mpita, ndi ngodya ya mdziko. Ine ndikuyembekeza inendiri mmenemo. Ine sindikudziwa komwe nditi ndidzakakhalendiri, koma kulikonse kumene kuli, ngati ine ndiri mu gululimenelo, palibe kanthu kangathe kundiletsa ine kukakhalandiri kumeneko! Mukuona? Ndipo ine sindikusowa kudzakhalandiri pa malo ena ake aliwonse. Malo okha amene inendikuyenera kukhala ndirimo ndi mwa Khristu, pakuti iwoamene ali mwaKhristuMulungu adzawabweretsa palimodzi ndiIye. Ine sindikusamala komwe uko kuli, Iye adzawabweretsa…Ndikwirireni ine mwa Yesu.263 Tayang’anani pa aneneri awo kumbuyo uko. Iwo ankadziwamwa maganizo enieni, tsopano, kuti chiukitsiro choyamba,zipatso zoyamba, zikadzakakhala ziri mu Palestina. Abrahamuanawagula malowo, ndipo iye—osati—ndipo iye anakamuikakoSarah. Ndipo iye anabala Isaki. Isaki anaikidwa pambalipa abambo ake ndi amake. Isaki anabala Yakobo; Yakoboanakafera mu Israeli—mu Igupto, anabweretsedwanso muPalestina. Ndiyeno, Yosefe nayenso anakafera kumeneko.Ndipo iwo anabweretsanso mafupa a Yosefe, chifukwa iyeanati, “Anapangitsa…” anachita kumulumbiritsa Yosefepa izo—Yakobo, kuti iye sadzamuika iye kumeneko, koma

1070 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

adzamubweretsanso iye ku dziko lolonjezedwa. Yosefe anati,“Tsiku lina Ambuye Mulungu wanu adzakuchezerani inu.Undirole ine—mafupa anga adzapite ndi kukaikidwa limodzindi bambo anga.” Ndipo iwo anatero, chifukwa, pokhalaaneneri, iwo ankamvetsa kuti zipatso zoyamba za chiukitsirozikadzakakhala mu Palestina.264 Tsopano, Baibulo linati…Ndipo ngati inu mukunditchaine mneneri, ine sindimanena kuti ine ndiri; koma ngati inumumanditcha ine zimenezo, kumbukirani, ine ndikunena kwainu mu dzina la mneneri (mukuona?)—mu dzina la mneneri,chiukitsiro ndi mkwatulo zidzakhala za konsekonse mu dzikolonse! Ziribe kanthu kumene inu muli, pamene ora limenelolidzabwera, inu mudzakwatulidwira mmwamba kukakomananaye Iye! Ndizo zonse! Palibe kanthu kati kadzakuletseni inu,ziribe kanthu kumene muli. Ndipo ine ndikungoyembekeza kutiine ndidzakhala kumeneko, mmodzi wa iwo. Ine ndikungodalirandi kuyembekeza mwa Mulungu kuti ine ndidzakhala mmodziwa iwo ndipo aliyensewa inu adzakhala umo—mofanana.

Tsopano, kodi ife tiri nayo nthawi ya lina? Ndiye iyoingokhala ili basi (mukuona?)—basi pafupifupi 1:00 koloko.

274. Wokondedwa M’bale Branham: Akazi anga ndi inetinasiyana. Iye akundisumira ine pofuna chisudzulo. Iye siMkhristu, ndipo ine ndikukhulupirira Uthengawu ndipoine ndikufuna kuti iye apulumutsidwe (Kodi zimenezosi zabwino? Umenewo ndiwo mzimu weniweni waChikhristu. Mukuona?) ndipo ndikukhulupirira. Kodi inendichite chiani? Ife tirinso ndi anyamata awiri. (Alembapodzina lawo.)

265 M’bale, penyani, ndiroleni ine ndikuuzeni inu, iyeakakusumirani inu pofuna chisudzulo; uyo ndi Satana.Mukuona? Akanati asachite zimenezo, koma ngati inu muliMkhristu ndipo simunachite kanthu mu dziko koti kamutchingemkazi ameneyo, ndiye ndi Satana akuchita zimenezoyo. Iyeakungoyesera kuti akung’ambeni inu apo.266 Tsopano, ngati iye ali mmodzi wa osankhidwa aMulungu, iye adzabwera kwa Iye. Ngati iye asali, iyesi woyenera kumudandaulira. Ndiye ngati izo zitero…Ngati inu muzidandaula izo ziphwasula thanzi lanu, ndipoizo ndi zimene Satana akufuna kuti achite. Iye akugwirantchito, ine ndikudziwa, pa inu. Kotero inu mungochiperekachinthu chonsecho kwa Mulungu ndi kupitirira patsogolokumamutumikira Mulungu mosangalala basi momwe inumungathere. Mulungu asamalira zina zonse zakezo. “Onseamene Atate andipatsa Ine adzadza kwa ine.” Zigwadani pamawondo anu; ine ndipemphera nanu inu kapena chirichonse.Ine ndipempherera vutolo. Muzingoti, “Ambuye Mulungu, inendikumukonda iye; iye ndi mayi wa ana anga,” (ngati iye

