lowezani mabuku a m’baibulo—gawo 1 · ezara anathandiza kuti anthu ayambenso kulambirayehova...
Post on 20-Aug-2020
2 Views
Preview:
TRANSCRIPT
Lowezani Mabuku a M’Baibulo—Gawo 1Dulani makadiwa kuti akuthandizeni kuloweza mabuku ena a m’Baibulo a Malemba aChiheberi. Funsani anthu a m’banja mwanu komanso anzanu.
GenesisBuku lofotokoza
mmene paradaiso anathera
EkisodoMulungu anapulumutsaanthu ake modabwitsa
LevitikoMalamulo a Mulungu
anawathandiza kukhalaoyera tsiku lililonse
NumeriEna analephera kukalowa
m’Dziko Lolonjezedwa
KHALANI BWENZI LA YEHOVA � ZOCHITA
s
PINDANI
PINDANI
www.jw.org � 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of PennsylvaniaTsamba 1
DeuteronomoAnalimbikitsidwa
kuti akhale omvera
YoswaBanja lililonse
linali ndi malo awoawo
OweruzaAnthu a Mulungu
ankachita zinthu zodabwitsa
RuteAnapeza mwamunandiponso pokhala
KHALANI BWENZI LA YEHOVA � ZOCHITA
s
PINDANI
PINDANI
www.jw.org � 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of PennsylvaniaTsamba 2
1 SamueliMulungu anasankha
Davide kuti akhale mfumu
2 SamueliM’banja lake munali mavutochifukwa cha machimo ake
1 MafumuUfumu unagawanika,
wina kumpoto wina kumwera
2 MafumuNgakhale kuti
ambiri ankachita zoipa,ochepa anali okhulupirika
KHALANI BWENZI LA YEHOVA � ZOCHITA
s
PINDANI
PINDANI
www.jw.org � 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of PennsylvaniaTsamba 3
1 MbiriAnaphunzirapo kathu
pa zochitika zakale
2 MbiriMtunduwo unakumana ndi mavuto
chifukwa cha mafumu oipa.
EzaraAnathandiza kuti anthu
ayambenso kulambira Yehova
NehemiyaAnathandiza kuti mzinda
ndi mpanda wake zimangidwenso
KHALANI BWENZI LA YEHOVA � ZOCHITA
s
PINDANI
PINDANI
www.jw.org � 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of PennsylvaniaTsamba 4
EsitereAnayankhula molimba mtima
pa nthawi yoyenera
YobuKukhala wokhulupirika
kumasangalatsa Mulungu
MasalimoNyimbo zotamanda
chikondi cha Mulungu ndimphamvu zake
MiyamboNzeru zopezeka m’mawu ake
n’zothandiza kwambiri
KHALANI BWENZI LA YEHOVA � ZOCHITA
s
PINDANI
PINDANI
www.jw.org � 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of PennsylvaniaTsamba 5
MlalikiKutumikira Mulungu
n’kosangalatsa kwambiri
Nyimbo ya SolomoChikondi chenicheni
chimakhalapo nthawi zonse
YesayaMmene moyo udzakhalire
Yesu akadzayamba kulamulira
KHALANI BWENZI LA YEHOVA � ZOCHITA
s
PINDANI
PINDANI
www.jw.org � 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of PennsylvaniaTsamba 6
top related