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1071

ali) ndi kuti, “I—i—ine ndikungochipereka chinthu chonsechikwa Inu, Ambuye. Ine ndikufuna iwo kuti apulumutsidwe,Inu mukudziwa kuti ine ndikutero; koma ine sindingapitirirepatsogolo pena. Iye apita kukandisudzula ine mulimonse. Inesindinachite kanthu kalikonse; ngati ine ndatero, ululirani izokwa ine; ine ndipita ndikazikonze zimenezo. Ine ndikachitachirichonse.” Ndiye chiperekeni icho kwa Ambuye ndipomungozisiya izo zokha ndiye, mungozisiya izo zokha. Zipitaniapo pomwe kumakhala moyo chimodzimodzi basi—ngati kutipalibe chimene chachitikapo konse. Ndipo Mulungu asamalirapa zina zonse za izo.275. Tsopano: M’bale Branham, kodi ndi chiani zonse izi

za anthu (O, kachiwiri!) kusamukira ku Arizona?Tafotokozani izi. Apo pali mtundu wina wa malembedwe.Onani, mukuona?Chabwino, ife tafotokoza kale zimenezo (mukuona?),

chomwe zimenezo ziri.276. M’bale Branham, kodi Mkwatibwi adzadutsa mu

kuzunzidwa momwe atumwi a mpingo woyambiriraanachitira?

267 Ayi, ine ndangofotokoza kumene zimenezo maminiti angapoapitawo. Ayi, chinthu chotsatira ndi mkwatulo tsopano.Kumbukirani, ife tiri pa dziko lolonjezedwa; ife tiri pa malire.Inu mukukumvetsa kuyenda kwa Israeli?277. Kodi ndi kololedwa—kugwiritsa ntchito mtundu uliwonse

wa kuteteza kubala?268 Ine kulibwino ndizisiyire zimenezo mpaka madzulo ano(mukuona?), chifukwa ziri…ine ndikufuna kuti—ine ndikufunakuti ndiyankhule chinachake pa izo.278. M’bale Branham, ine basi…(ine ndikudikirira basi

maminiti atatu ena ngati ine ndingathe. Ndiroleniine nditenge chinachake chachifupi pano mwina.) Inesindingathe kudzipereka kwathunthu kwa Yesu. Kodi inendiri ndi mzimu woyipa?

269 Ndiroleni ine ndingotsiriza nthawi ina yonseyi pa iloapo. Inu simukutha kudzipereka kwa Yesu? Iwo sakutha…Mukuona, ine sindikumudziwa kaya mwamuna kapena mkazi;ine sindikanatha kudziwa yemwe iye ali. Mulungu akudziwazimenezo.270 Inu simungathe kudzipereka kwa Yesu. Bwanji? Chavuta ndichiani? Ngati inu muli mkazi, inu simumakhala mukudziperekakwa mwamuna wanu kuti mukhale mkazake, dziperekeni zonsezimene inu muli? Dona wamng’ono pamene inu munakwatiwa,waukoma, munamenyera moyo wanu wonse kuti mukhalewaukoma; koma tsiku lina inu munamupeza mwamunaamene inu munamukonda. Inu munali wake kwathunthu.

1072 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Zinthu zimene inu munkamenyana nazo moyo wanu wonsendi kumayesera kuti muzikhala woyera, ndi momveka, ndimwaukoma; tsopano, inumukupereka pang’ono paliponse pa izokwamwamunammodzi. Kodi ndi kulondola uko? Inumwadziikanokha kwathunthu mmanja mwake; inu ndinu wake. Zonsezomwe inu munaziimira mwa ukhondo, ndi mwakhalidwe,ndi chirichonse monga choncho, tsopano inu mwazitembenuzaizo kwa mwamunayo, chifukwa inu mwadzipereka nokha kwamwamunayo. Kodi inu simungathe kuchita chinthu chomwechokwa Yesu Khristu? Kungodzipereka nokha mwanjira imeneyo—zonse zimene ine ndiri, malingaliro anga onse, maganizo angaonse. Ndithudi.

271 Ine sindikuganiza kuti inu mwagwidwa ndi mzimu woipa;ine ndikuganiza kuti mzimu woipa umakudzozani inu ndimaganizo awo a mtundu umenewo, kumayesera kukupangitsaniinu kumaganiza kuti inu simungathe kudzipereka nokhakwa Mulungu. Pamene…Ndiroleni ine ndikusonyezeniinu chinachake. Chifukwa chiani inu mungamafune kutimudzipereke kwa Iye? Chifukwa pali chinachake kunja ukochikuitanira kwa inu kuti mudzipereke. Icho ndi chizindikirochabwino kwambiri kuti inumukuyenera kudzipereka nokha.

272 Tsopano, zonse zimene inu mungachite, M’bale kapenaMlongo (akhoza kukhala munthu wachichepere kapenawachikulire, chirichonse chimene ali), inu munati…Sangathekudzipeza okha basi chotero kuti iwo angathe kudziperekaokha kwathunthu. Kungodzipereka nokha uko. “Ambuye,kuganiza kwanga, zanga zonse zimene ine ndiri, i—ine ndikufunakuti ndizipereke kwa Inu. Moyo wanga, ine ndikuwuperekangati moyo wa kutumikira. Nditengeni ine, Ambuye, ndikundigwiritsa ine ntchito basi momwe ine ndiri.” Ndipo ndichinthu chophweka chotero; ine ndikukhumba mpingo ukanatikwenikweni…ine ndikukhulupirira ng—ng—ngati kachisiyutsopano, akanati apindule pa mafunso amenewa…Kodi inumukuwakonda iwo? Chabwino. Iwo athandiza pang’ono.

273 Tsopano onani, pa izi, ngati mpingo ukanamafunsa kokhamafunso amenewa (inu mukuona?), kufunsa zinthu izi: ngatiiwo angati azichita izi, kapena kuchita izo, ndi chirichonse,ine ndiyesera kuti ndichite mopambana zomwe ine ndingathe.Ngati ine ndakulangizani inu molakwika, izo sizinali konsemu mtima wanga kuti ndichite zimenezo. Ngati ine ndanenachirichonse cholakwika kungoti ndikweze maganizo ena angaanga ndi zinthu, osati—p—podziwa kuti izo ndi zolakwika kutindichite zimenezo kapena kuti ndikuuzeni inu zimenezo, inendingakhale ndiri wachinyengo wonyansa. Ndiko kulondola.Koma kuchokera mu mtima mwanga, ngati ine ndikulakwitsa,Mulungu akudziwa (mwaona?) ine ndazichita izo ndi zonsezomwe ziri mwa ine kuti ndiyankhemafunso anu.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1073

274 Ndipo kwa inu atumiki uko mu dziko kumene tepi iyiidzapita, ine sindinanene zinthu izi kuti ndikupwetekeni inu.Ine ndinanena izo chifukwa ine ndimakukondani inu. Mukuona?Ndipo ine moonadi, ndi mtima wanga wonse…Ndi…Tsopano,ine sindikuyesera kugwirira ntchito kuti ndikusonyezenizimenezo—kuti i—ine ndikudziwa chinachake chimene inusimukudziwa za icho. Icho si chimenecho, m’bale wanga. Inendikungochita izi chifukwa ine ndikukukondani inu, ndipo i—i—inumukundikonda ine, ine ndikukhulupirira.275 Bwanji ngati inu mukanandiwona ine ndikupita mmusindi mtsinje mu ngalawa yokalamba, kunja kuno pa mtsinjeuwu, pafupi ndi kumene ife tiri pakali pano, kuno ku kachisi,Mtsinje wa Ohio; ndipo mtsinjewo nkukhala uli wodzazandipo ukusefukira; ndipo mathithi ali basi mmusi mwanga.Ndipo inu mukudziwa kuti ngalawa imeneyo siikadutsa pamathithi amenewo; iyo basi siichita zimenezo. Ndipo apaine nditakhala mmenemo ndi mutu wanga ntaugonekerammbuyo, ndi kuimba, ndi kupuma, ndi kupita mmusi momwe—kuyandama chammusi umo—mosangalala kutsika ndi mtsinjeumenewo; ndipo inu mukudziwa kumusi uko ine ndikachitangozi. Ngati inumukundikonda ine, inumungakuwe, kapena inumungalumphire mu ngalawa, ndi kuthamangira kumeneko, ndikudzandikhoma ine pa mutu ndi chinachake, kundibweretsa ineumo. “M’bale Branham, inu mwasokonezeka malingaliro! Inumwasokonezekamalingaliro; mathithi ali apa pomwe!”276 Ndipo ine ndikanati, “O, khala chete! Ndisiye inendekha!” Ndipo komabe inu mukundikonda ine mulimonse.Inu mungachite chirichonse mu dziko; inu mungandigwireine. Ngati inu mukanati—ngati inu mukanati muiphwasulengalawayo, inu mukanandichotsamo ine mmenemo, chifukwainu mukundikonda ine; inu mukudziwa chomwe chitichikachitike.277 Ndipo m’bale, ine ndikudziwa izo ndi zomwe ziti zikachitikekwa chipembedzo chimenecho. Icho sichilimba mu mafunde.Mukuona? Inu mukupita molunjika kumene ku Bungwe laMipingo ya Mdziko; ndipo tsopano, inu mwina muyenerakutenga icho kapena icho ndi choti chitulukemo momwe ifetiriri tsopano. Kotero, izo ziri basi ndendende, inu muyenerakupanga kusankha kwanu. Ndipo i—ine sindikutanthauza kutindikhale…Ine ndikanafuna kuti ndiiphwasule ngalawayo,chabwino; ine ndikanafuna kuti ndipange chirichonse chimeneine ndikanatha, osati kuti ndikupwetekeni inu, m’bale,koma kuti ndikudzutseni inu kuti inu mukulakwitsa. Musatimuzichita zimenezo!278 Ndipo ubatizo wa mmadzi uwu mu Dzina la Yesu Khristu,palibe munthu pa nkhope ya dziko lapansi angathe kuwutsutsaiwo mwa Lemba. Palibe munthu angatsutse izo. Palibe Lembalimodzi…Anthu inu, abale inu—inu abale, mu kumbukira,

1074 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

muzingokumbukira, kafufuzeni mu Baibulo; kapezeni maloamodzi pamene wina aliyense anabatizidwapo konse muChipangano Chatsopano (iwo sankabatizidwa mu Chakale,koma mu Chipangano Chatsopano)—pamene wina aliyenseanabatizidwapo konse mwa njira ina kuposa mu Dzina laAmbuye Yesu Khristu; ndiye mubwere mudzasonyeze izo kwaine. Kapena pitani mukapeze bukhu la mbiriyakale pameneiwo ankabatizidwapo konse kwa mazana a zaka pambuyo paimfa ya atumwi otsiriza…Mpingo wa Katolika unayambitsaubatizowo. Katekizimu wawo amanena chinthu chomwecho,wogwiritsa ntchito dzina la Atate,Mwana,MzimuWoyera.279 Pa kukambirana ndi wansembe, komwe kuno ku Mpingowa Mtima Woyera, anandiuza ine chinthu chomwecho. Anatimpingo wa Katolika unkabatiza monga choncho, pamene inendinamuuza iye kuti ine ndinamubatiza msungwana wa aFrazier uyu, pamene bishopu ankafuna kuti adziwe. Iye anati,“Kodi iwe ungalumbirire pa maneno awa?”

Ine ndinati, “Ine sindimalumbira konse.”Iye anati, “Bishopu akufuna kuti iwe utero!”

280 Ine ndinati, “Bishopu ayenera kuti atenge mawu angakapena musati muzikhulupirire izo, china chirichonsechimene iye angafune.” Mwaona? Ine ndinati, “Baibulo linatitisamalumbire konse.”

Ndipo iye anati, “Chabwino, nha…” Iye anati, “A…”281 Ine ndinati, “Ine ndinamubatiza iye mwa ubatizo waChikhristu mu madzi, ndinamumiza iye pa phazi la SpringStreet mu Dzina la Ambuye Yesu Khristu.”

Ndipo pamene wansembeyo anazilemba izo, iye anati, “UmondimomwempingowaChikatolika unkabatizira kale.”

Ine ndinati, “Liti?”Iye anati, “Mumasiku a atumwi.”Ine ndinati, “Inumumawatcha iwoAkatolika?”Iye anati, “Zedi, iwo anali.”

282 Ine ndinati, “Ndiye ine ndine Mkatolika wabwinoko kuposamomwe inu muliri. Ine ndimatsatira chiphunzitso chawo.”Ndiko kulondola. Mwaona, mukuona? Iwo amadzinenerazimenezo, koma siziri choncho.283 Mpingo wa Katolika unakhazikitsidwa ku Nicea, Roma,pansi pa Konstantini, pamene mpingo ndi boma n—zinalumikizana palimodzi, n—ndipo boma linaupatsa mpingochuma, ndi zinthu monga choncho; iwo makamaka ankaganizakuti iwo anali mu Zakachikwi. Iwo ankaganiza iwo analiatagunda Zakachikwi. Zimenezo zinali zakachikwi za Satana.Ndizo ndendende kulondola. Inu musati muzikhulupirira zinthuzoterozo. Inde, bwana!

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1075

284 Tsopano, koma…Ndiye pamene iwo anapanga—kapenaanali mmalo mokhala nalo—fano, iwo anamuchotsa apo—iwoanamuchotsa apo Venus, anaikapo Maria; anamuchotsa apoJupiter, anaikapo Paulo kapena Petro. Komwe uko k—kuVatican, uko komwe mu—Roma tsopano, mu Mzinda wa Vaticanmomwe, choimikidwa cha mapazi naintini cha Petro, iwoamadzinenera kuti apsyopsyonapo zitatu za zala zimenezo zaphazi la choimikidwa chimenecho. Mukuona? Ndipo chirichonsechiri…285 Zonse kumatsika…Tinapita ku tchalitchicho, Billy ndi ine,mmawa wina kumeneko, tinapita mmusi mu chipinda chapansikumene amawaika mamonki onse ndi zinthu monga chonchondi kuwasiya mafupa awo azivundira mu fumbi limeneli—fupa limodzi kuvunditsidwa ndi limzake kumeneko—ndiyenonkutenga mafupawo ndi kupangira zolumikiza za zolumikizazopepuka za manja amafupa zikulendewera monga chonchi,ndi zigaza; ndipo anthu obwera mmenemo azipukuta zigazazimenezo mpaka zayera, kuyesera kuti azipeza madalitsokuchokera ku zigaza za anthu okufa amenewo. Ndi machitidwea zamizimu. Mukuona?286 Ndipo ndi kumene izo zinayambira uko komwe, mu Roma,ndipo uko ndi kumene mpando wa chirombo uli, ndipokuchokera kumeneko kunabwera manthu hule wamkulu. Ndipoana ake aakazi ali timahule ndendende basi momwe iye aliri,chifukwa iye analipatsa dziko lonse chikho cha mkwiyo wake—chikho cha umboni wake, chimene chinasakanizidwa mmenemondi ndulu ya dziko lapansi. Ndipo iye anali ndi umboniwake. Iye anati, “Ine ndikukhala ngati namwali, ndipo i—ine ndikukhala ngati wamasiye (ine ndikutanthauza), ndiposindiri wosowa kanthu”; ndipo iye sakudziwa kuti iye ndiwomvetsa chisoni, wopandapake, wakhungu, wosauka, ndiposakudziwa izo. Ndi zimenezozo. Ndipo zimenezo ndi za mpingowa Katolika kuphatikizapo chipembedzo cha Chiprotestantichirichonse! Koma mu chisokonezo chonse icho kunja uko, ukokuli anthu ofunika amene amawakonda Ambuye Mulungu ndimtima wawo wonse, solo, ndi malingaliro. Ndipo iwo akuganizakuti akulondola. Iwo akuganiza kuti iwo akuchita zolondola.Mulungu adzakhalaWoweruzaWamkulu.287 Kwa ine, ngati Mulungu ati adzauweruze mpingo ndidziko—mpingo wa Katolika umenena chomwecho—ndiye inendinamufunsa bambo uyu amene ine ndinkafunsidwa naye…Iye anati, “Mulungu adzaweruza dziko ndi mpingo.”

Ine ndinati, “Utiwo?”Iye anati, “Mpingo wa Katolika.”

288 Ine ndinati, “Mpingo wa Katolika wake uti? Iyo ndiyosiyana umodzi kwa umzake.” Mpingo wake uti? Wa GreekOrthodox kapena wa Chiroma? Kapena ndi uti umene Iye ati

1076 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

adzaweruze nawo ilo? Ngati Iye ati adzaliweruze ilo ndi mpingowa Chiprotestanti, utiwo? Wa Methodisti, Baptisti, Chilutera,Chipentekoste; kodi Iye adzaliweruza ilo ndi uti? Baibulo linatiIye adzaweruza dziko ndi Yesu Khristu, ndipo Yesu Khristundiye Mawu. Kotero kwa ine, ndi Mawu a Mulungu amene Iyeati adzaliweruze nalo dziko lapansi. Ndiko kulondola. Ndipo inendikukhulupirira ziweruzo Zake ziri mu dziko lapansi tsopano,ndipo ine ndikukhulupirira…Tiyeni ife tifunefune ndi mtimawathuwonse kuti tithawemkwiyowa chiweruzo chamkwiyowaMulungu umene uti udzatsanuliridwe pa dziko losakhulupiriraili; ndipo palibe njira yina konse yomwe ilo lingathawire izo—kuzithawa izo.289 Sizidzatheka nkomwe, nkomwe, nkomwe kubwerachipulumutso kwa dziko kenanso. Iwo adutsa mzere wawopakati pa chisomo ndi chiweruzo. Pali…Inu mukhoza kuikaAbraham Lincoln mu dera lirilonse la mu United States, ndipoizo sizidzatha kutembenuza nkomwe gulu ili la “Marike” ndi“Maelvisi” kubwerera kwaMulungu.290 Pamene inu munawona mu pepala (ine ndiri nazoizo. Ndibweretsa izo kwa inu madzulo ano ngati inumukufuna kuti muziwone izo usikuuno), kumene mpingowa Chipresbateria (ambiri a inu mwina munaziwona izo)—mpingo wa Chipresbateria ukudutsa mu misa kapena k—k—kupyola mu sakaramento ndi roko ndi rolo. Abusa ataimapamenepo akuwomba manja awo monga choncho; ndipo iwoanali akudutsa mu njira ya mtanda ndi “kumavina izo” ngatiroko ndi rolo mumpingo wa Chipresbateria.291 Ndipo pamene gulu lapansi motsika ili, likufuula, lauve laMabitolozi, limene likutchedwa chomwecho, limene lafika pansipamunthu ndipo akufuna kuti akhale tizirombo…Iwo anakanachigwirizano cha ntchito ya madola zikwi zana mu St. Louismasabata angapo apitawo; sakanalola kuleka pofuna zimenezo.Anabwera kunoko, gulu la achichepere, zigawenga za anthuAchingelezi kumeneko ali ndi tsitsi lawo likulendewera pansimpaka mmaso awo. Ndipo tsopano, iwo ali ndi chipembedzochao chao chimene iwo akuyambitsa. Inu mwaziwona izo mumagazine ya Look. Mukuona?292 O, momwe dziko lino lavundira. Palibe chiyembekezo kwailo konse; iwo adutsa mzere wolekanitsa pakati p—pakatipa kulingalira ndi nzeru zawamba, nanga tikati pakati pachipulumutso.293 Anthu sakutha ngakhale kuweruza. Ife tiribe amunapanonso monga ife tinkakhalira nao. Ali kuti Patrick Henry? Alikuti Abraham Lincoln?—amuna amene angathe kuima chifukwacha kukhudzidwa kolimba.294 Ali kuti amuna awo amene angadzuke apo ndikuwapangitsa akazi openga awa kunja uko, odzivula okha

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1077

ndi—ndi kumatuluka pamaso pa amuna awa; ndiyeno—ndikumawayendetsa iwo kunja ukomonga gulu la odzivula, ndiyenonkumamuika mnyamata mu chilango amene angamunenemmodzi wa iwo? Kuli kuti kungalira kwanu? Nzeru wambandi chiani? Ngati iye akudziika yekha kunja uko, musiyeni iyeazipita ngati galu. Inde, bwana! Ngati iye sati apitenso ku…makhalidwe a wamba a iye oposa awo…Ali kuti malamuloamene angaziletse zimenezo?

295 Komwe kuno mu Louisville, Kentucky, masabata awiriapitawo pamene mkazi uja ali ndi—amayesera kuti apange—ayike dzina lake mu pepala, anavala kabudula wosambira wapulasitiki, anayenda napita kumeneko kuchokera ku BrownHotel; ndipo mpolisi anayesera kuti amuimitse iye, ndiposanaime ayi; anamuseka iye. Ndipo iye akanaponyera mfuti paiye kuti amuimitse uyo; iye anamukankhira iye mu galimotondipo anamupangitsa iye kuti akakomane naye ku siteshoniya polisi chifukwa chovala mopanda khalidwe ndi zinthumonga zimenezo, ndipo iye anapita ndipo anakakomana…Inumukudziwa zimene iwo anachita pa izo? Anamuchotsa ntchitompolisiyo.

296 Mulungu thandizani fuko limene lavundali! Iwe sungadutsenazo kupatula ngati utachita zolakwika. Ife tikhoza kusadutsanazo, koma tingathe kukafika kumwamba; ndipo uko ndikumene ife tikuyembekezera. Tiyeni ife tiweramitsemitu yathu.

297 Ambuye Yesu, lolani M’busa wamkulu abwere ndikudzatichotsa ife mu izi, Ambuye. Ife tikumuyembekezeraIye. Ife tikuyang’anira ora limenelo. Pamene ife tikuliwonadziko litavunda kwambiri. Inu munati ilo likanadzakhalamwanjira imeneyi. Aneneri anu aakulu ananenera kuti maoraawa akanadzakhala ali kuno. Ife tikuwakhulupirira aneneri,Ambuye; ife tikuwakhulupirira iwo.

298 Ndipo tsopano, ife tikupemphera, Mulungu, kuti Inumutipatse ife aneneri kuti atanthauzire Mawu awa kwa ife, kutiife tikhoze kumadziwa ngati tikulondola kapena tikulakwitsa.Ife tikuwona aneneri abodza akuwukapo; iwo ali mu zipululu,Mzinda wa Salt Lake, madera onse a fukoli, mitundu yonse yazipululu, ndi mitundu yonse ya zipinda zobisika, mitundu yonseya Atate Aumulungu, ndi zina zotero, kulikonse.

299 Powawona abale osauka achikuda awo, alongo kunja ukotsopano; iwo amafuna kusakanikirana. Mwamsanga pameneiwo anakupeza iko…Uko nkulondola; iwo amayenera kukhalanako iko; iwo ndi abale ndi alongo. Tsopano, pamene iwoakupeza iko, iwo ayipirapo kuposa kale. Izo zikusonyeza kutindi zodzozedwa ndi chikominisi. O, Mulungu, kodi anthuosauka awo angawone zimenezo? Kuti izo zimangochitidwa…Chabwino, izo zikuyenera kuti zichitidwe, Ambuye.

1078 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

300 Bwerani, ndi chimene ife tikufuna. Inu mungobwera,Atate. Ife tikuyembekezera. Bwerani, Ambuye, titengereniife mkhwapa Mwanu. Tikhululukireni ife machimo athu.Palibe ayi—palibe chilungamo panonso mu dziko muno.Chinthu chimodzi chikukoka motsutsana ndi chinacho, ndipokomabe izo zangokhala zodyedwa kwambiri ndi mphutsimpaka inu—mulibenso zomveka mmenemo. Inu munati thupilonselo langosanduka ngati mabala onunkha. Zoonadi, gomelirilonse liri lodzaza ndi masanzi. Inu munati, “Ndani ameneine ndingamuphunzitse chiphunzitso? Nndani amene inendidzamupangitse kuti amvetse mu tsiku limenelo?” Gome lonsela Ambuye liri lodzaza masanzi. Ife tikuziwona izo, Ambuye. Ifetikuliwona oralo pano. Tithandizeni ife, chonde.301 Wokondedwa Mulungu, ochuluka a mafunso awa panookhudza anthu kubwera ku Arizona. O, wokondedwa Mulungu,lolani anthu okondeka, ofunikira awo…Iwo akamvetserakwa tepi iyi kumeneko. Aloleni iwo adziwe kuti ine sindinewolamulira mwankhanza kuti ndiziwauza iwo koti azikakhala,zoti azichita. Ndipo mulole iwo amvetse bwino bwinozimenezo. Ngati iwo akulikonda dziko limenelo, inenso ndiri,asiyeni iwo akhale kumeneko, Atate. Koma pamene iwoakuphunzitsa kuti mkwatulo uyenera kubwera kuchokerakumeneko, ndipo uko kokha, kapena kuti iwo akuyenerakumakhala ali ndi ine, wochimwa wosauka, wosayenera, wauve,wopulumutsidwa mwa chisomo cha Mulungu—kuchita kutiazikhala pondizungulira ine…Ambuye, ine ndikufuna kutindikhale pozungulira—ine ndikufuna kuti ndikhale pomwepali Paulo; ine ndikudziwa kuti iye apitako. Ndi Petro,ndi Yakobo, ndi Yohane, iwo ali mu Palestina anaikidwapenapake kumeneko. Ine ndikudziwa ine ndidzapita limodzinawo iwo ngati Inu munali nalo dzina langa pa Bukhulija chikhazikitsireni maziko a dziko. Ine ndidzakhala ndirikumeneko. Ndipo ine ndikupemphera, Mulungu, kuti aliyensewa iwo adzakhale ali kumeneko. Ndithandizeni ine, Ambuye,kuti ndiwasonkhanitse iwo onse abwerere kuno kwinakake,kumene iwo angathe…Iwo akufuna kuti azimvera uthengandi aphunzitsi aakulu awa monga M’bale Neville, ndi M’baleCapps, n—ndi abale ena onse awa kuno: “Junie,” ndi M’baleRuddell, ndi o, J.T., ndi onse awo—onse awo: M’bale Collins,ndi M’bale Beeler, ndi M’bale Palmer, n…Mulungu, inendikupemphera kuti Inu mungopereka izi kwa awa…

L—l—lolani iwo abwere kuno kumene iwo amaumva Iwokwenikweni, ngati iwo akufuna kuti aziumva Iwo, osatikuthamangira kutali uko ku chipululu icho. Iwo akuyeserakuti azichita ndendende zimene Lemba ili linawauza iwo kutiasachite. “Onani, iye ali mu chipululu; musazikhulupirire izoayi! Onani, ziri mu chipinda chobisika; musakhulupirire izoayi!” Ambuye, ine ndikuyesera mwa kupambana kwanga kuti

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1079

ndiwachenjezo iwo, koma izi zonse zikusonyeza kuti oralolafupikira tsopano. Mithunzi ya usiku ikugwa.302 Ine ndikupempherera chifundo, Ambuye. Khalani ndichifundo pa ine; ndithandizeni ine. Izo zikundipangitsa inemanjenje, Atate. Ine ndikupemphera kuti Inu mundithandizeine. I—ine sindikufuna kuti ndisindikize moyo wanga…Ntchito yanga yonse kuno ikhale ili kunja kuno wotengekawina akutsogolera gulu lina kapena kachiphunzitso kotsatiramunthu mu chipululu kwinakwake. Musalole dzina langakuti lipite pansi monga choncho, Ambuye. Ine ndamenyeramolimba pofuna izi. Ndine wodzipereka mu izo momwe inendingakhalire ndiri. Mulungu, musalole izi kuti zichitike.Ndithandizeni ine mwanjira ina. Ine sindikudziwa zoti ndichite;ine ndikungodalira pa Inu, koma Inu mundithandize ine. Inendichita chirichonse chimene Inu muti mundiuze ine kutindichite. Ine ndine wantchito Wanu; awa ndi ana Anu. Ambuye,awa…Ochuluka a anthu awa, nainte naini pa handiredi,Ambuye, ndi olimba kwenikweni. Iwo akukhulupirira; iwoakudziwa; iwo akumvetsa. Ndipo iwo akudziwa kuti siineyo; koma ine ndikudziwa zinthu izi ziyenera kuchitsatirachitsitsimutso chirichonse, ndipo ichi chiribe kutetezeka kwaizo. Kotero ine ndikupemphera kuti Inu mutithandize ifetsopano.303 Tithandizeni ife pamene ife tikupita kukakhala ndichakudya chochepa cha masana lero, Ambuye. Dalitsanikusonkhana kwathu palimodzi. Dzatisonkhanitseni ifemobwerera muno mofulumira madzulo ano. Ambiri a iwo asowakuti apite kwawo tsopano, Ambuye. Iwo ayenera kuti apite—kwawo, ndipo ine ndikupemphera kuti Inu muwathandizeiwo. Mulole iwo akakhoze kutha mwanjira ina, Ambuye,kuti adzaipeze tepiyo kuti adzamve mafunso ena onsewo.Mwinamwake lawo silinayankhidwe. Ine ndikupemphera kutiInu muwathandize iwo, Ambuye.304 Ndithandizeni ine mwaliwiro kwenikweni usikuuno kutindingoyankha mafunso awa ndi kutengeramo lirilonse la iwoamene ine ndingathe. Mpaka ife tikomane muno madzulo ano,Inu mutatidalitsa ife. Mu Dzina la Yesu ine ndikupemphera.Ameni.

Ndinkonda Iye, ndinkonda Iye,Poti Iye anayamba kundikonda,Nagula chipulumutso changaPa mtengo wa Kalvare.

305 Zinalemba pamenepo, ine ndinalemba izo kuti nthawizonsezizikhala patsogolo panga: “Khristu patsogolo panga, pameneine ndikuyankhamafunso amenewa.”Kodi inumukukhulupirirakuti ine ndimanena izo kuchokera mu mtima wanga?Chirichonse ndi chochokeramumtimawanga kuti ndithandize.

1080 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Ena a iwo akhoza kubwera kudzatenga maphukusi awopano.306 Wokondedwa Mulungu, apa pali mipango, maphukusiali apa. Izo zikupita kwa odwala ndi osautsika. Lolaniwotanthauzira wamkulu wa Mawu, Mzimu Woyera ameneanawalemba Iwo, mulole Iye abwere pafupi tsopano chifukwacha gawo ili la utumiki ndipo adzadalitse zovala izi. Ambuye,ngati ine ndikuganiza za inemwini, ndine yani kuti ndigonetsethupi langa losayera, lauve molambatitsa pa mipango iyi imeneikuima pakati pa imfa ndi moyo kwa ochuluka? O, Mulungu,ine ndikunjenjemera. Koma pamene ine ndikuganiza kuti…Inu simukundiwona ine, Inu mukungomva liwu langa. Ilolikubwera kupyolera mu Magazi a Ambuye Yesu kumeneko.Tsopano, ine ndikukhulupirira kuti Inu mundiyankhira inebasi monga Inu munamuchitira Iye, chifukwa Iye anapita inendisanabwere kuti akakhale pa dzanja lamanja, kumwambauko, la Ufumummwamba umo. NdipoMagazi Ake ali kumenekomonga chitetezero, ndipo ine ndaphimbidwa pansi pa Magaziamenewo.307 Ine ndikukhulupirira, Ambuye, kuti Inu mukawachizaiwo, pakuti iwo ali osowa. Iwo sakanati akhale ndi izizitaikidwa apa. Ine ndikupemphera kuti Inu muwapangitsealiyense kukhala bwino. Pamene ine ndikudziyika ndekhamodzilambatitsa pa izo, monga…Iwo amati anatengakuchokera ku thupi la Paulo…Iye anali wochimwa basinayenso, Ambuye, wopulumutsidwa mwa chisomo Chanu.Anthu ankamukhulupirira iye, ngakhale iye ankawazaziraiwo ndi chirichonse, koma iwo ankadziwa kuti iye analiwolishya. Iwo ankadziwa iye—anatumizidwa kuchokera kwaInu, chifukwa Inu mumadzitsimikizira Nokha mwa utumikiwake. Mulungu, anthu awa akukhulupirira chinthu chomwecholero. Ine ndikupemphera kuti Inu muwathandize iwo tsopanondi kumuchiza aliyensemuDzina la YesuKhristu. Ameni.308 Kodi inu muli ndi njala? Chabwino. Ine ndiri ndi njalayofuna mafunso enanso. “Munthu sadzakhala moyo ndi mkatewokha, koma ndi Mawu alionse amene atuluka kuchokeramkamwa ya Mulungu.” Tsopano, ine mwinamwake…Ena amafunso awa, ine ndikhoza kusakhala nawo iwo molondola; inendangochita mopambana momwe ine ndingathere. Usikuuno,ine ndiyesera kuti ndiyambire basi pa 7:00 koloko. Chabwino,tchalitchi chitsegulidwa pa 6:30. Ndipo inu amene mungathekutsalira…Inu amene simungathe, ife tikumvetsa; zimenezoziri bwino bwino. Koma ine ndiyesera kuti ndilitenge lirilonsela awa momwe ine ndingathere kutero usikuuno. Mulunguakudalitseni inu mpaka ife tidzakomane.

Tsopano, tiyeni ife time pa mapazi athu ndi kuimba nyimboyabwino yakale iyi, nyimbo yathu yobalalitsira, Tenga Dzina laYesu Limodzi Nawe. Chabwino.

MAFUNSO NDI MAYANKHO 1081

Tenga Dzina la Yesu nawe,Mwana wachisoni ndi watsoka;Lidzakusangalatsa ndi kukutonthoza,Litenge, kulikonse upita.Dzina lofunika, kukoma kwakeko!Chiyembekezo cha padziko ndi chisangalalocha Kumwamba;

Dzina lofunika, kukoma kwakeko!Chiyembekezo cha padziko ndi chisangalalocha Kumwamba.

309 Ine ndikufuna kuti ndipange kulengeza uku. Billyanangonena kuti anatenga chopereka chachikondi mmawawu(mukuona?), ndipo anati iwo anali ndi chopereka chabwinochachikondi. Ine ndinamupangitsa iye kuti apite kumbuyo kwanyumbayi ndi kukaima kumbuyo uko. Kwa anthu kuno amenesanabwere atakonzeka, mulibe ndalama ya chakudya chanu,Billy akupatsani inu ndalama ya chakudya chanu ndi za—kutimukalipirire mtengo wa hotelo kapena mtengo wa motelo,chirichonse chimene icho chiri. Inu mutenge ndi kukalipiriraizo tsopano. Ngati inu muli…Ngati inu mungathe kukhala…Billy akakumana nanu inu kumbuyo uko ndi kukatenga dzinalanu ndi kumene inu mukukhala, ndipo ife tilipirira chakudyachanu ndi mtengo wa hotelo yanu kuchokera mu choperekachachikondi chimene ananditengera inemmawa uno.

Mpaka tidzakomane! mpaka tidzakomane!Mpaka tidzakomane pa mapazi a Yesu;

Khalidwe Dongosolo ndi Chiphunzitso cha Mpingo, Bukhu Lachiwiri(Conduct, Order And Doctrine Of The Church, Volume Two)

Mauthenga awa a M’bale William Marrion Branham olalikidwa ku BranhamTabernacle mu Jeffersonville, Indiana, U.S.A., anatengedwa kuchokera pamatepi ojambulidwa ndi maginito ndipo anadindidwa mosachotsera mawuena mu Chingelezi. Ndipo kumasulira kwa Chichewa uku kunadindidwa ndikugawidwa ndi Voice of God Recordings.

CHICHEWA

©2009 VGR, ALL RIGHTS RESERVED

VOICE OF GOD RECORDINGS, MALAWI OFFICE

P.O. BOX 51453, LIMBE, MALAWI

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. BOX 950, JEFFERSONVILLE, INDIANA 47131 U.S.A.www.branham.org

Chidziwitso kwa ofuna kusindikiza

Maufulu onse ndi osungidwa. Bukhu ili mukhoza ku printa kunyumba kwanu ngati mutafuna kuti mugwiritse ntchito inuyo kapena kuti mukawapatse ena, ulere, ngati chida chofalitsira Uthenga wa Yesu Khristu. Bukhu ili simungathe kuligulitsa, kulichulukitsa kuti akhalepo ambiri, kuikidwa pa intaneti, kukaliika pakuti ena azitengapo, kumasuliridwa mu zinenero zina, kapena kugwiritsidwa ntchito ngati njira yopezera ndalama popanda chilolezo chochita kulembedwa ndi a Voice Of God Recordings®.

Ngati mukufuna kuti mumve zambiri kapena ngati mukufuna zipangizo zina zimene tiri nazo, chonde mulembere ku:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org